Mutharika to appoint MEC commissioners in two weeks

Advertisement
Mutharika facing impeachment calls

The Malawi leader Peter Mutharika will appoint commissioners for Malawi Electoral Commission (MEC) in two weeks time.

Confirming the development, press secretary Mgeme Kalirani said Mutharika is finalising the process and soon the electoral body is to have new commissioners.

Mutharika facing impeachment calls
Mutharika to appoint the commissioners soon.

“The process involves a lot, for instance the intelligence bureau is supposed to scrutinize the names whether they once committed a crime because the law blocks such people from being commissioners,” said Kalirani.

Following the expiry of the terms for MEC commissioners on May 18, the Malawi Electoral Support Network (MESN) has been pressing government to appoint a new team to lead the electoral body towards the 2019 general elections.

MESN argued that the delay will affect prepations for the seventh general elections since Malawi adopted democratic type of government.

Advertisement

32 Comments

  1. Ndi ife amalawi wokonda dziko lathu ngakhale tili kunja kwadziko koma chofunika ndi choti dziko lathu tiliyike mmanja mwa mulungu ndikumapemphera mafuno abwino.ndimalikodwa dziko langa kwambiri,timakhala mokondwa zedi kusiyana ndikumene tilili lero kuno.

  2. kkkkk kodi kusankhàko kwayamba nďi Peter muthalika anasankha mbeñdera ndani nanga anawina chisankho çha 2014 ndani? akongolesi tikudziwa kuti ndinu olephelà ndie musapeze pothawira demet

  3. Dave Chigalu, kkkkkkkkk, ukunena zoona. Zao zimenezo ku Malawi kwawoko. Ine ndili phee pa Capetown, nanga ndi nthawi yoti nkumavutika ndi ndale imeneyi, mmalo moti ndipange zanga.

  4. Dave Chigalu, kkkkkkkkk, ukunena zoona. Zao zimenezo ku Malawi kwawoko. Ine ndili phee pa Capetown, nanga ndi nthawi yoti nkumavutika ndi ndale imeneyi, mmalo moti ndipange zanga.

  5. It must be a pointed independently eaither both opposition party must choose otherwise it will be favouring governing party

  6. Bwanji kuika njira ina yosankhira adindowa ? chifukwa izi ndimaona ngati sizimavuta munthu osankhidwayo kunsangalatsa amene anamusankha ndicholinga chokometsa ntchito yake.

Comments are closed.