Muslims angry after bar plays Islamic music

Advertisement
Ramadhan

Angry Muslims stormed a drinking joint in Chinsapo in Lilongwe on Monday, demanding the bar owner to stop playing Islamic music.

According to Daudi Lulanga, one of the Muslims leaders in the area, the Muslims invaded Chifwafwifwa Pub because they heard Islamic music and Quran recordings coming from the bar.

Muslims-at-prayer-600x399
Muslims clashed with bar owner

The angry Muslims forced the bar owner to stop playing Quran recordings and Islamic songs saying he was tarnishing the image of Islam.

The dispute was reported to Chinsapo Police Unit and officers went to the bar and cooled down the Muslims.

The law enforcers also forced the bar owner known as Mr Chifwafwifwa to delete all Islamic files on his laptop.

The police then assured the Muslim community in the area that they will conduct a campaign to tell all bar owners not to play any Islamic related items in their bars.

Chifwafwifwa has since apologised to the Muslim community in the area for tarnishing the image of Islam.

Advertisement

626 Comments

  1. ku ERITREA 50% ndi asilam pamene50% akrstu koma amakhala bwinobwino molelana koma amalawi mwina umphawi koma zikupindulilani chani poti kaya umunyoza msilamu ,ngat umagona pa saka ukafikilaso pompo nyt ino palibe akulipile

  2. Kaya ndi kumowa kaya sikumowa,gospel music or islamic music should be played,mulungu amatilankhula mosiyana siyana,Saul in the bible was changed ali mu mood yokapha omutumikira Mulungu,ngati mukufuna nyimbo zanuzo asilamu musamazijambulitse ndikumatigulitsa ife,muzingoimbirana nokhanokha…,ndichifukwa chani mumafuna kumadziyeletsa akhristufe nkumatitenga kukhala oipisitsa? Inu ndi ife timakhulupirira zosiyana koma Mulungu mmodzi,mmodzi mwa ife akuyenela kusamala chifukwa ndithu ali wake wa satana

  3. Kaya ndi kumowa kaya sikumowa,gospel music or islamic music should be played,mulungu amatilankhula mosiyana siyana,Saul in the bible was changed ali mu mood yokapha omutumikira Mulungu,ngati mukufuna nyimbo zanuzo asilamu musamazijambulitse ndikumatigulitsa ife,muzingoimbirana nokhanokha…,ndichifukwa chani mumafuna kumadziyeletsa akhristufe nkumatitenga kukhala oipisitsa? Inu ndi ife timakhulupirira zosiyana koma Mulungu mmodzi,mmodzi mwa ife akuyenela kusamala chifukwa ndithu ali wake wa satana

  4. Wina Analap Atamver Nyimb Ya Chikhristu Ku Bar Up To Now He Is A Born Again Christian Akuyener Kuter Remember Ena Samapit Ku Church Or Mosque Kom Ku Bar Alalikiridwe Bas Maimbidwem

  5. Ngati m’dima udetsa kuwala ndivuto limenelo,koma ngati kuwala kuyeretsa m’dima muletselanji kuti uwalitse malo akudawo?

  6. Abale anga zulo ndayankhula kuti chonde nkhaniyu isiyeni… Anzathuwatu umenewu ndimtopola angofuna kuyambana ndife aslam….. Nde chonde aslam siyani kuyambila lero pls

  7. Really I m not a Muslim but it’s so good to RESPECT OTHER PEOPLES CULTURE if u don’t follow that culture don’t undermine the others have a respect like u want to be respected.
    If u can’t RESPECT YOUR SELF don’t go and UnRespect others.
    Come people

  8. guyz mukungoti nyimbo nyimbo. nyimbo yaji ikufunitsa kubwretsa udani kdi ndie kti nyimbo zacisilamu zoletsdwa kuveredwa palipose asilamu azanga musadandaule mwina mkutheka kti nyimbo inaikidwao ikhoza kusitha athu uku akuvina kenaka mkukaamba cisilamu Amen kkkkkkkkkk

  9. Mulungu akukululukilen nonse amene muma yambisa kuyika nyimbo za chisilamu ku bar. Vuto ndiloti mumatiyamba dala tikabwezela mumati ndife oyambisa ziwawa koma apapa mwati yamba. Ngati mumafuna kugwirisana mungoti pepetsa osati kutipwesa m’mitima ndi makomet anuwo.

  10. I remember a joint on the hill side of the highway north of Zomba called The Afghan Bar and Grill run by a so-called Muslim who, I guess, doesn’t know that Afghani Muslims dont touch alcahol.

  11. amene sanachimwepo ayambitse zogendana, and asilamu ena ndamene amayambitsa kuika gospel ku bar koma sagendedwa. Za Mulungu oweluza ndi mwini!! Amen!

  12. Mukwanitsa kumenyera ufulu chipembedzochi? Analephera Saulo zimene mukuchitazo mapeto ake adamenyedwapo makofi ulere ndi ambuye, zotsatira zake adalapa atamenyedwa mbama. Osangolapa bwanji, chipulumutso ndi chisankho chawekha.

  13. aaaa ndechamba ichi iwe ndeosazindikiraka zoona munthu wakuti mutu wako ukungwila bwino bwino ungatenge bible yakho Ku bar kuyamba kwapatsa anthu orenzela uthenga wamulungu anva chani amenewo chifukwa chake anthu anaganiza zomanga ma church kuti anthu azikumanilana mmenemo osati kukachaso

  14. Kwangokhala kusazindikira ngati palimalo oyamba otiuthenga wa mulungu ukagawidwe ndikuphuzisidwa ndendiku bar chifukwa ndikomwe kumakhala anthu osochera angakhale oyimbawo amafunakuti uthenga wawo upite kwaanthuomwe aliochimwa

  15. Komaso kwa ife ma DJ tikumavutika pamane nyimbo zina akumabwera okha kumatipatsa kut azivera kodi tikhale olakwa ndfe ma Dj kapena aslamuwa tiunikilepo bwino pamenepo (with DJ GINTY)

  16. Komaso kwa ife ma DJ tikumavutika pamane nyimbo zina akumabwera okha kumatipatsa kut azivera kodi tikhale olakwa ndfe ma Dj kapena aslamuwa tiunikilepo bwino pamenepo (with DJ GINTY)

  17. Kodi iwowo akapita ku mashabeen ko samavina nyimbo za zipembezo zina?or tryin to bring boko haram kuno u guys makes my lungs full of laughtr

  18. Kodi iwowo akapita ku mashabeen ko samavina nyimbo za zipembezo zina?or tryin to bring boko haram kuno u guys makes my lungs full of laughtr

  19. Be care of God u people wherever u r,u hav to know that judgement day is realy soon coming…come again with stupidty….ndzakuzingan..

  20. Be care of God u people wherever u r,u hav to know that judgement day is realy soon coming…come again with stupidty….ndzakuzingan..

  21. Guyz uthenga wa mulungu umayenera ulalikidwe paliponse komawako nso nkumene kuli athu ochimwa ena akhoza kutembenuka ntima kuzera munyimbo zomwe zikuimbidwa ku bar ko.

  22. Guyz uthenga wa mulungu umayenera ulalikidwe paliponse komawako nso nkumene kuli athu ochimwa ena akhoza kutembenuka ntima kuzera munyimbo zomwe zikuimbidwa ku bar ko.

  23. dere is no problem & the drunkers can make them to change deir long ways itno muslim or christ through the songs so what if some one deai 4 siners ;j who am i to stop the masege from allar? kkk dont clos the door while athers want to enter. ur selfnes people mmm

  24. dere is no problem & the drunkers can make them to change deir long ways itno muslim or christ through the songs so what if some one deai 4 siners ;j who am i to stop the masege from allar? kkk dont clos the door while athers want to enter. ur selfnes people mmm

  25. nyimbo-yo kodi adajambula ndi wa bar-yo? ndiponso z possible kti shehe wina anali atalezera ndiye ndi amene adapempha nyimbo-yo.m’malimbana ndizopanda ntchito bwanji masakha.

