All eyes on Nomads new Nigerian signing


Amos Bello

They have perhaps found a new haven  in Nigeria, and now Mighty Be Forward Wanderers have permanently signed another Nigerian by the name Saheed Oluwa Shinaayomi.

Amos Bello
Amos Bello to be joined by fellow Nigerian at Nomads.

The striker has been cleared by the Football Association of Malawi (FAM).

FAM’s International Transfer Matching System Manager, Casper Jangale, has since confirmed of the clearance.

Shinaayomi has been under the watchful eye of Shiba Football Academy.

The Nomads now have Japanese Genki Nakamura who is yet to play in competitive games due to delayed work permit procedures but Nigerian Amos Bello has already been key to the Lali Lubani side so far.

The Nigerian deals have been masterminded by Nigerian legend Jay Jay Okocha according to sources.

154 thoughts on “All eyes on Nomads new Nigerian signing

  1. kkkkkkkkkk congratulations neba. kunja mpaka? mukuitha but problem ndi yoti ma player mukugulao kukabwafu ndi nsulupi gunners aliko ambirimbiri moti amadya thabwa kusowa malo osaziwa ku noma aliko malo awo.koma osadanda ndi chikhalidwe cha2 a Malawi ndi zija zomati sindingakwatire wa chimizi ndagwira wa mtauni ukunena mayi opanga maganyu ochapa kapena ogulisa masamba mtauni osasamba komanso Osaoneka bhoo ndi zomwe akupanga a noma.kkkkkkkkkk umatha neba

  2. Omse othawa Boko Haramu in Nigeria bwerani ku noma akusungani bola mungonama kuti mumasewera mpira basi akutengani,Boko Haramu wecom to Nyerere team yamakape mxieeew! Kodi china chikungodwaladwala chija mumati (nagamura) kapena Jeke? mchani paja ine ndaiwala!

  3. Nomads are really killing malawian football,malawi has not even reached that stage of buying foreign players! instead of kufufuza ma player m’midzimu shame!!

    1. Amalawi amapita kunja kukasewela mpila bwanji? Kumeneko kulibe maplayer midzi mwao oti angasewele ? Kumanganiza , kodi amalawi mumadziyang,anila pasi bwanji? Mudzidziwa kuti ifenso amalawi tikhoza kungula ma player kunja ngati tilinazo zoyenelezazo

  4. Neba uli ndi vuto zampira zimakukanika bola uzikapitiliza kulima kampopi bas,inu ndalama mulibe player wakunja mumpatsa chani,adikire mukagulitse kaye fodya ndi lit limenero

Comments are closed.

Discover more from Malawi24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading