DPP orders police to stop Chakwera rally

Advertisement
Lazarus Chakwera
Lazarous Chakwera
Lazarous Chakwera saw his supporters stopped from meeting him on his arrival.

The opposition Malawi Congress Party (MCP) has claimed that the ruling Democratic Progressive Party (DPP) ordered Police officers to stop its supporters from meeting their leader Lazarus Chakwera at Kamuzu International Airport.

Chakwera who was in Portugal, was stopped from meeting his party loyalists at the airport on Monday.

Party members were also blocked from the first checking point at the airport such that they could not catch a glimpse of their leader.

About 30 officers who were not in uniform but used police cars were seen at the airport trying to scare away MCP members.

Chakwera has since expressed concern over the decision to block him from meeting his party followers.

Meanwhile, the DPP are yet to comment on the matter.

Advertisement

142 Comments

  1. Zachamba eti munayamba lit ndale (MCP) mwawina kangati nanga zolinga zanu ndi chan poti nanga misonkhano munayamba kale kale koma bwanji anthu samakopedwa ndi mfundo zanuzo? Khalani pasi muganizenso mfundo zna zokopela anthu osati kumangoti angwazi angwazi tkhalire zomwezo kambani zna mufunse agogo a Ungapake Zenas Tembo zomwe adaziona mbwelela zokhazokhazi

  2. Ine ndiseka pakuona ndale za .demone calasi .izi zizapwetekesabe mitu mpaka kutha kwaziko!! Abaleanga.vuto si chipani kapena presdent AYI! VUTONLAKUTI tili mu ulilo WA demoni kapena kuti wasatana! Olo MCP ilowe mboma iZ sizitha abale anga!moene zinkhond mmaiko.aaa.komainu!

  3. what does the law say about head of state(president wa dziko)and party presidents.zina tikunenazi ndi umbuli sitiziwa zomwe lamulo likunena.chakwera is a mere party leader ha nothing to do with the provision of security equeted to head of state.this is not time for compain.ndale zanji mukupanga amalawi.

  4. what does the law say about head of state(president wa dziko)and party presidents.zina tikunenazi ndi umbuli sitiziwa zomwe lamulo likunena.chakwera is a mere party leader ha nothing to do with the provision of security equeted to head of state.this is not time for compain.ndale zanji mukupanga amalawi.

  5. what does the law say about head of state(president wa dziko)and party presidents.zina tikunenazi ndi umbuli sitiziwa zomwe lamulo likunena.chakwera is a mere party leader ha nothing to do with the provision of security equeted to head of state.this is not time for compain.ndale zanji mukupanga amalawi.

  6. what does the law say about head of state(president wa dziko)and party presidents.zina tikunenazi ndi umbuli sitiziwa zomwe lamulo likunena.chakwera is a mere party leader ha nothing to do with the provision of security equeted to head of state.this is not time for compain.ndale zanji mukupanga amalawi.

  7. [READ MY STORY. ON HOW I GOT MY HIV CURED].
    Truthfully, i was tested HIV + positive for the past 8 years. I keep on managing the drugs i usually purchase from the health care agency to keep me healthy and strengthen, i tried all i can to make this disease leave me alone, but unfortunately, it keep on eating up my life. So last Two Months i came in contact with a lively article on the internet on how this Powerful Herb Healer get her well and healed. So as a patient i knew this will took my life one day, and i need to live with other friends and relatives too. So i copied out the Dr Collins the herbal healer’s contact and I contacted him immediately, in a little while he mail me back that i was welcome to his Herbal Home whereby all what i seek for are granted. I was please at that time. And i continue with him, he took some few details from me and told me that he shall get back to me as soon as he is through with my work. I was very happy as heard that from him, as i was just coming from my friends house, Dr Collins called me to go for checkup in the hospital and see his marvelous work that it is now HIV negative, i was very glad to hear that from him, so quickly rush down to the nearest hospital to found out, only to hear from my hospital doctor called Browning Lewis that i am now HIV NEGATIVE. I jump up at him with the a test note, he ask me how does it happen and i reside to him all i went through with Dr Collins. I am now glad, so i am a gentle type of person that need to share this testimonies to everyone who seek for healing, because once you get calm and quiet, so the disease get to finish your life off. So i will advice you contact him today for your healing at the above details: Email ID: [email protected] or you can also add him up on whataspp +2349036950737. CONTACT HIM NOW TO SAVE YOUR LIFE AND DOCTOR ALSO CURE ALL KIND OF DISEASE AND SICKNESS: [email protected] AS HE IS SO POWERFUL AND HELPFUL TO ALL THAT HAVE THIS SICKNESS.

