Malawian man cuts his own neck


Chikwawa

A 25-year-old man in Ntchisi district has committed suicide by cutting his own neck using a panga knife.

The incident happened on Saturday June 4 2016 at Chimkombero Village.

Police have identified the deceased as Leonard Zakalia of Chimkombero
Village in the area of Traditional Authority Malenga in Ntchisi.

Blood.A police report indicates that the deceased who was living with disabilities moulding bricks and after his work he went to his house where he cut his neck using a sharp panga knife.

The deceased was found lying dead blood oozing from the neck.
Police visited the scene of crime and took the dead body to Kamsonga
Health Centre.

Sponsored

Postmortem conducted at Kamsonga Health Centre revealed death was
caused by loss of blood due to a big cut wound on the neck.

*Gladson Mbumpha is Police Publicist for Ntchisi district.

180 thoughts on “Malawian man cuts his own neck

  1. Latani kodi dziko lathu lamalawi abale…likulowera kuti? Kuphana, kudzipha, zingozi ndiye osanena …ambuye atiyendere ife tonse ndi dziko lathu lomwe liyenderedwenso mmmmmm R.i.p

  2. week simatha tisanamve za ku ntchisi ku ntchisi ku matchuka ni nkhani izi: kuphana, kuphedwa. kudzipha. kugwirira ndiyo ntchisi imeneyo

  3. Uyu ayenekela kuti azemba kenakache, mwina aphapo anthu ambiri makamaka ma Albinos. Tsopano awona kuti akapitiliza zokhapakhapa zakezo iyenso azakhapidwa nde wangozipangapo yekhe. yimfa ya plan. siyangozi. ine ndingachite chisoni.

  4. iii ayi koma mbomali ndaona zodabwisa zambiri maka ulamulilo uwu. Kaletu sitinkamva ngati izi. Or kutha kwazikoko langotha kumalawi kokha??????/??

Comments are closed.

Discover more from Malawi24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading