Samalani ziwalo zanu zobisika, odula ziwalo ayambilanso

Advertisement
knife-blood

Palibe kothawila mu dziko muno. Pa nthawi imene chuma chasokonekela, chiopsezo cha njala chakulira ndipo anthu ena oipa akuchita nkhanza anthu a chi alubino, kwabwelanso anthu odula ziwalo.

Mnyamata wina wa zaka 18 ali pa ululu osaneneka pa chipatala chachikulu cha Kamuzu mu mzinda wa Lilongwe, anthu a chiwembu atamudula ziwalo zake zobisika. Izi zinachitika mu boma la Nkhoktakota.

Malingana ndi mkulu wa apolisi pa polisi ya Nkhunga ya mu boma la Nkhotakota, a Labani Makalani, chiwembu chomudula maliseche mkuluyi chinachitika lachiwiri pa esiteti ya Illovo ya mu bomalo.

knife-bloodA Makalani anauza ife kuti zigawengazo zimafuna kukagulitsa maliseche a munthuyo.

Malawi24 yauzidwanso kuti mmodzi mwa zigawengazo wagwidwa ndipo ali mmanja mwa a Polisi pamene anzake ane akufunidwa ndi a Polisi.

A Makalani ananenanso kuti mnyamata amene anadulidwa malisecheyu ndi mkulu ochita malonda a Kabaza. Iye anapezedwa ndi a Polisi ali mu ululu osaneneka zigawengazo zitamusiya kuti afe.

Kupatulapo kuti anamudula ziwalo zake zobisika, mnyamatayu anapezeka ndi bala mmutu komanso anamuthyola msagwada.

Mkulu wa zaka 41, a Rangerson Mashikudu, ndi amene amangidwa ndi apolisi okhudzana ndi chiwembu chimenechi.

Zomvetsa chisoni kwambiri ndi zokuti ngakhalae apolisi anapeza ziwalo zimene zinadulidwazi, achipatala ati sangakwanitse kuzibwezeletsaponso pa munthuyu.

 

Advertisement

228 Comments

  1. Akumafuna zasize yanji cz azibambo ena ndi chikhoswe kAle kukula chimuchiracho nawo azi mayi eeena eee ndibowo loti madzira ankhuku awili kugwera pakamodzi kkkkkkk maybe ali zazikulu ali bho mwina sizingayende kaya changa chachikulu kwambasi 5kg nde uyelekedze kufuna kudula yangayi tizathana

  2. Vuto sii Peter koma ma boma awa Mulanje, Tyolo, Phalombe, Chiladzulu, Chikwawa ndi Nsanje anamvota kwambiri galu ameneyu, today they were starting complaining about him ndisamveso

  3. All this is due to laziness, we don’t want to work hard under God’ s blessings, but easy ways of getting rich. It is written in the bible eat your sweat, and with these people whose sweat they eat? Very sad, you can get rich by taking someone’s life but you shall die too living your dirty wealth behind.

  4. koma Malawi in its state of misery,pple r finding their means to make quick cash at the expence of other pple’s lives,first it was the albinos but now hish.kwatsala akamaliza kutidula ziwalozo ayamba dza agalu coZ it seems bussiness yothentha ku malawi kuno ndiyadziwalo#dulani mutimalize mulemele ndinu

  5. inu amalawi ulesi unakula kwambiri kuthamangira zofa ifa zowona munthu wamamuna wa mphabvuzake kupha m’zako kutsa m’chila? mudziko muno muli nthaka ya ndalama tiyeni tiphuzitse boma makumbidwe amiyala ya miyala inu ku Dowa’ Salima’ Dedza ‘Mchinji ‘ Ntchewu’ gold alipo chuma chawulere’^

  6. nkhani yosakhala bwino imeneyi amalawi ziko likupita kuchionongeko ili koma chodabwisa ndichoti tili ndi apolice ambiri koma palibe chomwe amachitapo tingolimbikila kupemphela basi

    1. Vuto ndilakuti apolice ali mugulu lomwelo, ndicho chifukwa mukuona magulu azauchigawenga akupezeka ndi futi zoopsa, dziko lili mmanja mwa agalu basi.