  26. nyimbo-yo kodi adajambula ndi wa bar-yo? ndiponso z possible kti shehe wina anali atalezera ndiye ndi amene adapempha nyimbo-yo.m’malimbana ndizopanda ntchito bwanji masakha.

  27. Fotseki y dont u burn that bar.dont provoke us we dont want nonsese.eve yesu anayambitsa zipolowe myelusalemu ataona kuti akupangilamo malonda.ifeso asilamu tapanga zimenezi potsatira yesu khristu. Ngati mungakhuzike ndi chithu chomwe apanga asilamu musanayambe kunyoza ask bible.muzapeza kuti chilichose timachita asilamu zinalembedwa mmabuku amulungu.

  28. Kumeneko nde kuwaputa anthu ,asilamu mwatani ? chibwana eti ,mumamvera nyimbo zanu zokha ? simoyo wabwino umewo ,kungokhala anthu oyipa moyo basi. zandinyasa musazachitenso .

  29. Ngati mwati ochimwa amapezeka ku bar atumizeni abusa anu akalalikile ku barko osati kuika nyimbo zachisilamu zompusa bansi mukuyenela kuthamanga

  30. Those are moslems in my Chinsapo town, why dont they storm Ukhondo rest houses which is contributing to kids and sheikhs breaking the God’s law and dying of HIV? You people of little faith,you are not even sure that your God can fight his own battles. Before it was Chewa tradition now is muslim music in bar. Set ur mind straight believe in ur God, he can fight his own battles if he is real.

  31. musathe mau pokamba kt ma muslim nd osaphuzira nop!!!!ku school tdavayako ,khanie iri yapa ndiyoti ayika bwanj nyimbo mu bar, ????yomwe ili ya halal Dj ameneyo ali ndimwai moti kuno mkuno malawi koma kunakakhala kwinaku #wallah ameeneyi akuyenera shariya law,kkkkk alubain(sadaka) aftrr 40days ndithu,

  32. Kutenga nyimbo zamulungu kukamvela ku bala ndi chimodzimodzi kutenga mowa kukamwela mtchalitchi.nyimbo zachisilamu sichiloleza mowa zimene zikutathauza kuti ku mabala sikupezeka asilamu,ngati wapezeka malamulo achisilamu akuwaphwanya ndipo ndimunthu wochimwa.munthu samanva bwino chinthu chomwe amachikonda chikasokonezedwa,,monga inu mungalore kuti mwana wanu amuchitile zoipa?asilamu amaoneka ngati anthu opanda mtendere chifukwa amapanga umodzi pofuna kuthana ndi zinthu zoononga chipembedzo chawo zimene kuchikhilisitu kulibe koma pankhani ya kupha, ndewu,chigololo ndi zina ananunso muli pomwepo…aliyense akhoza kuchimwa ndi kutembenuka .mukadzafuna kudziwa chisilamu,mudzawelenge malamulo ake osati kungoona zonwe wina akuchita chifukwa nayenso ndiochimwa.pakhani ya mitala ,pachiwelengelo chaanthu amuna alipo ochepa,,nde muzifunse funso kodi enawa azawakwatire ndani aliyense akatenga m’modzi m’modzi..Mulungu analengelanj akazi ambiri? Mudzifunse?

  33. Many just wright for the sake of commenting but their arguments do not hold any water.are we really reasoning here or its a platform to attack islam by expressing our fallacies? Islam will remain islam and may be you dont know that the fastest growing religion islam in the world. People we are not debating here about islam and christianity but we are on the issue above dont be mad with ur stupidity.a malawi muzakhala aphunzira mpaka lit?

  34. Mwini bar sanalakwitse populumukira. munthu mwina ndiku bar komwe ko masiku ano ndimasiku otsiriza mauthenga ayenera kumveka paliponse kumene kuti munthu adzasowe chowiringula pamaso pa mulungu wake kuti mwina angadzayambe kunama kuti nthawi yopita Ku church ndinalibe uthenga uyenera kumveka paliponse ndithu .Inu asilamu asiyeni anthu m’ma bar mu naonso apezemu chipulumutso chao . umbombo ndi mau a mulungu omwe ? Shame eeeeeeeeeeeeee

  35. Guys mukushoshatu boko haram,koma asilamu mukangoyamba zandeu zanuzo tizakuthamangisani mmalawi muno,mukasewere ndi anzanu akupha anthu osalakwa ku nigeria uko.

  36. Guys mukushoshatu boko haram,koma asilamu mukangoyamba zandeu zanuzo tizakuthamangisani mmalawi muno,mukasewere ndi anzanu akupha anthu osalakwa ku nigeria uko.

  37. Kagulu kopembedza mwezi ndi nyenyezi kumphatikizilapo mwala wa Kaba popembedza amayang’ana ku mecca osati kumwamba kwa Yehova..Sapembedza Mulungu wa abrahamu, isake ndi yakobo israeli..Amadziwa kuyeretsa thupi zakunja koma #mtima wao wakuda bii ndi uchimo, zigololo ndi bodza.Akutsatira bodza la makolo awo.. Masalamusi ndie mbali yawo.. Muhammad sangakhale mneneri chifukwa analemphera kusunga Malamulo 10 a Yehova koma anali ndi malamulo ake a mitala, kupha, mafana a mwala wa Kaba, mwezi, nyenyezi mpaka lero safuna kubvomeleza choonadi cha Yesu Khristu kuti ndie njira ya kwa Mulungu wa israeli, Mulungu wa mose, Mulungu wa eliya si mwala Kaba ayi

  38. I always say,islamic is not a religion but a group of wariors or rebelions.They don’t know what peace is all about.However,we as Chrician community must make sure that, we maintain peace according to what our LORD JESUS CHRIST told us.

  39. all muslim we r 2gether. our akufuna Bukuhar itabwera ku MW amangomvera m ma wailes, Tv, newspaper then anthu. kp go ahead on that muona zotsatira zake

    1. Is ok ndie bwera kuno kumangochi mupange play nyimbozo tione siku LL ko mukuwaona kupunsa tipezeni ku MH bas nkhondo mukuifunayo iyambika komanso zomacommenta pa fb ndi zauchikape mungobwera ndikuika nyimbozo mut malo ochimwila anthuo(Bala) bwera mudzalandirdwa kuno MH. sindilemba coz tizingoponyerana mau no prft apa!!!

  40. Musiyika sanu somweso sachikiristo mabaramo ife asilamu tikamapesa kuti mwayika santhu sa muslim tizikumenyani mukafuna kumvera nyimbo santhu musibwera ku sikiti mwamva wana wa adam!!

  41. muslims need to learn nonviolence approaches in order to defend their belief as peaceful! head and tail cannot appear at once when a coin lays down. they are two exclusive events, so is peace and violence.

  42. Enanu mukaika ma comment anu mumakhala ngati oduka mutu bwanji. Just imagine even inuyo akhristunu kuimba nyimbo zauzimu m’bala pali mnzeru pamenepo? chisilamu chili ndi malamulo ake ndipo sazasinthidwa pogonjera munthu ai.Amene simuli asilamunu chonde musatipepusile chisilamu chathu, chili ndi malamulo okwanira osakondela.Ndiye ngati mukuona chanzeru ku chikhristuko kuika nyimbo zauzimu ku bar izo ife sitingalowelere.Munthu akamachoka pa khomo kupita ku bar amakhala ali ozindikila, Ndiye angasinthike bwanji kumvera atalezera.Muziyamba mwaganiza posatengera chipemphezo kapena mpingo.

  43. chisilamu? ndentchito zao palibe bungwe la chisilamu lamtendere nde ndikonkuno ku Malawitu, koma siyawa akuyamba ziwawa?

  44. chisilamu? ndentchito zao palibe bungwe la chisilamu lamtendere nde ndikonkuno ku Malawitu, koma siyawa akuyamba ziwawa?

