Date for the demonstrations aimed at forcing Malawi President, Peter Mutharika, to sign a death sentence for people found guilty of killing people with albinism have been announced.
According to a statement Malawi24 has seen, the demonstrations which will see people walk naked will be done in Lilongwe.
The statement which has been released by Member of Parliament for Mulanje South Bon Winiko Kalindo indicate that the demos will be held on the 23rd of June 2016 with marchers staging their naked parade from Lilongwe Community Centre to Parliament building.
The statement has further said that all those who feel ashamed to have their private parts broadcast to the public should put on red underwear.
Malawi24 will keep you informed.
108 thoughts on “Breaking: Date set for naked demos”
Comments are closed.

Go Konko!????????✔
Nanenso ndidzayenda maliseche wakuntchito.
date set 4naked demos???
Wooooooooooooow tikawone tchende lawankulu ndili pambuyo panu sir winiko
bravoo winiko, thats what we call commitment
Anthu nkumati winiko wapenga winiko mzeru zatha, koma ndikuona ngati ameneyi akuziwa chimene akupanga ofcourse kuyenda malisecheko nkochitisadi manyazi koma guys tiyeni titenge drama nkuisiya apo, munthuyutu sikuti umunthu alibe ali nawo ndithu i think akuziwa chomwe akupanga munthu wamzeru zake sangakakamire mtunda opanda madzi, remember wamisala anaona nkhondo, Nkanakonda nkadakharapo ndithu
plz guys tell me the #DSTV chanel where they are going to air this program coz ineyo ndikufuna ndione #buno_bwamuswe wa winiko
These are last days. There is nothing mostly respected than private parts. I fully agree to the aim of demo but abandon nakedness coz its crazy.
Ndiye pakhala nzele waakazi ndi amuno u can,t be naked male and female apa if ndiyezatundusa nanga tili ku Zambia
Imeneyi ikakhala TRADE FAIR ya akatigole okhaokha
Ife tizakondwa kukajambula maliphyata a tiziwakumbukila akazatisiya. Zopusa eti munthu wanzeru akayende buno bwamuswe dzuwa lili mbee? Koma awa ndi maloza ndithu. Waku mento wakwanapo apa.
ena amayenda mbulanda cos team ya mpira imene amasapota yaluza nde kuli bwanji kuyenda mbulanda chifukwa choti anthu achi albino akuphedwa kukhale kolakwika ine ndidzayenda nao mbulanda palibe kuchitila mwina mbulanda woyeeeee mpaka boma livomeleze opha albino nayenso aphedwe basi
woow!
Bola osadzatota opanda chilolezo……..enafe tidzabwera ndi ana musadzatichititse manyazi.
Komanso onse mudzabwere mutasamba fungo loyipa sitikufuna
Nzelu zimenezi ndizabwino kwambiri nanenso ndikubwela u Malawi Komko ndidza thandize nzanga kalindo kuyenda ili pa mbalambanda neec
Kikikiki ivutatu imeneyi