  8. A DPP akulakwitsa kwambiri chifukwa nthawi ino siya kampeni,chomwe akuchitila zimenezi ndi chiyani?apa zikusonyezadi kuti zisankho zamu 2014 zija MCP Chipani chafuko m’malawi muno anachibela ma vote!ndipo akuona ngati A MCP Tiwalanda Boma lomwe likuwalephela kulamulilari!ife a MCP sititopa kupanga misonkhano chifukwa cha chipani cholephela ngati Cha DPP pamodzi ndi tsogoleri wawo!pepho lathu ndilakuti tiyeni tipatsane mpata chifukwa nthawi ino siya kampeni!!KWACHAAAA!!!

  9. MCP IDALAMULIRA 31YEARS,NDIYE MUDIKIRE ZAKA ZINA 31.KOMANSO CHAKWELA ZIWA ICHI;ZIKO LINO PRESIDENT NDI MMODZI PETER BASI UDIKILE 2019 WAMVATU.SHUPITI ZAKO.

  10. My psychic readings focus on positive thinking & positive change. It may assist in bringing clarity to a confusing situation, help you prepare for the future in a more focused way and may empower you with positive potential. If you are seeking spiritual guidance with your relationship, marriage, love, family, career, money, health matters, or life’s daily issues, my insightful accurate psychic reading will help you answer the questions that weigh heavily on your mind. I would love to assist you with making the best decisions for your Future. No matter where you live I can help you.Call +27738951830 MUNIL SALEH, I do Whats-App, Face book/munilsaleh, Phone and personal readings.

  11. My psychic readings focus on positive thinking & positive change. It may assist in bringing clarity to a confusing situation, help you prepare for the future in a more focused way and may empower you with positive potential. If you are seeking spiritual guidance with your relationship, marriage, love, family, career, money, health matters, or life’s daily issues, my insightful accurate psychic reading will help you answer the questions that weigh heavily on your mind. I would love to assist you with making the best decisions for your Future. No matter where you live I can help you.Call +27738951830 MUNIL SALEH, I do Whats-App, Face book/munilsaleh, Phone and personal readings.

  12. How can I explain this testimony to the public about a great man who help me out in serious illness I have HIV AID for good 3year and I was almost going to the end of my life due to the way my skin look like all I have in my mind is let me just give up because life is not interesting to me any longer but I just pray for God every day to accept my soul when ever I’m gone lucky to me my kids brother run to me that he found a doctor in the internet who can cure HIV online he help me out on everything, the doctor ask for my details, so he can prepare the herbal medicine for me from his temple after all he ask is done one week later I started getting more stronger my blood start flow normally for 4 to 5 days I start getting Wight before 6 days my body start developing my skin start coming up after 8 days which he told me that i will be completely healed, I went for HIV test and I was tested negative I’m so happy that I can say I’m not a HIV patient if you have HIV/AID or any sickness he can still help you in getting your ex-back to you please contact him via his email: [email protected], or whatsapp him on +2348143143878.