  45. alakwitsa ngakhale nyimbo zawo sizidziwika mutu wake kkkkk, ngati kuli anthu akupha pa Dziko lapansi ndi asilamu, bokoharram,ashabab,Islamic state zonse zigawenga pa Dziko lapansi NDA silamu. kukana nkhumba koma chigololo, akanzi mpaka 4 achani? tinene kuti zonsezo ndi nthiti zanu kkkk. koma kumwamba ndiye kuli Ku Venture. Pepani lapani kanyimbonso ndi kachani.

    1. If u are not a Muslim don’t put ur stupid comment, we all one pipo please respect urself

  46. alakwitsa ngakhale nyimbo zawo sizidziwika mutu wake kkkkk, ngati kuli anthu akupha pa Dziko lapansi ndi asilamu, bokoharram,ashabab,Islamic state zonse zigawenga pa Dziko lapansi NDA silamu. kukana nkhumba koma chigololo, akanzi mpaka 4 achani? tinene kuti zonsezo ndi nthiti zanu kkkk. koma kumwamba ndiye kuli Ku Venture. Pepani lapani kanyimbonso ndi kachani.

    1. iwe ndi galu ngat umamva kut maiko a slama akumenyena nkhan zake ndi zimenezi. Apa mslam amalorera kufa wasiye abale ako apitirize then w shll c wat ll b zotsatira

    2. ndeee mufa mulipo angati, ife azikazi tikumawatenga konko mu M’balula umo pano NDA christu anadziwa chowonadi inuyo mukupusako Ku Mangochiko

    3. chonsecho akuti ndi msilamu ngati mwawona kutli walakwisa munayenera kumungolera yet you call aperson a DOG nde umbuliwo shariya inakupusisani

    4. asilamu ndi mbuzi za satana.. sapembedza Mulungu wa abrahamu, isake ndi yakobo ayi..Koma nyenyezi, mwezi ndi mwala wa Kaba ku mecca.. sasamala Malamulo khumi a Yehova kuyambira muhammad anamphwanya koma anayika malamulo awo a mitala, kupha, bodza, ufiti, kusamala thupi osati mtima kuyeretsa.. ngati salapa gehena ikudikira

    5. Ziwani izi christu,, olo mutanyoza aslamu motani koma ngati simukhulupilira kuti Mulungu alipo modzi ndipo sanabeke komaso sanabelekedwe kumtendele simukalowa,, olo mutatukwana ndi kunyoza chislamu simupidula chilichonse ponkha ponkha mutakhulupilira Mulungu modzi ndikusiya kupembeza mafano

    6. Ndakumvani akakhala Muhammad zinanya ndi nkhumba amafuna mpikisano ndi yesu kkkkkkk Guys mukutibowa mu mdziko lathu la Christu.

    7. Apa paphulikatu mabomba apa,muli ndi mwayi kuti mauwa angochita kuponyedwa munakakhala kuti muli limodzi apa bwenzi enanu mutasiya kukomenta coz munakakhala mutaphedwa poti anzathuwa kupha mkafili in their faith are assured aplace kumalo abata kumwamba

    8. Apa paphulikatu mabomba apa,muli ndi mwayi kuti mauwa angochita kuponyedwa munakakhala kuti muli limodzi apa bwenzi enanu mutasiya kukomenta coz munakakhala mutaphedwa poti anzathuwa kupha mkafili in their faith are assured aplace kumalo abata kumwamba

  47. nyumba yina yiliyose imakhala ndilamulo lake,monga ife asilamu timakhulupilira kuti mowa ndiwolesedwa pakati pamulungu .pomwe mkristu wina aliyese amati mowa ndiwabwino chifukwa choti mulungu wawo yesu anasintha madzi mkukhala mowa.msilam amakhala wowopa mulungu, koma kwa munthu amene sawopa mulungu amangobwebweta zopanda pake ngati munthu wamowayo ndiye chifukwa chake ma comment enawa akumati aslamu ankhondo ,ena ansanje, koma zonsezo pachifukwa chakuwuzidwa chilungamo

  48. nyumba yina yiliyose imakhala ndilamulo lake,monga ife asilamu timakhulupilira kuti mowa ndiwolesedwa pakati pamulungu .pomwe mkristu wina aliyese amati mowa ndiwabwino chifukwa choti mulungu wawo yesu anasintha madzi mkukhala mowa.msilam amakhala wowopa mulungu, koma kwa munthu amene sawopa mulungu amangobwebweta zopanda pake ngati munthu wamowayo ndiye chifukwa chake ma comment enawa akumati aslamu ankhondo ,ena ansanje, koma zonsezo pachifukwa chakuwuzidwa chilungamo

    1. Mmmmm man aslam ena simmene akamamwera mowa ndipo nkhumba akumaidyanso kwambiri ineyo athu amenewa ndithu ndawaona ndi maso anga ndipo alipodi ndiye usadane ndikuika nyimbo zanu ku ma bar nyimbo nkachaniso ngati athu antundu wanu ku naigeria a boko haram amaimba nyimbo zanu zomwezo akamapita kukopha athu iwe ukufuna utiuze chiani apa??

    2. Mmmmm man aslam ena simmene akamamwera mowa ndipo nkhumba akumaidyanso kwambiri ineyo athu amenewa ndithu ndawaona ndi maso anga ndipo alipodi ndiye usadane ndikuika nyimbo zanu ku ma bar nyimbo nkachaniso ngati athu antundu wanu ku naigeria a boko haram amaimba nyimbo zanu zomwezo akamapita kukopha athu iwe ukufuna utiuze chiani apa??

  49. Direct thing, pipo do what they like and sometimes what they always do its islamic pipo proposed the muzic if you kill my bar man iwill shoot you hahahahah!

  50. Direct thing, pipo do what they like and sometimes what they always do its islamic pipo proposed the muzic if you kill my bar man iwill shoot you hahahahah!

  51. Nanga nyimbo ija imati “Ndikufuna ka hijabu” tisamakasewerenso?Chifukwatu zidakwa ndi azimayi oyendayenda a chisilamu amaikonda

  52. Nanga nyimbo ija imati “Ndikufuna ka hijabu” tisamakasewerenso?Chifukwatu zidakwa ndi azimayi oyendayenda a chisilamu amaikonda

  53. Abale anga nonse nchipembezi cha Islam… Ndikukupemphani kuti chonde chonde basi nkhaniyi isiyeni ndipo musayipitilize…. Tawonani ena pompano akuyamba kumunyoza ALLAH munkhani zopanda ntchito anga uzi SUBUHANALLAH يا الله اعوذبالله من الشيطان الرجيم آمين Oh Allah titalikiseni kuchokela kwasatana othamangisidwa ((ndizizukulu zake anthu omwe ali okanila omwe akadali mpaka lero lino mumdima ))

  54. Abale anga nonse nchipembezi cha Islam… Ndikukupemphani kuti chonde chonde basi nkhaniyi isiyeni ndipo musayipitilize…. Tawonani ena pompano akuyamba kumunyoza ALLAH munkhani zopanda ntchito anga uzi SUBUHANALLAH يا الله اعوذبالله من الشيطان الرجيم آمين Oh Allah titalikiseni kuchokela kwasatana othamangisidwa ((ndizizukulu zake anthu omwe ali okanila omwe akadali mpaka lero lino mumdima ))

  55. Kkkkk kodi mesa nduthenga wamulungu?eyaka zidakwa mwina mkutembenuka mitima mawu alah akakhudza asiya mowawo balibepo chokwiyira apa mwangofuna ndewu aa inu mmene amayikila song za Akhristu mu ma bar munavapo akhristu Akwiya bwanji wayika song za mulungu mmalo Omwela mowa? Munthuyi sanabwele mkachisi kusokoneza ayi tizi Ozitsata kwambiri Zaziiii zopanda salt chokwiyira sindikuchiwona apa ayi . Soma chitabu afe oti moti muzipempherera dziko lanuli momwe likuyendela mukapanga aganest chidakwa hahaha yebo

  56. Kkkkk kodi mesa nduthenga wamulungu?eyaka zidakwa mwina mkutembenuka mitima mawu alah akakhudza asiya mowawo balibepo chokwiyira apa mwangofuna ndewu aa inu mmene amayikila song za Akhristu mu ma bar munavapo akhristu Akwiya bwanji wayika song za mulungu mmalo Omwela mowa? Munthuyi sanabwele mkachisi kusokoneza ayi tizi Ozitsata kwambiri Zaziiii zopanda salt chokwiyira sindikuchiwona apa ayi . Soma chitabu afe oti moti muzipempherera dziko lanuli momwe likuyendela mukapanga aganest chidakwa hahaha yebo

  57. WHAT IS ISLAM???

    Islam means “surrender and submission of one’s will 2 the will of Almighty Allah “in sincere obedience and peace. ((mundimvese nonse ma Christians )) It is the last religion and the final message sent by Allah 2 all of mankind in order 2 guide them to the right path : to worship and resort to him Alone,, without ascribing to him any partners or taking any intercessors to communicate with him. Allah conveyed his religion of Islam by sending down his revealed scripture, the Qur’an to his beloved and last chosen prophet , MUHAMMAD صلى الله عليه وسلم through the angel Gabriel .so what are you people saying ?? You are just talking no sense muchepese muzikhala nimanyazi nthawi zina aaaaaaa

    1. Islam is just another foolish and evil scam to spread hate and intolerance among the innocent.Throw the religious fools in jail;christian and moslem bastards alike.

