Anthu okana kuti kuli Mulungu achita msonkhano, anyadila poti chiwelengelo chawo chikukula

Advertisement
george thindwa

Bungwe la anthu okana ndi okayika kuti kuli Mulungu kunja kuno, la Association of Secular Humanists (ASH), la ku Malawi kuno linachita msonkhano wawo wa pa chaka pachiwelu mu mzinda wa Lilongwe.

Cholinga cha msonkhanowu chinali chofuna kudziwana kuti alipo angati amene akuletsa zoti kuli Mulungu ku Malawi kuno komanso kuchitilatu ndondomeko ya zinthu zomwe akufuna kuchita mu zaka zikubwelazi.

Malingana ndi mmodzi mwa anthu amene amakana kwa m’tu wagalu kuti kuli Mulungu kunja kuno a George Thindwa, bungwe lawo ndi lokondwa kuti tsopano anthu ambiri ayamba kuzindikila kuti kukhulupilila Mulungu ndi kutaya nthawi.

george thindwa
Thindwa adasogolera anthuwa.

“Chiwelengelo chathu chikukula, ndipo iyi ndi nkhani yabwino,” anatero a Thindwa amene ndi munthu otchuka kwambiri pa nkhani yokana kuti kuli Mulungu.

Iwo anaonetsanso kukondwa kawo Kamba koti achinyamata ambiri akuzindikila kuti kuli bwino kusakhulupilila Mulungu, bola kuzikhulupilila mwa umwini okha.

“Pakubwela achinyamata ambiri, iyi ndi nkhani yabwino. Dziko lino likupita kotukuka ndithu ngati achinyamata athu angazindikile kuti kulibe Mulungu,” iwo ananyadila motero.

Bungwe la ASH limalimbikitsa kukhulupilila mwa munthu ndipo limanena kuti dziko silizatha, ufiti kulibe ndiponso nkhani ya Mulungu ndi nthano chabe.

Advertisement

886 Comments

  1. Poti tikudziwa bwinolomwe kuti mulungu mwini ananena kuti asatana azaonekela pamaso paanthu ndiye ndiamenewa wallah pachedwe pasachedwe chilango chamulungu akumana nacho.

  2. Anthu amenewo amafunika ma Bomba atinke nawo aja ndi amenewo chifukwa ndiamene akubweretsa chitsonezo mziko lino ndiamenewo.

  3. I can get anything if I ask it in the name of God even nachipanti from Ndirande was running away if u say “go away satan in the name of Jesus!” U r doing this bcoz God is not lyk a man, he doing things always in tym,tym to warn n the tym to punish n I’m happy with him bcoz he can’t punish a human being b4 he warns.I’m 100% show that u have been in this way of deceiving his pple for a long tym but u r stil alive,u know why? As I said b4 God hv got a tym n I know so many pple hv been warning u for this bcoz its the tym of warnings n if u r not changing next shud b tym of punishment I’m not 100% pure but if u sat down,think properly,pray hard n read the bible{ u r saying that its full of false stories}patiently read it one book after another I’m telling u revelation is going to b given to u .who hv got eyes must read,who hv got ears must hear, this is my last tym to put a comment on this post hv a blessed day bye.

  4. Many Millions Have Suffered Terribly And Lost Their Lives Because Of This Etheistic Way Thinking.Atheists Are At The Forefront Of Efforts To Legitimize Abortion,euthanasia, drug Taking,prostitution, pornography And Promiscuity.

  5. aaaah koseku ndikutengeka ndi kuchindana kunvelera kukoma kwa kuchindana nde kumangobelekana ngati nkhumba kuwonjezera umphawi wa dziko osaziganizira zamawa nde amvekere popeza amalawi ndi ogona chilichose titanene avomelezana nazo ndichifukwa akumawanamiza kuti mulungu kulibe komano pawekha uli mun2 umafumila kuziganizira osati kuphunzisidwa ndikale lija timanamizidwa pano chilichose chinasintha ndichifukwa ana alero obadwa 4days time akuwonelera TV akukhala wochenjera especially obadwira mayiko olemera loools laughing for my poor Malawi country fuck dis

  6. kkkkkkk nsokhano aaaa mamvuto sanakupezeni akazakupezani muzaziwa kuti kuli mulungu king of god panopa bakhalani koma yaaa ndie mumafaso popeza kulibe yawee! lafuso mumafa? ngati mumafa mumati msimuzauka sichoncho inu amene mukusatilanu bwino moto,moto!! samalani abale azanga ananena kale matsiku wosiliza ambiri azakana kuti mulungu aliko koma wochuluka zeedi azasochera ndithu apandie kuiputa phiri ili phee! ndikanakhala ine mulungu ndikanaku wonetsani jahena ndithu

  7. Lisanalengedwe dzikoli mulungu analiko ndipo alipo komanso adzakhalako mpaka muyaya ndiye wina akakhuta mkumati kulibe mulungu ndizomvetsa chisoni paja mdima ukachuluka ndiye kuti kukucha tili mmasiku omaliza yesu akubwela kudzaweluza dzikoli zachisoni kwa nyamata iwe waijoina nkhalambayo ukapsela zaweni iwo adyelera za satanazo tonse tinene amen wamkulu kwa yehova namalengayoooooooooooo!

  8. Bungwe limenelo ndi lazizilu zazikolapasi ndi anthu aja samaziwa kuti akuchokela kuti alipati akupitakuti azakulupilila kuti kuli mulungu chitupicho chikasaziya kupuma place kwa anthu amene tikukulupilila kutikuli mulungu tatiyeni tipitilize kukulupilila pakana malaka limawuti azatichose moyo tili anthu okulupilila ini shallah sallam allaikum wallahamtullah wabalakatuh

  9. Ndiodwala ameneo asamukenso Malawi angatiipisile dziko mwinanso minyama mudzikolathu ikubwera chifukwa cha anthu amenewa

    1. Akamatikulibe mlungu akutathauza chiyani anthuamenewa? Samaonazimene zimachitikakumwamba kuti kumathakuda zuwalikuswamtengo.Amawelengakuselikwa baibulo anthu amenewa.

  10. jas let dose part foolz dey doo knw wat dey r sayin in a nutshell z nt dere fault bt de one who z in dere heart z de one who coz dem to say doz din ….. all wat i can du z to ask almight GOD to forgiv

  11. Kodi iwowa samazifusa kuti zinatheka bwanji kuti apezeke padziko pano okhulupilila iye apitilize ndipo asatope mulungu akudikila nthawi yake nthawi yakusazidi analekeleladi

  12. Kodi iwowa samazifusa kuti zinatheka bwanji kuti apezeke padziko pano okhulupilila iye apitilize ndipo asatope mulungu akudikila nthawi yake nthawi yakusazidi analekeleladi

  13. Munthu chuoyamba azifunse kut, kodi ine ndinalengedwa ndindan? Osati maganizo anu achambao mukakhuta mgaiwa mvekele kt mulungu kulibe eeeeee!! Mulangidwa modzi modzi

  14. Kikikikiki People who think criticise others with facts. Other people in our society are claiming that God does not exits. There is a reason for that in similar way an Adventist claim that wholly Sabbath is satarday not Sunday as others claim. Comments like nzitsiru. Zopusa. Need special prayers. Devils. These comments there nothing one can get. Pipo are saying there is no Devil, No God. Not even evidence for angels. That’s it. No evidence of God. Pipo are not saying those who believe in God arefoolish. No. But human its do not believe in the existentence of God. Why believers are using unbelievable language an an attempt to defend their belief. I wonder. I think religion bring hatred. Why not use constructive ideas to prove that your God does exist. For somebody commented to say my God exist because there are rocks and oceans. That’s a swallow statement to say because oceans and rocks have their line of originality in Geology. Thanks believers as for me there is substance in what these pipo are advancing and am writing my pastor to announce my intention to quit religion.

  15. I am a zambian bt am feal ashame 2 malaw kumamva nkhan yopusa ngt iyi dats y amalawi nkhan yanu ili ma newz pepa kt kumalawi kuli umphawi reazon mumatenga matemmbelelo munjira ngt imeneyi so i cnt coment on dis bkz even de bibo said usatchule zina lamulungu wako pa chabe so ndikuopa nane kutembeleledwa kamba ka coment yanga komanso bibo lomweli limanena kt chtitsiru muntima mwake chimati kulibe mulungu so plz take care othowize muzingotembeleledwabe dziko lanu .

  16. These pipo r crazy they r saying there is no God but now the same people r telling us that they had lunch n drink with there god what do they mean? Why they r not saying publically that they r idol worshippers?

  17. May almighty God reserve special punishment for you people, open your mind and realize that there is God that’s for real, example if I say this fones we are using no one made It made itself are you going to believe me not? u will say am mad right? So if fone can’t make it self then who create you and me? who created moon, Mars, sun haven, earth and many more.? Stop thinking like chickens people hy….

  18. May almighty God forgive them, example if say this fone we are using made itself no one made It do you believe me? the answer is No, then if those fone never made it self then who created haven and earth, moon, Mars, oceans, lakes and many more, people stop thinking like chickens,

    1. Mixing apples and Oranges very archaic thinking. If man a Cell Phone so the world was made by some one ? My food think outside the box you are very limited

  19. GOD IS REAL! Chiuta waliko! Mulungu aliko! believe if you are non-believers.Kwatsala kanthawi pang’ono.GOD IS KNOCKING ON OUR DOORS.

