Msonda azitaya, atuluka PP

Advertisement
Ken Msonda People's Party Joyce Banda

Chipani chija chikutha anthu akuona.

Mneneri wachipani chostutsa cha Peoples’ amene anakakamila ngalawaya chipanichi ngakhale mtsogoleri wake atachithawa, a Ken Msonda, alengeza kuti basi iwo alekana nacho chipanichi.

A Msonda analengezaizi pa tsambalawo la pa Fesibuku kuti tsopano iwo simmodzi mwa anthu a mu chipanichi ndipo aganiza zopuma kaye mu ndale zachipani.

Ken Msonda People's Party Joyce Banda
Msonda: Atuluka PP.

“Ndakhala ojijilika pa ndale kuyambila 1994, tsopano ndikufuna ndipumulile kaye,” anatero a Msonda polengeza za chiganizochawo.

Koma a Msonda anatsindikanso kuti kutulukakwawo mu chipani cha Peoples’ sindiye kuti basi azitayilatu pansi ndale.

“Nditulukilanso, mu zisankhoza 2019 ndikupita kukaimila ku Rumphi East. Anthu a ku Rumphi musadandaule, ndilinanu,” anatero a Msonda.

Dera la Rumphi East padakali pano phungu wake ndi a Kamlepo Kalua amene ndimkulu wavuta ndiphokoso podzudzula boma la a Mutharika. Iyendiwa chiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha Peoples’.

A Msonda akhala mmodzi mwa anthu okhulupilika kuchipani cha Peoples’ anthu ambiri atachitaya kutsatilaku luzachitsankhokwachipanichindikuthawam’dzikomunokwamtsogoleriwachiapnichi.

Pa nthawi ina a Msonda anapeza mavuto atalangiza a Malawi kuti aphe anthu onse ochita mathanyula ati chifukwa Buku lopatulika limaletsa mchitidwe umenewu.

Advertisement

75 Comments

  1. Pp Lero Ansonda Manyunyu Chani? Chinatha 2014 Ndikale Ndie Iwe Nsonda Sumaona Umangoti Kaka Wagwanazo Bwanji Manyazeee!

  2. Mwachedwa Ansonda Anzanu Anaonela Patali Achena Khumbo Anathawa Msanavote Nkomwe Ndie Apamtani Mlowera Kuti? Poti Zipani Zose Zasedwa Zako Izo Wekha

  3. Pp singathe cz nsonda watuluka apo ndiye mukunama mukamalemba muzuganiza ngat ndinu oohunzira vuto ndilot amalawi ditimaziwa kusiyanisa chabwino ndichoyipa umphawi suzatha munthu wankulu but ubongo nduwa bankha mungaganize zolonhosoka choncho shirt

  4. Yonse mkabati zinazi abale mkangamwala. Ine kudabwa nangiliya anachoka koma ena angoti kakaka pamene mwini wake chipani anachithesa welcome baba nsonda to dpp.mcp.udf

  5. Tisadabwe nazo, ndi umboni wakuti maboma wa anthu sangathe ulamulira mwa chilungamo tizingo uyembekezera ufumu wa Mulungu basi.

  6. Kkkkkkkkk pp ndingat mwana olowelera poti msonda waganiza kt abuele kwa atate thats DPP but here u are not welcome jus stay out there .ndalama zimakhala m ‘matumba not under pitcot

  7. Kkkkkkkkk pp ndingat mwana olowelera poti msonda waganiza kt abuele kwa atate thats DPP but here u are not welcome jus stay out there .ndalama zimakhala m ‘matumba not under pitcot

  8. kkkkkkkkk ine ndisekepo apa osaona anafusa woona kuti ada bridge ili pati ndie ona unja anamuuza kuti ndikafikapo ndikuuza apatu asonda samaona amayi amaona ndie anangoti ndikafikapo ndikuuzani asonda anangoima kudikira auzee malo moti akanango muuza wina alondorere anapezeka agwera madzi inu kumaganiza sonda sunalakwitse koma popeza wanyowa kale ndiebe aaaa pita ku mcp basi utani nanga poti watani kale ndiline aaaa ndikanalowa boma kudyanao basi kosusako iiiiiii azawina ndakaika awoo mulungu anatemberera basi

  9. Kuganiza mwa nzeru osakwera basi yoti yangoima ayi, mwina njoonongeka, muchedwa nazo,,,pp mwaleromunso,, weldone Nsonda osamakhala ngati mwabadwa lero ayi….

  10. Malawian politics full of greedy lions who do not even care about the people they represent. Keenly following to see his next move.

  11. Anthu adyela inu Ntaba mutchulayo pano adakwilirika sadzavekaso ena ndi amenewa aNSONDA akana chidodo ngati cha Jumbe tikuva mawa kuti alowa DPP, adalakwitsa anafuta D Kuti ikhale pp.

  12. Afuna kulowa DPP galu uyo, ndale zmenezo, akukaima ng@ phungu oima payekha kuRumphi akazawina azalowe DPP, aaaaa….

Comments are closed.