Man sent to prison for stealing from his wife

Advertisement
Arrested

The Ntchisi First grade magistrate court has sentenced a 50 year-old man to 3 years imprisonment with hard labour for stealing from his wife.

ArrestedThe man has been identified by the police as Pearson Phiri from Chikhala village in the district.

The court heard that the convict on July 14, 2014 stole ten 50Kg bags of beans worth 135,000 Kwacha belonging to his wife.

Police later arrested Phiri and charged him with theft which is contrary to section 278 of the penal code.

When passing the sentence, First grade magistrate Dorothy Kalua said the offender deserved a custodial sentence to deter other would-be offenders.

She then slapped the him with a 3 year jail term.

Phiri hails from Chikhala village in the area of T/A Kalumo in Ntchisi district.

Advertisement

105 Comments

  1. MMMMMMMMM MA JURGE AKU MALAWI AMENEWO!!!! KODI NDIYE KUTI MALAMULOWA ANANGOBWELELA ANTHU OSAUKA?

  2. Koma amalawi tafika potengeredwa ku mtonso ngati maliro a njoka tona mulandu wa m banja mpaka 3yrs koma mulandu wa anthu olemera amangoti auyimitsa tonani mulandu wa muluzi wokuba ndalama lero nde ndiyankhula osabisa ma jaji akumalawi nonse mulungu akulangani ndithu mudzingofa zoona zimenezi commentiyi ngati mwawerenga musunge padera sipapita miyezi 4 jaji wina asanadutse MULUNGU wakwiya chifukwa chopereza anthu osauka

  3. Koma amalawi tafika potengeredwa ku mtonso ngati maliro a njoka tona mulandu wa m banja mpaka 3yrs koma mulandu wa anthu olemera amangoti auyimitsa tonani mulandu wa muluzi wokuba ndalama lero nde ndiyankhula osabisa ma jaji akumalawi nonse mulungu akulangani ndithu mudzingofa zoona zimenezi commentiyi ngati mwawerenga musunge padera sipapita miyezi 4 jaji wina asanadutse MULUNGU wakwiya chifukwa chopereza anthu osauka

  4. [READ MY STORY. ON HOW I GOT MY HIV CURED].
    Truthfully, i was tested HIV + positive for the past 8 years. I keep on managing the drugs i usually purchase from the health care agency to keep me healthy and strengthen, i tried all i can to make this disease leave me alone, but unfortunately, it keep on eating up my life. So last Two Months i came in contact with a lively article on the internet on how this Powerful Herb Healer get her well and healed. So as a patient i knew this will took my life one day, and i need to live with other friends and relatives too. So i copied out the Dr Collins the herbal healer’s contact and I contacted him immediately, in a little while he mail me back that i was welcome to his Herbal Home whereby all what i seek for are granted. I was please at that time. And i continue with him, he took some few details from me and told me that he shall get back to me as soon as he is through with my work. I was very happy as heard that from him, as i was just coming from my friends house, Dr Collins called me to go for checkup in the hospital and see his marvelous work that it is now HIV negative, i was very glad to hear that from him, so quickly rush down to the nearest hospital to found out, only to hear from my hospital doctor called Browning Lewis that i am now HIV NEGATIVE. I jump up at him with the a test note, he ask me how does it happen and i reside to him all i went through with Dr Collins. I am now glad, so i am a gentle type of person that need to share this testimonies to everyone who seek for healing, because once you get calm and quiet, so the disease get to finish your life off. So i will advice you contact him today for your healing at the above details: Email ID: [email protected] or you can also add him up on whataspp +2349036950737. CONTACT HIM NOW TO SAVE YOUR LIFE AND DOCTOR ALSO CURE ALL KIND OF DISEASE AND SICKNESS: [email protected] AS HE IS SO POWERFUL AND HELPFUL TO ALL THAT HAVE THIS SICKNESS.

  5. Malawi 24 iiiiiii kkkkkkkkkkk ka mtundu aka ka anthu kamandipasa mphwete bwanji stealing for his wife????? No meaning pliz pliz i cn unlike ur page now coz simuli sryc ai

  6. Mamuna ndi mkazi sabelena ngati banja lilipobe nanga izi zatheka bwanji mpaka kumumanga munthu. Mmmmmmmmm penal code yake iti?

  7. Koma abale munthu amazibera yekha mesa ndi 1body kapena pali nkhani zina zikuluzikulu za banja mwao musatipusitse kkkkkkkk apolice akumalawi shame on u kungomva kuti osauka alibe mau. God will judge u o eeeeee mwaonjeza

  8. Bible teaches us that man and woman are one body when married.So why have you left the other body?That judgement is wrong though iam not a lawyer.lawyers take advantage of the poor people.They are failing to pass judgement on cashgate offenders. Why do you do this??Labour community was better…….

  9. our judiciary system needs Jesus to begin with. Ppo charged wth murder or found wth human parts get lesser jail terms, even those responsible for misappropriating our taxes are hiy wth lighter punishments.

  10. Koma akaziwa penapake ndi anthu osaganiza bwino, nkhan ngat imeneyi mpakana mamuna kukamusumira kucourt!? Ok, can u see nw ur husband has been charged with 3years doing ahard work, do u think is it fair to ur husband? Then u’re going to suffer nw since ur supporting point has gone to exile. Akazinu komanso a court kumaona nkhani zina, nkhan zam’banja ngat imeneyi,timangowaitanitsa ndikuwasonkhanitsa pamodz ndikuwapatsa malangizo abwino oti banja lawo liyende bwino, not reaching @ the extent of imprison a husband with the simple issue like this one.

