Man poisons wife in Lilongwe

Advertisement
Vanessa Thom

The sudden demise of a woman in Area 36 of the capital city Lilongwe has been linked to a number of causes making it hard to establish as to what might have killed her.

The young lady whose name is understood to have been Vanessa Thom but was fondly called Zawo, is reported to have died on Saturday at her Area 36 residence.

Although different versions of the same story have been told through social media, most fingers point at one cause.

Vanessa Thom
Vanessa Thom slain.

Most people believe Zawo was poisoned by her husband while others have strongly refuted the claim. As efforts to get to the root cause intensify, a woman identified as the deceased’s friend has told her side of the story.

She has testified that her late friend was poisoned by her husband who is currently on the run. The bereaved has also warned other girls never to accept the suspected killer’s love proposal.

According to the woman, the suspect already had a wife before hooking up with Zawo. He was renting the Area 36 apartment for her.

However, this remains an unconfirmed Facebook report. The remains of the late Zawo have been taken to her home at Bunda just outside the city.

Advertisement

121 Comments

  1. Thats gud ti hear mwina akazinu mungasiye nchitidwe omakonda amuna okwatila, ife tilipo tili pheee kuchita kusowa nkazi inu mukulimbana ndi amuna aini, amuchita bwino, ndipephelo langa kuti enanunso amene mukuchita zotelezi akuthilileni poison nanu mufe mu dzina la yesu….amen

  2. zonse mwalankhula komanso maganizo anu tawamva koma zoona zake za imfa imenei mulungu yekha ndiye akudziwa mamuna wake wa vanesssa thom sanatengepo mbali pa imfa imenei…!!!! zinakhala chonchi usiku wa pa 17/06/16 anali limodzi monga banja ‘zawo’ amaonera film pa ‘starsat’ mamuna wake anatsanzika ‘honey’ ndukagona mkati mowonera film ‘zawo’ shouted ‘kafa!!!!’ ndi pamene mamuna wa zawo amapita ku kitchen mkupeza zawo wagwa pansi kenako anaitana guard ndi kunyamuzana ‘zawo’ mkumuika mu galimoto ulendo ku chipatala ku abc area47 komwe doctor anawauza kuti mwabweretsa munthu wakufa ‘kafa’ sanakhulupirire izi usiku womwewo ma uthenga anapelekedwa kwa onse oyenera kulandira m’mawa pa18/06/16 mawu thenga atapita mbali zonse anthu angapo tinanyamuka kupita ku area3 police station komwe tinatenga ma cid awiri kenako tinapita ku ‘kch’ komwe kunali thupi la ‘zawo’ akuchikazi ndi amene anabwera ndi maganizo a posmotam anapeza okha doctor yemwe anagwira ntchito yonse kuyesa thupi la ‘zawo’ ndipo panali abale amkazi awiri apolice awiri komanso nduna ya amfumu aphwetekele atamaliza doctor anapereka zotsatira motere malemu wa afa ndi bp komanso anali ndi mimba ya miyezi inayi kuchoka apo tinatenga thupi la zawo ulendo ku 36 kenako linapita ku mudzi kwawo ‘chiseka’ along bunda road maliro anaikidwa m’manda pa19/06/16 mtsikanayu ana badwa 1991 wasiya ana atatu mwana m’modzi bambo ake ndi ‘kafa’ dzina lake JOHN 2yrs old awiriwo bambo wawo sakudziwika mwachidule zomwe ndikudziwa ine monga m’bale wake wa Gilbert kumanja ‘kafa’ ndi zomwezi…..