  20. Mukamapanga za u Gay and Lesbian amakuletsani ndi ndani. Asiyeni anthu ndi chiasankho chawo. Kutsata Yesu sakakamiza

  21. Its difficult to understand God bcoz we r not in the same route but don’t b worried we r praying to the one u r saying that is not there to open ur eyes

  22. Liar u r under someone’s control but u don’t know . Don’t worry very soon u wil b delivered and see the light and I’m 100%sure that one day u gonna supprised when people reminding u this

  23. Its just funny that your God is not here to defend himself and you guys have to do it for him. Now tell me, dont this look like men created God and they’re trying so hard to defend a dying idea? RIP Yahweh

  24. Its just funny that your God is not here to defend himself and you guys have to do it for him. Now tell me, dont this look like men created God and they’re tried so hard to defend a dying idea? RIP Yahweh

  25. I like the comments here, if god existed then i can clearly see majority of his followers would’ve qualified to go to hell lol

  26. Ngat amafuna kutchuka adutsa njira yolakwika mulungu si osewera naye

  27. George thindwa u must not punished for this until the Almighty God u r saying that “is not there”show u the right way so that u gonna delivered from the darkness where u r and turn into his servant 2gether with ur colleagues

  28. Pempho langa kwa anthuwa nali ngati munkachita izi ndicholinga choti mutchuke ndikhulupilira zinatheka,panopa chonde vomelezani ndikukhulupilira mwa mwana wache #YESU akufunisisa inu mukapulumuke!

  29. Akuchedwelanji ndi zinthu zopanda pake, pano wanzeru ayang’ane komwe wachokera, nyengo yomwe tili komanso komwe tikupita. Adzadziwa kuti kuli Mulungu, watsala pang’ono mwana wa munthu kubwera chifukwa zonse zinalembedwa mu baibulo zikukwanilitsidwa. Asiyeni azikondwelera choncho, nthawinso ya Nowa anthu anali kudyelera ndi kusangalala Luka 17:26-27. Tiyeni tilape machimo athu tili masiku osiliza. Odala yemwe adzindikila kuti kuli Mulungu.

  30. Hey hey hey plz don’t miss lead people..if ur working under satanimism then do it for yo self ..I bealive n i’ll,don’t talk shit against God..

  31. These are not the last days why do the faithful want to bring unnecessary Panic among the populace embrace the most important virtues of life I.e work hard always try to be innovative strive to get a good education etc

  32. There is an organisation that gives money to those gangs to those sons of snake to speak like that. For we are the followers of jesus lets blow a trumpet of gospel orver this world of evil to let those pple know jesus.may the Loard god forgive them,amen

    1. What Organisation ? Why can’t you not mention the organisation too much superstitions. Let god defend himself not you I heard he is all powerful and all knowing why are you wasting your energy.

    1. Ine ndimaona ngati anthu ngati inu muli pa chilango chosantha as you do not exercise your freethinking capacity. Ever heard of the parable of the Eskimo and a Pries?

    1. And you do not even know the history of the book of Psalms very sad

  33. chimene ndingakukangizeni kwaathu amene simunakumanepo nawo,,,,,ndibwino osamayandikila ndiathu oti zimene amalakhula atha kukungwetsa and ambili mwaiwo anali ma zibusa ena ambili aku univesity……alindifundo zawo zofoila……..at zoti kuli mulungu anachita kunena zungu cholinga athu aziopa kupanga zolakwika aziti akapsya kumoto or zakabadidwe kamuthu amalongosola,,,,,,,ndilibe nawo mau agalu amenewa

  34. Malawians God believers indeed do little thinking. Look at Denie Chitsulo comment and think. If God was real why do you believe in him. If God was fact the issue of believing or having faith in him would not arise as FACTS are not believed. This God of yours is fake, Jewish myth brought by Azungu and does not make sense to people who think. Thats is why all thinking people have let go of this God belief- go to Sweden, Denmark, Norway- there is no God believing there and they are doing great in all indicators. Come to Malawi, the poorest of the poor. I think your God likes you to be poor! Anyway the God concept appears very appealing to poor people in that it promises goodies in heaven. and where is heaven? nobody knows but believe. Kaya zanu zamabilife izo. Mukupusa nazo!

  35. Let us say you are right and I give you 50% there is no God, you die and I die that is the end nobody has lost anything. I take my 50% that there is God, we both die and Jesus comes we resurrect and realise there has been God all along, I inherit eternal life and you lose everything. Which is a better option? Live like there is no God or live like there is God?

    1. i love your thinking sir, if regretting in this life is painful and we live with the pain till we die what more regretting on Judgment day? I would rather die a fool believing in God that to die trying to be a wise man with no hope. I have my hope in Christ Jesus and i will always do. Assumimg God did not make man then who made man? Because it bothera me how a man functions, just think about it how you sleep and wake up….is it not wonderful? I believe in God

  36. Psalms is number one fool including all of you who say chitsiru says there is no go. Because the heart does not say anything. the job of the heart is to pump blood. Pitani ku biology class. you need help!

    1. Like for real for 2000thousand years i didn’t see one coming in front and claim here is the evidence of gold or god and no facts at all.. Just threatssss!!!

  37. Munthu ukamafa amayamba kugontha ndi makutu komanso maso ndiye tawasiyeni ndalama zomwe akulandilazo ndi yemwe akuwatumayo kuti azinyoza mulungu azawasesera limozi

    1. Do you know where Gehenna is ? Zinazi mumangonena chifukwa ndinu mbuli.

    1. If indeed god existed, as powerful as you guys make him appear, would you really have to waste your time to defend him. Iyeyo osangobwela ndikuzichita defend bwanji ? Madness imayamba chinchi.

  38. Ola asakhulupire zero Namalenga alipo iye wapamwambayo Ali Nazo zambiri zolengedwa zomwe Zuma my lamb it a moga nyama mitengo miyala Angelo nyenyezi. I think akudya madrug too much

  39. OSALIMBANA NAWO AZAFA CHIIMIRE, KOMA NDITHU MUNTHU WABWINOBWINO WOTI UBONGO WAKE UKUYENDA NDIPO AKUPUMA AZIKATI KULIBE MULUNGU? AYI AMBUYE AZITIKHULULUKIRA

  40. Munthu Ndi Gagu olo utampaxila mbale amakhutulira pansi,mulungu anakupaxa moyo woti adzimtamanda nawo lero akumunyoza ambuye muwakhulukile popeza sakudziwa chomwe akuchita,onse akunena kulibe God talangeni akudziweni,

  41. Ndlbe mphanvu yokupanglan judge mulungu ndye azwa zonse.muzandkira bwno pasogolo mutapeza vuto lofuna nawo mulungu lero mukudya kumakhuta zanu zlbwno.

  42. Anthu ofunika kuotchedwa aja ndiamenewa anthu omvetsa chisoni

  43. Anthu akulu owoneka ngati oganiza bwino koma ali opanda mzeru ndi omwe angamasangalale kuti akuchuluka mu chipembedzo cha Paganism-chi.Maphunziro ndi Uzimu ndi zinthu ziwiri zosiyana.Anthu ambiri amaona ngati akaphunzira kwambiri school ya pa dziko lapansi ndiye kuti akahalanso madolo odziwa kwambiri nkhani ya uzimu.There is not theory in whatever one can learn in school about the existence of God.Ngati mumaona ngati mapepala anuwo akhoza kukuuzani za Mulungu mungotaya nthawi.Nyadirani poti ma Pagan mukuchulukadi.This is one of the group of Satanic Worship.Owerenga khala maso.

  44. ku blantyre nanga? ine ndi okayikila,chifukwa zoziwa zanga ndi zopelewela,koma okanawa ndi ovomela ndi ngakonde kumva zomwe zimiwo limitsa mtima kuti iwo ndiye wolondola, CHONDE TIZAKUMANE TONSE AMAGANIZO OSIYANA TIZA CHEZE,MWINA TITA MVETSETSANA,TIKHOZA KUYIKA MITU PAMOZI NKUPINDULA MUNJILA INA YAKE…

  45. Chitsiru Chimenecho Molingani ndi baibulo.God is real,you are experiencing him because you are not seeking his power.Chitsilu Chimenecho.

  46. Unless you tell me that the history of moses, Jesus and Muhammad doesn’t exist then wana believe you. But if the history of these great men of God is there then be assured that God is there 100%

    1. History may exists but distorted, the problem when you have marginal level of knowledge everything you are taught by preachers who have not even gone to theological schools or have been panel beaten by church dogmas all you get is junk and one cannot exercise own wits because you there is none. Most of the contributions have been done by men. Irenaeus asserted that four Gospels, Matthew, Mark, Luke, and John, were canonical scripture while there was already Marcion’s edited version of the Gospel of Luke, which Marcion asserted was the one and only true gospel. Already here you can sdee confusion which most believers cannot see and appreciate. Its sad that the most poor countries are wasting time with these things.

    2. Burden of proof is on you who say Jesus did exist, you prove it but then again you can always read ’10 Beautiful Lies About Jesus by David Fitzgerald’ that should clarify few things for you. Osapanga ulesi yanu ija a khristu welengani bukuli musanapange phuma apa!

    3. Tru fix the history of Jesus and Muhammad is clearly indicated in our history books. I can’t refer you to the bubble or Quran but purely secular history clearly stipulate the existence of Jesus and Muhammad. Remember Jesus was there when octavius Caesar was ruling and do not forget there was a powerful ottoman empire that existed after the death of Muhammad and it enhanced the Islamic rule

  47. Satan in action,where do they think they are from if there is no mighty God?God have mercy on them so that they should come to realize that there is NO ONE like YOU

  48. Ngat akukana kut Mulungu aliko nde Satana aliko? Mundifunsireko anthuni.. Fact- anthuwo akumukana atakura kale nde zili ngat kukana kumene anachokera, poti ndionenepa #Shame!

  49. Let them believe what they’re coz kut mpaka akafike saiz yomweyo kunena kut mulungu kulibe.Who told them about such stupid!! They are as of age,sine oweruza kuopa kuweruzidwa.zonse atate akuziona ndipo akuzinva.Ameeen!!!!!

