Man kills himself in Blantyre: ‘He got tired with life’

Advertisement

 hangingA 25 year-old man in Blantyre has committed suicide by hanging himself to a branch of a tree.

According to assistant Public Relations Officer for Limbe police Widson Nhlane, the deceased has been identified as Ben Christopher who was staying alone in his house at Chipanda village in Blantyre.

“The deceased was staying alone in his house and he committed suicide on 19 September this year,” said Nhlane.

He added that people found the man hanging from the tree on Monday and they reported the matter to police.

Officers went to the scene and took the body to Queen Elizabeth Central hospital.

The deceased hailed from Chipanda village, Traditional Authority Machinjiri in Blantyre.

Advertisement

148 Comments

  1. Kkk watopadi ndi moyo akapume ameneyo ndinthu watopa ndiku va za mavuto ali dziko muno bola pamenepo mawa ndine ndikuzi pachika nane aishi

  2. a Tisaweluzane pa imfa, mau akuti tisadziyetsele adzeru mwa ife tokha, ndipo siwose opezeka pa chingwe amachita kuzipha, zinachitikapo kuno ku CapeTown munthu wina anaphedwa ndikupachikidwa pachingwe ngati wachita kuzipha. Soka kwaiwo wozipha wokha pamene mau aMulungu akuti tisaziweluze tokha kuweluza kuli kwa iye mwini atelo ambuye pa AROMA 11;12VC 9 (Zamakhalidwe okoma otiyenela),

  3. mmmmh anthu ambiri ali muzipatala kufuna chithandizo kut akhale ndimoyo koma ena kuma wuseweletsa moyo aaah uthana ndi mulungu kumwambako.

  4. Why do people choose a permanent solution to address a temporary situation? God gave us life to enjoy and make the best of it..am sure for every situation one should strive to make the best out of it. All in all rest in peace brother

  5. Guyz zimafk pna sungaplir, lok wher Mw goin.Evn i ma self im pasn though dfcult tmes. i nid som one 2 …So dat i sld hv piec in ma mind.0885557555

  6. Pamene ena akuyamika namalenga kuti “ZIKOMO YEHOVA”Pondisungira ine moyo ngakhale akudwal,ndipamene ena akudzipha Hmmmmmm!!! sindidziwa ngati kuli mpumulo wa bata kwa awo akuzipha.Ambuye atithandize

  7. Mau akuti Go and sin nomore ” akutan2auza omwe azindikira mavuto awo! Koma omwe sanapite kokalapa ndiye kuti sanazindikire adakali ndi satana wavindikirabe Koma iwo aziwa ndi kumasulidwa azapeza mtendere munjira iliyonse azaduse Haleluya?

  8. Ngati sanamujudule kwawo kapena Adani ake! M’modzi wa anthu Opepera m’maganizo pa dziko Lonse! anali ameneyu. ndani umoyo! wa matsiku ano! anganene kuti Alibe Mavuto?. komano sizimatanthauza kuti ufikile podzichosela moyo.

  9. Apa tingoti achimweneo zawagwe zatha zimu wawo usakause mumtendele koma ukazuzike pempho kwa apolisi chingwecho chimangidwe osachisekelera

  10. After suffering yoyoyo aben watchuza njila yolakwika .mwaona tsopano a police akukusakani RIP kumene uli pakali pano

  11. So,at 25 he was tired of living on this planet earth. I feel sorry for him but killing one’s self is and will never be a remedy to any problem no matter how tough it is.

  12. Mau akuti Go and sin nomore ” akutan2auza omwe azindikira mavuto awo! Koma omwe sanapite kokalapa ndiye kuti sanazindikire adakali ndi satana wavindikirabe Koma iwo aziwa ndi kumasulidwa azapeza mtendere munjira iliyonse azaduse Haleluya?

  13. Fuso ndi lakuti kodi ozimpha yekha amausaso mu mtendere? Tiyeni tiziyamika nthawi zonse kamba ka moyo omwe tiri nawo chifukwa Mulungu anapereka Ambuye Yesu kuti akakhetse mwazi ndi chifukwa tiri moyo lero.