  58. WHAT IS ISLAM???

    Islam means “surrender and submission of one’s will 2 the will of Almighty Allah “in sincere obedience and peace. ((mundimvese nonse ma Christians )) It is the last religion and the final message sent by Allah 2 all of mankind in order 2 guide them to the right path : to worship and resort to him Alone,, without ascribing to him any partners or taking any intercessors to communicate with him. Allah conveyed his religion of Islam by sending down his revealed scripture, the Qur’an to his beloved and last chosen prophet , MUHAMMAD صلى الله عليه وسلم through the angel Gabriel .so what are you people saying ?? You are just talking no sense muchepese muzikhala nimanyazi nthawi zina aaaaaaa

  59. Kodi munthu woti abadwe mwatsopano tingamupeze kuti? Kuchalichi,kusikiti kapena kumene kumapeka anthu ochimwa ngati kuma bar. Uthenga timaunva munjira zosiyana siyana.

  60. Kodi munthu woti abadwe mwatsopano tingamupeze kuti? Kuchalichi,kusikiti kapena kumene kumapeka anthu ochimwa ngati kuma bar. Uthenga timaunva munjira zosiyana siyana.

  61. Koma mphuno salota mmene asilamu akutikitila nkhuma wina nkumati izi ndi pulobulemu eeeee kaya pita pa Kachele if you are from Mangochi mi jomba ikujegweda ganda sizinaoneke

  62. Onse amene mukugwilizana ndi zoika nyimbo za chisilamu kuma bar
    , zikuchita kuonesa kwatunthu kuti mudakali mun’dima wadzaoneni. ndipo choti mudziwe asilamufe sitimatengela zachikunja zomwe ena anabweletsa masiku amake dzana……akhristu pitilizani kupanga zomwe mumafuna osati zomwe Mulungu amafuna.

  63. Onse amene mukugwilizana ndi zoika nyimbo za chisilamu kuma bar
    , zikuchita kuonesa kwatunthu kuti mudakali mun’dima wadzaoneni. ndipo choti mudziwe asilamufe sitimatengela zachikunja zomwe ena anabweletsa masiku amake dzana……akhristu pitilizani kupanga zomwe mumafuna osati zomwe Mulungu amafuna.

  64. Kuimbisa Nyimbo Ndikutukwana Chipembezocho Chabwino Ndichan Kod Nyimbo Zimaimbidwa Zija Za Anthu Ena Vuto Limakhala Chan Lets Think Like Pipo Who Have Live Brains In Our Heads

  65. Kuimbisa Nyimbo Ndikutukwana Chipembezocho Chabwino Ndichan Kod Nyimbo Zimaimbidwa Zija Za Anthu Ena Vuto Limakhala Chan Lets Think Like Pipo Who Have Live Brains In Our Heads

  66. Anthu amene Ali oyipa ndiyawo amalimbana ndi amzawo,, kulowelela zanzawo, kulimbana ndizochita zanzawo, kumakhala kusaupexamtima ndi mtima wa jealous . Jealous ndi ufiti opanda mangwala…. Ndipo mangwala ake mkulapa kwa (Allah ) mulungu.. Inu akilisitu ndichiyani chomwe chikukusangalatsani apa? Ndinu anthu olimbana ndi amzanu achisilam….. Khalidwe ili palibe chomwe mungapezemkati mwake kupatula kuinekela kuyaluka kwanu ndi mtima wanu omwe mulinawo wa jealous woo. Ndichiyani chimwe chimakupangitsani kumatenga ma stuff aslam kumawapanga ngati ndiyanu??? Chepesani guys….

  67. Anthu amene Ali oyipa ndiyawo amalimbana ndi amzawo,, kulowelela zanzawo, kulimbana ndizochita zanzawo, kumakhala kusaupexamtima ndi mtima wa jealous . Jealous ndi ufiti opanda mangwala…. Ndipo mangwala ake mkulapa kwa (Allah ) mulungu.. Inu akilisitu ndichiyani chomwe chikukusangalatsani apa? Ndinu anthu olimbana ndi amzanu achisilam….. Khalidwe ili palibe chomwe mungapezemkati mwake kupatula kuinekela kuyaluka kwanu ndi mtima wanu omwe mulinawo wa jealous woo. Ndichiyani chimwe chimakupangitsani kumatenga ma stuff aslam kumawapanga ngati ndiyanu??? Chepesani guys….

    1. Yanu ijatu yongoganiza za destroying basi…simungamuwuze allah wanuyo 2 forgive th bar..anthu oyipa kwambiri inu

  68. munthu odwala ndi yemwe amafuna dotolo,mmayesa nyimbo zawozo zimalalikila za uthenga wa mulungu kufuna anthu asiye machimo akapulumuke. kumowako mmayesa mkomwe kumakhala anthu omwe mumati ngochimwawo?palibe cholakwika apa kapena nyimbo zake ndi zija zoti tikaponda patuluka mpunga kkkkk ngati zili zimenezo ndiyee aaaa zili bhoo koma ngati zili zoti tikamvela mwina tisinthazi ndiyee aaaa simunaithe ti bena zina

  69. munthu odwala ndi yemwe amafuna dotolo,mmayesa nyimbo zawozo zimalalikila za uthenga wa mulungu kufuna anthu asiye machimo akapulumuke. kumowako mmayesa mkomwe kumakhala anthu omwe mumati ngochimwawo?palibe cholakwika apa kapena nyimbo zake ndi zija zoti tikaponda patuluka mpunga kkkkk ngati zili zimenezo ndiyee aaaa zili bhoo koma ngati zili zoti tikamvela mwina tisinthazi ndiyee aaaa simunaithe ti bena zina

  70. Ngati zachi khristu zo mumaika nkuma nvela kuma bar tisiileni nyimbo zanthu zoyelazo. Zizi nveledwa poyela. Islam sichosewelasa.akhristu mukula kwisa kwambiri

  71. Ngati zachi khristu zo mumaika nkuma nvela kuma bar tisiileni nyimbo zanthu zoyelazo. Zizi nveledwa poyela. Islam sichosewelasa.akhristu mukula kwisa kwambiri

  72. Ngati ziri zofalitsa uthenga wabwino ndiposalakwika uthengawonso ufikire kuzidakwa ndi mahule ndinjira imodzi atha kuzindikira choona cha moyo wao zambiri zimayambidwa za akhristu zija alipo anatsekeledwa bar?Hahaha mtima ozikonda uwu lekani komanso nyimbo zake ziti zosamveka zomwezi?????

  73. Ngati ziri zofalitsa uthenga wabwino ndiposalakwika uthengawonso ufikire kuzidakwa ndi mahule ndinjira imodzi atha kuzindikira choona cha moyo wao zambiri zimayambidwa za akhristu zija alipo anatsekeledwa bar?Hahaha mtima ozikonda uwu lekani komanso nyimbo zake ziti zosamveka zomwezi?????