    1. noun 1. an outlook or system of thought attaching prime importance to human rather than divine or supernatural matters. Humanismis a philosophicaland ethicalstance that emphasizes the value and agencyof human beings, individually and collectively, and generally prefers critical thinkingand evidence ( rationalism, empiricism) over acceptance of dogma or superstition.

  50. Nkhan yabwno kwambir pa chikhulupiliro chawo koman akadayamba aganizira kt iwo asanabadwe anali alikut?, kod mbiri ya Fir’awn (Falawo) iwo sadaimve? Koma ngat chili chuma tisafike ponyoza nacho Mulungu. Asiyen azadziwa posachedwapa.Satana wayala midzu mwa iwo ife tisalimbane nawo amenewa chftkwa amene Mulungu wamuongola palibe yemwe angamusocheletse ndpo amene Mulungu wamusocheletsa palibe yemwe angamuongole.Mulumguakudalitsen nonse amene mwakhulupilira mwa Mulungu ndi tsiku lomalidza.

  51. Mmmmmmm! amene akunena zoti kulibe mulungu chonde msamuwelengere pagulu la anthu, kma ndiwakufa ameneyo!!!! Ndpo anamulenga iye ndindani?? mwna wusatanic wawazunguza bongo!!!!

    1. Grace Rhemah Rehema lack of knowledge or more knowledgeable. I’ve read the Bible back to front, I advise you do the same. The Bible has been edited, translated several times and this has been proven several times as well. No original document can be found. Half the authors are unknown and you expect me to believe it’s the word of God just because the Bible itself says so?

    2. Grace Rhemah Rehema Even if he did exist, certainly a god I’d have trouble worshiping. The Bible condones slavery, it marginalizes women, it’s factually incorrect, it shows god as a serial mass murder, it promotes discrimination, the Ten Commandments sound like they came from a child. Plus there are more than 2500 religions on earth. Are you telling me we are all damned to hell.

      1. Rehemma needs to go back to school. She heavily brainwashed. The few years Malawians have subjected to Christianity they think they are saved if you believe your God exists please go to southern Sudan visit Juba and come here to preach to us that God exists. Knowledge is power do waste time talking Religious Crap when evidence is there.

  52. Zikanaveka bwino mukanati “Anthu amisala koma Ovala komanso Osagenda” Achititsa msonkhano….awa ndiye Angelo eni eni s Lucifer omuimilira kunja kuno tsono ena they are just victims. ..

  53. chiwerengero chawo chachuluka kufika pati? Sakutiuza. i think akuchepa thats why amapanga msonkhano kuti awone kuti asala angati

  54. Genesis 2:7 And the LORD God formed man [of] the dust of the ground, and breathed into his nostrils the breath of life; and man became a living sou….From this script. let me know the one who create them ..????sinanga akuti kukibe mulungu.?

    1. indeed that is foolish .. I speak holy gohst fire upon them …let them realize that there is God ….May he teach them a great lesson

  55. Mulungu akamapanda kutilanga, sizimatanthauza kuti akukondwera ndizimene timachita. chikondi chake always gives us a chance to make a second choice of coming to him. however, sizokakamiza izi

  56. Anthu amenewa ndimawona ngati ndi ziwanda zimene zimakhala zikuwalamulira nchifukwa chake amachita kuyima pa chulu mkumanena zot mulungu kulibe sikut sazazindikira,,azazindikira kulakwa kwawo koma nkhwangwa ili m’mutu

  57. Nanunso Ukokoshera Nkhani Bwanji? Nkhan Zanu Mumaika English Tsopano Apa Mwaganiza Zoika Chichewa Bwanji Buku Loera Likuti Nthaw Yotsiriza Anthu Azidzawerenga Ndipo Makutu Awo Azidzava Kuti Kuli Mulungu Koma Sadzazigwilitsira Ntchito

  58. Sizachilendo mmasiku a Nowah analipo anthu ambiri kuposa amenewa koma chigumula chinachitika , abakana koma ife tikudziwa kuti Chauta alipo ndipo ndiwamphamvu

  59. malemba ananena kale kuti masiku otsiliza kuzachitika zambili matenda,nkhondo,njala bible said musakayike nthawi yasala pang,ono. tingowapemphelela Mulungu awankhululikile ,awapase nzelu zawuzimu ndi maso kuti awone.

    1. Njala nthenda nkhondo zinaliko even b4 great great great agogo Ako asanabadwe! Sign of ulesi, kusiyana maganizo, ndizotelozo basi

  60. Aroma 1: 20,21
    Chilengedwere dziko kupita m’tsogolo, makhalidwe a Mulungu osaoneka ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa, ngakhalenso mphamvu zake zosatha ndiponso Umulungu wake, zikuonekera m’zinthu zimene anapanga moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.

  61. Ndi ana Anjoka awa,bambo wawo ndi Satana,kuti muwafufuze mupeza kuti ndi achuma chosaneneka koma mukati mufufuze kuti anachipeza bwanji musochera kapena kuti mukhumudwa,anthu wa ndi ma member a Illuminant group,omwe uli ndi anthu otchuka I means ma President,ministers,pastors and more famous business men around the world,cholinga chawo kuti inuyo mukomedwe nalo dziko,zoti Mwana wa Mulungu akudza inuyo muyiwale,mavuto onsewa ndizochita kukonza ma plan anapaanga kale nkusauka kwanuko muvomera zinthu zomwe musakudziwa pamene mudzadzidzimuke kufika mwakuzindikira idzakhala too late chifukwa mudzakhalaa mutatsimikiza zoti mulungu kulibe,ndipamene iye adzafike ,Bible linakamba kale lomwe kuti masiku omalizaa adzafika aneneri onyenga,komanso zoyipazo zikuyenera kuti zidze koma tsoka iye adza nazo,Bible linakamba za izi,so my question is;ngati bible linanena za kubadwa kwake kwa yesu amene ali mwini mphamvu,chifukwa mukawerenga bwino mudzamva zoti palibe munthu angaze kwa atate osadzera mwa iye,iye ndiye kuwunika kwa dziko lapansi,tsono ngati mau anaanena zoti iye adzazuzika nkuphedwa,ndipo iye mwini amawawuza ophunzirayo za izi ndipo zinachitikadi,ndiye mukuganiza kuti zachimaliziro cha dziko ili chiyiwalidwa???!Anthu onsewo akutsutsa za umulunguwo,aakudziwa bwino za iye ndipo mphoto zaa zintchito zawozo akudziwa kale,kumbukani kuti satana yo poyambapo anali ngelo koma chifukwa cha zichito zake anatsitsidwako,ali pano kuchimwitsa ambiri.Anthu dziwani nyengo ndi nthawi yomwe muli,mau a Mulungu sadzapita pachabe,samalani m’machitidwe anu.

  62. koma anthu amenewa akuti anachokera kuti?sikukhuta kumeneku kapena amasuta chamba.moyo akupumawo akuti ndiwawo?inetu sindikufuna kuchimwa mwamva anthu inu komanso musapangitse kuti anthu achimwe kamba kowawidwa mitima ndizolankhula zanuzi.cholinga mukakhale nonse kujahena ayi.ngati kulibe mulungu abale anu anafa aja alikuti?mukalambe bwino osati muwachimwitse anthu.ngati mukutero olo kupemphera mumapemphera inuyo?ine ndikuti mulungu akulangeni inuyo kuti mumudziwe amene mukuti kulibeyo.mwakhuta kondowole eti?

  63. paja chitsilu chimati kumwamba kulibe mulungu. Uwu ndimpingo wasatanic, asiyeni akubwera mwini chilengedwe adzawakantha mopanda chisoni akawufusa makosana akusodomu.

  64. athu amenewa ngamisala musawavele amalawi akusocheletsani zimenezi zandikwiitsa kwambir munthu onyoza mulungu ali nditsoka kwambiri komaso ndifiti zimenezi zidzalangidwa ndithu zimenezi

  65. Umbuli choyamba~ azungu kale zaka za -jon chilebwe adabwelaku malawi ndi baible nkumati kumwamba kuli mulugu amauzamakolo athu ;(kalelo abwelaso momuja akuti kumwambakujaso kulibe mulugu maziDala amasikuano akuti ndizona ana ife kukhwefula trauz akuti amwano bola ife kuchitira mwano makolo osati mulugu M’menewakulila Dalayu aziti kulibemulugu ndizoona wamwano ndindani,,,,,,,,,,,,,,,,awasibabo anga sanga ndilagize ine

  66. Arise O Lord for them to see your mighty power, why they are playing with you AlMighty God? let them know that you created everything may you create a stuation to let them fear you my God in the mighty name of Jesus.

    1. I like this comment alot…it is a request to the supposed Lord to show their self to mankind. Good one, as an Atheist I know this won’t happen but for sport sake ‘lets wait’

  67. Ndipo panopa tilidi mmatsiku otsiriza,owerenga khala maso.ndipo pano pakufunika tiziwerenga baibulo la king james,mabaibulo asopanowa anthu awa alitembenuza,zoona munthu nkumati kulibe Mulungu?last days,ine ndi apa banja panga tizatumikira Mulungu.wamoyo.

  68. Ndikupempha kwa mulungu kt gulu limenelo aliononge basi” inde ineyo mulungu ndimamulakwila koma awawa awonjeza@ kunali falawo, hamana amazincha kut ndi mulungu lelo alikut ol mtembo wafalawo panopa ulipo sunaole ai ,ichi ndichilango chamulungu” chosecho kunali kut anthu aziwe kut kulimulunga chitsanzo

    1. Ma eguputo amapanga embalm matupi amafalawo kut asaole mwachangu, linali dala, sichilango ayi hehe, now ndikukafufuzaso ngat nkhan yakoyi ili yoona ndipo!

