Albino killers arrested in Ntcheu

Advertisement
Albinos Malawi

Police in Ntcheu district have arrested three men suspected of killing Fletcher Masina, a 45-year-old man with albinism, last Wednesday.

Ntcheu Police spokesperson Gift Matewere said yesterday the three were arrested after the law enforcers were tipped off about them.

Albinos MalawiHe identified the suspects as Jussab Saiton, 36, of Zintambira Village, Traditional Authority (T/A) Chakhumbira in Ntcheu, Dou Mkwaila, 49, and Francisco Kamtsimtsi, 40, both from Phumula Village, T/A Kachindamoto in Dedza.

“The three suspects have been charged with murder. However, investigations are still underway,” said Matewere.

The murder of Masina occurred two days before Parliamentarians provided their suggestions on dealing with killings, abductions and exhumation of graves of people with albinism.

Advertisement

160 Comments

  1. Ndigwirizane ndi Arabi wa Leverpool sukunama,kodi chiyambireni cha nkhaniyi Ngati Boma palokha lachitapo chani? Ndipo an2wa amawatulusa pa bail komaso akulephera kuwapana kuti aulure za misika yao,Y? Akuopa kutchulidwamo akuluakulu a maudindo. Komaso malamulo akuno alibe mphamvu nde ife amene zikutikhuza tapanga malamulo athu ongogwirizira podiklira boma kuti likazapanga awo tizasiya ndipo malamulo ali motere:

    Yemwe apezeke ndi mlandu wa izi aphedwe ndi kumuotcha

    Ngati anamangidwa ndipo watuluka pa bail ayenera kuphedwaso

    A malawi tisapusisidwe malondawa Boma likuziwapo kanthu ndipo ena mwa anthuwa ali mu gulu lomwelo nde olo pachedwe ZIZAULULIKA

  2. Im very very disappointed with them let them vanish in thin air how can one think the way of dwindling poverty by killing an innosent person like dat please please we dnt wont to see them in our clean society again even if u can find them not guity but we r not ready to see them again find them a place to live not in our society we not

  3. Eti chapikane kuti walamwile yaka nsano (5) kukaidi,kaneko kwakoposya.Ajimanjaji nambo kwajocha moto. Umi wa mundu ngawa kutenda geni.Yachanasa

  4. apolic amakonda kumanga anthu osalakwa,nanga olakwawa atani nawo? tikuonani kupusa kwanu apolic

  5. Please please Malawians we known as peace loving people stop malpractice of killing our fellow humans,they are like any of us I beg I beg

  6. iwo tsakufuna malbino mungowadula zokozelazo kuti nawotso atsabeleke albino sinanga amawachatsa koma chomwe tingaziwe ndi anthu ngati ife tomwe

  7. So please don’t arest them coz the can’t leave there system of kill the abnal people the best solution is when u find them burn then or kill them as hw they kill the abnal mukuwatsekela mukundamusewu with ur demonstration kuimba nyimbo concerning abnal killings coz u wasting your time in doing that if caught the suspect burn or kill him/her end wy government there ar not seting the strong rule on that issues of kill the abnal please malawi work up we ar losing they of lnnocent people coz of those stupid people u malawians end the government ur a watching of that my Lord our God do something Amen

  8. order yanga apangeni kanyenya mukapanda kutero mdzaphulitsa inu makopolo mmabwana anuwo

  9. idont know what’s going on to Malawi and may be those they arrest the suspect have no Albino children. just think kut mwana wanu wachi albino wapangidwa chipongwe choipachi how do you feal? kubereka mwana nkowawa ndie ena azikakuphera moipaso ngat momwe akuchitilamu anthu amene agwidwawo muwafusitse yemwe akumaatuma then muwapatse anthu athane nawo the best way is to kill all barstad and foolish guys watani mzathu albino? iye simunthu? ndithu ndikanakhala ndili in country ndikanazijoina kupha anthu oterewa ngat kutapasidwa chilolezo nkwabwino kukapsa kumwambako koma kuli koti umamenyera ufulu wa ena

  10. Dziko lavunda ili. Chilango chawo musachite kungowapha once, amve kuwawa, muwamange then muyatse plastic nkumawadonthetsera paliponse. Amve ululu wa imfa amenewo. Shame

  11. Afitiwa ndawaona lero pa MBC TV koma zandimvetsa chisoni coz m’bale waphedwayi ndimamudziwa ine amakhala ku Soche anathawira kwao ku Ntcheu kuopa zomwezo. Ndadaona kuti eish anzathuwa ali pamavutodi eti. The only solution ndikungopeza kumene amakagulitsa mafupawo apo bi sizitha izi tizingophana basi ndipo zikuchititsa manyazi ziko la Malawi ndie kaya mwina ndi AKULUAKULU M’BOMAMU ngati ai tiona ACTION yomwe apange kutidi izi zithe. ZIKOMO.

  12. ndizovuta kunvetsa coz akudziwa ndithu kuti munthu amugwilayo ndiwakupha koma ati akufuna maumbo,maumboni omwe mukufuna ndi achani koposa omwe mwaupezao?ifetu tidakutulukilani inu anthu amum boma zomwe mumachita,zigawengazi mumazituma ndinu nomwe ndipo akazigwila mumapanga njila yoti muzilpulumutsile.njila yake imakha yoti kuhoti amathi kuzilamula kuti zigawengazo ziphedwe or zikakhale kundende moo wao onse,koma inu anthu amum boma mumazitumiza kunja zigawengazo kuti zizikakhala kumeneko.ife timangoti adazipha or zili kundende pamene inu mudawatumiza kunja.njia yabwino yothanilana ndi zigawenga zimenezi ndi kupha anthu akuona ndipo kupha kwake ndiofunika kuwaponya muthobwa loti lili pamoto or else kuwadula chiwalo chimodzichimodzi kufikila ataulula.

  13. Ndili okhumudwa kwambili ndi inu agalu a za human rights. Ife ngati mbadwa zokhudzidwa ndi makhalidwe/machitidwe onunkhawa tikufuna zilango zokhwima kwa fiti zimenezi. Zigawengazi tikazipeza tiyeni tizotche moto osatiso kumakachedwa ku police ndi tima court todzadza ndi oweluza ofoilati ai. Mphavu!!! Ku anthu!!!!!!

  14. Nkhandwe zimenezo zachosa moyo wa nzao(uchifwamba). Zitsilu za ku court zikangopeleka ti zaka 12 zopusa. Plz plz plz tadzituluxani anthu a mmudzi achitenadzo moyenera

  15. I think the key thing here is information, the police needs to know who is buying these body parts and deal with these heartless individuals accordingly, only then are we going to get to the bottom of this…May we as Malawians continue being vigilantes against these devils

  16. Ofunika kuwafunsakuti amakagulitsa kuti? Nangaamawagula ndani? Nde nkuyambira kumeneko kunyongako osati opezeka pa ground yekha ayi chifukwatu kuti tionetsetse ndi chain cha anthu chimenecho.

  17. Apolisi athu ali ndi vuto kuti anthuwa agwidwe ndi anthu akumudzi amene amapeleka imformation koma kenako akagwidwa palibe ndi chimodzi chomwe chimamvekamso.Zimachita kuonekeratu kuti ziphuphu zimalowapo

  18. Gud News Frm You Gues Bg Up Kma Stkufuna Tmve Kt Mwawatlutsa Pa Belo Agalu Amenewawa Coz F U Do Then Chnyengo Chalowato And Death Sentence Period!!!!

  19. Malawi24 follow the proceedings of this matter we need to hear more!keep updating us as the events unfold!To the Police Job wel done ihope you have also included the one buying the parts before coming to the media,we need to get out this together we can!

  20. nkhani ikhale imeneyi Ku Malawi??? izi akutuma ndi Pitala izi,,,, nthawi ya Kamuzu kunali Makako,,, nthawi ya Muluzi kuchosa mano, maso ndi mabele, Muthalika ndiye wabwera ndiyivuta yama Albino shAaaaaaa Malawi sazathekanso basi

  21. Don’t arrest killers,use mob justice period. If not mob justice then throw them into a crocodile infected river then wait till the water is red then leave.

  22. Anthu amenewo alibe chifundo eti? Kodi nkhuku,ng’ombe ndi mbuzi zikuwasowa zomwe akhoza kupha? Let those silly idiots rot in prison 4 the rest of their lives bcoz they’re a disgrace 2 the society,shame on them!

  23. lamulo ligwire ntchito opha nzake nayenso aphedwe poti pamene amapanga zimenezo samamva chisoni nde nawonso ansaveledwe chisoni

  24. Kill dem bomboclaats..let mob justice flow like water

  25. Yaa chilango chabwino ndikuwadula ziwalo koma osawapha ndibwino akalowe kumwamba alibe mwendo kapena diso koma atalapa ndi ena atatengerapo phunziro.

  26. Ndi a Malawi anzathu amenewo osawapha chonde, koma aduleni chabe mitu yawoyo chonde ndagwira mwendo wanu

  27. Aphedwe basi! and should be by hanging . Lamulo lilipo kale death sentence on homicide cases. Sizahuman rights apanso,TISAMVE ZIMENEZO! AFE NDITHU Period!!!

  28. musawanyengelele afiti amenewo akuyenela kunyongedwa basi! Okupha mzake nayenso aphedwe. Abale athu achi albino anakulakwilani chani agalu inu?

  29. Tionera pamenepa ngatii anthu a ku ntcheu ndi a chikondi ngatii akudedza kapena chikwawa,chifukwa madela amenewa zikatere timanyamuka ndikupita ku police konko ,ndikuthyola polisiyo,then ndikuwatulutsa kenako ndikuwachita mob justice kapena kuti kuwapha a police akuona bassi,kadziko konunkha ka Malawi komwe dzigawenga dzimakhala ndi ma rights ochuluka kuposa innocent citizens,mmxxieee,azungu zitsiru ndi amene akupangitsa zimenezi ndi demon class (democracy) yawoyii,dziko lovetsa chisoni,KAMUZU WAS THE REAL PATRIOT.

  30. Vuto lina ndikuliona apa ndiloti zikuoneka ngati ena mwa amene amapanga zachipongwezi amatumidwa ndi anthu odziwika bwino nde ogwidwawo akaponyedwa m’ndende amatulutsidwanso. Apapa pafunika kuti akapezeka basi akayimbe ndi angelo nthawi yomwe

  31. Tikuyembekezera Kumwamba Kwatsopano Ndi Dziko La Tsopano Limene Tidzakhala Mwa Mtendere Inu Zichedwani Ndi Machimo Omapha Anthu Anzanu Nkumat Zikukuyenderan But Dont Fo Get Lif Z Too Short Tasinthani Ndi Nthawi Yotumikila Yehova Mokhulupilika

  32. well done Malawi Police, though it baffles me when i imagine that even if the big fishes are revealed because of their financial muscle in society the dream of bringing them to justice is a nightmare. I have a case in point of mponela and madisi suspects who revealed their buyer to the whole IG of police, but whats the progress?

  33. Ngati ndalama zogulira petrol owotchela palibe tiwuzeni tisonkhe , pangokonzedwa malo ofanana ndi amwenye achibatiya koma Ali awotchela zigawenga zimenezi . Kulimbana ndi ma bwalo amakhoti nkutayisana nyengo .

  34. Kulibe chisoni, ma trial and all that nkungowononga money yaboma, extract info from them basi nawonso adulidwe mmene akuwadulira ma brothers and sisters athu omwe ali ma albino

  35. mufera zayeni anzanuwo pano ali phee inu mukukagwira ndende iwo alemera kodi osaukafe bwanji timangotengeka ndi za ziii

Comments are closed.