  74. Ma Muslims ndianthu osowa ntendere,,samafuna azawo apange zomwe akonda and they believe in violent,,let me tell u the dyombaz muzakhara anthu antendere mukazasiya azanu apange zomwe amakonda eg food,music etc izafika azanu axakutoperani ngati ku central African republic and izi zizabwino,,,ngati sakumwera kunyumba kwanu or muzititi what’s your problem,,, nkhondo imakoma ili patali mufuse abale anu a Isil,,,

  75. Ma Muslims ndianthu osowa ntendere,,samafuna azawo apange zomwe akonda and they believe in violent,,let me tell u the dyombaz muzakhara anthu antendere mukazasiya azanu apange zomwe amakonda eg food,music etc izafika azanu axakutoperani ngati ku central African republic and izi zizabwino,,,ngati sakumwera kunyumba kwanu or muzititi what’s your problem,,, nkhondo imakoma ili patali mufuse abale anu a Isil,,,

    1. Umbuli too much,, Malawi ndi secular state according to our constitution. Ndie wina akamati Malawi is a Christian national he or she is totally out mind kkkkkk

    2. this is a shit talk amene mukulankhula mopusa like this mulibe nzeru ndinu zidakwa agalu komaso ma prophets inu achina bushiro mbuz zachabe chabr

    3. this is a shit talk amene mukulankhula mopusa like this mulibe nzeru ndinu zidakwa agalu komaso ma prophets inu achina bushiro mbuz zachabe chabr

  76. Dzina la Mulungu likuyenela kulemekezedwa, silikuyenela kutchulidwa pachabe. Palibe analapa machimo ake atanvela nyimbo ya mau Amulungu Kubara.Nyimbo iliyonse yotchula dzina la Mulungu sikuyenela kuimbidwa kubara.

  77. Islamic music? There z no such thing as Islamic music. Islam is not associated with music. Hence i see no problem playing any type of music in bars. Mentioning Allah or His prophets doesn’t make a song Islamic.

  78. Asilamu kudzitama, amachemelera ngakhale chigamba chapa chovalatu, kkkkkkkkkkk. Ndipo nyimbozo zisasiye, ngati kuli kukapsa moto akapse, iya. Amakhulupilira kuti kuyankhula chi Arab ndi chiyelo, kkkkkkkkkkk.
    Za ziii!

  79. Chipembezo cimeneci mtumiki kti citipeze kuno anacimvela kuwawa ndye wina kumacipepuxa ife xitingalole kti wina atero. iwexo amene ukti ndiwe Muslim kma xukuwonapo colakwika ukuyenela kulapa pamaxo pamulungu walakwila Allah kmaxo wacipeleka cixlam

    1. kodi bwanji nyimbo zina za uzimu ziyimbidwaso mu ma bar ndi ya chislam yapambana bwanji kuti isambidwe ndipo palibe amene amapanga fight chinthu osamvela kuwawa ngakhale yesu adamva kuwawa kumene

    2. kodi bwanji nyimbo zina za uzimu ziyimbidwaso mu ma bar ndi ya chislam yapambana bwanji kuti isambidwe ndipo palibe amene amapanga fight chinthu osamvela kuwawa ngakhale yesu adamva kuwawa kumene

  80. even drunkuds they need spiritaul message nomatter how or where stop your nosense u so called muslims this is a free country not Kwa Alluya mixiiiii

    1. may God for give u n show u the straight path, naver encourage pple to do that will bring the anger of God, you may call it a free country to u, but we muslims we submit to the will of God, once we surrender to creator alone we are no more free, coz He gave us the book n law to follow, I. wish I. could explain to u.more but.may God forgive u

    2. may God for give u n show u the straight path, naver encourage pple to do that will bring the anger of God, you may call it a free country to u, but we muslims we submit to the will of God, once we surrender to creator alone we are no more free, coz He gave us the book n law to follow, I. wish I. could explain to u.more but.may God forgive u

  81. kkkk! nyimbo za chisilamu zingakomedi kumvera utaleze ndinthu ndipo nyimbo iliyonse utha kumayimba nao coz sizivuta kuloweza kkkk! tiye nazo barman timvere zimenez

  82. zidakwa nazo zitava uthenga wabwino kuchokela munyimbo zachisilamu zi kodi sizingatembenuke mtima ndikuyamba moyo wasopano, naneso kumowa komweko ndinavela nyimbo ya kamuzu barracks yoti mulowelelepo ambuye ndipo ine inandisutha mtima wanga mwawona. tizivelepasi thawi yakwana yovela nyimbo zovinika bwinozi.

  83. Mungamayimbe Layilala yilala Muhamad allah sulula pa tarven, mukufuna muone Boko halamu chani? Koma mulindidzibwana heavy, sinyimbo zapamowa mapeto ake mudzangomva Allah-u wah kubalu, kenako ndibomba. Osawaputa dala anthu amenewa

  84. Mukapanga ma coment anu mudzilingalira Kaye… Inuyo simudziwa china chilichonse cha chipembedzo chathu ndiye mpaka kuti nkhumba? a Kaulesi… Kodi mumaganiza kuti mwabisala? Titakufunanitu titha kukupezani , ndiye zinyozani koma wina adzaleka nzache taona zosaona. Bola usadzakhale iweyo…

  85. Nyimbo zimenezo anasankha ndi Marriam ndi Hawa.. Mahule achisilamu…so osawaphera ufulu wawo,mwina tsiku limenero sanapite ku mzikiti dats y anafuna angomvera music yokha..

  86. 34 of Muslims are uneducated that’s why they drink beer up to kachasu and satchets then I don`t see anything wrong about playing Islamic music in bars

  87. Kkkkk but if they put those songs #kusadaka yoh yoh sikusangalala kwake… they think like they are in paradise after eating too much food,,, nyimbo ndi nyimbo olo kubara ziziyikidwa mesa we are in last day….

  88. Mawu amulungu afikile pena palipose bola lali anthu nde akubala adzatwmbenuka bwanji mitima ngati akusalidwa,? Nchifukwa chake ndimakana zoti chisilamu ndi chipembedzo ndigulu la nkhondo ili

    1. brother stop insuit muslims plz,even if u dont like us muslims dont let that to be a means of u getting the anger of Almighty, no try to encourage pple to do gud n dont encourage pple to do bad even if u may dislike others, may Almighty grant u guides

    2. brother stop insuit muslims plz,even if u dont like us muslims dont let that to be a means of u getting the anger of Almighty, no try to encourage pple to do gud n dont encourage pple to do bad even if u may dislike others, may Almighty grant u guides

      1. Since your god is so weak that it needs help from rioting criminals to defend it,why don’t you find a more powerful god who can defend itself.A religion that is based in reality would help as well.

    3. brother stop insuit muslims plz,even if u dont like us muslims dont let that to be a means of u getting the anger of Almighty, no try to encourage pple to do gud n dont encourage pple to do bad even if u may dislike others, may Almighty grant u guides

    4. brother stop insuit muslims plz,even if u dont like us muslims dont let that to be a means of u getting the anger of Almighty, no try to encourage pple to do gud n dont encourage pple to do bad even if u may dislike others, may Almighty grant u guides

  89. uwundie tikamati ntopola ndiumeneu zikatinyasa tikayambapo muziti aslam ndiankhondo chibwana chimenocho muzipanga kuchikhristu komweko musatiyambe dala ayi

  90. no let them pray…..mwina angatembenuke mitima pot sapeza thawi yokapephela….zindisangalatsa kuona chifukwa chitasiya zonse nkuyamba kutumikila chauta

  91. Mmmmmmmm,koma zinazi ndye kuzitengeratu pa mgoong’o,mmene akhutira mowa asilamuwo,eeeeeehhh…koma zilipo,timamwera limodzitu koma chosechoo uku akuvina gospel,tiyeni tikondaneni osati zilizonse basii ziwawa,its ok ngatii samwadi mowawo..

