Malawian man commits suicide for being HIV positive

Advertisement
HIV Test Malawi

HIV testIt certainly is not a death sentence but it appears a man from Dedza in Central Malawi could just not accept that one can live a full life despite their HIV status.

Information that Malawi24 has indicates that a 44 year-old man on Saturday hanged himself to death in his house days after being tested HIV positive.

The man has been identified as Gerald Phiri.

Police said that Phiri felt sick on 12 August and he went to Golomoti Health Centre where he was tested HIV positive.

“Since being tested HIV positive the deceased has been unhappy,” police said.

On Saturday, the depression got the better of him and he decided to hang himself in his house.

Post-mortem conducted revealed that the death was caused due to strangulation and police say they are not suspecting any foul play over the death.

The deceased hailed from Chagunda village, in the area of Traditional Authority Kachindamoto in Dedza district.

Advertisement

110 Comments

  1. Anzawo ndiye anachilatu mpakana akuyika ma 4n number kuti ngati paliena alinako azafone, kodi wakutuma ndu bushiri eti kkkkk koma ndiwe opusa kobasi ndakukutulukila kkkkk

  2. Mwakangalika kunyoza pamene anatengela HIV mukuti ndi pamkazi inu amenewo poti munayezesa sanakupezenakon muli bho pitilizani kupewa komaso ziwani kupezeka nako kachilombo sichiwelewele chokha ayi.amweneo angolakwisa kuzipha

  3. RIP ngakhale sitidziwa kuti anayitenga bwanji,,,,, tiyeni amalawi tizisunge matsiku ano kwaopsa,, tisayende zip yosegula segula kapena skirt yosegula segula!!! Mapeto ake ndamenewa

  4. Its sad. Government late him down for not providing proper counselling. We are in difficult times there is no need to lough, tomorrow may be your sister, brother,child late teach others for Eventuality.

  5. Hello my name is john I want to give a testimony about my HIV virus that was cured by a great spell caster. Since last 4years I have being a HIV AID patient. I never think I will live long again and am so grateful to Dr sule who help me cured my HIV AIDS last 3 weeks. I was in a great pain so I told one of my best friends; he told me that there is a great spell caster that can cure my VIRUS. I asked him if he had his contact, he gave me his contactl, I contacted him he talked to me and he perform the necessary things and sent it to me through corrier delivery company and deliverd to me at my place and he told me that after two weeks I should go for a test. Which I did, when the doctor told me that am now a HIV negative I couldn’t believe myself I went to see another doctor the result was still the same, I was human on planet earth, so I emailed him and thanked him. Please if you are having a similar problem please visit him/contact him via whatsapp +2348162447651

  6. You people you only know one way of getting the Virus.

    You all think about sex only, according to your comments.

    But there are so many ways of getting that virus, that man he committed suicide by himself maybe because he failed to find out where and how he got it.

    Ngati anali ma plain mukunenawo ndiye udzidabwa bwanji ukapezeka nako?

    Try to understand someone’s side before you judge.

  7. My name is Bogadi kgaogano and this a testimony of how i became HIV NEGATIVE, i have been suffering from HIV for the past four years, i have spend a lot of money finding cure for HIV/AIDS until i found this true man who cured me completely with his powerful herbal medicine, i have tried different means to get this virus out of my body, all the possible ways i tried did not work out for me, i came across doctor olumo through some amazing testimonies concerning how Dr Olumo has cured different people from various kind of sickness like HERPES,HIV/AIDS, CANCER, with the help of his powerful Herbal Medicine, so i was encourage and i contacted Dr Olumo i told him about my Sickness, He told me not to worry that he was going to prepare some Herbal Medicine for me, after some time in communication with Dr Olumo he finally prepared for me the herbal medicine which he sent to me through courier service and he also gave me prescriptions on how to use it, after taking the Herbal medicine for some days, i went for test to confirm and the result was totally negative ,i went for test again in a different hospital still the same negative , Today i am fit and healthy to live life again, I am so happy for the good work of Dr Olumo in my life, if you are having a simillar problem kindly email HIM on { [email protected]} OR CONTACT HIM WITH HIS NUMBER OR CHAT WITH HIM ON (WHATSAPP) (+2348138956767) together we can live an HIV free life.

    1. what do u mean what kind od suicide. suicide is a suicide as long it has sombre connotation of death

  8. Ndizomvetsa chisoni zimenezi, sanakatero ayi, anakalapa kwa mulungu wa kumwamba, ndipo iye amakhululuka. Kutenga matendawa si mapeto a zonse ai koma ndi chiyambi chamoyo wa tsopano. Wadzilanga chifukwa chiyani? Mzimu wake uuse my mtendere. Zandikhuza.

  9. Wacita bo ameneyo kukhala nd aidz mkufakomwe,inu nose ophwanya tangodziphani edzi ithe..ndkanakhala president ndkanalamu asilikali akuombelen mufe nose mumationongela misokhoya2 kumakugulilan ma ARVZ.:-(:-( asshole!!

  10. This then means if all HIV infected people die we can live in the world free from HIV. Hey… What if all the remaining HIV positive people follow what their fellow has done? How many of us can remain? I guess this is the only solution to this infection for rest to live free from HIV/AIDS.

  11. Ndendege, Koma Ameneyu Akanakhalapo Okwana 100, Bwenzi Njala, Kashigeti Kulibe Ndithu, Timuyamikile Pokula Osaziwa Kufusila Nkukafikila Pa Hule Ku Bar. Ndizimenezo

  12. Koma khalidwe lozipha ukapezeka ndikachilomboka lidakadayamba kalekale sibwenzi HIV ilipotu adawa awonesa chisanzo chabwino i can call him a freedom fighter.Ukakamila bwanji kukhalabe moyo pomwe 99% ukunziwa kuti you’re a dead walking person?.Kuuchosa basi upite kwa ena moyowo ambiri akudikila moyo omwewu kuti abwele pa dziko pano.Kuzipha there is nothing to loose.Think wise and deeply guys love your country.Iye anaona kuti achimwa koopsya kuti akhalebe moyo,ena akufesa cholinga kuti azapite ochuluka while dis dude he doesn’t want to take many i congratulate him for what he have done.Palibe wambewu or ukhale padziko pano kkkkkkkkkkkkkkk

    1. Maganizo olakwika amenewo, imfa imadza posawona health status, financial status or social status ya munthu.

      AIDS singathe chifukwa anthu ambil amene akuchita spread matendawa ndi onwe Ali nako koma sakudziwa chifukwa sanayedzetse and sanayambe kudwala.

      Unless u say aliyense apite for compulsory testing & all those found with it r killed regardless of whether they have started getting sick or not. But that would be inhumane, after all ndi ndani sadzafa ? Enanso mwachangu kuposa munthu wa HIV

    2. Is your idea wise enough than mine i think you didn’t understand me so just explain the way u think don’t oppose someone who have contributed his views.Reread my comment again and again then u will understand me.

  13. Let us not insult the self-life terminator. The main Question should be, ”Was he offered a professional post test counselling?” Some VCT personels are so cunning, they do not know how to bring hope for a desperate person. Inquiry and further research must be carried out by even the government so that such cases must be eradicated.

    1. You’re 100% right some counsellors mmmmmm amakalipa man.Amvekele mukuonatu ma results ama plain,apa muzisunga zamatabwa basi kkkkkkkkkkkk mmalo momulimbisa mtima koma akupitiliza kuuphwanyanso

  14. Ugalu wache kkkkk Chitsiru chenicheni cha Munthu anamuuza ndani kuti Munthu ukukhala ndi H I V moyo wathera pompo ? Kamutayeni galuyo Iya !

  15. i feel sorry for him, one cn enjoy good healthy besides kukhala ndi virus ya HIV as far as akuzitsamalira ndikupewa njira zowonjezera ma virus. umbuli ndi matendadi shaaaa

  16. TISEKE KWAKANTHAWI KOCHEPA
    Nkazi wina amafuna kumuyesa
    mamuna
    wake…. Analemba ka note
    nkukasiya pa bed
    iye nkumbisala pasi pa bedi…
    kanalembedwa motele:” Ndanganiza zopita kaye
    kwathu
    kukapuma kwa miyezi iwiri,
    Musale bwino!”
    Mamuna uja atawona kapepala
    kaja analemba mawu ena kuseli kwake. Kenako anatenga
    phone yake……(mamuna pa phone)
    “honey
    Ndikubwera pompano
    Ndizakutenge,
    pumbwa uja wapita kwawo ati mpaka miyezi iwiri
    Ndiye tinjoyatu!” mamuna uja
    atasitha zovala ananyamuka
    kumapita.
    Nkazi anatuluka pansi pa bedi paja
    misozi ukuvumba m’maso
    ngati mvula. Anatenga kapepala kaja
    kuti
    awone zimene mamuna uja
    analemba kuseli
    kwake……. Kunalembedwa kuti: “STOP PLAYING
    SILLY GAMES HONEY, MIYENDO
    YAKO
    IKUONEKERA KUNSI KWA
    BEDIKO. TELEKA TEA
    NDIKUKAGULA ZOMWELA

Comments are closed.