  7. Chitezo,Chilungamo,Chitukuko zinathera pati? Kodi dziko lathu mkulipeleka kuti kodi mwaiwala kuti Dr John Chilembwe anatimenyela ufulu wa dziko lathu, koma ngati muli ndizeru muyenela mgwade Kaye ndikulapa machimo anuwo.

  8. Zithu zimakhala zomvuta ngati busa oweta ziweto ali osiza,ogona,kapena nditi chitsilu ziweto zake zimalowa minda yawathu iziso zikungofanana ndi anthuwa palibe chomwe akuyakhulapo poti titi akulira moyenda ndie ife alibe nafe ntchito

  9. Koma Malawi ndi dziko laling’ono kwambiri. Dziko lovutika koma moti mukhale olimbika ma. Pemphero koma mbiri zoyipa zokhazokhza.ayi tatopa kumva nkhani zonyasa yesesani kusintha ..

  10. Luck of security due to poor governance since the security gurd are the ones who involved in the situation, what we can do cause we love our country we cant run to exile they also deported us since we will be l foreigners echiiiiiiiiiii aayi shame Malawi!!!

  11. Analosera kalekale,aneneri kalelo (achina yohane).zimangokhala tsoka lake odza ndi choipayo.

  12. ngati ndi umphawi zitivuta, tingopempha mwini chilengedwe kuti adzaweluze. Anthu adzitetezera motani! abale titani kodi? Ambue tilipano ife dzatiomboleni. ciembekezo chathu chilipainu.

  13. mmesa mumati a Peter akulisokoneza zikoli ndiye pot mukufuna ndalama tiyen bac pali ndalama pali magazi ndiye osamadandaula ayi ndizimene timafuna,Noo money no more kudula ziwalo!!!!!to hve money they will take out our pvt parts!!!!!! Thats O

  14. Ayiii, tiwerenge mau, ayesu mukadzaona zizndikiro izi, mudzie kuti ndiri pafupi, tikurira azathu achiarubin pano aierenga kuti akuchedwa koposa kudura maliseche ndie akathaanthu ayamba kuzidula. Aaaaa god atithandize ndthu?? Patonkha takanika??

  15. Hello my name is john I want to give a testimony about my HIV virus that was cured by a great spell caster. Since last 4years I have being a HIV AID patient. I never think I will live long again and am so grateful to Dr sule who help me cured my HIV AIDS last 3 weeks. I was in a great pain so I told one of my best friends; he told me that there is a great spell caster that can cure my VIRUS. I asked him if he had his contact, he gave me his contactl, I contacted him he talked to me and he perform the necessary things and sent it to me through corrier delivery company and deliverd to me at my place and he told me that after two weeks I should go for a test. Which I did, when the doctor told me that am now a HIV negative I couldn’t believe myself I went to see another doctor the result was still the same, I was human on planet earth, so I emailed him and thanked him. Please if you are having a similar problem please visit him/contact him via whatsapp +2348162447651

  16. Zikangopezeka Zigawenga Shaliah Law Igwile Ntchitn Basi. Amalawi Kupusa Tidzasiya Liti Mot Tokha Osawona Kuti Chuma Siziwalo Za Anthu? Mubwele Pachankhungu Ndi Pachezi Mudzawone Azanu Olemela Ndi Ulimi.

  17. AMALAWI NGTI MULUNGU SADALEMBE UZANGO VUTIKA ULELE OLO SINGANO OSATOLA.ODULA ZIWALO IWE UNGOTENGAPO THEMBELELO TAMUFUTSA YESU KUTI UKATHANGE UFUMU WA KUMWAMBA.KOMA UZAPINDULANJI UTAZI KUNDIKILA ZAPANSI PANO PAMBUYO PAKE NDIKULUZA UMFUMU WA KUMWAMBA. Samalila!!

