A Kaliati agwila a Nankhumwa ufiti

Advertisement
Malawi Patricia Kaliati

Ziwanda zandeu zinabisala kuchipani chotsutsa cha Kongeresi chija tsopano zavumbuluka ndikupita ku chipani cholamula.

Malingana ndiu thengaumene ukufalitsidwa, nduna yoona zama boma aang’ono a Kondwani Nankhumwa ili ndivuto loti ikumankakunena mabodza nduna zimzake ndicholinga choti akome kwa President Peter Mutharika.

Uthengawu umene ukuoneka kuti unajambulidwa ndi Mayi Patricia Kaliati, amene ndinduna yoona zophunzitsa anthu, ulindi munthu wina okonda MayiKaliati amene wawayimbila phone kuti awachenjeze kuti asamale pocheza ndi Nankhumwa chifukwa mkuluyu ndinjoka mu udzu.

“Akufunaudindowanu,” mkuluwina akuchenjeza Mayi Kaliati amene akungokhala kumamvela. “Ndalamazimenemumalandilangatindunamukayendapaulendozimamupweteka.”

Uthengawu ukumveka kuti unajambulidwa nthawi imene Mayi Kaliati anali induna yoona zofalitsa nkhani ndipo anali pamseu pafupifupi tsikuli lilonse ukuakumapatsidwa makobili aja amatchedwa ma alawansi.

Mkulu amene akuchenjeza a Kaliati akuwauza kuti bamboo Nankhumwa ali pa kalikiliki kuphamika phula a President ndicholinga apeze udindo umene tsopano wapitakwa a Malison Ndau.

Advertisement

161 Comments

  1. Iwe Pedro kuyambira iwe kaliati hulleeee ngati mayi anga ndihuleeeee iweso mako ndihuleeeee ife tikunena zimene zikuchitika Ku Malawi ndizosayenera magesi kuthimathima mazi nawoso kusowa tawona kundilande zuro amapanga demo bcz of magesi ana sakuphuzira salary wosawapasa aziphuzisi km ndawona galu mu lhomwe Pedro akungovomereza zilizose kusaziwa ndikufa komwe ukanakhala wins ukanasiya ky commenter ngati uli ndizeru sindingalimbanw nawe iwe galu yosayenda muzakhaula siku ndilimozi frishiii nose alhomwe ndi Dpp khozani zithu anthu akuvutika

  2. Mesa kaliati ndiye mwini waufitiwo that bitch she don’t know what she is talking about?
    The problem they don’t fuck her that is why she is becoming so stupid
    This is new era kaliati we can fuck you nicely and sound sweet in your life ;
    Stop nonsense

  3. Kkkkkkk’kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk’kk ine zopusa ayi mwayambaso kugwilana ufiti osamangogawana ndalama zimene mukubazo bwanj zauchitsilu bas

  4. Mufuna mubise za cashgate pobweletsa zopusazi….aah kapangani ZANU izi…..akapezeka ogula Malawi agula bola tikhale mmana mwawanthu amene azatiganizire kuposa izi zanuzi

  5. Chuluke Chuluke Gwanjuchi Umamaona Yakuluma, Chilungamo Chioneke Basi Mutanyoza Chotani Mufune Musafune 2019 Mcp Boma

  6. aaaa ayiwala kut ku sogolo 2019 kulizotan aaaa waiwala ameneo wasiyini aziona wonkha kusogolo zisilu kwabasi zisiyen azat funa ife kut tiwapase vot palibe zimenezo

  7. kkkk malawi24 ndi nyatwaa kkkk paja lamulo limati chiyani?onena mzake kuti ndi mfiti amangidwe!! apatu lamulo ligwile ntchito,malamulowa osati muzingopangila ife osauka

  8. kkkk makwacha avutu,mpaka kugwidwa ufiti?nde kuti iye ndi mfiti ,l think nchito ikuwayenela ndiyazisamba,sing,anga. mr president apaseni undunu wogwila ufiti mwina awukwani ,

  9. Zakhala bwino kwagwira umfiti akaliat komatso ndi amayi apakamwa.kaya ali ndi banja lotani mayi amenewo koma nthawi imakwana

  10. Mumanyoza Winiko ndi Wandale kuti ndi a misala,nanga mpaka ufiti anthu olemekezeka kutamba ngati awa. Timadabwa makani ndi mfiti eti basi.

  11. Kaliati my Sister ufiti uliko ndipo ku dziko kuno ndi kwao sungathe ndithu, koma Yesu Khristu is your solution no need to fight or quarrel. Osavutikana nazo izi Mulungu is greater than these issues mufune fune Yesu Khristu basi. God be with you.

  12. Ngakhare zitavuta bwanji palibe angalamurire dziko mokomera anthu onse ndi Mulungu yekha amene angakwanitse kutero tizingo uyembekezera Ufumu wake basi.