  11. 2600 muthu mukummika mundende for 5yrs hw possible iz zat Dorothy kaluwa en 50yrs old man for stealing bags of beans did u investgate kuti sanalimile limodzi en whn u sent zat kuind. of old person did u think that mkazi odandaulayo azifuna amuna akeo plz Dorothy u went to ntchisi to wrk nt to put. punishment to our fellow pipo in ntchisi. En its only u Dorothy u got terible gudgement in whole malawi sunave kuti mundende yamalawi is 2 clouded why don’t u sentace them comunty work? Oh maa God Dorothy plz plz we need pipo who think whn they pas chiweluzo I feel sory for ma pipo of ntchis Even Minstry of Justice there quite they don’t ask this woman wht kind of judgement is zat

  12. Stupid women that’s family issue nde njala imupha ameneyo nanga mwamuna ampedza kuti wina

  13. Waba mzake ndindani?panenepo waba ndimkaziyo wamuba mwamuna ndikukamusungisa malo,oti sangamuone kwazaka zitatu iyeyo mkaziyo angapite kundendeko kukamuona?Mkazi uyu waponda mwala

  14. Mwamuna ndi mkazi ndi thipi limodzi apa mwamunayo wangochotsa thumba lina kuyika thumba lina,munthu sadzibera yekha.Kodi adzibambo mumatida chifukwa chani?

  15. Mwamuna ndi mkazi ndi thipi limodzi apa mwamunayo wangochotsa thumba lina kuyika thumba lina,munthu sadzibera yekha.Kodi adzibambo mumatida chifukwa chani?

  16. How can I explain this testimony to the public about a great man who help me out in serious illness I have HIV AID for good 3year and I was almost going to the end of my life due to the way my skin look like all I have in my mind is let me just give up because life is not interesting to me any longer but I just pray for God every day to accept my soul when ever I’m gone lucky to me my kids brother run to me that he found a doctor in the internet who can cure HIV online he help me out on everything, the doctor ask for my details, so he can prepare the herbal medicine for me from his temple after all he ask is done one week later I started getting more stronger my blood start flow normally for 4 to 5 days I start getting Wight before 6 days my body start developing my skin start coming up after 8 days which he told me that i will be completely healed, I went for HIV test and I was tested negative I’m so happy that I can say I’m not a HIV patient if you have HIV/AID or any sickness he can still help you in getting your ex-back to you please contact him via his email: [email protected], or whatsapp him on +2348143143878.

    1. Banja sikuberana,ungadzibere bwanji wekha?? Thanks #Bobby Rio for your extraordinary comment

  17. Ndikudabwa ine Kale pamene boma limalamulilidwa ndi anthu osaphuzira bwino ndipamene zinthu zamayenda bwino koma lero ophunzira achuluka mbola yokhayokha chimakhala chili chani kwenikweni za mubanja salowerera mukukhala ngati ziko la South Africa kuyika malamulo pa azimayi bwanji tangokambani za chuma apa.

  18. Ndikudabwa ine Kale pamene boma limalamulilidwa ndi anthu osaphuzira bwino ndipamene zinthu zamayenda bwino koma lero ophunzira achuluka mbola yokhayokha chimakhala chili chani kwenikweni za mubanja salowerera mukukhala ngati ziko la South Africa kuyika malamulo pa azimayi bwanji tangokambani za chuma apa.

  19. Malamulo adziko lathulo muwawunikilenso bwino zoona munthu angazibere yekha? Mayesa mamuna ndi mkazi amapanga thupi limodzi, nanunso akhoti muzafera za weni mukulimbana ndiza banja la munthu kusiya mbava zikuwononga ndalama za boma. No sence mbuli anyapala inu

  20. Malamulo adziko lathulo muwawunikilenso bwino zoona munthu angazibere yekha? Mayesa mamuna ndi mkazi amapanga thupi limodzi, nanunso akhoti muzafera za weni mukulimbana ndiza banja la munthu kusiya mbava zikuwononga ndalama za boma. No sence mbuli anyapala inu

  21. Choncho bolanso kungokhala Single tu…….hahahaa koma maCourt aku Malawi kuno…Shame on U!!!!…..nkhani zikuluzikulu ndie mpaka zakazaka..ndie kt nkhani zazikulu zimakuvuta kuweruza?..kapena Education-level yanu inalekeza pankhani zazing’ono?………………Bible teaches Us not to Judge others.

  22. Choncho bolanso kungokhala Single tu…….hahahaa koma maCourt aku Malawi kuno…Shame on U!!!!…..nkhani zikuluzikulu ndie mpaka zakazaka..ndie kt nkhani zazikulu zimakuvuta kuweruza?..kapena Education-level yanu inalekeza pankhani zazing’ono?………………Bible teaches Us not to Judge others.

  23. akadakhala-zimayi-tikadava-nkhaza-kwamayi-ndiye-kuti-mayiwa-aponda-mwala-zaka-zitatu-kundende-wachikondi-wawo-Eishiiiiii-bwanji-osangokambilana—

  24. akadakhala-zimayi-tikadava-nkhaza-kwamayi-ndiye-kuti-mayiwa-aponda-mwala-zaka-zitatu-kundende-wachikondi-wawo-Eishiiiiii-bwanji-osangokambilana—

Comments are closed.