Mutharika bows down to University of Malawi students

Advertisement
Peter Mutharika

Long at last! President Peter Mutharika has finally given in to students’ demands to meet him over the University of Malawi (Unima) fees hike issue.

Peter Mutharika
Mutharika; Will meet the students.

According to a press statement from the presidency, Mutharika will meet students union presidents from constituent colleges of Unima on 4th August 2016 at Kamuzu Palace.

This comes after students from public universities requested for an audience with the president.

In the press release, the president said it has pleased him to grant the students union leaders their request.

The students wrote a letter asking to meet the president over the decision made by the university council to hike fees.

Last month students from the country’s public universities staged protests to express their anger over the fees hike.

Advertisement

83 Comments

  1. Bow Down Means Kuyalama Kosonyeza Ulemu Or Kugwada Kapena Kupanga Zinthu Zosonyeza Kupeleka Ulemu.Koma Pitala Anga…A..A…Gwa,,,,,,deeee!!?.Meeting The Student Is Not Bowing Mwina Akukapanga Clarify Za Hike Dont 4get Kuti Ndi Mphuzitsiso.Nde Dont Cheat Us.Lets Wait What The Meeting Will Bear.

  2. when u want 2 critisize u must follow protocal! mbuzi yanuyi yakupatsani manure kuti atola nkhani anyozedwe! i’ll not entertain!

  3. Nothing tangible will come out from this meeting! Muyesere kupita ndimakani akakuchititsani manyaz muli live pa DPP TV pajatu safuna kukakamizidwa. DPP ikapanga decision basi imakhala yomweyo! Worsestill the Unima council has repeatdly said in the media tthat the fee hike will not be reversed no matter what.

  4. Not too late, its okay. Amalawi ambiri azalemekeza mtsogoleri yemwe aziwapasa Ufa, ndalama, nkhuni, nyama, shuga, buledi, nyumba, chidule ktwapasa ma Services aulere.

  5. you would say he has bow down before students had it been that he has met the demands of the students. Meeting has nothing to do with their demands because we do not know what that meeting will yield. Edit stories before you release dem..

  6. U must be very stupid!. U are afool to post ur story inthis way. Aliyense motima iri mmwamba waiting kuti this whole issue itha bwanji and u are shamelessly potraying the final decision maker as weak.. are u insane..???.. Nkhani iri apatu ndiyama university aukachenjede osati mmakuka mmene mukumaphunzisana za u mpeka nkhani mkumati u are qualified kutola, kulemba ndi kufalitsa nkhani nooo…. Sindingasekere zopusazi. mmalawi ochititsa manyazi iwe.

  7. Nazo nazo atola nkhani apa malawi ngakhale ife aku muzi ndiwosa phuzira tikuziwa kuti BOW NDI KULAMBA nanga apa ziliso pati komaaaa eeee ati ndiye kuziwa nchito kali konse kupotoza maka maka zikangokhuza musogoleri

  8. Nazo nazo atola nkhani apa malawi ngakhale ife aku muzi ndiwosa phuzira tikuziwa kuti BOW NDI KULAMBA nanga apa ziliso pati komaaaa eeee ati ndiye kuziwa nchito kali konse kupotoza maka maka zikangokhuza musogoleri

  9. Anthu opusa sazindikira zina zikamachitika kulola zokambirana sizikusonyeza kuti zonse zatheka President sangagwadire munthu mudziwe mungoyamika enanu mukanaferamo osakumana ndi APM chenjerani mungaonongeke

  10. Anthu opusa sazindikira zina zikamachitika kulola zokambirana sizikusonyeza kuti zonse zatheka President sangagwadire munthu mudziwe mungoyamika enanu mukanaferamo osakumana ndi APM chenjerani mungaonongeke

  11. Bow down ndiye kuti chani? Tamalembani english yabwino not provoking

  12. Inu mpaka bow down a malawi 24? Mau obweretsa ziwawatu amenewa. Tamalembani chizungu chabwino osati zoonongazi

  13. Anthu olemba nkhani ndinu zitsiru ndi ngati cholemba simaziwa kodi munthu walakwaso kumvomera akhale chitsiru????**********

  14. Anthu olemba nkhani ndinu zitsiru ndi ngati cholemba simaziwa kodi munthu walakwaso kumvomera akhale chitsiru????**********

    1. That is not the point. Why he didn’t meet with them longtime ago to avoid protests. How many pple arrested and injured? Finally he has done a good thing. But lets wait the outcome of the meeting. Running away problems wont sort it out, rather sit down and face,discuss the facts and come with better ideas.

    2. That is not the point. Why he didn’t meet with them longtime ago to avoid protests. How many pple arrested and injured? Finally he has done a good thing. But lets wait the outcome of the meeting. Running away problems wont sort it out, rather sit down and face,discuss the facts and come with better ideas.

    3. michael u should know as a chancellor him has his vice and he is not technically more aware of the issue and cannot just overturn any decision by council otherwise the council powers will be robed and would fail to act in any future university cannot be run at state house ka mvuto kameneke ku mw kuno sikadzatha coz univesity is full of politicians no wonder ukapeza a opposition mphuno biii ku university to lead students in sth coz they know if they frustrate the calmness they frustrate their enermies. ..if all public varsities were being managed by ours which is managed by politicians éducation std would hv been very pathetic like ours

    4. michael u should know as a chancellor him has his vice and he is not technically more aware of the issue and cannot just overturn any decision by council otherwise the council powers will be robed and would fail to act in any future university cannot be run at state house ka mvuto kameneke ku mw kuno sikadzatha coz univesity is full of politicians no wonder ukapeza a opposition mphuno biii ku university to lead students in sth coz they know if they frustrate the calmness they frustrate their enermies. ..if all public varsities were being managed by ours which is managed by politicians éducation std would hv been very pathetic like ours

    5. michael u should know as a chancellor him has his vice and he is not technically more aware of the issue and cannot just overturn any decision by council otherwise the council powers will be robed and would fail to act in any future university cannot be run at state house ka mvuto kameneke ku mw kuno sikadzatha coz univesity is full of politicians no wonder ukapeza a opposition mphuno biii ku university to lead students in sth coz they know if they frustrate the calmness they frustrate their enermies. ..if all public varsities were being managed by ours which is managed by politicians éducation std would hv been very pathetic like ours

Comments are closed.