  13. eeeee ineso ndikuona choncho anankhumwa akaliati nose ndinu afiti palibe wabwino ndithu malo moti muzipanga za njala mufuna basi kumalozana zala ine zimenezo zandikwana nanuso anyasa mitu yanu simagwira aaa aii tamakambani zaphindu basi kukangocha khani eeer koma mcp eeer koma pp eeee koma dpp osakamba za mulungu kuti akubwera posachedwa ai koma basi mukakhuta kumangolota ndale iiiii

  14. Mbava zigwilana bwanji ufiti, anthu andale unu mukapya moto ndithu mumanva bwanji anthu a m,dela lanu akugona ndinjala inu muli busy kuba ndalama, ana anu mkumasangalala, mkumakhuta kumachita kutaya tiyi, zachisoni ndithu

  15. Agalu awa apeza penapake amasambilana makhwala kt bwapini aziwakonda kwambili makamaka huleeee la chilhomwe kaliati sopano makhwala a huleeee kaliati achepa phavu wakumana nazo za kondwani nyanga km ziuluridwa zambili pamenepa mbava zenizeni popeza bwapini nayeso ndimbava yaikulu frishiiii agalu inu a Dpp muyaluka nazo muwona Ana a njoka

    1. Iwe Ulemu Chigoma zeru ngati huleeee kaliati undipeze cape town at Water Frant undipeza pamozi ndibwapini wopusa asilikari aziba futi zaboma kt azikabera paliwusogoleri apa bwapini zoona malawi wake up munasakha molakwika galu yachabe yimeneyo apolice azisowesa mafuti ndizipoloporo zinaliko izi kale ayi km ulamuliro wabwapini frishiiii ndi
      womusatira ake wose a Dpp

    2. Iweso ndiwe galu pamozi ndi huleeee kaliati komaso bwapini ndipo sindingawope agalu achabe inu ndipo iwe Ronex Kanduna chisilo ndiwe ukuwona anaku primary akupanga mademo bcz of bwapini sakuwapasa ndalama zawo aphuzisi huleeee kaliati kungana ndi kondwani zopusa

    3. Koma zinazi utha kungochimwirapo ndithu asaaaaaa ukungoonetsa kusazindikila kwako coz kutukwana sikungakuthandize rather than kubwera poyera ndkufotokoza mavuto osati kutukwana munthu but anyway ndkutha kukuvemtsa paja chidebe chopanda kanthu kuchulutsa phokoso…same as u.

    4. IFE NDYE TKUMVA KUKOMAAAH..DPP WOYEEEH..WATIKOZERA NSEWU PANO TILI MUTALA..MAULAMULIRO OSE APITAWA PALIBE ANABWERETSA CHITUKUKO CHONGA ICHI..APETER NCHIPOLOPOLO DZIKO LOXE LAMALAWI WINA AFUNE ASAFUNE..TUKWANA UKATOPA USIYA UKANAKHALA WANZERU UKANADZANGOSAMUTSA MTUNDU WAKWANU UKAKHALE KUNJAKO SINANGA WANYOZA KUNO NGAT UNABADWIRA ULIKO..AMAT OSAPHUZIRA KWAWO MKUNYADA UWU NDIUMBULI OLO AKHALE HULE KOMA ANAPHUZIRA KUKUPOSASO POMWE IWE UKUGWIRA YAULONDA..UKUONA NGAT WATUKWANAMU OTSUTSA AKUPATSA NTCHITO YOWAPUKUTIRA MAGALIMOTO..PEPA NIGGAH OSAPSA MTIMA AKAMAT NDALE NDICHONCHO OLOWELERAWE UMAPUSAH

    5. Koma man awa ndi akapee. Munasankha wolakwikaaa? Iwe unali kuti kusankha woyenerawoo? Popeza ndi udindo wako. Ndeee umbuziwo umenewo. Iwenso Nyapapi eetii

    6. Iwe Pedro Sozinho Sag Khofison ufuse azako Ine simulonda ndikugwiraso ntchito yahoo kaya iwe ndi huleeee kaliati kaya nose ndinu alhomwe wopanda zeru chomwe mlungu amakhala ndicholangira chake azidyera misokho wosauka mwayamba kuyaluka ndipo pamene ndikugona ine or ndalama yomwe ndikugwira iwe galu sungandifike ine ndilibe chipani ku Malawi ko km iwe wawonesa umbuli wako ukuvomereza zopusa anthu akuvutika ndikachipani kachilhomwe iwe nose a Dpp pakana Bwapini samalani thawi yizakwana mlungu si bwapini or iwe galu muzachoka pamene muli frishiiii pple of Dpp plus lhomwe pple.