  3. zonse mwalankhula komanso maganizo anu tawamva koma zoona zake za imfa imenei mulungu yekha ndiye akudziwa mamuna wake wa vanesssa thom sanatengepo mbali pa imfa imenei…!!!! zinakhala chonchi usiku wa pa 17/06/16 anali limodzi monga banja ‘zawo’ amaonera film pa ‘starsat’ mamuna wake anatsanzika ‘honey’ ndukagona mkati mowonera film ‘zawo’ shouted ‘kafa!!!!’ ndi pamene mamuna wa zawo amapita ku kitchen mkupeza zawo wagwa pansi kenako anaitana guard ndi kunyamuzana ‘zawo’ mkumuika mu galimoto ulendo ku chipatala ku abc area47 komwe doctor anawauza kuti mwabweretsa munthu wakufa ‘kafa’ sanakhulupirire izi usiku womwewo ma uthenga anapelekedwa kwa onse oyenera kulandira m’mawa pa18/06/16 mawu thenga atapita mbali zonse anthu angapo tinanyamuka kupita ku area3 police station komwe tinatenga ma cid awiri kenako tinapita ku ‘kch’ komwe kunali thupi la ‘zawo’ akuchikazi ndi amene anabwera ndi maganizo a posmotam anapeza okha doctor yemwe anagwira ntchito yonse kuyesa thupi la ‘zawo’ ndipo panali abale amkazi awiri apolice awiri komanso nduna ya amfumu aphwetekele atamaliza doctor anapereka zotsatira motere malemu wa afa ndi bp komanso anali ndi mimba ya miyezi inayi kuchoka apo tinatenga thupi la zawo ulendo ku 36 kenako linapita ku mudzi kwawo ‘chiseka’ along bunda road maliro anaikidwa m’manda pa19/06/16 mtsikanayu ana badwa 1991 wasiya ana atatu mwana m’modzi bambo ake ndi ‘kafa’ dzina lake JOHN 2yrs old awiriwo bambo wawo sakudziwika mwachidule zomwe ndikudziwa ine monga m’bale wake wa Gilbert kumanja ‘kafa’ ndi zomwezi…..

  4. It is absolute inhuman to keep hearing of murder come each day. Through papers- radios- facebook- homes- murder! murder! murder! What is wrong Fellow citizens? Malawi was known from here and beyond as a God-fearing nation. Where are we heading to? May the good Lord bring back peace in our homes!!!

  5. It is absolute inhuman to keep hearing of murder come each day. Through papers- radios- facebook- homes- murder! murder! murder! What is wrong Fellow citizens? Malawi was known from here and beyond as a God-fearing nation. Where are we heading to? May the good Lord bring back peace in our homes!!!

  6. kodi olo nafesotu amunafe titha kumwesedwa mankhwala osamangoti akaziwa atengerepo phunziro ifeso ndolakwa sitimakhutitsidwa ndi mkazi mmodzi

  7. Mw24 is one among idiots papers in this country,they report things not based on facts.See their heading and the story,imbecile reporters.

  8. Eshiii,,,, nthawi ikakwana yakwana basi,,,, mulungu akangoona mu mtimamo kuti ndimotani,,,,,Aliyense ali ndi njira yake yopitila kumwamba,,,, Tiyeni tidzingokhala onkonzeka nthawi zonse,,,poti imfa imabwera ngati wakuba!!!

  9. koma zina zikamachitika abale mamuna ameneyu mmene amkamukondela mkazi ameneyu I can’t believe kuti wamumwetsa tamek ndakhala ndikucheza nawo kukumana nawo pa border akamakaombola katundu ali limodzi zawo mayi ako alire bwanji mzimayi wa mkono umodzi you were like other arm to her may your beautiful soul rest in peace

  10. wafera zi ntchito zake uyo nanga inu muzafera pa ntchito yanji?

  11. “”Chodabwitsa pankhaniyi zamamuna sakunena yemwe ankachita naye tchimolo”” Anaimba kale Mlaka Maliro…Tatiyeni timveko za amuna awiri mukunewo nangatu

  12. Akazi simumva kukonda ndalama nzanu wafa uyu ena mutengelepo phunziro osamangoti bola mamuna ali ndindalama. Ena mukuchezera kuyamwitsa njoka kufela ndalama

  13. Very bad and sad news. analakwa chani mwana wam’kazi mkazi okongola ngati uyu?.amuna ena alibe kaso wati? KUMENYA or kumwetsa poison siku solve mavuto am’banja.ngati pena zavuta just leav dem.mmmm nkhani yoyipa

  14. Mkazi wake amadziwatu koma zoti Ali ndi mkazi wachibwenzi ndiponso Kafa timapemphera naye Anglican ya kwa Biwi ineyo koma amaoneka munthu wabwino zoopsatu koma

  15. nkazi wake ndiyemweyu, mamunayo anali ndi mkazi wina uyu anali wachiwiri? anali naye mwana kaya ndiye amaopa ziululika kwa nkazi wake oyambayo basitu

    1. Zikumveka kut waphedwa ndi mkazi nzake coz dat man waz alredy married this gal zikumveka kut analanda mamunayo,,,,dats zomwe ndamva

    2. amuna onsewa bas akalimbe mtima kumayenda ndi mamuna wa mwini?
      wakolola zomwe anadzala
      sungakolole mtedza utalima soya

Comments are closed.