  13. Olakwa ndiye anabetsa Malawi Kupatsa Mfiti yotchedwa Pitala pali vuto apa tiziwona sitinati Amalawi tingokhala One Party System kuti mwina paliponse Pakhare DPP kuti mwina akondwe mokwana

  14. Respect±police u did a mavelous job after all Chakwera is not President of the Nation and being a poliyical leader doesn’t mean he must have a mass rally at National Structural figure such Air port

  15. Koma abakha a DPP mukuwonjeza , mukufuna kupha muthu wa opposition kuti muziba bwino , kapena muzizunzabe amalawi?

  16. All Malawian we cry now about freedom, where is that freedom we leave in those day’s,,, Chifukwa chani tikuvutika popeza lilidzikolathu, musatenge kukhala president Ngat ndi mpando wakunyumba zimemezi usiye iwe wa Dpp “””means Dark people party tisiyeni tikhale ndi mtende omwe tinali nao popeza munapha athu akale ndi chipani chanu kom aaaaaaa sitikukuopani ayaiii tithana ndi inu ngat zakukanikani siyani kuyendesa boma popeza ndiwe nkhalamba? ??

  17. plz tiyeni tiphuzire democrasy ya amathu ku tsidya kwa zambezi .or ususa amaoneka pa tv ya boma,i hope mr president adakulila ku ulaya and he knwz that.bwana ndinu profasir anthu asakusokonezeni inu.

  18. plz tiyeni tiphuzire democrasy ya amathu ku tsidya kwa zambezi .or ususa amaoneka pa tv ya boma,i hope mr president adakulila ku ulaya and he knwz that.bwana ndinu profasir anthu asakusokonezeni inu.

  19. Ok, chakwera’s supporters were not allowed to welcome their leader. Next time when peter mutharika goes abroad his party followers shud not be alowed to welcome him at the airport, only govt officials shud be allowed to do so. I hope the police will abide by what they hav started to level the playing field. This govt must also know that the time to use the police to intimidate opponents is over. We are now in demcracy where pple hav all the right do do whatever they want at any given time provided they are not violating someone’s rights.

  20. palibe chimene chingandipindulirepo apa ndikhale wabwino kwapita kapena kwa chakwela ndiye kuti mutu wanga sukuyenda akudziwana chimene akuchita ndiye kkuti ndizingoika ndemanga zosagwira mutu ndizosayenda

  21. mcp can neva rule this country ndipo musamanamizan pipo sufferd durin the mcp time…chikwera is apastor not apolitcan his role is to drive pipo to salvation he missed God call ndie akulandila punishment pansi popano until he quits this dirty politics

  22. A jafali mukumunena amene ali ku joweni ? Inu mmapanga chani ? Ngati mumagwira mu Office malipiro ake ndi 80000 mwinaso ndachulutsa ngati wa police akulandila 50000 nde wakujowene yopuputa magalasiyo akulandila 180000 ali otsogola ndi uti Vuto mukakhala kuno mumanyoza azathu omwe amapita ku joweni mwinaso simugwira job ndinu atelala tikambe izi zomaletsa ma saporter ako kuti asakulandile pomwe unasowana nawo Apetera ndachitsuruka sindingabakire puludzu wamunthu

  23. Chakwera’s Trip Was Fully Funded By The Instution In Portugal Where He Went To Recieve His Award.No Tax Payers money Here Ndi Zonama

  24. Musachite mantha a Dpp uyo olumala mapewayo sangati tutumuse chotimudziwe Dpp timayikonda ngati m’mene amayikondela anthu ku SA ANC .

  25. Amalawi kumazimvera chisoni zinazi. Amalawi mngafanizire ndi anthu aku south Africa kuchangamuka? Mwatani kodi? Amalawi munthu ali mbuu ntchitu kuwombera manja president bola ndi wakwathu. # a Jafali mwatani msatisanzise apa!

  26. Chakwera ndimalephera kumumvetsa alipo anthu ena anali a ndale ndipo anasiya anatembenuka mtima anasiya zamdziko pano amamtsata Yesu. Koma kumsiya Yesu ndi kuyamba zandale ndi zodabwitsa kwambiri , mundale mulibemo Ambuye!

  27. True. It’s only the high office of the country that can be welcomed by the crowd of people like party members not anybody.
    Suppose an accident has happened, which side of the government can be involved? Automatically it’s the government not the opposition side. That’s what I know, I do not know deeply.

    1. It’s not not so much part of government. And you point it yourself saying “opposition” meaning that it’s duty is to be against. Be wise please.
      Let me ask you ;Can you you jump on, or grab a plastic bag from the hands of your child as he or she appears to your house as the welcome?
      But them can jump on your feet to welcome you, even your wife can do the same to you.