    2. Ok ukaone bwino ndiponso mofatsa” nanga bwanji mtembo wafalawo amati akaukwilila dothi limam’beza pamwamba, akasonkha moto silimapsa mpaka anakaliponya m’madzi, komaso madzi ndikum’bwezela kumtunda chinali chiyani? Mulungu kuonetsa kwiyo kwakapolo ake omukanila iyeee.

  69. Nthawi yake bas palibe zachilendo kutengela bible zinalembedwa kale kut nthawi yotsiliza tizaona zoteli tsoka kwa iye okwanilitsa lemba abale be care ndinyengo imene tili

  70. Musadabwe anthuni,,poti masiku anowa ndi omwe adanena yesu,kuti kuzatele masiku osiliza,,nanga akukana moyo omwe ali nawo ukuchokela kwa ndani? Kwa inu mufuna kuziwa zambili muwelenge,,,aloma 1,,,buku limelo muva zose,,masalimo52,,

  71. Mulungu aliko tisamanamizane.tamvani kankhani aka:mnyamata wina woyerekedwa atagula 4n yovutirapo anazafatsa ali ‘ndikufuna ndi zoomle ndione pomwe pali Mulungu’ atangomaliza kukamba zmenez 4n inathma samespot ndpo inapoila 4gud! panopa analapa.ndye kaya ndikukhuta muzingokhala basi

  72. Zitsiru Zimati Kumwamba Kulibea Mulungu,,inunso Inu Amalawi 24 Muziwona Zolemba Pagulu Osati Ndizopusa Zomwe Ngat Zimenezi,timakunyadirani Koma Mwalembazi Sindingakusapoteni,umenewo Unali Msonkhano Wazitsiru Kubwera Poyera,tsono Inu Nkumalemba Zazitsiruzo??

    1. Iwe Thindwa Iweyo Nde Ukukhulupilira Zopanda Umboni,kudzipangitsa Wekha Kukhala Chitsiru,,ngati Ulindiumboni Bwera Poyera Ndikutsukuluze,inenso Ndikupatse Wanga Umboni,

    2. Thindwa Muzingolimbana Ndizaufiti Zomwezi Basi,osat Izi Mwayambazi,mukulimbana Ndi Wamkulu Amene Adalenga Satana Akukutumaniyo,sindingapikisane Nawenso Ayi Chifukwa Alimwayine Yesu Khristu Ndiwamkulu Koposa Ndipo Alibe Wopikisana Naye

  73. Mulungu mmodzi yekha aziwakhululukira, maso ndi makutu ali nawo mdima wakuta olo kunganima kutawalila bwanji sangawone komanso zangamve….Alemekezeke amene amene analenga dziko lapansi ndi kumwamba

  74. Mukakutha m’gayiwa ndine kupwesa kwache musitsatira zotuma satana amene akukusokonyezani kuti musiyambitsa magulu ophuza ngati amenewo.mowona zakazake ndizino mulungu akulangani kuchokela padziko lapansi mpaka kumwamba.Anthu osauka ngati inu.

  75. Ngati Mkulu Wako Satana,demon,devil,lucifer Amati Kuli Mulungu,nde Iweyo Wabadwa Liti?Ngati Sukudziwa Nkulu Wakoyo Satanayo Akufuna Kungokugwilitsa Ntchito/akupepeletse Kenako Ku {hell}azakukana,eish Iwe Ndiwe Omvetsa Chisoni,ukudziwa Chomwe Ukupanga Koma Dala,banja Lako Litha Kupita Ku Moto Coz OF U Stupid What U Call So Called Father,ngati Kulibe Mulungu Kuli Ndani?Satana Wakoyo?U R Very Stupid Old Man,look At Ur Self,ana Ako Ndinkazi Wako Akakuona Amati Ndiwe Bambo Kapena Agent Wa Lucifer,eee Anthu Enanu.Anzako Ochimwa Amati Kuli Mulungu Koma Iwe Nde Waonjeza,

  76. just look at fresh air we breathe the ants mosquitoes the lizards in your house and say there is no God thus being Stupid he is creator of everything Sataniyi akupusitsani

    1. seems alot of these comments are from the uneducated, the reasoning here is ridiculous

  77. Chithinda icho ntchifwiti, chikusambizga ba bawene kuuluka mu chihengo. Very stupid fool.

  78. Chinachitika ndichani kuti munene zimenezo! Mulungu alipo Inu abaleathu aku Lilongwe.zonsezimene mbuye Yesu ananena zikuchitika pazikopano! Ambuye Yesu akubwela mawa

  79. I dont have to waist my time saying of such stuped people I wish they must remain like that til the great day when our and their and everyone elses eyes will see Him coming with His glory.

    1. at Tru Fix, the way u hv reacted, the bible already writen that God will every one to remember what was told abt the heavens.

  80. akapsa ndi mano omwe amenewa ngati ndichamba chikuwapangitsa zimenezichi angosiya kusutako dziko limene akukhalali analenga mndani ine mkanakhala mulungu ngulu limeneli ndikanakalitaya mnyaja somba zikawadye

  81. Aliyense amayoyoka wa mulungu ndi osakhulupirira chimodzimodzi amulunguo milandu tolo ufiti uhule kupondereza kuba ngati mulungu alipo azaweruza yekha

  82. ..zilibwino bakanani kuti kulibe YEHOVA..ife ana ake a Mulungu kumangodyadira Mlengi wanthu Namalenga..mwini chilengedwe..inu ndi satan wanuyo bakhalani. komaso ndie bwino ku Paradise tingakadzadzeko, tingamakathinane..chisankho cha bwino ana anjoka inu.

  83. A Satanic amenewo mxieee… God show them that there’s no-one above you strike them with heavy thunder so that they should come and testify about your greatness

  84. Baible Limanena Mosabisa Kuti : Chitsilu Chimanena Kuti Kulibe Mulungu ! Ndiye Kunsonkhanoko Kunasonkhana Zitsilu Dzokhadzokha .

  85. Anthu ena adavomeleza kugwiritsidwa ntchito ndi satana ndie sibwino kumakhala bize ndi anthu amenewa. Akadzaziona adzatsimikiza kuti MULUNGU Alipodi.

  86. Ife tiza khulupilila mwa ambuye thawi zose ndi ma siku wose ndipo tiza mugwadila pano pasi ndi ku mwamba sitiza vela wosa khulupilila awo koma ise tizakhupilila mwa ambuye alipo ndipo azakhabe mupaka kale

  87. My bible on yobu 12 v7 says, but nw ask the beasts and they wil teach u and the birds of the air and they wil tel u and fish of the sea wil explain to u, who among all these does not knw that the hand of the LORD has done this, nzanja mwache muli mpweya wa zamoyo zonse ndi nzimu wa zamoyo zonse, RESPECT GOD

    1. Birds don’t have vocal cords my friend unayesa kuifunsa mbalame simayakhatu bwana! bwana wanga nsomba siingakuuzeni

  88. Enaso bambo kumalawi konko amatukwana mulungu ndikumati kumwamba kulibe mulungu.mvula itavuta atanyoza bamboyu mmawa mwake kunagwa chimvula chimene sichinagwe pa minda yake yokha chimvula chadziko lonse koma minda yake yokha posagwa mvula ndipo tsikulimenelo anapita kukapemphela ku church kukalapa ndikupempha chikhululuko kwa Mulungu.pano ndimunthu mmodzi olimbikila kupemphela

  89. Joswa 24 :14 Ngati Kutumikila Yehova Kukuipilani Muzisankhire Mulungu Kaya Wa Aamoori, Wa Baala Kaya Wa Igupto Koma Ine Ndi Banja Langa Tidzapitlizabe Kutumikila Yehova Wa Makamu & Am Proud To Be One Fo Jehovah’s Witiness For Ever

  90. Panali madala ena ake amkakanila kuti kumwamba kuli Mulungu,amkanyoza ngati mvula yavuta.tsikulina anapita kumunda kwawo anapeza chimanga chawo chonse chitawotchedwa chowotcha chosadziwika munda wawo wokha koma panali minda yoyandikananawo sanasye.Kumundaku analila ndikutukwana,,atakafika kunyumba anagona usiku nyumba yawo inangwa anali ndi ana awili ndimkazi anangofa iwowo ana ndi mkazi alipo.Mulungu siwosewela naye guys tiyeni tisewele ndizina not God

  91. Plz dont ever post this nonsense here.anthu ndi akanyimbi who they think they are?where they came from?who created them? Munthu ukakhuta usamasewele ndi mulungu,chilango azalandile azachisiya

  92. Yaaaaa zoona inu mungamasangalare kuti chiwerengero chanu chikukula ,,zoona inu inu,,ayi ndithu dikilani nthawi ya chiweruzo chifike ndinu ndani kuti mukati kulibe mulungu,,pitilizani poti inu mukungokwanilisa zolembedwa mu bukhu lopatulika dziwanisoni kuti mwangoyamba azikulu akulu anu akubwera muchulukanadi,,Ndingopempha mulungu kuti atipatse mzimu wachidziwitso komaso maso auzimu kuti tikhazikike mu mawu ake,,ooooh God

  93. Sunganene kuti palibe chinthu chomwe suchidziwa. Ngati ungati ku Lilomgwe kulibe nyanja zikutanthauza kuti nyanja umaidziwa. Anthu amenewa mwa iwo muli idea ya Mulungu koma angokhala amtudzu nde mwini kuweluza adziwa chiweruzo chowayenera.

