Man killed over K200

Advertisement
Police

PoliceA man in Nkhotakota district has murdered his uncle who wanted to collect a K200 debt from him.

According to a witness, the deceased Noah Phiri, 63, went to the house of the suspect, Maxwell Mtenje to ask for his money back.

While at the house disagreements erupted and the suspect hit the deceased who fell down unconscious.

Phiri was taken to Nkhotakota District Hospital where he was admitted and he later died.

The incident was then reported to Nkhotakota Police Station. Police in the district have since launched a manhunt for the suspect.

The deceased hailed from Chiboko village, Traditional Authority Mphonde in Nkhotakota district.

Advertisement

45 Comments

  1. Mvuto ndi maluzi achuluka. Akanakhala kut tsbweniwo analinako ka soap sakanakakumbutsa. Zangochitka chifukwa chakusamvetsetsa kwa mnyamatayo.RIP.

  2. There also reports of kidnappings and killings in this area. The police must keep an eye. I was stopped from visiting a neighboring village on the day the deceased was buried. The fears are quite strong so much so that it will be easy for the police to get some leads. This is the only place in Malawi I have been warned about kidnappings.

  3. Ngongole Ya K200 Moyo Wapita? Ngakhale Soap Osakwana Shaaaaaa!!!!! Maranatha (Ambuye Bwerani Nsanga),

  4. abale zina zikafuna kuchitika siziona thawi kapena nkhanu ihope muthuyo sanali ndi aim yakupha koma satana ndithawi yake yamuthuyi inakwana

  5. What matterz iz how the deseased approched the muderer, mwina analibe cholinga chti aphe mkozi yake, koma tsoka likalimba????!! enao RIP, winayo ASOVA!!!

  6. MK200? MK200? Ndatii MK200??? Mwina maso anga sakuona bwino kapena ndi Mk2000? Kuchofa moyo malume anu chifukwa cha MK200. Apa nde amwene mukajoba yaulele kwazaka zambirikuposelanso ndimumene mukana jobela kubwezeretselapo MK200 ndikuposera mwina MK20,000 kapena MK200,000. Mlandu wa Mk200 mwauthesa tsapano mwalowesapo wa KUPHA. U judges at the courts try to give stiffer punnishments to murderers so that others should learn a lesson. Akakhale kundende 40yrs without presidential paddoning.

  7. UTHENGA WOPITA KWA OSALA: sibwino kukumbutsa ndalama mwamwano kuti anthu akutameni nanga tawonani m’baleyu wangofapo ndi zaziii… IYA KUMANGOVUTA NDIZILIZONSE?

  8. WAKUPHAYO mkuti akumaliza kumene kusuta CHAMBA CHA NKHOTAKOTA,ndie choncho ati LEGALISE GANJA??? tizizaphedwa pokumbusa K50 yatomato ukampeza akubandika.

  9. Koma amalawi muzingophana ngat nkhuku coz of senseless reasons!!!!!!!!!!

Comments are closed.