  28. golide ndi ģolide olo kumpaka chitosi adzakhalabe golide ndie inu a kongelesi olo mutapanga ma propaganda otani ku chipani cha dpp a Malawi sitingabwerere mbuyo ķuchikonda chipani çha dpp mwina muźinamidzaña nokhanokha achewa inu koma mtundu wa a Malawi sungamvere zopusa źanuzo ñdiponso màu oti malawi congress party(mcp) musinthe chikhale chewa congress party coz mchipani cha achewa, and chipani çha à Malawi ndi democratic progressive party (dpp) kapeña kuti malawi democratic progressive party (mdpp)

  29. Bwana chakwera yyy mukuyenda kumapita kunja pamene mdziko lino muli njala?????simukuwn kt mukuwnnga ndalama zomwe ndimisonkho yathu??????kodi muuchtapo chani kt njala iri mmalawiyi ithe???

    1. Iiiiiiiiiii ndiye ukuwn ngati boma silimaleka ndalama ku opposition??????????????iiiiiiiiiitsopano umayembekeza kuti anthu tidzingot boma boma boma litipangire pamene amene ndinamuvotera ngakhale sanawine ndimusekerere???????

    2. You are worried with Chakwera’s foreign trips?Kusiyana kuli pati wina ali m’dziko momwe muno koma ntchito zogwira nduna akugwira ndi iye?Do you know how much a local presidential trip costs?Find out

    3. Lonjezo Kachule kulibe akatswiri andale kwathu kuno iwonso ndi andale amafuna kutchuka akamapotoza zomwe aboma achita komanso boma limapereka ndalama kwa leader of opposition

    4. Benson anthuwa sakudziwa cz chomwe adziwa ndikunyoza boma.ineyo ndinavotera munthu wosawina koma akchta zosemphana ndi udindo wake ndisalankhule??????

    5. #robbin u r a gud cat meaus wat u dnt knw…………remember our #chakwera is part of gvt so he s also responsible so no personalisation against my #malawi interest

    6. #robbin u r a gud cat meaus wat u dnt knw…………remember our #chakwera is part of gvt so he s also responsible so no personalisation against my #malawi interest

    7. To #chakwera and #peter akumatisokoneza pamene ena mukuti dpp ena mukut mcp.dziwan kuti zipanizi si peter kapena chakwera cz onsewa anadzipeza so tisiynitse zimenezo and we ordinary members to those partyz no to the peter and chakwera

    8. To #chakwera and #peter akumatisokoneza pamene ena mukuti dpp ena mukut mcp.dziwan kuti zipanizi si peter kapena chakwera cz onsewa anadzipeza so tisiynitse zimenezo and we ordinary members to those partyz no to the peter and chakwera

  30. A rally at airport ? Is it true or false? I think da president himself he dont know da job of malawi police dats y even his late brother he used de police to kill de citizens insted of protecting dem. Police r here to protect not to disturb ppo n u police officers u must say no to rubish.

  31. enanu mumalemba ma coment opanda mutu.akamati ndale ndi chani?akamati ma opposition leaders amatanthauza chani?musiyeni chakwera aliyense ali ndi chipani chake ndiotsatila ake.Anthu akumutsatao ndiomwe ali ma fans ake.Even peter alinaonso omutsatila nde lekani kulemba apa zomunyoza chakwera coz nao apolice amutsata peter coz ali m’boma.Nkhani yaikulu ndi chilangizo ka peter aleke kumapa malamulo omwe mu book lamalamulo amalawi mulibe.

  32. enanu mumalemba ma coment opanda mutu.akamati ndale ndi chani?akamati ma opposition leaders amatanthauza chani?musiyeni chakwera aliyense ali ndi chipani chake ndiotsatila ake.Anthu akumutsatao ndiomwe ali ma fans ake.Even peter alinaonso omutsatila nde lekani kulemba apa zomunyoza chakwera coz nao apolice amutsata peter coz ali m’boma.Nkhani yaikulu ndi chilangizo ka peter aleke kumapa malamulo omwe mu book lamalamulo amalawi mulibe.