  18. Kumalawi kulibe migodi kapena zitsime zamafuta,musaphimbidwe maso abale ndi alongo.zonsezi atsogoleli a boma amakhala akudziwapo kanthu..pakatipa nsika wa anzathu ma #ALBINO unatentha kwambiri.pano ziwalo zalowa mu chat sopano.takumbukilani nthawi yaulamuliro wa chipani cha UDF.ndiye pano mulungu wakwiya ndidziko lamalawi lero akuti kuna kadansana kkkkkkkk.malawi sopano ili pa number 1 padziko lonse ndi mchitidwe ochita upandu.kadziko kachepelenji ngati mabo oyendela bawo koma eti president wa #satanic kupezeka kumalawiko.COLD HEART OF AFRICA.ndiye Mpanje

  19. amalawi ndichani tangofika pomvetsa chisoni kwambiri, moti mzoona tizitchuka ndikhani zausilu, zochititsa manyazi za kupha albino and kumapitiliza kumadulana ziwalo why?!chifukwa chauphawi? mudzikangolima kudimba agaluinu.

  20. Hmmmmm Akapezeka Wachiwembuy Naye Kuyamba Kumudula Zalaza Mmanja Kenako Kudula Zambuy Kumalizila Mtengo Wakewo 50 50 Game Shit Akuzolowela Alah !

  21. Zoonad Ayambiranso Dzana Kuno Ku Dwangwa Cha 19:25 Hours Pano Odulidwayo Wamwalira Dziko Lathuli Umphawi Wavuta Ambuye Akanangoweruza Dzikoli.

  22. Ku Malawi Anthu Akunja Amalowa Mosavuta, Kamba Kokonda Ndalama Achitetezo Athu, Zimenezi Zikudza Ndi Anthu Obwelao, They Use Malawians Just Last Week A Nigeria National Was Caught At Kia Using Amalawian Passport, The Question Is How Dd He Get The Passport, Aliyense Asamale Ziwalo Dzake Basi.

  23. Eiiish ku Malawi zanyanya eti ngati ali maluzi bwanji osapeza ma ganyu? Mukufuna kulemela chifukwa cha ziwalo za anzanu bas ayi (shame on u)

  24. Kusamala kwake kotani popenza timamvala zovala kusonyenza kuti timazisamala,wangokhala Satan wayenda ndi mwendo yake mu dziko Kathu,dzikolo nde laling’ono koma zochitika zikuluzikulu zokhazokha,kumapeto a dziko.

  25. dzika dzmalawi.tichitepo kanthu.mukagwila chigawenga wotchani mdule khosi muphe.mukamva kuti kwabwela dzigawenga mdela mwanu panganani musake.dzikapedzeka muphele pompo basi.tired of no sence.

  26. Ndinadziwa ine kuti kumapeto kwa ndulidwe kuzafunika maliseche onse osatinso nsonga yokha ayi NDIFE OTSOGOLA TASANKHA NDULIDWE WA MALISECHE

  27. This News Makes Me To Remember The Lucius Banda’s Song Which Says
    Lilikuti-lilikut Mnzanga Dziko Lija? Lomwe Ana An’kangolira Poti Ndiwana Koma Osati Njala..
    Lilikuti-lilikuti Nzanga Dzikolija? Lomwe Anthu Ankangothawa Kuopa Njoka Osat Munthu Koma Lero Munthu Ndiyemwe Akuopsa Kuponsa Mkango
    Moti Ukamayenda Nde Wadeledwa Ukawona Munthu Akubwera M’mbuyomwako Ngati Nkotheka Liyase Ndithu Liwiro Osamudikira Kut Muyende Limodzi Kalezimatheka Koma Pano Nde Ayi Ndinso Ukawona Munthu Akubwera Kapena Wayima Kutsogolo Kwako Koma Ndimadzuro Usanyadire Mwayi Yambiratu Pomwepo Kupemphera Kut Mulungu Akuthandize I Will Ask My Musician Lucius Banda Andibweledzere Kanyimbo Kaja
    Lilikuti Dziko Lija?

  28. Malawi dziko laling’onong’ono ngati fullstop,koma dzichitochito dzokhadzo ndiye ndimaquestion mark okhaokha…kungodzadza anthu otembeleredwa basi….osayamba adula dziwalo dzaodzo kaye bwanji?shame!God forbid!

