Kamlepo is not done talking: Goes angry on fellow PAC members

Advertisement
Kamlepo Kalua

Vice chairperson of Public Accounts Committee (PAC) Kamlepo Kalua has blasted his fellow PAC members for denying that there are cabinet ministers implicated by a cashgate audit report.

The development comes at a time when the opposition People’s Party (PP) legislator has disclosed to the public that President Peter Mutharika has cabinet ministers who are implicated in the 13 files submitted to the Malawi’s Anti-Corruption Bureau (ACB).

Commenting on the matter, some members from PAC have downplayed Kalua’s claim that the committee has names of the seven ministers believed to have stolen money from Malawians.

Kamlepo Kalua
Kalua rails at fellow PAC members.

But speaking on the local press during a program ‘Views Triangle’ on Zodiak Broadcasting Station (ZBS) on Sunday night, Kalua said that he still insist that the committee has names for the ministers involved in the plundering of taxpayers money.

“Ndalama za boma zabedwa, ineyo ngakhake wa PAC yo akane ine ndilibe naye ntchito… (Public funds have been stolen, I don’t care whether PAC agrees or not) Tsiku lina a Malawi azaziwa choonadi (one day Malawians will know the truth).

“Khaya china chakana, khaya china chikuti chani, ineyo ndikunena zomwe ndaziona, zomwe ndikuziziwa, ndipo sindisiya mpaka ma ministers amangidwe, sindisiya mpaka Ndalama zibwezedwe (I don’t care what others are saying, what am saying is what I have seen and what I know and I will not stop until the ministers are arrested, until the money is recouped),” said Kalua.

However government spokesperson Patricia Kaliati urged Kalua to present the names to the authorities arguing that Malawians need to know people who have been stealing money from public coffers.

“Ndizithu zosangalasa kuti mboni ya boma ilipo kale, a ACB awatenge a Kalua ngati mboni (We are happy that the state already has a witness, the ACB should use Mr Kalua as a witness,” said Kaliati.

Advertisement

92 Comments

  1. Kod kumangolimbana ndiatidye nawo ngat alidi munthu ofuna chilunga ine ndikuona ngat anakaitana yemwe anali kutsogolera ,kod joyce banda alikut bwana ife tikufuna ameneyo enawa sazafuta azanena yekha ,osatibowaso kumangolimbana zinthu zikuvutakale pa nyasa ,

  2. i know kamiepo when i was still young he has got a demonic spirit of fighting with leadership look at his eyes is he a Lil human being kkkkkkkkkk

  3. Awa anadzolowera kunena mabodza ngati akutsusana ndi anzawo amu comet ndiye timve ziti? Kuti achule mainawo akukanika chifukwa ndi zabodza

  4. Tangomumanga ,,,mumuuze kut aulure mayinawo kupanda apo samumasula coz zikusonyeza kut munthuyu akupenga komaxo musaiwalire kut wamisala adaona nkhondo,naziwisa anthu koma chifukwa chot ndiwamisala amaisatira nkhondoyo ndipo adakafera koko,pamene fanz youzidwa ija idamulumuka,so take care kamulepo akuwaziwad anthuwo koma sakuziyendesa mwadongosoro

  5. Those wh r describng Kamlepo as CRAZY,they r themselvs BEHIND THEMSELVES.It is ONL a MAD person wh can CLAP HANDS FOR ppl wh hv STOLEN from them.BE PATRIOTIC NOT SELFISH.Be ASHAMED.May b u had a share of it.

  6. Mambwiye yari Anepa kahikini ejini, Kahikini echilhechilhe mwambe ovonya ochipatara yo mento… Anamavoreyiwa yolha musombweolha…. Ejini too much! kkkk.. Munenowo onisona iseru.. sowera onovoreyiwa khansuwelha…..

  7. Big up Mr. Kalua, help Malawians to arrest the seriously murders. Reveal the truth about cashgate.

  8. He once mentioned about mapwefvupwefvu, secondly the top up of presidential convoy, annual budget convinces IMF not malawians, 7 hyenas in cabinet, all these yeilding us nothing, every come in govt always dont listen to opposition accusations.

  9. i wonder why it takes time to act on the said files?? this the root cause of people saying ur involved.take speedy action pliz as this will iron out those implicated

  10. If he has access to media houses and has the president’s blessing to furnish the public with the names, I would expect Kalua to score this penalty as soon as possible or else we just treat him as one of the best comedian of all time…

  11. Eee zovuta boma likamaba limapha umboni Kapena ma files koma boma likazuzulidwa nchocho pamakhala kuti thawi zina palidi vuto chifukwa usi sufuka opanda moto

  12. Komanso apapa mene zafikamo tiyeni amalawi ,,tizingolimbikira kupemphera ,chfkwa,zandalezi tizangochedwa,panene angonena choncho kamlepo yo,ntchito yake ikuyenda,nanga iweyo ndine tikalozana dzala,ana athu adya???, tiyeni tipange zoti pakutha kwatsi Ku tipeze kajumbo kuti kukhomo mabanja athu apeze kolandila,,that’s all,!!!!!!!