  33. koma chakwela akungolimbikila koz he doesn’t know the background kamuzu banda was a dictator aliyese al nd umbon he was killing apolice ankavala makabudula not because kut kunalibe matrouser koma selfishness nthawi ina anakataya anthu mnyanja koz he was opposed now chakwela wathamanga zamupingo et kumat mcp iwina umfuse Kaye john tembo how was the struggle

  34. If GOD planned dat chakwera wil takeover this coming 2018 nobody can change it & if DPP spices up hatred among opposition parties it won’t help the DPP to remain d rulling party!..either DPP or MCP wil take over!!..palibe chamuyaya…malawians r nt going to b ruled by DPP forever!!

  35. Chifukwa chake dziko la Malawi lika kakamira anthu ngati awa adyera ofuna zonse zikhale zawo sitizatukuka lizingosawukirabe, anthu ake ndi omwe omweo lero awasankha ma minister mawa ma ambassador akafoira ati reshuffle antenga ku ministry iyi kukamponya ministry yina choncho anthu ake omwe omweo sitingalemere amalawi.

    Tikazachosa ndale, nde kuti tachosaso dyera ziko lizatukuka.

  36. ku south africa kwakenso kuti iwe, umangokhala nyumba sumayenda kupukuta magalasi nyumba za a zungu. zitsiru zakunozi ungafanizire, ndi aMalawi ozindikira Malema Julius zija amachita ku paliamenti zija ndi zabwino?

  37. Bravo ! we have one good leader in the name of prof.Mutharika.chakwera?who is that one to be welcome at the airport?ufatse wamva!

  38. ngat ndchoncho, achta bwino. Chmene amalawi mungadziwe n’chakut chakwera simtsogoleri wadZKO ayi. Choncho kunali kosayenera kut achpani apte ku airport. Ndbwino kupasana mpata panthaw yomwe amdzathu ali pampando. Ukazichepesa mulungu adzakukweza…inu a mcp n’chifkwa chyan mumakonda zakaduka…mulungu wanu ndiuti kod? Mukane kut nd mulungu wakumwambayu, ine ndikutsutsan kt ay even God himself whom i know, nayenso atsutsa.

  39. Vuto ndi apolice,anasiya kuteteza mzika zonse maso awo ali pa APM.kodi asala masiku angati kuti afe?tanifusilani kwa TB JO.

    1. Nanunso a Flex Mphumulo, tsiku lokufa munthu palibe amadziwa. So don’t say that APM afa tsiku lakuti? lakuti? May be you wil be the first to die before APM.

  40. 1 day they will be cival war in Malawi ,we can’t be treated as foreigners in our own land,john vhilembwe & so many others lost their lives for this freedom,but now u use police to hinder our freedom,watch this out

  41. kod andalenu bwanji ife ayi takana sopusa tinaleka mu2014 muja muzingo mphana bas khaya mupangana chan ife mulibe mwatikwana andale apampanje mukagwele chomwe mukufuna ndikuchuka bas mchukani koma ife mulibe mmenemo

  42. Apm is a disgrace. He is supposed to be a learned man and should act as one. This is a democratic country, if he is not happy with it he should just declare a dictatorship. We shall be just as glad. Mec, you landed us into a frying pan.

  43. These thieves will try all they can to frustrate MCP but to no avail. Instead of sending policemen on the streets to deal with criminals they send the police to harass innocent people at the airport

  44. Stopping some Political Parties on their own Ralies it just mean Muthalika is not matured in Politics.I think this Man need some EdPolitic Educations.
    NOTE:Mr Muthalika what you must know is before there was Dr Hestings Kamuzu Banda he left alive on President.Secondly was Bakili Muluzi he left alive on his Presidency time.Thirdly was your Brother Bingu left his post through death.Fourthly was Joice Banda who left her position after you steal the Votes with MEC,She left her Office alive and she is a common person now.What you must know is the way you treat to other people today you will meet same way down if you will never die like your family brother did.What do think how many cases gone with your brother if he didnt die?

Comments are closed.