  14. HE WAS SAID ;befor he Hangitt Himself: I now , people there going to think toomuch , but God is going to look the reson only.

  15. Ndimaluzi akewa munthu angaleke kudzimanga? panopo palibe chomwe chikuyenda.pano akunjoya ndi akawalala nde utakhala ot kubako sumadziwa mmmmmm

  16. Oh poor Ben! Yes loneliness can be terrible indeed. But great minds use loneliness for deep creative thinking! Think positively at all times. Nothing is impossible under the sun. There is always someone for everyone under the sun! The best gift we should all be asking from God is knowledge and good health. The rest will just follow. Please,don’t give up on yourselves. Soldier on till your last God given minute on this earth.

  17. I may agree with you EthelMakamo. Koma kufika point yoti nku lozedwa, kumakhalaso kuchepa muchikulupiliro mwa Mulengi wathu Mulungu.
    Ndikuphempeni anthu aMulungu nonse
    Tiyeni tikhale ophempera komaso ozindokira kuti Mulungu anatilenga ndocgolinga ndipo nthawi yochokela paziko anayi pangaso yeka osati ife kuzipangila.
    Kuzipachika ndichimolomwe Mulungu saakululuka ayi chifukwa munthu aliyense moyo alinawowu Yesu anachita kuzatifera kuti tikhale nawo. Werengani Bible ndipo mukhale mumawu. Amen.

  18. Nanga munthu uvutike ndikusaka chimanga, chikapezeka ukagone kuchigayo chifukwa cha magetsi, kufika kunyumba madzinso kulibe oti uphikile chakudya mipope idauma kalekale. Kuti onjezelanso mavuto pamwamba pa mavuto omwe tilinawo kale. Any way u could wait my friend kudziphako ndiye wangodzilakwila . 25 years ukadali mwana ,kuli bwanji ife tikuthamangila 90years ? Tikudikilabe podziwa kuti tsiku lina mulungu adzatitumizila Mose

  19. Kkkkkk nde akuti anatopa ndi moyo kapena bonya amene akakumane naye ku jehena akamuudze kuti ife nde dziko tikuyenda nalobe or zosakuyenda ndiposa mapazi ake ameneyu

  20. Is he a Europian?Ben Christopher,what is his surname?We din’t need such names to appear on our National ID.We need people to knw their real surnames like Banda,Phiri etc.RIP.

    1. Incase u don’t know,there no such thing called national ID in Malawi yet, currently all you have is only MEC Voters ID, so that make your comment invalid. Thank u Nyirongo.

  21. Ndiye waonjezera mavuto pa mavuto.Umenewo ndi waa ku gahena man.Aliyense ali ndi mavuto koma na size imeneyoyo ndiye siyabho

  22. I think munthuyu chamupha ndi chingwe. A police chingwe chimenechi musachisekerere, chithireni unyolo basi molingana ndi tsamba 170 la malamulo penal code 32. Kuti zingwe zina zitengerepo phunziro!!!

  23. GUYS ANTHU ENA AMADZIPHA OSATI KUFUNA KWAO ENA AMACHITA KUPEPETULIDWA SAMALANI POYANKHULA MAWA ZIKACHITIKIRA ABALE ANU

  24. Chiwanda ndichomwe chamupangisa kuti aziphe and chiwandacho chinayamba akali mwana.Mulungu adzamukatha kothelatu.Anakhuta Napwiri.

  25. apepe poti zomwe zinamutopesa mumoyo mwake ife sitiziziwa..moti tikanakhala ifeso bwezi titatani…ifa imawawa kwa amene amakukonda ngakhale mwini sumazikonda kapena umaziona wachabechabe.

  26. nde wapindulapo chan poziphapo? amalawi vuto likatipeze basi tinathamangila kukazimagilila mmalo mowasova mavutowo ok zagwa zatha napepe

Comments are closed.