  13. Akamulepo akungozikumbila okha manda fukwa apulezdent anawapasa thawi 24awaz kuti atchule maina mmalo motchila mayina analowesa nyimbo zawo nde musayiwale ndale kkk ndichimozi mozi kusewela ndi infa

  14. kwake ndikulimbana nditsongoleri wina aliyense analimbana ndikamuzu,,, bakili,,, bingu apa ndiuyu akubwebweta ngati mkamwa mulibe manu

  15. Bwanji osampititsa kuchipatala ameneyu nd nthenda yake yakugwayo? Muntha akakhala kut ankagwa pafupafu ali wang’ono akamakulaso amatero zokamba zake zimakhala ngat za mizimu ya anthu akufa

  16. Utsi sufika popanda moto…koma moto uwu suyakapo apa….Kamlepo always talk but nothing he can do…..angofuna morale basi…

  17. we just back up on wat gvt says ,mind u by this time peter seemed to be the right person but he is a big vender .make a revase gea he was involved in the scandal of malawi housing when he was a minister.leave mr kamulepo, he is true

  18. BIG UP RUMPHI PPLE FOR SENDING THIS GUY TO PARLY. ZIKUWONEKERATHU KT ANTHU ACHINYENGOWA ALEPHERA KUMGONJESA NDI ZINDALAMA MPAKA PANO AYAMBA YAWO IJA YOMANGOLALATIRA PA MBC.
    Abusa Mzomera kaya analandira chibanzi. Nthawi yakampeni amaoneka ngat ndanzeru kma pano chibanzi chakakamila pakhosi. Mwina anayambisa mpingo?

  19. I’m sure Kamlepo saw something big, now he wants to put it down.

  20. Am not a fan of PP.but we have to pay credit where it is due. KAMLEPO is a genius he doesn’t fear to speak up when he sees that something is wrong. I remember the Kamuzus time he un blinded us all the Malawians who were folded with the black cloth at that time #Big up Kamlepo we need leaders like you…

    1. Remember he knows the rules and regulations of the government that’s why he is telling the President who is the head of the state and also chief commander to act

  21. Nanga bwanji zina simumatiuza. When comes to other party its about stadiums only. Then when comes to other party “bad publicites” why? Be neutral and fair. Dont take sides. We are the one should take sides not u? Biase journalism.

  22. Cham’sala chinaona nkhondo,chati delu chinaopsa m’lenje.577bilion ili kt? nkhani mukuidziwa koma popeza chala sichiloza mwini.wait and see

  23. ngat pali munthu wanzeru ndye kalua ife tikufuna ndi nduna 7 bas nkhan yatha chilugamo chiwoneke bas pitiliza kamlepo

  24. Sangaiyambe yekha nkhaniyo akudziwapo kanthu, mlekeni ayithe yekha, anatidziwitsa kale za chinsinsi cha boma lakale Lija zomwe amachita a MCP, panthawi yomwe timatenga multiparty yi,
    Samutha amene yo, analephera a abambo Ku Dedza.

  25. Kamulepo is un trusted source of imformation, ma drug omwe amamwa amamusokoneza bongo. Remember that 1986, he went mad @ kazuwe in SA. He back to Malawi due to madness. Sometimes zikamuyamba, amatha kubwebweta. His doctor is mr Samuel Kanyenda, ask him.

    1. If the information which Kamlepo is saying is untrusted why is the President and the entire cabinet so quite. Remember Wamisala adaona nkhondo. And let me ask you Fyson.Why did the parliament voted him into PAC knowing that he is a drug addict?? Why was this so called doctor kept quiet all along?

    2. Mukukana kuti Kamlepo ndi wamisala. Musatengere kuti ali chipani chanji olo kuti amachokera chigawo chiti. He is really a mad man. He talks nosense.

      1. Akaluwa Peter akuti nenani mainawo .vuto ndi Chani nenani mainawo ngati mulinawo apo bi nde ife tivomeleza kuti ndinu akhunyu.komanso iyi ikhala map to a kulongolola kwanu .paja ndikale munayamba kubwebweta zopanda pake sibweni

    3. Kuyerekeza ndi momwe Auditor General wachitira pankhani izi, wamisala sangakhale Kalua. Alipo ambiri omwe apenga kufuna kubisa chilungamo. Tiyeni tikhale chte Mulungu amadziwa zonse. Mwazi wamunthu ndiobvta ndipo ngati chuma chakuba chingawathandize asiyeni nthawi idzakwana nawo adzayankha kwa Namalenga.

    4. Kamlepo talks truth and ua sayin he is mad,ua the one mad aise …Can Peter gv a mad person 24 hrs. Osamangothamangira kubwebweta. Ngat ali wamisala amalankhula zoona. Mukusekelera mbava zikutbera dollar zo.

    1. Mbava siyingaulule mbava izake! We will go to polls without any solution to this! In fact this money will see them into the next govt KKKKKKKKKKK

  26. yesterday I toak about kamiepo that his boby is old enough but his brain is very chirdsh my point is kamiepo is not a leader to read people

    1. unapita sukulu iti iwe mwana wanjoka osaziwa kulemba komwe kapolo wamunthu?. ukayambeso ku primary akukudikira mwina kutheka kukaphunzirako kulemba. asaaaaaaaaa

Comments are closed.