Breaking: Date set for naked demos

Advertisement
Breaking News

Breaking NewsDate for the demonstrations aimed at forcing Malawi President, Peter Mutharika, to sign a death sentence for people found guilty of killing people with albinism have been announced.

According to a statement Malawi24 has seen, the demonstrations which will see people walk naked will be done in Lilongwe.

The statement which has been released by Member of Parliament for Mulanje South Bon Winiko Kalindo indicate that the demos will be held on the 23rd of June 2016 with marchers staging their naked parade from Lilongwe Community Centre to Parliament building.

The statement has further said that all those who feel ashamed to have their private parts broadcast to the public should put on red underwear.

Malawi24 will keep you informed.

Advertisement

108 Comments

  1. bravoo winiko, thats what we call commitment

  2. Anthu nkumati winiko wapenga winiko mzeru zatha, koma ndikuona ngati ameneyi akuziwa chimene akupanga ofcourse kuyenda malisecheko nkochitisadi manyazi koma guys tiyeni titenge drama nkuisiya apo, munthuyutu sikuti umunthu alibe ali nawo ndithu i think akuziwa chomwe akupanga munthu wamzeru zake sangakakamire mtunda opanda madzi, remember wamisala anaona nkhondo, Nkanakonda nkadakharapo ndithu

  3. These are last days. There is nothing mostly respected than private parts. I fully agree to the aim of demo but abandon nakedness coz its crazy.

  4. Ife tizakondwa kukajambula maliphyata a tiziwakumbukila akazatisiya. Zopusa eti munthu wanzeru akayende buno bwamuswe dzuwa lili mbee? Koma awa ndi maloza ndithu. Waku mento wakwanapo apa.

  5. ena amayenda mbulanda cos team ya mpira imene amasapota yaluza nde kuli bwanji kuyenda mbulanda chifukwa choti anthu achi albino akuphedwa kukhale kolakwika ine ndidzayenda nao mbulanda palibe kuchitila mwina mbulanda woyeeeee mpaka boma livomeleze opha albino nayenso aphedwe basi

  6. Bola osadzatota opanda chilolezo……..enafe tidzabwera ndi ana musadzatichititse manyazi.

    Komanso onse mudzabwere mutasamba fungo loyipa sitikufuna

  7. Agaru inu muziziyalusa ngakhale muyende naked palibe chingathandize . President ndi amenenso akuyambisa bwanji akungoonelera osachitapo kathu ? And chomwe mukuwaphera anzanu ndi chiani ? Tiyeni nazoni paja mumati mukufuna wophunzira ndameneyotu

  8. kkkkkk ndikanakonda nditazakhalapo koma Eeeee!!! Sindikwanisa zindivutilapo cz ndidakali patali pang’ono kkkkk komano fuso langa n’kumati Ovula malisechewa Azakhala A zibambo okha kapenaso Atsikana azavula nawoso?kkkkk.

  9. Akakanabe pafunika chionetsero cha dziko lonse choti iye atulepansi udindo palowe yemwe angakwanilitse zofuna za anthu .

  10. yaah zowona broo adzalakwitsa kuyenda maliseche awinikowo koma njila imene apanga ndiyabwino kwambilili yademo demo ndiyofunika kwambi

  11. this is narrow minded n stupid!

    this won’t change HE’s mind, otherwise pple nid critical thinking rather than letting mad pple walking naked!

    I wonder wat criteria pple of his constituency chose him? n this may lead to his down fall ,
    walking naked won’t solve anything!

    n alot of pple are just supporting this only to see if he really can walk naked!

    1. quite a good observation u hv there…but hes doing that after realising that the so called government is implementing things on paper and not on the ground…ofcoz he has gone to the extremes but if you would only see how Albinos r being butchered that’s wen u could appreciate what hs up to..the message by hs excellency to stop the killings that’s not enough..It’s just the same as he shld zip his mouth but we longing for action..action is all we need .albinos r pple like us.its no gud that they shld b living in fear no way…i pray one of the ministers shld bore an albino and experience how heartbreaking it is..

    2. u hav a gud thinking2! however those behind the killing have no human spirit, they don’t care about human life let alone walking naked! wat messege are u trying to tell the youths? this is satanic way of solving problems!

      how many pple do u think can do this? many r lyk supporting, but they won’t take part, trust me, this naked parrade! is insane!

    3. What do you want govt to do? Should the president leave his home and start going out hunting for those who are killing the albinos? If that dramatic parliamentarian start walking naked, do you think it will solve the problem? Lets apply logic you as a citizen what are you doing, just sitting back and criticising the govt from a distance? I agree with Chin

  12. Bro Winiko maganizo anu ndi abwino kwambiri kungoti bwampiniyu ndi amene apangise dziko kuti liyaluke. Chikumpangisa ndichani osasayina lamulori b4 naked demo isanachitike. Olemekezeka Mr bwampini ngati inu kholo la dziko la MW imvani kulira kwa ana anu ngati mukuchita mantha kusayina tipaseni chilolezo anamfedwafe tichitepo kanthu kuti inuyo ngati munthu wamkulu mumve zothayitha. Winiko more fire!

  13. For all the possible ways to go about solving this problem, you think being a mad man in the streets would help? Seriously Malawi- why not be serious for once. We need to learn from our neighbouring countries on how they strategically diminished these habits

  14. Hw do u pretect dem in d community cs dose ppo who killed dem stays there? I fully support naked dem for d whole world to force gvt to cum wit concrete solution

  15. Hw do u pretect dem in d community cs dose ppo who killed dem stays there? I fully support naked dem for d whole world to force gvt to cum wit concrete solution

  16. TIYENI NAZO A BRAZ MUKUYITHA TIPANGA ZOMWEZO BASI, MAKAPE AYALUKE

  17. Bravo Kalindo coz u r man of action unlike many who have been flooding the social media with suggestions without any action. We are fully behind u during the demos and we promise our active participation. We cant wait until the last albino dies!

  18. Bravo Kalindo coz u r man of action unlike many who have been flooding the social media with suggestions without any action. We are fully behind u during the demos and we promise our active participation. We cant wait until the last albino dies!

    1. this is action of narrow minded n stupidity! n I hop he won’t win again as a legislator, he doesnt hav constructive ideas!

      next time samthing goes wrong in Parliament will also loby pple to walk naked again! this is stupid!

  19. Koma bambo winiko alimbikilatu zimenezi.. Maganizo awowa oti boma likhazikitse lamulo lonyonga awo opezeka ndi milandu yokupha ma albino.. Ngabwino kobasi chizaipe nde kuzayenda malisecheko…. Kuzakhala kulawula dziko kumeneko tapezani njira ina yowumiliza boma kukhazikitsa lamulo limenelo not zozaenda malisechezo… Musalowetse drama nkhani ndiyayikulu zedi imeneyi

  20. Koma bambo winiko alimbikilatu zimenezi.. Maganizo awowa oti boma likhazikitse lamulo lonyonga awo opezeka ndi milandu yokupha ma albino.. Ngabwino kobasi chizaipe nde kuzayenda malisecheko…. Kuzakhala kulawula dziko kumeneko tapezani njira ina yowumiliza boma kukhazikitsa lamulo limenelo not zozaenda malisechezo… Musalowetse drama nkhani ndiyayikulu zedi imeneyi

  21. We need politics of Principles & maturity +Great developmental. Ideas.We should be able to think & solve our problems with great minds.why do you want to move naked? Because those people who are killing albinos they don’t think wisely.lets protect them in our communities & report any person who want to kill these innocent people to police. Stop that naked stupid. Thing

  22. We need politics of Principles & maturity +Great developmental. Ideas.We should be able to think & solve our problems with great minds.why do you want to move naked? Because those people who are killing albinos they don’t think wisely.lets protect them in our communities & report any person who want to kill these innocent people to police. Stop that naked stupid. Thing

  23. Basi ndikwela ndege ngwisa ndizayende nawo mbulandayo basi nditalimanga lakumanzeleli kuti lizatipe nde ndizalila nankha sikupwetekako

Comments are closed.