Man missing after boat capsizes on Lake Malawi

Advertisement
Lake Malawi

Authorities say a search is underway for a man who went missing after the boat he was in capsized on Lake Malawi on Sunday.

Nkhotakota Police Public Relations Officer Sub Inspector Williams Kaponda has identified the missing man as Henry Chirwa who is a fisherman in the district.

Lake MalawiKaponda said Chirwa together with five colleagues went fishing on the lake at Bua Fishing Dock but the boat they were using capsized.

The other five managed to get back to the shore and they were treated as out-patients at Bua Health Centre.

Meanwhile the surrounding communities are searching for the missing person as police in the district have no boat.

Chirwa hails from Makuta 2 village, in the area of Traditional Authority Malengachanzi in Nkhotakota district.

Advertisement

35 Comments

  1. Comments Still Coming Bt I Wonder Pple R Commenting Saying Rip Y? Let Malawi 24 Say So `Rip’ppp Hey We R Waiting For You Kut Mnen Wapezeka Bt ‘He Was Bin Killd.. Shee Bt To Fishermen It Is My Advi To Collect Mor Info Abt Weather Of The Current Day N Anthr

  2. Ngati zachitikira ku senga bay mukuika photo ya anthu ena bwanji? Anthu amene ali pic enafe tikuwaziwa bwino lomwe mmodzi anthu ndimayankhulana nawo dzulo osamatero pic muziika kuchokera mbali imene zachitikira zinthuzo

  3. Nkhani zi mudzinena mbali imene zachitikira chifukwa pic yomwe mwaikayo ndiya azibale anga. Ena mukuti ku senga bay ndi Salima imeneyo koma photo mwaikayo ndiya ku Mangochi monkey bay timva ziti

  4. pepani kubanja lofedwa. But kumalira ndi chiyembekezo coz Onse amene anamwalira Jehova akuwakumbukira mosasamala kanthu kuti anafera Mmadzi. Jehova azawaukitsa.

  5. zomvetsa chisoni zedi,komabe asodzi ena samvera zomwe anyengo akunena,izi zikuthandizira kuchuruka kwamgozi zam’madzi,chonde asodzi tyeni tizimvera mauthenga azanyengo tisadarowe m’madzi,

    1. Choyamba upeze mpingo ndiye umphunzire za chilengedwe cha muthu ndipo udziwe za ife. Ndiye udzadziwa kuti moyo ndi chani ndipo imfa ndichani nanga munthu akafa chimachitika ndichani? Pamapeto pa timupemphe Mulungu kuti akuchotse mu mdima ndikukuika mukuwala. Ameen @ Loyce Kabango

  6. These boat operators must also be going to road trafik to get driving license, trafik ID card, COF of their boats and they must also issue a comprehensive insurance. There’s also need to hav speed trap police officers on the lake. 3 passengers per seat in the boat, and also MRA shud collect road tax from them!

    1. We Are So Tired With These,when We R Driving.You Tke These As One Way To Provivde Money Mwatsalar Pang’ono Tizikupatsani Ndalama Zachitika

Comments are closed.