  94. Paja Amat Mmayamba Nd Mkhutu Kugontha,ndikuwona Ngat Anthuwa Umunthu Alibe Coz Iwowa Amaganiza Kt Anabadwa Mumchifanizo Chandan

  95. Bible limati kwa yense nonnena kuti kulibe mulungu ameneyo ndichisilu chifukwa umboni onse oti kuli mulungu uliko, angakhale chilengedwe chimaziwa kut kuli mulungu hw more munthu

  96. Chitsilu chimati Kulibe Mulungu…… koma ife Tikuti Mulungu Alipo ndipo Yesu christu. ndi Mpulumutsi wanga….ndipo or mutachuluka bwanji. or nditasala ndekha sindingamvere zanuzo… ndipo mkwabwino kumwarira koma ndikukhulupirira Mulungu. kusiyana ndikumwalira mkukapeza Mulungu alipo nzoopsya kwambiri kuyakhula mopanda nzeru ngati zimenezi…MULUNGU.. NDIWAMKULU!!!!!!!!!!

  97. Aaaaa kutelo ndikulakwa iyo anachokela kuti? Ndipo anapezeka bwanji paziko lapansilino? Ndiphazu yasatana ndiyemwe akuwanyenga komano ayenela kuziwa kut mulungu alipo

  98. The power of the wicked is to take Malawi on his hand. Christians,let’s unite in prayers to overcome the wicked one. Its nothing but the ending times. Tikhale maso a Khristu.

  99. Ndikupempha Mulungu mwini chilengedwe chonse amene analipo alipo ndipo adzakhalapo(wamuyaya) kuti chonde anthu amene akunena kuti Mulungu kulibe modzogozedza ndi uyu akuti Thindwa kuti awakhaulitse ndipo imfa yawo adzafe yowawa Chonde Mulungu wanga wamoyo mfumu ya mafumu wonetselani ukulu wanu kwa anthu wokanilawa ngati m’mene munapangila ndi pharao pamodzi ndi anthu ake chonde apangeni zowopsya

  100. panali munthuwinawake munthawi yamtumiki muhammad ((mtendele komaso madalitso amulungu zimfikile iye)) amene amachita mwano komaso makani ndimulungu kufikila pomwe vesi ((ayah))inatsika kuchokela kwamulungu lomufusa kuti; kodi iweyo madzi atani asowa ukhoza kuwatenga kuti? ndipo ndimwanowakewo adayankha kuti: tikhoza kugwilitsantchito makasu kapena Mapiki kukumba;;ndipo atangoyankha wamwano chonchi adangozindikila madzi ammasomwake awuma ,choncho adakhalawakhungu moyowakeonse “””ndipo anthuamenewa sadzamwalila mazuzoamulungu asadawalawe!!!

  101. Chonde,chonde abare ANGA,anthu awa akfuna atisocheretse,koma tiyeni tizieapempherera kt azaone ukulu wa mulungu kuti oipayo azachite manyazi

    1. mulungu anallipo pa meeting yathu. anadya nafe lunch. and ananena pa meeting kuti wokhulupirira iye osamuwona ndinu a galu!

    2. mulungu anallipo pa meeting yathu. anadya nafe lunch. and ananena pa meeting kuti wokhulupirira iye osamuwona ndinu a galu!

  102. why mchitidwe oipawu mukuulengezetsa malo mongousiya???? timadziwa ndithu kut choipa chimakhala pamwamba kuposa chabwino nde izizi kwa ife ndizopanda ntchito lembani nkhani yina

  103. Moto onyeketsa ugwere iwo…Namalenga adzawayatsa…chitsilu chimati mu ntima mwake kulibe Mulungu…koma ine ndizakhulupila mpaka kale kuti kuli Mulungu Jehova wazisomo…

  104. Ukamufunxe satana kuti anachoka kuti? Akakuwuza kumwamba NDE iwe uziti kuribe mulungu nkhani imeneyo Ireke kamba ina

  105. Becareful gyz musamayese anthu inu mwamva et. Mudzasowatu. Mpakana kunena kut kulibe mulungu. Kufuna kutchuka chani. Koma mupeze potchukira mwamva za mulunguzi sizotchukira samalani

  106. Mudzakhala pachilango choopsa tsiku lachiweluzo komaso tsiku lakufa ndi zomwe mumalakhula mukakhutazo zoti mulungu kulibe

  107. Eee koma zoopsa ndithu,Mulungu kulibe? Chokhacho chokaikira kuti Mulungu kulibecho zikutanthauza kuti Alipo, Idzawafikira nthawi ndipo chilipo chomwe chidzawapangitse kuankhula okha ndipakamwa pawo kuti zoonadi Mulungu alipo.

  108. Nkhani Yaipa, Haaa Nikumati Kulibe Mulungu? Nowa Anapulumuka Cifukwa Ca YEHOVA Loti Anapulumuka Cifukwa Ca YEHOVA Daniyeli Munzenje Lamkango, Nanga Kod Ndani Yemwe Anausa Yesu Kristu? Mwaci Onekele Tmat Ndi YEHOVA, Oh Nditha Kukumbuka Bwnobwino Paja Malemba Amat {m,masiku Osiliza Kuzakala Okana Kristu} Tawaonad Nanga Siawa.

  109. I question the reasoning of these people who say there is no GOD,ibelieve something that doesn’t exist can not be known even by name,the fact that we mentioned the name GOD that shows HE exisist

    1. But Harry Potter, Ironman, wolverine, etc are all very well well known, so does that mean they exist too

  110. Nthawi zina kuputa zithu zakumwamba ndikumanena kuti mulungu kulibe ndimavuto akulu.Chonde maphunziro sizifanana ndi mulungu, mudzafa imfa yowawa

  111. Masiku Osiliza Anthu Azakhala Ozikonda Okha Onyoza Akudyelekeza Asiyeni Mulungu Adzawalanga Aheberi 9 Ves 27 Kwaikika Kwamunthu Kufa Kamodzi Kenako Chiweluziro

  112. Psalms, 53:1 – ” The fools says in their hearts, “There is no God.” They are corrupt, and have done abominable iniquity. There is no one who does good.

    1. Am more educated than you and I know alot but I can’t join your satanic religion….I believe in Jesus ,the holy spirit and the father and you can’t change it.

    2. Any educated person would know snakes don’t have Vocal cords, the idea of someone sacrificing themselves to themselves is ridiculous, the earth was never floded, that there is no proof that Jesus ever existed if your a Christian assuming, that the idea of an omnipotent omniscient God is faulty zambili bwana and you cannot prove that God blessed you ukanangokhala sukanalemela iwe! munagela Kwambili Chan accounting nde how does that make you a better thinker wider reader et kuli anthu much richer than you and sapemphela

    3. Another Lucifers agent ……but you can’t change me .Am a Christian for good…..and I will continue serving the living God….do you know? …his name is Yahweh. …

  113. All i know is every living things are pressing a living God. Then to carry the story short you are not living people your eyes will be open when trouble has strike on you is when you will call God sorry man i feel about you.

  114. In the name if Jesus i pray for them so that they receive the Holly sprit and fill its power in them one by one. I pray for them to be the preachers of the kingdom of God, i pray for them so that God may use them as He did with Paul.I pray for them not to die b4 they know Him. In the name of jesus i pray and shall pray

    1. This is far the best prayer from a Christian so far, Ena akupemphela kuti mulungu aakhile onse osakhulupilila, kudos mayne you’re a progressive Christian!

  115. i refuse to be a fool.my mighty God,tje creator of the whole universe exists and he knew u evem b4 u were concieved im yo mums woumb jelemiah 1:4-5.Behold even the hairs on yo head are numbered..yo money is never an excuse for escaping his mighty hand…

    1. Zomwe mulungu amapanga it’s not what human mind thinks…..zikanakhala mphavu zamunthu bwezi mikango itapha nyama zambiri mu chombo,koma chifukwa zinali mphavu za Mulungu nchifukwa chake nyama iliyonse inali yotetezedwa….

  116. Misala, MChimodzi-Modz Nyerere Yomwe Ili Pa Bread Ikudya, Nkumati, ” Ndikukayika Ngat Ku Dziko Kuno Kuli Compony Yopanga Bread”

  117. Let them enjoy on earth but they will cry in heaven. If u want join them. Am proud to be a christian becoz my rewards for my suffering is in heavens.

  118. Muzaona zomwe adaona anthu a m’bado wa Noah ngati muchita muchita chibwana,,, do you know that God is silent deliberately,, time will come when you will need his mighty attention,,, I know that behind you money lie,, but remember gold and silver are his’,,If there is no God do you think Michel Jackson would want to repent? Why was he willing to cast out his evil deeds to God?,,,

    1. michael jackson repented???? u guys need to get ur facts ryt….stop defending ur god with lies, u only make us assume tht ur god is also a lie

    2. Where do you get such Micheal Jackson nonsense Evangelist ? God is silent deliberately nonsense Evangelist? Aah you are deceiving people iwe Evangelist!

    3. Bwana Felex follow what you believe,, but if you can have time try to study the bible not reading because in reading you will get nothing,,, from that you will find the truth that will set you free,,,

  119. Olo atachulula ngati nthawi ya Daniel.Iwe gwilitsitsa chomwe ulinacho munthawi yoyenelera adzadziwa mulungu wa moyo.Daniel anapilira ndipo anaima pachoonadi

  120. Ambuye kukhululuka ndikhalidwe lanu,munakhululukira mbala ija pamtanda paja,chitani chimodzimodzi ndi anthu amenewa ndipo kuti akudziweni,palibe chokukanikani.

  121. Kuyambila lero osaza gwilaso osuta ndi kugulisachamba mukuvomereza zigawengazo kupanga nsonkhano wawo kuma tsekera osuta chamba

  122. Ikudza nthawi imene anthu adzatukwana mulungu ndikusokeretsa akhristu ofoka kuti kulibe mulungu awa ndi masiku omalizadi ndiye muwauze kuti ine ndi amnyumba mwanga tidzatumikila mulungu abatengeka ndi satana wawoyo

  123. Maonekedwe okha kuonetsa kuti zachikunjadi izi.otere amakhala nthawi yayitali osafa.kuti asokoneze anthu ofana ndi Iwo.(chicken brains).

