Prisoners escape from Mangochi prison

Advertisement
Prison

PrisonReports reaching Malawi24 show that seven prisoners have today escaped from Mangochi Prison.

According to Mangochi prison officer in charge Jonas Chimoto, the prisoners escaped between wee hours of one to two o’clock on Sunday using a channel that they had dug at the toilet.

Chimoto added that the channel led a way out of the prison and they dug it using an old axe and knife.

The seven escapees are believed to have been led by two notorious criminals who are answering murder charges.

The remaining prisoners said they were afraid to to alert the warders on duty since the escapees threatened to kill the remaining prisoners if they dared to shout.

Meanwhile, the police have launched a manhunt for the inmates.

(MORE TO FOLLOW)

Advertisement

123 Comments

  1. Shaa zigawenga zovuta azitulusa camma 2am? Tisamale mmacottage plz.

  2. apolice akumalawi ndakutulukila ndinu makape kukuyimbilani 4ni kuno akumba muva kulibe driver kodi simumatha galimoto eeeeti

  3. Koma akayidi athawawa ndiwoti adapha anthu pogwilitsa ntchito zikwanje, m’mawa lino ali kwanuko, ngakhale mukuti achita bwino

  4. Andende amasulidweee!!!,amudima awone kuwala,kundende sikofela,ngati akufa munthu amene ali kunja akuyesayesa kugwila ntchito koma mavuto pwilikiti even njala,ndiye wakundende atani?alimbako?ndiye ngati mpata wapezeka atani?kuthawa kaaaa

  5. [READ MY STORY. ON HOW I GOT MY HIV CURED].
    Truthfully, i was tested HIV + positive for the past 8 years. I keep on managing the drugs i usually purchase from the health care agency to keep me healthy and strengthen, i tried all i can to make this disease leave me alone, but unfortunately, it keep on eating up my life, this is what i caused myself, for allowing my fiance make sex to me unsecured without protection, although i never knew he is HIV positive. So last Two Months i came in contact with a lively article on the internet on how this Powerful Herb Healer get her well and healed. So as a patient i knew this will took my life one day, and i need to live with other friends and relatives too. So i copied out the Dr Collins the traditional healer’s contact and I contacted him immediately, in a little while he mail me back that i was welcome to his Herbal Home whereby all what i seek for are granted. I was please at that time. And i continue with him, he took some few details from me and told me that he shall get back to me as soon as he is through with my work. I was very happy as heard that from him, as i was just coming from my friends house, Dr Collins called me to go for checkup in the hospital and see his marvelous work that it is now HIV negative, i was very glad to hear that from him, so quickly rush down to the nearest hospital to found out, only to hear from my hospital doctor called Browning Lewis that i am now HIV NEGATIVE. I jump up at him with the a test note, he ask me how does it happen and i reside to him all i went through with Dr Collins. I am now glad, so i am a gentle type of person that need to share this testimonies to everyone who seek for healing, because once you get calm and quiet, so the disease get to finish your life off. So i will advice you contact him today for your healing at the above details: Email ID: [email protected] or you can also add him up on whataspp +2349036950737. CONTACT HIM NOW TO SAVE YOUR LIFE AND DOCTOR ALSO CURE ALL KIND OF DISEASE AND SICKNESS: [email protected] AS HE IS SO POWERFUL AND HELPFUL TO ALL THAT HAVE THIS SICKNESS..

  6. Akuluakulu let’s not concetrate on their escape bt on who aided them with materials they were using. However busy u might b dont u supervise n check the infrustractures or akamalowa? As u r aware that prison institutions r different from others whereby pipo r punished n find hard,stiff,difficult life to endure. unlike health, education institutions where pple stay free life. Banthu bachimbira awa nivigewenga vyakofyelapo sono mtovwilenge uli kuti maumoyo ghithu na katundu vivikililike???

  7. Sizachilendo ineyo ndili kumalawi mzanga adaba ndalama za aziphunzitsi nthawi imeneyo asanayambe kuwalipira udzera ku bank. Koma atagwidwa adathawako ku mawula in LLZ. Then ndabwera kuno ku RSA anthu adathawaso ku vereeniging preson why? Wakuba nthawi zonse amakhala wa jakapu.

  8. Apo achita bwino kuthawa ngati woba ndalama za boma amathawa iwo angalephere kuthawa or amati munthu wakuda alibe nzeru amagani moopya muja.

  9. Ine chikhalireni sindinayambepo ndanva kuti ndende ya ku nsanje kapena ya ku lunzu kaya ku kasungu kuti akaidi athawa ayi……koma #mangochi basi ndiye sipamatha mwezi athyola-athyolanso……ngat akuona kuti dzaola osangomanga dzina bwanji???……

    1. Ooooo kodi zafika potukwanizana????……bola ndikanakhala kuti ndaponda pakhomo pako kapena kuntchula dzina lako ndikanati wayenera kutero koma apa pokha wandionjeza m’bale wanga…….stop it!!!!!

    2. Ndipo ku Mangochi last month zinagwidwa zigawenga ndipo nkhani itafufuzidwa zidapezka kut asogoleri ake adali anyamata abeni omwewa. Ndiye ndi momwe zachitikiramu we r not surprised,anyamata abeni omwewo ndiomwe akudziwa game imeneyo.

    3. Kkkkkk……….apapa zangoonetseratu kuti atopa ndi ntchito yawo ndiye sikuti adzingokhalira kumangoguba #pelete kuno nooooo. ..,,,,,, zimafunika onse atachotsedwa ……..mwina tione kuti adzikagubila kuti #beni waoyo

    4. Kkkkk ndiye wina adzabwere kudzandimanga ine ndidzamuthamangitsa moti sadzandifunanso……….nanga ngat anthu akungothawako ndiye kuti awonako chiyani???……..mwina sakudya kkkkkkkkkkkk

  10. Ayende bwino mbava kumalondera zokhazokha kkkkk nzeru zambava zaboma zinachepera kaba.thawani zanzeru akangokupezani mbava mwaithawayo shaaaaa muli madzi

  11. Prison ya mbola imeneyo komanso #maguardjail ake ogunatha line akuidziwa eee mmene ndimaziwala tindende taku Malawi munthu sungathawe chisawawa kalipokalipo

  12. anthu opusa b like achita bwino kuthawa. these are the same pple who will b breaking ur houses in the middle of the night n killing innocent people .

  13. Guyz or mwathawa koma mulibe ntendere muntima nafeso tidziona nkhani tisanaikepo comment athawawo akuti anapha munthu kodi saphaso ena powopa kuwaulula kuti wathawa ku ndende uja ndiuyu ine ndikuti sanapangebwino komaso ayika moyo wao pa chiswe bcoz the can be killed from police or prison officers

  14. Mable Maybe Mhedziso, Clementi Cledow Stima, Pollina Mwanza, Hera Chipeta Roberto Mlenje, Petros Gowoka Nyangulu, Eliardoh Mkwanda, Stan Chitex Chitedze, Esther Kapesi, Chikondi Mugabe, Dali Mgabe, Stephano Samson, Leoh Arnold Chilongo, Mcdonald Josiah Nyangani EMINEM

  15. Anthuwo mmasiya mpaka kumakagula bonya kw M’baluku okhawokha ndiye mmati asathawe? Ndiye mukufuna kumatinamiza kuti athawa podzera mgalande yomwe inakumbidwa ndi zikwanje mbali ya ku toilet? Ngakhale muvutike kuwasakasaka simungawapeze coz onsewo anali ndi mapasiport mmakwawo mwakut panopa alowa kale Mozambique lachiwiri atulukira jonzi

Comments are closed.