  92. Angoni inu taphunzirani,mitundu ya chilankhulo chanu inu amalawi musamachifanizire ndi chipembedzo. Mesa mumati ndinu ozindindikira? Islam is areligion while Ngoni,yao,lomwe these r just languages for the human beings ndiye ndikamamva ugalu wanu wa umbuli ndi umve wakusavinidwa kwanu,mumandimvetsa chisoni koma Allah adzakuzindikiritsani if he wills

  93. I hope thats an excellent job by muslims from Lilongwe, I hope some other muslims from different areas has got a got example. This behaviour seems to grow now but people must know that #_ISLAM is totaly different from christianity, you can be playing achina ” mulowelelepo ambuye” or whichever christian song and you’l be free. #_BUT_ ONCE YOU PLAY ANY ISLAMIC TUNE IN A BAR or any ‘beer drinking place’ we muslims WILL NEVER LET THAT ACT GO FAR. ” Kusamala mano sikusuka mkamwakokha, but on this case am saying ” kusamala zoyimbirazanuzo sikuzipuputakokha koma kusayika nyimbo zachislamu”. Musadzati aslamu ndiankhondo tikadzakuphwanyilani, (y) #_RESPECT_MUSLIMS_PLEASE, and you’l will be given respect too.

  94. dela limeneli kunachuluka anthu achi slam ambili ndiye ndiokha okha amakaikitsa mimbozo kwa DJ anyamata ambili omwe amapezeka malo amenewo amakhala achi slam komaso kuti muonetse mahule omwe amapezeka ma bar amakhala achi slam nde akumafuna adzivina zachi pembedzo chawo musawaphere ufulu

  95. Achita bwino kukaletsa coz such songs can not lead people to salvation, in fact, it was God’s command but some of you can’t discern that. When God speaks even the devil obeys.Christian songs only should be played in such places coz they have a saving power since they are God’s words.

    1. Ziwani izi,,ngati chinkhulupiliro chanu simukukhulupilira kuti Mulungu alipo modzi, sanabeleke komaso sanabelekedwe, ndikukhulupilira kuti Mulungu anatumiza aneneli ochuluka kuzaphuzitsa za ufumu wake ziwani kuti chikhulupiliro chanu chakufa ndi patsiku lachimalizo Jannah simukainukha

    2. Ziwani izi,,ngati chinkhulupiliro chanu simukukhulupilira kuti Mulungu alipo modzi, sanabeleke komaso sanabelekedwe, ndikukhulupilira kuti Mulungu anatumiza aneneli ochuluka kuzaphuzitsa za ufumu wake ziwani kuti chikhulupiliro chanu chakufa ndi patsiku lachimalizo Jannah simukainukha

    3. There is One true God,The Father,The Son and The Holy Spirit. If your god does not constitute the said “members” then that one is not God

  96. Choti muchiziwe chisilamu chimadana ndi zinthu zoipa komanso polankhula tiziganiza chisilamu sichikhala cha yao ayi

  97. Asilamu amakhala akumat ndi anthu a mtendere.Kma tsopano apapa mtendere waonekapo?Palibepo nkhani yomakangana apaa!

  98. Izi zinaliko nthawi ya nowa ya roti coz akamati chisilamu si dzina lamunthu iai chisilamu ndi chipembezo cha mulungu nde anthu akufunika kusatila chifuniro cha mulungu nde ngati mwawina ofooka akumachita izo sikuti muchiipise chipembezo cha mulungu iai nonse amene mukupezelapo mwayi nde kumayankhula mopusa marabichi ana aimbwa sanya inda mafontini

    1. Iwe Bolfman… Usamaname, kapena amakuuzawa anakunamiza, Muslim sichipembezo cha Mlungu, ilo ndi bumgwe chabe, chomwe uziwe nyimbo za Mulungu ziyenela kupezeka pena paliponse.,komanso tabwela pano pa Durban Central on fraiday amzakowa akamachokela kuNZIKITI Kwanuko akavula Mikanjo yawoyo timakumana kuMOWAko ndipo akalezela mahule nkati nyimbo za Quaran pakamwa, MUSATINAMIZE AKUMUZI WAAWAAA.. ..

  99. I m a muslim but I don’t see any problem playing islamic songs in such places. I’d rather be happy when such things are happening. And in Malawi we have alot of problems to deal with together as Malawians. And I’m not sure whether those attackers are true muslims or mere extremists.

    1. It just shows that u r an ignorant Muslim…u don’t see any problem playing Islamic muzic in pubs, r u a true Muslim? Foolish u. Islamic songs r full of praising ALLAH wishing peace to our beloved Prophet …..and u don’t have a problem with those songs to be played in pubs? I don’t what kind of Muslim r u?…. Let me tell this… The biggest enemy of Islam is the ignorant Muslim like u , whose his ignorance leads him in tolerance, and his action destroys the true immage of Islam and when pipo sees at him they think that Islam is what he is… My brothe may ALLAAH give u good understandi on this…

    2. Ine ndimkatolika.Ndikamva nyimbo yathu ku bar zimandinyasa kwambiri.Aslam sanalakwitse,chimenecho ncipongwe kwa Mulungu.

    3. Ine ndimkatolika.Ndikamva nyimbo yathu ku bar zimandinyasa kwambiri.Aslam sanalakwitse,chimenecho ncipongwe kwa Mulungu.

    4. Plz spread GOD’s message evrywhre n wodwala nd amene akufuna dotolo osat wangwiro.I see no mstek 4 dat,A DJ pitrizan kufalitsa uthenga wa mulungu.

    5. Sambani mind your words,hw can you call us zitsiru just b coz we are protecting our religion????? Shame on you !!!!!! Haterz

    6. wawooo mwedyi adaudi mweedyi ,mmwedyo msilamu dyatchaina ligongo lyakwe mukuwechetega yausilu, mwedyo kafiliii ,#Andy_chimchere mind your own language dear, hygiene its necessary thing , kod manyiwo iwe sugwra? aaaaaaah u think like a human

    7. olo titati tiwauze chotani sangave chifukwa choti amayesa mulungu ndu nsuweni wawo.chipembeZo cha chi khrist iz full luxiuly.pali mau amat kwa munthu okhulupilila dziko lapasi ndi ndende,ine ku bele la mai anga ose ndi akhrstu koma ndimayamika mulungu ,powaziwitsa mai anga njila ya chiongoko.uwona kut anthu mkachisi kuvina mpaka kuiwala xot kuli njala ati ati kuvina mwa ambuye,pomwe olo yesu yo munava kuti akavina

  100. Ife zotiyamba dala ayi ngat achina Gwalad akutopesa ikani Grace chinga moyo kusiyana ndi za chislamu mboli zanu achewa nonse

  101. It Is Normal To Play Christian Songs In Bars And Abnormal To Play Islamic Songs. Nkhani Ikakhala Ya Asilamu Ma Comment Amakhala Olakwika. Dzulo Panali Pastoral Letter Alemba Anthu Amapanga Ana Mathanyula Sakwatira Aja Koma Makomenti Four. Any Provacation Will Be Resisted As Malawi Is Not A Christian State.

    1. if we hard to word in that way ISLAMIC STATE, that means even if we have to explain u wont understand brother Welllngton, but may Almighty show u the ryt path,

    2. if we hard to word in that way ISLAMIC STATE, that means even if we have to explain u wont understand brother Welllngton, but may Almighty show u the ryt path,

  102. Vuto ndaliwonapo kumbali yanga ndiloti…masiku ano achinyamata achisilamu nanunso mwawonjeza chifukwa munamizilamu munyimbo zanu. Inu zoona nyimbo zachisila mpakana madrum…komanso magitala ndizitolilo?

  103. angakhale yesu amene anadana nawo anthu omwe ankagulisa malonda nkachisi coz anakhala ngt adelera kachisi wamulungu……abale zamulungu pelekani kwa mulungu zakaisala mpaseniso kaisala sndkukhulupilira kut mene amaziimbra nyimbo zachslam muja munthu angakaike mu bar szoona kmeneko nde kuyesana. anthu ena zkamachitka zotelezi mumat aslam ndi ovuta. chidziwika nchakut ndiudindo wa aliyese kuteteza zamulungu ndkutaliklana ndizonyasa zose…..pali mumat mukamuona amzanu kaya ndiomudziwa kut nd mslam akumwa mowa kapena kupanga chilichose chosemphana mumaona ngt aslam onse ndiotero kma ayi sichoncho abale kuchislam mowa , katapila , kuba, ndi zina zom,nyasa ndizolesedwa en ngt wina atamachita izi kapena bussines ndekut ali kunja kwachislam!!!