  124. Eish kdi khunyu kpna kamwazi? mwina sakudziwadi kathu amenewa, ekisodo 20 vs 1 mpaka 5 akut ine ndine mulungu wa sanje wakulanga ana kamba ka makolo awo, ndkukhulupila kt anthu amenewa anasokelesa kale ana ao!! kuwapweteketsa ana osadziwa kathu, pepani tingoti mulungu akudalitseni mudzina la yesu, mulungu anati ndimadikila mau anga ndikwa chita. ine ndingo moto onyeketsa ulinanu pafupi!! aheberi 28vs12 ine ndine moto onyeketsa! AMEN

  125. Thawi zina muthu sudziwa kuti uli pantendere mu thawi ya mtendere komano mtenderewo ukakuchokera mpamene umazindikira bwino amzathuwa phavu ya mulungu samaiona kamba koti palibe chowaonetsa kuti kuli mulungu. Akakumana nazo mpamene azadziwe kuti kuli kuli mulungu poti amati pathawi yakusadziwa Yehova analekerera ali mu thawi yakusadziwa amenewo.

    1. anthu amakumana nazo asanalakwe…..anthu osapemphelawo ndikumatukuka chifukwa akupanga zozithandiza….muchedwa mukamadikila kuti ena avutike ndiye chikhristucho chili pati pamenepo????

    2. Hehehe bwanj man Fatsa, Janet akupeleka sense koma sukumuyankha bwanji? Kapena nawenso waiona sense et?

    3. Janet u r right we r having blackout everyday n pple r busy praying or blaming each other instead of finding solutions eish malawi @52

    4. Ella’ where is Janet who is complaining about electricity? This malawi eish up to when this will go on. This makes me to stay here for another year. Road shedding everyday”””’ its worse now

  126. Humanists are free lancers pursuing their course with free mind. Religious people are held by the chain of their religion so they disguise themselves under the silhouette of religion yet they are mostly liars good fools. They are not trustworthy because they aren’t committed to the course they pursue. They rarely succeed. In fact they live and enjoy in the land of humanists yet demur to be called such.

    1. Take the example of christians, no christian lives the life of Christ himself, they only pretend. They are liars. They are fools to lie that they are christians. Otherwise if we had real Christians this world would have been a better place. I repeat all are humanists in their behavior and act as secular individuals yet call themselves christians ndipo ndi amakani safuna kuvomera kuti ndi ochimwa makani ngati Fox Ardon Van Wyk ndi Yohane Moyenda Chirwa. Mahule, zidakwa, akuba koma samasuka kunena kuti ndi ma secular humanists they prefer kubisala kuchipembezo. Anthu opanda nzeru.

    2. A very wise comment Willes, just look at the comments here, we have stuff like “let’s kill them” from supposed Christians, is that Christ like? and you claim to be peaceful? Name one murder that was done in the name of Atheism/Humanism, i bet you can’t. Now how many people die everyday in the name of religion?

    1. To begin wth go back to school nd learn english or else yankhulani chichewa.
      Now in responce to ur question, do you believe that there is air? How does it look like?…..Bro we dnt see air but we know its real cz we see its effects…it keeps us going.
      We know God exist coz we see his effects in our daily life…that is to us who believe. if you dnt believe in his existance good luck with that…..you shall need it on judgement day.

  127. End times, if you’re foolish enough not to see what next, beleive them and you’ll regret. Its the power of dackness ruling in their hearts.

  128. Koma zina utamanva ngati ukulotatu, moti wina ndikumayima pamtetete nkumati kulibe mulungu ndithu?? Hooooo!!! Zammalemba izi. Tiyeni tichilimike kupemphela nthawi yosokeletsedwa ndimmeneyi..

  129. The fool says in his heart, “There is no God.” They are corrupt, their deeds are vile; there is no one who does good. Do all these evildoers know nothing? They devour my people as though eating bread; they never call on the Lord .
    Psalm 14:1‭, ‬4 NIV

    1. The heart says nothing apart from pumping blood. you are fools because you cannot even know the functions of body parts like the heart.

    2. its nice that you acknowledge the foolishness of your imaginary friend…..the wisdom of man has created the phone you are using to post even facebook

    3. Romans 8:35 Who shall separate us from the love of Christ? shall tribulation, or distress, or persecution, or famine, or nakedness, or peril, or sword? 8:36 As it is written, For thy sake we are killed all the day long; we are accounted as sheep for the slaughter. 8:37 Nay, in all these things we are more than conquerors through him that loved us. 8:38 For I am persuaded, that neither death, nor life, nor angels, nor principalities, nor powers, nor things present, nor things to come, 8:39 Nor height, nor depth, nor any other creature, shall be able to separate us from the love of God, which is in Christ Jesus our Lord.

  130. zomvesa chisoni kwambiri akanakhala kuti mulungu kulibe satana akanatimeza amoyo ,indee ndizoona zamasiku otsiliza koma ndimadabwa kuti anthu oterewa akagweredwa vuto sikubuulira kwake kuti mulungu awathandinze

  131. azika vomela satana kuti kuli milungu ķulibwanji iwe nyapaphi ukaziona m.manda uzalaka laka kukhala ndimoyo kuti ulape ķoma mpata siuza pezeka

  132. inu anthu mulimbana bwanji ndi anthu asatanic,ndine ochimwa!koma awa akufuna ndichimwisitse,komabe Mulungu wamoyo wabweza lilime langa,aliwokondwela nane,ndipo ndimamupembeza achoka nane kutali kuzafika lelo lino,masiku osiliza anthu akumapembeza ndalama komaso,musamale ndi anthu omwe achula zamamilakozi osati chipulumuso! Mulungu akale nanu omukulupililanu!

  133. Bunch of IDIOTS, remember fools say in their hearts that there’s no God. But shame satan has blindfolded their eyes and hell fire is waiting for them.

    1. There are over 2,500 religions and billions of people that don’t believe in your God. Are we all damned to hell. If it even exists??

    2. And for your imfomation, the BIBLE is the word of God that we knw as beleavers. What can separate me and My Jahova? NOTHING not even non beleavers like you!!!

    3. And for your imfomation, the BIBLE is the word of God that we knw as beleavers. What can separate me and My Jahova? NOTHING not even non beleavers like you!!!

  134. Oky ngati ndi umphawi pezani njila ina koma iyo mwasakhayo ndi IMFA ndiye musaiwale kuti (chibwana chimabala uchimo,uchimo ukakula nsinkhu umabala IMFAYO)

  135. Koma munthu kuti usakhulupirile kuti kuli mulungu, simisala iyi ? Ok amakhurupilila kuti bambo wawo ndi bambo wawo? Ngati amakhurupilila ndichiyani chomwe chimawapangitsa kuti usakhulupirile ? Popeza anangouzidwa kuti awa ndi bambo wako?

    1. Ukhoza kuziwa kut awa ndi bambo Ako utafuna DNA test and all that! Koma sungapeleke umboni oti mulungu alipo nanji mulingu Wako Iweo!

    2. Nthawi zina kufanana ndi Bambo ako is enough. Sometimes he is your father because he raised you. He may not be your biological father but he raised you and you can see him.

    3. Bambotu umango uzidwa, koma mayi umachokera mwa iwo, ndichimodzi modzi mulungu timangouzidwa timakhulupilila monga momwe timakhulupilira bambo

  136. Anthu openga amenewa ngat kulibe mulungu zinthu timaziwonazi anazipanga ndi ndani , mumagona tulo tofanalo kma mulungu amakuzusani ambuye awonetsereni ukulu wanu anthu kut azindikile kwanu kukhale matamando ndi ulemelero amen

  137. Even Satana knows that Allah(God) exist and He knows that is Only One, God, the Eternal Refuge, He neither begets nor is born and Nor is there to Him any equivalent.

    1. Bro how many proof you need to know that God Exist and do you know y Satana is busy deceiving people? It is because he knows What God hv prepared for those who believe in Him and if you believe in God mean Satan believe more than you because he created be4 God created Adam and Hava… so if you need more proof about God existence u will tell me

    2. A simple reply about the proof that satan is aware of existence of Almighty God is this. A satan is also a God’s creation and was created before you and me, at first before he become a satan he was worshiping God but later he didn’t listened to almighty God the he sent down after he has been cursed by God and from that time he named satan.

    3. It means that he knows God because at first he was good and praising God, do you think he was praising Him without knowing the one he was praising ?

    4. God in a holly book ( Qur’an says ; there are some other people whether you tell them or not they cant believe…. you are amongst them, to tell you or not, it can’t change anything….

  138. the problem with mankind is that we think and believe that what we believe in is more superior than what others believe in and this is,the major source of strife,on eaerh

  139. sizoona kuti anthuwa chiweregelo chawo chikuchuluka, koma anthu ene samaziwa kuti kuli ngulu lina lomwe amafanana nawo zochitazo ndi zitchito zawo, ndiye amati akazindikira ndi kukajowina azizawo amawona ngati akuchuluka, kuti muwafuse athu amane angozowina kumene kuti poyamba munali achimpembezo chanji akuwuzani kuti palibe. panopano apedza zitsiru zizawo zolimbisana nawo mtima

  140. Mdima wakula kwambiri padziko lapansi, anthu amenewa ndizigawenga za satanic. Akuyenda akumulambira satana padziko, ndiongofunika kusamala tili munyengo yomaliza.