  29. I dnt care GOD fight 4 mi kma ndimbola bwanj! nebourhood everywr MG tchito, more funds tithane ndi umbandawu!! Malawi is apeace country lets unite mumodzi muli mphavu!!

  30. kodi kwenikweni dziko lathu lamkaka ndi uchi likupita kuti kodi sopano malawi wotchuka ndimtendele uja zikukhala bwanji kodi kodi naye amene akti mtsogoleli wadziko akupangapo chani pazomwe zikuchitikazi mdziko lake kapena zikuchitika zimenezi mumphavu yasatana komatu zimenezi ndimathelo aziko basi

  31. Kkkkkkk komaso kumalawiko kwawonjeza eti?mpaka odula xiwalo?mawa mumva kuti kuli opopa magazi,samalani poyenda angakupopeni.nde odula ziwalowo afuna anthu akhale ndi ma pant achain?

  32. koma kuwaona achita zimenezi omvesa chisoni akuluakulu amalengeza asanacite kuti chaka chino agula galimoto lelo akagula kupolice komweko

  33. ndikhulupirira boma likumva koma poti limachedwa kuyakha limazayakha athu atatha tithandizeni apeter mukanangoti wopha zake aphedwe

  34. Ndizovesa chisoni kuti izi zikuchitika mziko limene anthu ake ndiosauka komaso vuto ndi boma lathu sirilambandira anthu ake akungokangarika kuthesa mphamva za zipani za azawo komaso akunama mulungu akuwawoma siku lina azawa mulungu azawa wocha mulungu sanama

  35. Pankhani yomweyo mwana winaso wadulidwa ziwalo lachiwiri madzulo ku Dwangwa M’boma la Nkhotakota panopa mwanayo ali moyo kuchipatala ziwalozo zili mmanja mwa apolice

  36. pamenepo Boma lichitepo kanthu komaso amene akupangisa ndiye pomfunika ife anthu tiyeni tiziwafufuza akuluakuluwo

  37. Apeter ali bweza dziko layambilaso zamu 2001 zijaso basi tizi enda okonzeka ku phedwa ndiku pha koma mwa chita bwino mwatiphe dulila coz ifeso tika gwila tilibe nthawi yopita ku boma kuka suma tizigwilitsa ntchito mateyala ndi petro tika gwila anthu opanga zimenezi siti ngaka sume ku boma chifukwa gen imeneyi amapanga ndia boma adzingova kuti nduna yawo ya pysa kwakuti choncho npaka adzatope ndikuva zoo ntchedwa

  38. Inu mwadziwa bwanji A MALAWI NEWS 24?nde kuti inunso mulinao mgulumo,komanso pali wamkulu yemwe alinao mgulumo.koma pangakhalitse zizaululika

  39. Owk takumvani amalawi24..tikapangitsa mwado wachitsulo ndetikhomelamo akatundu a2o basi koma mumuuze pitala asamale ndi a2 ake akuwatumao coz mphavu zikuchokera kwa iyeyo

  40. May the power of holyghost fire evil pple. God expose them. We are tired of crying Lord , intervene God we can’t do without you.

  41. nanga zisamalidwa motani ziwalo koposa kuvala mamwado ; zitenje ndi mabuluku, tichite kusoketsa ma underwear a malata?,ndi Wa mmwamba yekha akudziwa komwe dzikoli likupita, ndiyeyo ateteze anthu ake

    1. @Harrison;zikudabwitsatu kwambiri zikuchitika pa Malawi pano mmasiku otsiriza ano ;sitikudziwa kuti chitetezo chikhale motani pa umoyo wa munthu lerolino

    2. -iiiiiii @Nadah; iya tsono pa Electric shock ndiye pakhala kulimbananso pamenepo, odula ziwalowo adzangofikira kutola popanda kulimbana; nanga Shock sichiyamba kuwawula mwini wakeyo ndi ziwalo zake zomwezo

    3. chabwino palibe apo,za masiku otsiriza izi Ife tingovomereza kuti zatipeza mu m’badwo wathu uno kuti tizionere ndi maso za mmalemba

Comments are closed.