Malawi naked protests: Winiko presents the petition

Advertisement
Malawi naked protests
Malawi naked protests
One of the protesters denounces attacks on albinos.

Member of Parliament for Mulanje South, Bon Winiko Kalindo, has finally presented a petition to parliament which highly calls for a death penalty on attackers of people living with albinism in Malawi.

MP Kamlepo Kalua received the petition at parliament.

Kalindo sends a message
Kalindo sends a message

The protests was joined by hundred of people, most of whom said expected Kalindo and other leaders to be totally naked.

However, government has indicated it will not accept the calls, something which Kalindo says will fight for even to the last drop of his blood.

He has since called on government to consider the lives of albinos in Malawi arguing that without a functioning directive of death penalty on albinos, it equally means government is not concerned.

We have lots of feedback to come.

 

Advertisement

91 Comments

  1. Ngati anthu akuphedwa inu muzingo yang’ana.sichoncho kwanilitsani utsogoleli .God bless u Hon kalindo amalawi awone utsogoleli waluntha ndi chifundo kudzela mwainu tili pamodzi nanu.

  2. I Salut Winiko Pazomwe Mwachita Ndinu Nokha Amene Mwaonetsa Kusakondwa Kwa Nchitidwe Onyasawu Ithink Tigodikila Boma Kuchichitaapo Kanyhu Big Up Bwana Bon Kalindo

  3. Misala sakopera chifukwa ndi matenda a kumutu. Odwala misala sadziwa kuti wavula ndipo matendawa amagwira aliyese kaya mfumu,kapolo,mfulu. Mpofunika apite nao ku Zomba akayesedwe. Mutha kugaliza akupanga zionetsero koma mzanu atapenga.

  4. It takes people with real courage and concern like Hon. Bon Kalindo. You are one of such freedom fighters for your gesture shows selflessness. Critics will always be there but you have achieved the objective. Bravo honourable

  5. Munthu osadza mavuto a malawi aletsa bwanji kuphedwa kkwa ma albino amalawi munasankha molakwika winiko wawabadwa ndikukulira mmalawi akudziwa za mavuto amunthu koma bwanawo mmmmmm ndi a ku america adziadziwa bwanji ndangodutsa sindinathyole mnkhwani

  6. Do uthink boma lingavomereze kuti munthu ayende maliseche, izi sizingatathauze kanthu pa chitetezo cha alabino koposa kupempha unduna wa za chitetezo kuti akwimitse chitetezo kwa anthuwa. Dont be xtupit m’malo moti mudzikamba za njala ku nyumba ya malamulo mukukamba zovula, cholinga mudzisilirana kuti mudzigonana kufalitsa matenda, STOP THIS POUS.

  7. ndikanakhala ku malawiko Winiko ndikanatenga ndodo ndikukwapula ndi2 kuyalusa Malawi basi MP wa Mulanje kkkkkkkkkk mawa muzavoteso a2 aku Mulanje.

  8. We have to stand as One and Stops the act of kiling and abduction of people with abnism

  9. Ndiye kuti uthenga umapita patali ukakhala maliseche? Kungoyalutsa dziko lathu labwino bwino uku, nanga pamawa anyamatanso akazafuna uthenga ndiye akazavula muzati kutha Kwa dziko shame malawi

    1. Serious kuonetsa zimimba , zimapants azibambo azizukulu zawo, ndiye ana awo akamaona zimenezo mawa akamavula nawonso azatha kuwalangiza?

  10. It’s true that it’s unfair to see our relatives being illtreated. But Protesting while naked (uwunso siumunthu). Ngati boma silimamva, silingamve coz a honourable avula. Just as it is that an albino is just like any other person, how many have been found guilty of committing murder and have been charged with a death sentence? Ine ndangodana ndi kuvulako, umenewunso siukhwiri?

    1. Bola anzakowa awonetsa kukhudzika pazomwe zikuchitikazi sanavule munthu ayi, iwe wapangapo chani? Kusamapweke ndikudzudzula m’malo mothandiza

  11. A winiko anangoda nkhope koma mtima aonetsa apawu ndi woyenera kukhala woyera. Tipemphe a papa wathu atipatse winiko ngati woyera walero kuno kwathu!

  12. That’s what Mr Kalindo have done, showing great concerns to the victims. U n me what have we done? I afford to stay behind u Mr Kalindo. Well done. We want these evil acts to STOP.

  13. Winiko Ndi Wa Drama Zoona. Last Minute Nkunzasintha Akuti Tivale Boxer Nanga Uyo Sadamve Nawo Uthenga Wa Boxerwo Sindiye Kuti Wayenda Bwamuswe. Kkkk

  14. I salute honourable kalindo althought the government will not accept but u have showed that ur concerned and big up bwana ndi Mp yekhayo yemwe akukhunzidwa ndi zonyasa zomwe zuchitika Mmalawi not ma Mp enawa busy kubangulira ma allowances ndima loans God is watching for u

Comments are closed.