  141. Nthawi ina anashosha afiti kuti sangamuloze, sing’anga wina atazipeleka mkuluyo anawopa.Pano nde akufuna kulimbana ndi Sing’anga wa a sing’anga?.Ngati wakalamba angobwelela ku mpoto a zikatsegula manda kkkk!.

    1. A Amos? Thindwa ndi ameneyi tayankhulaniso timve mwati Chani? Ndinu abodza mwagwidwatu apa shame on you

    2. Witchdoctors are the ones running from George Thindwa because they know they can’t do anything since what they do is polony! The 1 million still stands, bewitch George and get your cash.

  142. Mulungu.. sazalanga.. munthu.. asanamuzuzule… Pemphero.. langa.. ndiloti.. chonde.. ambuye.. afikileni.. ngati.. momwe.. munafikila… achina.. Paulo.. amene.. anatayilira.. osakuziwani.. inu.. Nawoso.. azakhale.. oyamba.. kufalisa.. uthenga.. wanu.. wabwino.. Inu.. ndinu.. Mulungu.. woyamba.. komaso.. ndiwosiliza.

    1. Masiku.. ano.. ndipofunika.. kuchenjela.. kwambiri.. poti.. mudyelekezi.. atchela.. misampha.. yambiri.. Yokopela.. anthu.. kuti.. amutumikile.. iyeyu.. Koma.. zonse.. tikuzikana.. mudzina.. la.. Yesu.. kuti.. zisakhale.. ndigawo.. pamoyo.. wathu.. koma.. Mulungu.. yekha.. alamulile.. miyoyo..yathu.

    2. Munthu.. akavomeleza.. tchimo.. lake.. ndikulapa… Mulungu.. amakhululuka.. ndipo.. sawelengela.. machimo.. ako.. koma.. amayamba.. kukugwilisa.. ntchito.. monga.. mwana.. wake… #Paul.. ndichisanzo.. kwa.. ife.. kuti.. ngakhale.. tili.. ochimwa.. koma.. Mulungu.. atha.. kutigwilisa.. ntchito.. tikangolapa.. kubwela.. kufupi.. ndi.. iye.

  143. I was going through all the comments but mmmmmh mukungoyika zoopyseza zokhazokha basi can you put facts (am not supporting them but putfacts to convince others)

  144. Satana amazithchanso mulungu 2Akorinto 4:4, 1Yohane 5:19
    Koma amamudziwa bwino kuti kuli Yehova mulungu, yekha woona pa thambo ndipadziko lonse. Salimo 83:18.
    Genesis 3:1,5, Yobu 1:7-10 malemba onsewa ukutionetsera kuti kungakhale Wolakwa, mdani wopambana wamkulu wa Yehova amene Ali Satana Mdyerekezi akudziwa bwino ndithu kuti kuli Yehova Mulungu wamoyo amene Ali mwini moyo wa zolengedwa zonse kuchokera kuthambo ndi dziko lonse la pansi. Masalimo 85:8-10.
    Ndipo onse otsutsana naye alibiretu mwai Masalimo 94:1
    Tonse amene tikudziwa kuti kulidi Yehova mulungu wamoyo, tiyeni timulambire. Masalimo 95:1-8; 103:1-4; 117:1-2; 118:1-29
    Ndizachisoni chopambana kulilira anzathuwa kuti aimira pati kukaniratu zoti kuli mwini moyo umene akupumawo.

  145. Kkkk mene ikuwonekera nkhope…yokayikira zili zonse.singakhulupilire zowuzidwa kapena zowerenga.ndipo singakhulupilire zizindikiro zosonyeza kuti kunja kuli mulungu

  146. Komangati ndindalama zidakupengatsani mukamamva kuti mbuli zophuzila nde zimenezi ndingoti chifundo ambuye kuanthuamenewa

  147. History of a person is so hard, if it comes to religious education, a man was created by God from dust, same teacher is coming with history saying a man was a monkey at first, what’s going on?

    1. Hehehe ” man was a monkey?” Unkagona mu class ya history iwe et? ine ngat mfana okonda History ndikhoza kukupasa ma kofi iwe!

  148. Mulungu alipo ndithu komaso chiweluzo ndi cha Iye mwini. Yemwe amakhulupirira Mulungu kuti alipo akuyenera kupitiriza ndipo onse omukana asiyeni akane ndithu chifukwa tili mu dziko lomwe oyipayo anathawira ndiye naye ali busy kukopa anthu kuti amutsatire asakhale yekha. Koma tsoka likugwa kwa onse okwaniritsa zomwe zinalembedwa mmasiku omaliza. Nanga iwe ndi ine tilipati?

  149. Akhungu sangalondolelane njira, zisilu zinati mtima mwawomo kulibe Mulungu, achita zovunda, achita zosausa, achita zinyasa.

  150. onyozanu zinyozani ine ndakubanja kwanga titumikira yehova, koma chomwe mudziwe ambuye agwirananu ntchito ndipo enanu muzakhala mboni zake, kumwamba kuli Mulungu dziko lapasi kuli ana anthu, Mulungu akukhululukireni pachisankho chomwe mwachita pomukana iye,

  151. Ngakhale tose aMalawi titagwirizana kuti kulibe Mulungu, koma iyeyo azakhalabe Mulungu. Moyowu ungakome maka, ndalama zanzungu zingakome bwanji Abale inu Mulungu alipo ndipo sanyozeka. Abale wina wanena kale kuti tikalangikile zina koma tikakhuta freezes wa bwemba mkumati kulibe Chauta aaaaaa kaya. Nkhondoyi ndiyake amamenya yekha.

  152. bola amenewo kusiyana ndi omwe amaoneka ngati opemphera koma ali ma satana otheletu(hule wamu bar or mu street asiyana ndi mayi okwatidwa koma akumamuzemba mwamuna wake kumakatchaisa)

    1. Bro..palibe zabhola…sikut anthu okhulupiria..Sachimwaa No!!..amachimwanso.alindizofowoka zawo……komano….ngakhale amachimwa they knw and beleive kut ku Mulungu in so Doing amakhala ndi mwayi olapa…thawi inayake….Koma Kukaniratu kut kulibe Mulungu Bro..nkumat Bola….Thats Big Sin

  153. Anthu ena opusa ndi achibwana ankafuna kukaona komwe kukhala Mulungu koma iye anawakatha powasiyanitsa ziyankhulo,inunso dikirani kathawi pang’ono mphotho zanu aza nazo posachedwapa.anthu openga mwapanga bwanji?

  154. Zachisoni,, munthu wankulu ngati uyu mpakapano sanaziwe kuti kumwamba kuli chauta, udzafa imfa yowawa ngati ya pharaoh. Nde akakhala ndi ana malangizo ake azikhala omwewa kuti ana inu chauta kulibe,, shame on u madala.

  155. Its true many people say there is no God or you can’t believe in Him because u can’t see God. I wonder why they believe that there comes tomorow but they don’t see it. They must not believe in tomorrow

    1. Unlike “God”, tomorrow has been proven time and again to occur, so we merely assume tomorrow will come if all constants are the same . Even though, tomorrow is simply a construct made by man ( so is God) tomorrow is subjective

    2. Bonifaci Kalele you need to understand this. Tomorrow is a man made construct based on time. It can be today in New York and tomorrow in Melbourne. If you want to see tomorrow, simply fly from New York to Melbourne at around 11:PM NY time and you will see tomorrow or whatever your talking about. Your argument is absurd.

    3. We cannot see God thus not prove he is real or not. Your belief is based on a book that tells you it is from God. Your book, I assume the Bible, has severely been edited translated then edited again, half of the authors are unknown, the original transcript of the cannon of the Bible is nowhere to be seen and you criticize us for not buying into it? There is no credible evidence that stipulates that the Bible is the word of God. It’s just circular reasoning. The only way to sell an invisible product is to threaten non believers with hell and to breed those who believe into hating us or thinking we are of the devil, who by the way does not exist either.

    4. Morena Morena no need for science, just look at the time in Melbourne and it will show you that they’re already experiencing “tomorrow” hahaha

    5. There is no name given to anything that does not exists. Once you mention something, others gonna need elaboration on that. Its madness to mention or call unexisted thing. God exists

  156. Kkkkkkkkkk asaaaaa Satana akunyadila apa kaya zawo zimenezo ife tigwiritsa chomwe tilinacho ndiye MULUNGU WAMOYO BASI!!!!!!!

  157. Ine Ndikamamva Zabambo Ameneyi Ndimamva Chisooooni Kwambiri.Mumati Kulibeyo Akuendeleni Mumziwe Ndipo Ndipakamwa Panu Muzaliuza Ziko Nokha Kuti Mumalakwa Ndipo Mwalapa.

  158. Bambo Thindwa choti mudziwe mukuzichotsera madaliso pa moyo wanu.Ndipo ife opempherafe tikukuikizani mmanja mwa Yehova Mulungu mulengi wakumwamba ndi dziko lapansi kuti akakuunikireni njira ndichoonadi chamoyo osatha.Sikuti kukana Mulungu mwayamba ndinu analiko Paulo koma ambuye analondolera choonadi nakhala mtumiki waMbuye.Kotero tikupha Ambuye Mulungu kuti akachite chimozimozi ndiinu kuti tsikulina muzakhale mukupangisa msonkhano okwezeka dzina la Yehova.