    1. A bwana mr kassim ku chisram mukuti mowa ndi olesedwa mwayankhula bwino ndithu cifukwa si kuchisram kokha koma muufumu wa allah mowa ndi wolesedwa komano ngati mowa uli wolesedwa ndi zoonanso kuti nyimbozi samangaimbe kolesedwako,tsono vuto mumadziwa kuti ma busines ambiri mmalawi muno amapanga ndi anzathu a chisram?
      Monga ngati ma bar,ma lesthouse ambiri malo ambili omwela mowa anthu ake nga chisram?Andinso ambili ndi akuluakulu a chisram taonapo ife ndiye zoterezi mukuganiza kt anthu angasiye kuika nyimbo za chi sram?M’ma bar mwini wa bar ndi chehe ndiye barman or dj waku bar ko angakanike kuika nyimbo zotelezi?
      Mwandilembela bwino bwana kassim mwanzeru ndithu,koma taganizaponi bwino pamenepo kuti nkutani.

    2. Ma Rest house pafupifupi amachita kulemba kuti Mangochi Resthouse ndiye kuchimake kwa chigololo mowa ndiye likhale tchimo loposa?

    3. Mb’ale wanga Lungu,zindikira kt sionse omwe ali akumangochi ndi asilamu vuto ku malawi simumatha kusiyanitsa pakati pa Ayao ndi Chislamu,munthu kukhala muyao sizitanthauza ktu automaticaly iyeyo ndi msilamu ayi.dziwani kuti chisilamu ndi chipembezo ndipo Chiyawo ndi mtundu wa Anthu
      .
      Omwenso akhonza kukhala azipembezo zina
      .
      Dziwani kt Msilamu sangakhale ndi business yogulitsa zoletsedwa mchipembezo nthawi yomweyo mkumadzitcha ndine msilamu
      .
      Onse omwe mumawaona akugulitsa mowa,chamba namalankhula chiyawo?amenewo ndi Ayawo osati Asilamu ayi
      .
      Ndikupempheni muzitha kusiyanitsa pakati pa Msilamu nndi Muyao,angakhale mutamuona atavala ka bada mkumagulitsa zoletsedwazo

    4. #kassim,The bible doesnt restrict where the word of God should be found. And you should remember that jesus came for sinners not for those who are holy. Remember that jesus was even found in the houses of those who were taken most sinful like zakeus. And you should know that there is a big gap between christianity and islam

    5. bwana @ plofesor sory my dad sitili pano kusiyanisa pakat pachslam ndichkhristu ayi coz the men problem anthufe bible timalimva ndikulitanthauzira mosiyana kmabe tonsefe ndi anthu amulungu

    6. bwana @ plofesor sory my dad sitili pano kusiyanisa pakat pachslam ndichkhristu ayi coz the men problem anthufe bible timalimva ndikulitanthauzira mosiyana kmabe tonsefe ndi anthu amulungu

    7. Am achristian,koma nkhani ili apa ndiyanyimbo ku bar so please osaisokonezela dala nkhaniyi bwana proffesor tiyeni tikambe za nkhani ili pa ground,kwaine sindikuona cholakwika chilichonse kuti nyimbo za Mulungu ziziyimbidwa mmalo ngati amenewa chifukwa ena amatembenuka mtima akangomva uthenga wa Mulungu kudzela munyimbozi.

    8. Am achristian,koma nkhani ili apa ndiyanyimbo ku bar so please osaisokonezela dala nkhaniyi bwana proffesor tiyeni tikambe za nkhani ili pa ground,kwaine sindikuona cholakwika chilichonse kuti nyimbo za Mulungu ziziyimbidwa mmalo ngati amenewa chifukwa ena amatembenuka mtima akangomva uthenga wa Mulungu kudzela munyimbozi.

    9. chamba, Chigololo, Kaduka, Mowa,Kuba, Kupha, mabodza. amene sapemphera ka 5 times a day, kunyoza Makolo/Akulu Akulu, kutukwana, kunama Etc ndizosaloledwa ku Chisilamu

    10. chamba, Chigololo, Kaduka, Mowa,Kuba, Kupha, mabodza. amene sapemphera ka 5 times a day, kunyoza Makolo/Akulu Akulu, kutukwana, kunama Etc ndizosaloledwa ku Chisilamu

    11. kukwatila phwiii,kuphya ntima mpaka nkhondo zimaloledwa muchisilam nanga mtendele ulipati ? tamangosatan zomwe mulungu akufuna osamalimbana ndi zaziko,suzumilan ku sudan muone

    12. eeeeeeish anthu ambri zikuoneka kut mavuto tkanali nawobe. @ mr luka en bro chinchere. nkhani zmeneziso nde ziti?? apatu skut tikukuletsani mowa kapena chilichose chomwe inu mumasangalala nacho ayi nkhani ili apa ndiyanyimbo zachslam ku bar basi. skut tkupanga nanu mpikisano ayi ndbwno nthawi zna kukhala m,modz mwa anthu omanga osat kuphwasura

    13. ccter @ cynthia. wina akutengara malonda kukachisi. wna akutengera nyimbo za uzimu kumalonda abar inu smukuona kut zkufana??? kodi yesu akafuna sibwenzi atangofika ndiulaliki kwa anthu omwe ankachita malonda nkachisi aja ngat znali zabwno?? zindkilan kut chiphumzitso chothamingsa amalonda nkachisi pali. phumziro lalikulu pakat pa inu ndne….m sorry pot ndayankhura kwambri koma chodziwika aliyese ali ndichikhulupiliro chake ife chikhulupiliro chathu skoyenera nyimbo za uzimu kukapezeka ku bar …..bwana anat kut akupanga zimenez akut ambir mwa iwo ndma sheikh ..bwana kukhala sheikh kapena m,busa sizikutanthauza kut ndiwe wangwiro ayi coz nawoso ndi anthu ali ndzofooka zawo chabe kut mtsogoleri amayenera kukhala wachitsamzo chabwno ..nde mwachidule mukaona ena akupanga zosemphana ndi chipembedzo mudziwe kut ali kunja amenewo olo atakhala ndi asheikh kapena abusa

    14. Akulu akulu nthawi zambili mudziwe kuti,Bible limati mau amulungu sapita pachabe,andinso anati pa YESAYA 55V11 chomwecho adzakhala mau anga omwe ndinawatumiza sindzawatumiza nkubwela chabe,komanso ku YOHANE anati thambo ndi ziko zizatha kma mau anga adzakhala chimodzimodzi.ndi chifukwa chani ndikunena izi nthawi zambiri mau ndi oopsa ndipo Mulengi amagwiritsa ntchito mau akati kuyele kumayela,akhale munthu amakhala munthu pa chiyambi panali mau ndipn mau anali kwa mulungu ndipn mau ndiye Mulunguyo iyi ndi verse yochoka pa YOHANE 1 kumasika mmunsi.Ambiri pakakhala nkhani pa fb ngati apa mumapezelapo mwayi otukwana,kunyoza ngakhale kuseka ena ponena kuti atokhala tikuonana olo ndinene tikumana kuti ndikuuzeni pamene ukulemba umakhalanso ukuyankhula nkati mwako amakhala mau atuluka ndithu,ndiye paja Bible pa LUKA anati samala ndi mau akutuluka nkamwa mwako chifukwa adzakhala mboni tsiku lina,ngakha pa MATEYU 25 kusika nawo pali mau Yense wonena nzake chisiru apalamula nganjo ya moto osatha,samalani okondedwa.