    7. Bwapini wapanga chitukuko chowapasa salary aziphuzisi ndi asikali azipolice aziba zipoloporo kt aziwopyezera anthu andalama zawo ndikupha albino ndicho chitukuko wapanga bwapini ndikuba Ndalama boma ndinduna 7 huleeee kaliati Ali mugulu nduna za cashgate Iwe Ulemu Chigoma ndimaganiza kundifusa kt ndilipati umaganiza ndikuwopa poyakha ine sindimawopa ndipo uziwe sindikutukwana or amako Kaliati ndi bambo wako Bwapini akuwonpo apa zomwe akupanga ndizopusa kwambili ndipo sindiwopa mdimapanga zanga ndalama ndipo sindonadyepo ndalama ya chipani chilichose ku Malawi uko anthu zamavuto akuwauza km boma la bwapini silovera agalu nose mukuziwa dyera lanu likupwetekesni frishiiii pple of lhomwe & Dpp

    8. iwe galu iwe ,,ku southafrica ungagwire ntchito yanji kuposera yosambisa agalu ndi kupuputa manyi a ana amabunu?forsake ,,mumayankhula ngati mukuyankhula za nzeru ziri zopepera zenizeni,,Atonga inu wathawa kunyera m’madzi kuno basi kungopita pa johnz pompa apa wati ukhale political analysis? xool yake iti?amvekere “pple of dpp plus lhomwe pple” just imagine xool yake iti mpakana pple of dpp?ati Capetown zachamba

    9. Iwe Davie Cena ndiwe galu ine sindimavota muphwanga wamva ndiziremeresa ana bwapini ndimakana ndimaganiza ndiwe wazeru km ulibe ngati ndiwe mu lhomwe wa Dpp tavomerezani kt bwapini zamukanika agalu inu frishiiii ndipo munasakha molakwikadi ndipo munabera zisakho ndani sakuziwa anyapapi inu vuto lagalu inu bwapini akamalakwisa or nduna zake chilichose kuvomereza zopusa frishiiii pple of Dpp

    10. Iwe Andy Cazorla Maley kuyambira iwe bwapini nose ndinu agalu wopusa kwambili ine ufuse usmaganize wose alikuno awora manyi agalu or kusesa munyumba ndipo or iwe kuyambira family yanu ndingakudyeseni ine sumungandifikeso mwava ndipo ndikunena mobwereza inu a dpp ndinu agalu pamozi ndi bwapini kuwonjezera mtundu wachi lhomwe wopanda zeru ntchito kukumba Gondolosi ndikupha mbwewa frishiiii

    11. Galu ndiiweyo mbuzibyachabe chabe..osabwera udzaimire upresdent iweyo bwanj?mbuli ngat iwe manyaka wachabe chabe..uwafuse ambuyako kuti 1949 kunalibe njala?Iweyo uwona bwanj vuto ngat ulikuno..dzasamutse mtundu wakwanu mbalame iwe..tamagwira yochapa matewerayo Jon kopita mbuli zikagwire manyi ndkusambitsa nkhalamba…wafa nayo n’gooioooooooooh..tiwaooze eeeeeeeeh ….tiwapepese eeeeeeeeeeh pepani…mufune musafune atilamula basi nomatta wat mbuz amadya pomwe ayimangilira unya magede

    12. Ngat sufuna kulemeletsa munthu y ukugwira ganyu?ukhale ophuzira osatsegula company bwanji iyaaaah ukakhala uhule anayamba ndi amako ndi abambo ako kuti iweyo ubadwe anavulana ndye zisakuwawe uliposo umamwa mankhwala aboma mahule apajon anakupha mkabudula mopeyukamo

    13. Mmmmm, sindikunyoza guyz ku Malawi ndikwathu, off coz ambiri alamulira dziko lathu koma awa alomwewa nde aonjeza kuba akuchita kupakula nsima tiyeni tinene chilungamo, ife anthu ovotafe tikati tadya chankhuli nde kuti ndi bonya, penanso kumagona nayo njala kusowa ndiwo ana athu atopa ndi mpiru, mmmmmm Malawi sadzatheka basi

  16. Mukugwirana bwanji ufiti anthu inu am’boma, poti ndinu nomwe mmati kulibe ufiti? Otchula mzake kuti ndi mfiti mumamumanga, nanga inu bwaaaa? Kapena mukuvomereza kuti ufiti uliko???
    Which is which????

  17. Pajatu onena mzake kuti ndi mfiti amamangidwa kwathu kuno ndiye apa tioneno kuti awa amangidwadi kapena amangomanga ife anthu akudzi tikanenana kuti ndiwe mfiti

  18. Too much is poisonous zakuchulukilani ndalama mwayamba kukangana kulimbila maudindo mmalo mogazinila zazofuna za anthu akumadela anu omwe anakusankhani kuti mfike potchulidwa ma Minster iyaaa

  19. Ndichoncho anthu akuba zochitika chifukwa mulungu samayandikila ndi anthu akuba .Motero anthu amenewa mkati mwao mulungu anachokamo kalekale ,ndiye chifukwa lero tikumva izi mawa zina .

  20. Chithelekitale cha amalume ndimati ndi chiponde apa chaponda ine ukamafunila azako zoipa zimakubwelela mbava zokhazokha izi

  21. Ndale mkanyama koipa kwambiri Agalu inu musatikole mwamva mudziti mukaba mkulephera kugawana bwino mudzigwirana ufiti. ?? imya kukamwa ngati kanyimbi 4 tseck

  22. Chithelekitale cha amalume ndimati ndi chiponde apa chaponda ine ukamafunila azako zoipa zimakubwelela mbava zokhazokha izi

  23. Umbamva, uchitsiru, ndewu, kusamva, kuzkonda zagona kuDPP, sindkudabwaso, lero nd izo

Comments are closed.