  159. Bible limatifotokozera kuti chitsilu chimati mulungu kulibe.ndiye sizingatheke kuti dziko lonse lamalawi zisapezekeko zitsiluzo .ziyenera kupezeka koma tsoka loopsa kwa zitsiluzo chifukwa azawona mkwiyo wa mulungu

    1. zimenezo mmauzana anthu okhulupilira nokha nokha,tangoganizani ku north korea ndi ku sweden 76% sadziwa mulungu koma ndimaiko antendele komaso umoyo wawo ndiwotsogola kulibe nsanje ndi nkhondo koma kuli chikondi chozama,,,,,

  160. Abale anga mwa Ambuye, chonde, chonde tisawaweruze anthuwa paja kuweruza ndi kwa Mulungu. Koma tiyeni tidziwe kuti tiri ndi tchito yayikulu yoti tiwanthandize. Siife opambana podziwa kuti Mulungu alipo koma ndi chifundo chake, Mulungu mwini kumatisungabe mudzanja lake. Mzimu woyera amatitsongolera ndipo kuwala komwe kuli mwaife tiyeni tiwawunikire anthu amene amati Mulungu kulibe osati kuwaweruza. Paja ndife nchere, tiyene tithirire umboni pa za ufumu wake.

  161. Asiyen azicita tsiku limozi azaziwa kt kuli MULUNGU. Anzao adaziwa kt YESU ndi mwana wa MULUNGU ali pamtanda. CONTINUE 2 BELIEV IN JESUS. VIZ R LAST DEZ

  162. Zitsilu za Anthu adazilenga ndindani?ndimafuna ndinekambe zambili mwachidule musapusisidwe ndi zitsilu zimenezi,Lemekezani Mulungu ndi amene adatilenga pamodzi ndi zitsilu zimenezi.Mulungu akusogololeni kwainu amene mum,nkhulupilira.

  163. Kakutsalilani Kanthawi Kochepa Zedi Mukanthidwa Ndi M,kwiyo Wayehova Anthu Otelewa Amanivetsachifundozed Akufunikila Kuphuzitsidwa Baibo Mokwanila

  164. #Babylon get down, curse upon dem go against da most high God, shame to Malawi government for accepting this, dem gonna face the harsh judgement before God, need Jesus Christ.

  165. mulungu samakakamiza aliyese kuti amukhulupilile kuti aliko ndipo amanena kuti chisilu mtima mwake chimati kulibe Mulungu….thindwa ndichisilu chamunthu ndionse omusatila koma ine strong faith kwa Yehova paka kufa ndithu ndipo dzikoli kuzalibwezelesa kukha paradaiso.zisiluuuuuuuuuuuu zachinathindwa Bible limatelo.

  166. Oky nkhani yabwino kwa iwo! komano tingokupephani kuti, muzatidziwisetso Akayamba kuyoyoka ndi chilango komaso m’kwiyo wa Mulungu Akumunyozayi! Mwa m’modzi m’modzi wa gulu lawori.

    1. Olo Lord yo atakwiya who cares. Taona anthu osalakwa akufa imfa yowawa ena kuphedwa kumene osalakwa. Zoona mmene ndakulilamu ndizikaopa punishment COME ON!!

    2. Many Of Those In The Highest Positions In Government And Education The Bible Would Call Fools.They Claim To Be Wise But Denying The Very Existence Of God.

  167. Anthu ochita zinthu ngati alibe mitima awa akuchulu kila chulu kilabe nde nanga mulungu atati atolele moyo wake lelo ndi lelo kungo kudzudzu mutsani kuti mupange wanu moyo munga kaunyele kuti anthu opusa inu ndi zitsilu mwazitsilu pano padziko lapasi

  168. AKusoweka mamvumbulutso,aroma 10;13,aliyense amene adzaitanila pa dzina LA mbuye adzapulumuka.ndi wina m’kumati kulibe mulungu,sakudziwa chimene akuchita.

    1. Ndimasiku omaliza, awa musadabwenawo, iwo adziwa liti kuti mulungu kulibe? siomwewa amaimbanawo nyimbo yafuko lathu ku school kuti akatenge ma certificate omwe akutumbwilawo

  169. kulibwino kukapsera zina kumwambako not kukana zoti kunja kuno kulibe mulungu iyo yokha nde yayi…#mulungu. .alipo mpakampaka

    1. is religion stupid n senseless are you sure? then everything u do like bathing z senseless. they r sayin kut there’s z no God kut munachokera kwa nyani. kod nyanio anachokera kut? akut they cant believe wat u cant c. y do they believe in tommorow yet u cant c it. chionongeko chili pafupi

    2. You have more things to learn, see life outside religions prospective you will understand how stupid and clueless religion is

    1. The Universe Can Be Shown To Have Had A Beginning.It Is Unreasonable To Believe Smthng Could Begin To Exit Wtht A Cause.The Universe Therefore Requires A Cause,just As Genesis 1:1 And Romans 1:20 Teach.God, As Creator,is Outside Of Time.

    2. It is really Unreasonable to Believe Smthng Could Begin Wtht A Cause when The First Of Things Should Exist Wtht Cause. So the popular statement ‘Nothing Can Exist Wtht Cause’ Is FAULTY

    3. If We Accept God’s Word,beginning With Genesis As Being True And Authoritative,then We Can Explain And Make Sense Of The Evidence We Observe In The World Around Us.

  170. Mulungu anawalekelera anthu ake kut achite momwe angafunile koma tsoka on judgment day.Tisaiwale kut ndintchito akungofuna ndalama.

  171. Okay, food for thought: Sweden is 76% secular, meaning a large majority of people don’t care about religion or are godless heathens. I would expect God to give such a country a thrashing, but what do we see? Everything that is supposed to be low is low, such as crime rates, corruption, illiteracy, mortality rates etc, while everything that is supposed to be high is high such as health care (it’s free), education, life expectancy etc… Compare that to highly religious countries like Malawi or Nigeria – such god fearing nations – and we see the opposite. Why do people utter such statements as “God is punishing Malawi for homosexuality/George Thindwa”? The only conclusion is that they speak Swedish in hell, because I would expect God to bless Malawi for being super religious over Sweden.

    1. Ur talking this coz our God z merceyful……Thats y u see The country u metioned..z doing Gud..not just they dont beleive in Living God…but they r doing gud coz our God z mercyfull one…en He loves everyone………………..in short u can hav two kids example ,,one who obey and doing good things to u ..as parents….but second one disobey and stealing from you…but still u can love them…en u cant even be happy to c that one who is always stealing 4rom u ..to meet any problem..like being poverty and arrested by police…y??…………U cant understand God coz of his love……..Think Deepily Bro as a Man!!!…….who created life?…think.?….even u can think of who made clothes,cars…so many things..u will find answers that someone Made t……so wat about life?..who?…….Dont hav Chicken mind bro…en Brain wash people

    2. You are looking at it in a very different way. To be God fearing doesn’t mean u can’t have problems. Refer to scriptures.

    3. Remember that “life” is still a mystery to scientists, if a living organism dies no one can bring it back to life, there are three state of matter water, air, light a man can only use but not create them that’s where God the Almighty exist!

    4. Zonse zimatheka ukakondeledwa ndi Mulungu Bwana, “For with God all things are possible”. Popanda Mulungu palibe moyo, the scripture says, “Do not lean on your understanding, trust in the Lord”

    5. If they do not believe in GOD,God believes in them,that’s why He showz His un imaginable love to them,the wayz of GOD my dear can not be understood by man no matter what,that’s why HE is GOD

    6. Why in “God fearing nation” there’s too much spill of innocent blood of albinos? Why too much mob justice murders? Why too much rapes and defilements of minors? The list goes a thousand times! My mind argues if Malawi is truely “God fearing”

    7. Shame to them that don’t believe that God exist due to high rate of crime yomwe ikupezeka mmaiko omwe amakhulupilira Mulungu mwina sadziwa kuti satana akuwatseka dala maso kuti apitilire kuona ngati kulibe Mulungu

    8. The devil can’t fight his own rather he fights those that belongs to God, no wonder those other countries try to force us to follow their ways in order to help us. That’s the devil fighting us but we’re just too blind to see and we busy admiring the countries that already belong to the devil. Work up

    9. the existence of God can not be proved by fortunes or misfortunes.The fact that you see the universe it is enough for you to believe that there is a creater.

    10. i think bible tell us crystal clear that to follow Jesus its not easy maiko onse amene ali olemera mavuto amene alipo ndi dauble than malawi or so called nageria and.kukhala pa ntendere sizitathauza mulungu akukonda malowo

    11. Ronaldi Keo Kaluma yes! If malawi was secular then people would be working hard to develop it instead of wasting time wishing for a new life in the sky and do nothing about bettering this one.

    12. u want To tell people dat those who dont believe..can..com Rich without hard working???……….Big issue ..z Satana dont want to go to hell alone…….He need some people to go with…………….So Thindwaa need some people kut apsere nawo..limodzi….dats Satana Mission……..Chifukwa iyeyo ngat khulupirira there z no need Chobwerera pa air, cholinga chake nchan??

    13. Hehehe ati u telling pple kut they can become rich without hardworking ah hehehe chizungu chavuta kumva apa! Lmaol nde wina ati the fact that there is a universe is enough for you to believe there is a creator ah hehehe which creator by the way? Nkoona sakukuyankhani simukubwelesa ma facts apapa!

    14. The Bible Say AFool Say There Is No God In Heaven.The Fact Is That Thindwa And His Clue Are Fools.Fools Had Ameeting In Lilongwe.

  172. Am afraid,yes i am.denieing the thet truth that God is there is suicide.lets play with something but not with Jehovah.am afraid of His fierce retaliation!!!!

    1. haha had you known the number of gods that people believe in you would have asked yourself that “how sure am I that my god is the right god I’m supposed to worship?” Dont just be driven by your culture, reason before you dogmatically believe something.

  173. NKHANI NGATI IZI ZIMANDINYANSA BWANJ. NDICHIFUKWA CHACHE MULUNGU AKALANGADI NDIPO ANTHU TIKULANDILA DZILANGO PADZIKOPANO CHIFUKWA CHAWANTHU OTELE.

Comments are closed.