Malawi receives $20 million for fighting hunger

Advertisement
Jill Biden

As people in the country are experiencing acute food shortage, the United States government has announced an additional $20 million donation to Malawi for food relief.

The announcement was made by Dr Jill Biden, wife to vice president of the United States of America after visi

Jill Biden
Biden: Announced the funding

ting hunger resilient projects implemented by her the US government in Machinjiri in Blantyre.

The announcement brings the total of money donated for food aid to Malawi since October last year to $75 million.

In April this year, President Peter Mutharika declared a state of national disaster over food shortages caused by erratic climate conditions.

“I declare Malawi in a state of national disaster following prolonged dry spells during the 2015, 2016 agriculture season,” said Mutharika.

About 14 million people face food crisis in Southern Africa because of a drought exacerbated by El Niño.

Advertisement

89 Comments

  1. Boma timangava zoti kwabwera thandizo pa news kapena pa radio koma komwe kumalowa thandizolo amadziwako ndi PETER ndi wakunyumba kwao

  2. Tingopempha mulungu awakhudze anthu amenewa poganizira mmene anthu akuvutikira ndi njala malawi muno,A tate tichitireni chifundo pofewetsa mitima ya anthu alandira ndalamawa kuti atiganizire amphawife

  3. Kuli Ng’ona Zolusa Ndi Njala Ya Ndalama Kuno Zimakhala Zoyasama Kukamwa Nthawi Zonse Ndalama Zikangofika Zimadya Ndi Ng’onaz Sindidziwa Ngat Ndalamaz Zifike Kwa Anthu

  4. Thus K15 billion kwacha. Sound much bt is not coz it wil be shared amoung the so called oficials. Otherwise the funds could make a big diference. Lets hope those oficials will think beter.

  5. Koma vuto ndlakuti ife osaukafe c mativela koma tilindfundindozoveka zot zthakuthandza, ngat fundo iy ndnanenakuti ngat dziko likukanikakuyenda kambakaumphawi tiyenitingogulitsa tigawane ndalamazo aliyese aziwonakolowa kusyanandkuti ndalamazo muzngodyanokha!

  6. Kuteloko ndalamazo zilowa m’mathumba mwawo zomvetsa chisoni amphawi fe chimangacho sitichiona, yah koma kumwambako kukakhala ntchito pa tsiku la chiweluzo. Allah tikupemphani muchitepo kanthu ndi anthu adyerawo

  7. Hello I’m Samuel Okizou by name, I’m giving a testimony about Dr.Sule the great Herbalist, he has the cure to all manner of diseases, he cured my HIV disease, though I went through different website I saw different testimonies about different herbalists, I was like: “Many people have the HIV cure why are people still suffering from it?” I thought of it, then I contact Dr.Sule via email, I didn’t believe him that much, I just wanted to give him a try, he replied my mail and Needed some Information about me, then I sent them to him, he prepared the CURE and sent it to me via UPS courier service, they told me that it will take 3-4 days before I’ll get the parcel, 3 days later I received the package and I started taking the medicine as prescribed by him, after 7 days of taking the medicine I went for check-up, I was tested HIV NEGATIVE… IF YOU ARE SERIOUS YOU WILL BE CURED!!! contact Dr Sule on whats-app +2348162447651.

  8. Ofcourse sikuti Malawi yalandila chithandizo a president ndi nduna zawo apita Ku UK holiday ndife amphawi maiko anzanthu akutsogola

  9. Ndalamazo ndibwino tonse tigawane aliyense chimanga akagule ekha chifukwa sizioneka bwino. Munva kuti 1 tone ya chimanga imagulidwa 45million. nde kaya masamu ake amayenda bwanji?

  10. I would have loved if that relief food money was channelled through NGOs other than directly to the govt. of malawi, which very much doubt would put it to good use as cashgate elements are still operating at capitol hill. We have so far received a substantial donation from wellwishers that can carry us to the next haversting season.

  11. The word to the president. That money is not for campaign. Its for disaster. We are watching u with an eagle eye. Maulendo chisawawa asiye. We are in crisis. Chimanga cha JB munakana kuti tilandile now u make sure dont take that money to Ndata.

  12. kubwela kwachithandizo kulengeza,mathero achithanizo osalengeza mene zayendela.ndaleee ndaleee ili apo othandiza,othandizidwa palibe ndikuonapo akupanga chaphindu palibe chitasinthe a America nawo ndale kwawoko poti ali muzisankho aMalawi nawo ndalee kufuna kunamizila asauka basi.njala kodi ili kwama mp/presi?mayazi kwaanthu osauka koma palibe osauka olo mumodzi ali mumacommit okhuza chithandizo chabozacho.tinkhani tina timangogwesa ulesi tandaleti.boladi uyo wanena comment yapira.

Comments are closed.