Members of Parliament (MPs) on Thursday passed the Copyright Bill to protect works of art from being pirated in the country.
The new law will see people found guilty of digital piracy paying a minimum fine of K5 million.

Copyright Society of Malawi (Cosoma) board member Rudo Chakwera has since applauded the bill arguing that it will promote art in the country.
Despite authorities getting tough on piracy, the malpractice has over the past years refused to stop being a thorn in the fresh of Malawian artists.
Some artists have been seen moving on personal campaigns of confiscating computers that are used to pirate art music in the country.
While fighting for piracy in the country, Malawi artists blamed government for not putting measures that could curb the malpractice.
61 thoughts on “Beware pirates: K5 Million fine for burning CDs”
Comments are closed.










Agalu inu eti and mwasowa chochita eti? Ife tizibenabe and muwonanso…..with no fear
Kodi Anthu enanu mukudana ndi bill ya piracy bwanji? Ndiinu amene mukumana lumukumaba eti? Mukhauladitu simunati coz ife wil fight for our Artists coz ndikale munayamba kuwabela.Ngati mumafuna kumabena chonde imbani zanu
Hahahaha well sell more to get fine money
H
Kenako umva ukabereka ana opitilira awiri msonkho hiyaaaa Malawi at its best ine kukumbuka voti yokhala yanga kundisenzetsa stress kkkkk
Yalakwatu apa
Piracy is also cashgate but in another form, komanso yaing’ono, ndiyeno gwirani kaye mbava mukugwira nazo ntchitozo kenaka bwerani ku piracy, timayamba kuthana kaye ndi mavuto aakulu then timakathera ku ang’onoang’ono, mwaiwala kodi? mesa ndinu anthu ophunzira inu, don’t run away from your responsibilities, mwatani kodi ma profesor ndi ma doctors? Tiziti school yanu ikugwira ntchito yake apa? Ndakaika!
Mungoti wopezekayo ndi ulendo wa kumanda
Mungoti wopezekayo ndi ulendo wa kumanda
Iyi yokha makape inu munyera manyi,sitisiya
Demeti gwirani kaye mbava…..pc n ma blank cds zonse zanga n kuburnako ndikusaka cash kukana kuba basi muzibwera ndi nzeru zopusazo……. Zopusa basi
that is better alemereko oimbawa
5mili kuitchula mosavuta
Wawa ine siningaleke yayi, ndipitiliza ku burner nithu
cash gaters should get lyf imprisonment then
konzani kaye economy yadziko, gwirani mbava za cashgate zonse zibwenze ndalama, pangani zoti ntchito zisamasowe mdziko muno, kenaka muzilmbana ndi piracy..
Ntchito yi ndinayamba nthawi ya Kamuzu mpaka pano koma sindinapezepo 5 million. Inu ndiye mukuti chiyani?
Ayamba kusewerako ukooo ku Parliament basi atseke mmesa budget inadutsa???
Closed yesterday boss