Police happy with decline in crime

Advertisement
Police

Malawi Police officers  in the southern region have hailed the decrease in crime during the first three months of this year.

According to police, a total of 6410 crimes were recorded from January to March in 2015 while this year a total of 5687 cases have been recorded over the same period, representing 11 percent decrease.

PoliceSouthern Region Police spokesperson, James Kadadzera said the development is due to massive sweeping exercises and patrols police have conducted this year.

Kadadzera further assured Malawians that the law enforcers will work round the clock to ensure crime is combated in the country.

He also advised Malawians to stop mob justice arguing that the country has a constitution that ensures fair trial to every citizen.

On the cases of increased abductions of people with albinism, Kadadzera said the police have launched a campaign aimed at sensitising people about the malpractice.

Advertisement

18 Comments

  1. Koma inuyo apolisi kudzikondela 2much pa malawi pano ,,kupempha # 1 koma munthu akavutika mummafunanso katangale even akhale odandawula olo olakwilika

  2. Koma zotimamenya anthu ntauni madzulo musiiletu ntchito yanu ndikutiyang’ira osati kumatimenya ife tikuweluka ku ntchito

  3. RA mumalo motumiza ku khoti la zachufundoli tumizani ku MOB JUSTICE KHOTI makamaka zimene zimalimbananso ndi miyoyo yanu mukafuna kuwagwira pokuwomberaninso ndi mfuti zawo. BOMA LIUNIKILENSO NTCHITO YANU. KUMAPHUNZIRO AMAKAKUPHUNZISANI MFUTI, POMWE PANTCHITO AMAKUPASANI ZIBONGA MWINA NGATI KULIKWA MWAYI NDI WA MFUTI MMODZI. KUJA MUKALIMBANA NDI MBAVA 8 ILI YONSE YILI NDIZIDA ZOOPYA KWAMBIRI KUPHATIKIZAPO AMFUTI MWINA 4. MUYITHA NCHITOYO??? MAPETO AKE AMATI INU APOLISI MUKULEPHERA NCHITO.

  4. Inenso ndine wosangalala nditsika kwa chiwerengero cha umbava komabe ndikanakonda kuti chisike mpaka pa 89% chisale 11%. Koma apa chasala ndichambiri 89%. Izi zithakutheka pakakhala ubale weniweni pakati pa aPolisi ndi aMob Justice. APOLISI ZIWANI KUTI SIMUCHEPESA UMBAVA NDI UMBANDA CHIFUKWA MUKAWATUMIZA KUKHOTI KHOTI LIMAKAWASUNGISA KUNDENDE. KUJA AMATULUKANSO NDIKUPITILIZA POMWE ANASIYILA. POMWE MOB JUSTICE IMATHANA NAWO POMPO POMPO KUSONYEZA KUSISA CHIWERENGERO MOONEKELATU. MBAVA ZOOPYA MUZIGWI

  5. How can I explain this testimony to the public about a great man who help me out in serious illness I have HIV AID for good 3year and I was almost going to the end of my life due to the way my skin look like all I have in my mind is let me just give up because life is not interesting to me any longer but I just pray for God every day to accept my soul when ever I’m gone lucky to me my kids brother run to me that he found a doctor in the internet who can cure HIV online he help me out on everything, the doctor ask for my details, so he can prepare the herbal medicine for me from his temple after all he ask is done one week later I started getting more stronger my blood start flow normally for 4 to 5 days I start getting Wight before 6 days my body start developing my skin start coming up after 8 days which he told me that i will be completely healed, I went for HIV test and I was tested negative I’m so happy that I can say I’m not a HIV patient if you have HIV/AID or any sickness he can still help you in getting your ex-back to you please contact him via his email: [email protected], or whatsapp him on +2348143143878.

  6. It is not because of you thieving police dogs; but the reason might be, because of mob injustice people have been giving to your fellow thieves. kkkk!

Comments are closed.