A 35 year-old man has died after hanging himself in his house in Area 24 in Lilongwe city.
Lilongwe Police Station Public Relations Officer Inspector Kingsley Dandaula has identified the man as Moses Zimba.
Dandaula proceeded by saying that the deceased was a motor vehicle mechanic who was staying alone in Area 24.
On Monday at around 5:00 in the morning his landlady went to his house and found Zimba hanging on the roof of the sitting room.
“The matter was reported to Kawale Police who visited the scene and took the body to Kamuzu Central Hospital (KCH) mortuary pending postmortem,” said Dandaula.
The deceased hailed from Kachenga village in the area of Traditional Authority (TA) Kachenga in Balaka district.
Meanwhile, Police are advising the general public that if there are issues that are affecting them it is best to seek advice from relevant channels such as faith leaders, marriage counselors or from the Victim Support Unit of Police.
53 thoughts on “Man commits suicide in Lilongwe”
Comments are closed.

Iiiiiii ndine mbuli pankhani imeneyo.
Bodza sanaziphe yekha, moses ndi anali brother wanga weniweni, brother wanga waphedwa then they hanged him kuti ikhale ngati suecide, a police awa ndi opusa akulephela kufufuza kuti apeze omwe
So sad!! May his soul Rest In Peace.
Eee koma ndizoonadi mukunenazi man? Sorry kwambiri
Ndi zoona moses cud not kill himself nomata what koma apolice awa kaya, we are not safe here.
So why not tell them
Iwenso sukuziwa munthu woti waphedwa ndikukolekedwa pachingwe position imasiyana ndiwozikhweza yekha mbuli ndi iwe sukudziwa ndie osanyodza cops wamva???
Akuiziwa nkhanyi tinawauza nothing has been done lelo akuti wazipha zikundwawa kwambiri.
A charles zikomo mulungu akupaseni moyo wautali.
Sorry.
muzwona khani zonyoza man,sory ma braza
Man koma ngati muli ndiumboni okwanira kadandauleni kwina.Pepani!!
Koma zimawonetsa kuti anazimangilira ineyo ma pic ake ndinawaona
h cud not kill himself no Mata wat?????learn to know dat omwe amazipha ndi omwe amaoneka ofatsa oukonda moyo……from pics wazikwizinga yekha…….
Za ziiiiiiii kaya wachita kuphedwa or kudzipha nde mudandaulanji iyaaasss upusa eti
Ogo!
Ogo ineeee
Thanx you kwambiri zikomo very much@ danta chikomora
Welkom
R I p
Bwanjinso amose?
Mara why,Jesus loved you so much and He die 4you but you decided to die like dog,yhoo!
Sidala kma nthakati zimangoimilirapo guyz
wathawa mavuto pa nyasa mozeh,rest in pieces not in peace
nde kuti ntengo wa lendi unali odula z ithink nyumba zake zinali zosadotha komaso sizinali za maudzu. inamangidwa ngati ya ku 47.
Aaaa yose man yayudasi penapake imatha kubwela bad man vayan pantumbo panuso man .
Kumeneko ndiye kukhuta mgaiwa wandiwo chigwada
amoze bwanji? ndimavuto anji m’paka kufika pozimpha?basi tikakupezani mani!! yamereyo kkkk
Amose kukhuta zinafika pati
KKKKKkkkkii kuchosamoyotu sidzimavuta koma kuti ubwelere umenewo eeeee waitha man # moses tikupeza konkooooooo?
Iiiiii js wait for my comment.
Bwanjiso Amoze …..
hey nd chan kod amalawi
hey! Chinekewoooo igwe must here this