    15. Akulu akulu nthawi zambili mudziwe kuti,Bible limati mau amulungu sapita pachabe,andinso anati pa YESAYA 55V11 chomwecho adzakhala mau anga omwe ndinawatumiza sindzawatumiza nkubwela chabe,komanso ku YOHANE anati thambo ndi ziko zizatha kma mau anga adzakhala chimodzimodzi.ndi chifukwa chani ndikunena izi nthawi zambiri mau ndi oopsa ndipo Mulengi amagwiritsa ntchito mau akati kuyele kumayela,akhale munthu amakhala munthu pa chiyambi panali mau ndipn mau anali kwa mulungu ndipn mau ndiye Mulunguyo iyi ndi verse yochoka pa YOHANE 1 kumasika mmunsi.Ambiri pakakhala nkhani pa fb ngati apa mumapezelapo mwayi otukwana,kunyoza ngakhale kuseka ena ponena kuti atokhala tikuonana olo ndinene tikumana kuti ndikuuzeni pamene ukulemba umakhalanso ukuyankhula nkati mwako amakhala mau atuluka ndithu,ndiye paja Bible pa LUKA anati samala ndi mau akutuluka nkamwa mwako chifukwa adzakhala mboni tsiku lina,ngakha pa MATEYU 25 kusika nawo pali mau Yense wonena nzake chisiru apalamula nganjo ya moto osatha,samalani okondedwa.

    16. Iwe wangoonetsa umbaali wako apa,,,, ma bar amapanga play ma track i chikhirisitu bt nobody has ever vandalised,,,, and ukakamba za chimo lililonse ndie loletsedwa bt anthufe timachimwabe,,,, ma muslim amaotcha or kung’amba kumene ma bible akalandira ma xull bt u never hear kt ma chrisians abwezera,,,, i dont c any problem playin dat song mu bar,,, upite ma lodge, bar and rest house ukapeza kt ambiri ndi ma so called muslim guys and woman,,,,

    17. ndakumvani bwana kassim nde mukuthanthauza kuti ochita zachikuja tiwasiye tisawaunikire kuti asithe. bax akapsye ndithu ndi moto pomwe inu ndi ine tikudziwa chilungamo. uthenga omusintha munthu umadzera mu ulaliki mu nyimbo ndi zina. nde uthengawu ukuyenera kupita ku malo amene kumachitika zosayenera pa maso pa Allah like ku bar. anthu opita ku sikit ndekuti ali kale ndikuthekera kokapulumuka coz chomwe chawasuntha kuchoka uko kutheka ndiuthenga omwewo. tiyeni tifalitse uthenga wake nthawi iliyonse paliponse.

    18. ccter @cynthia ndili ndi umboni kut aliyemse wa ife akudziwa ndthu chilungamo chake. pankhaniyi chabe kut pamene pali mbali zosiyana kumavuta kut amvane coz ambri mwa ife tinangozolowera kutsutsa angakhale chilungamo chake tikuchziwa. chinaso chot muziwe chemwali kupita kumzikit kapena ku church tsiku nd tsiku sizikutanthauza kut ndife ot tkumudziwa mulungu kwambri coz mwini kuweluza nkwamwini wake iye ndamene amaziwa zamitima mwathu…..koma tikanena nyimbo zauzimu aaaa akulu akulu sizoona kut tingaziike bar coz evn mwin bar yo zolinga zake en cholinga chake nkupangla ndalama basi kaya mwina nyimbo za amzathunu munthu utha kuvina nanga zachslam abale munthu angavine iiiiii abale zinaz kumaziona

  104. No iwowo azimenya zidakwa za chisilamu coz ndizimene zikupangitsa muslims also drink beer and they own bars and resthouses which are used for wickedness those songs are requested by muslim drunker

    1. wanena zoona…nthawi yomwe ndimkamwa mowa akaika nyimbo za great angelz ang Grace chinga ndimkamva kutsutsika pena pake…..ndiye ngati mu nyimbo ya chisilamu mo ngati muli uthenga wogwira mtima ndithu wina msilamu okonda mowa azazibweza kamba ka uthenga omwe uli mu nyimbozo…….another comment is wy they let muslims to sing and dance in front of politicians yet they are saying nyimbo zawo sakufuna malo oti pakuchitika zachikunja????????????????

    2. wanena zoona…nthawi yomwe ndimkamwa mowa akaika nyimbo za great angelz ang Grace chinga ndimkamva kutsutsika pena pake…..ndiye ngati mu nyimbo ya chisilamu mo ngati muli uthenga wogwira mtima ndithu wina msilamu okonda mowa azazibweza kamba ka uthenga omwe uli mu nyimbozo…….another comment is wy they let muslims to sing and dance in front of politicians yet they are saying nyimbo zawo sakufuna malo oti pakuchitika zachikunja????????????????

  105. Aslam Ndi Akhristu Pamenepa Simukusiyanitsa? Ena Amati Cholowa Sichiipitsa Koma Chotuluka Ena Amat Imenei ndi haramu ndiye enanu mwati palibe cholakwika?

  106. Aslam osamasekelela zachibwana zikuchitika kumeneko ndikutsika chikhulupiliro. Nyimbo mzambirimbiri zachikunja bwanji sakumayika zimenezo. Akufuna kutiyesa,ndiye otereyo osamunyengelela kut ena atengele phunziro. Mmakonda kunena Aslam ndi ankhongo mukuchita kuziyamba dala.

  107. Good we dont alow muslim songs to be played dirty place like pub ,just show some respect ndani mwa inu anatembenukila ku bala

    1. Kuweluza Ndkwamwin Wake Namalenga Muyambisapo Fight Apa Paja Ndizomwe Aslam Mumati: Jihad Kuphwanya Mitu Njila Kuwoyo Osatha Hahahahahahahaha

  108. This reminds me when one moslems phone rang in the mosque, the tone was Jesus loves yes i know!!!! For the bible tells me so!!!!, you could have seen the face if ba Shehee!

    1. Its a pitty that people are still using prejudice to create malady in a society, Islaam does not allow any form of music in a mosque be it its talking about Muhammahad! its totally forbidden! So if the faces of Sheakhs were upset upon the phone ringing, its not about the lyrics of Jesus but wrong place, wrong time! don’t mislead people into thinking that Islaam is an Anti-Christ! among the prophets named in the Quran, Jesus is one of them. So, how can Islaam be an anti-Christ?

    2. As a muslim I say: Yes jesus loves me and I know because the Quran teaches me so, and it teaches me to love, respect and revere but not worship him. You should take your war to Jews because up to now they still say: Jesus was a son of a prostitute because he had no father such a horrible thing for such noble character! shame and yet you idolise them and stand with them in world politics! are you goofed?

  109. u could have jst burnt it,panalibe chovuta chomulimbitsa mtima ncani mpaka pamenepo? mukutiyamba munya,ndewinawe uzipanga ma comment ako opusawo pamenepa chikukusangalatsa ndichani? lets respect other peoples religions

    1. Kassim ndi Ibrahim Mwina simudziwa chikhristu ndichamtendere ngati nyimbo zachikhristu zimaikidwa mma pub sidzikutanthauza kuti ndife akhristu tikupereka chilolezo komano kuti machimo sagawana komanso chipulumutso ndiwekha….nkosavuta kulalira uthenga koma nkovuta kumukakamiza munthu kuti alape………….its very easy kuitengera ng’ombe kudambo koma its obviously impossible to force it kuti imwe madzi.

    2. Si Akhristu Onse Amamvera Nyimbo Ku Bar Koma Aja Amatenga Mowa Kukagulitsa Mu Tchalitchi Pa Paper Sunday Aja. A Seventh Day Nyimbo Zawo Sizimveka Ku Ma Bar

  110. koma ngakhale mukuletsa mudziwe kuti chanucho ndi chipembezo,ndiye cholinga cha chipembezo ndiko kutengela anthu ku moyo wosatha,kutheka wina kunyumba kwake samakhala ndi nthawi yakunvera nyimbo za uzimu ntheladi pali chinsisi pa chinthu chili chonse cha uzimu,bible,ma novel qrn ndinso nyimbo za uzimu pali anthu ena kungonva zinthu ndanenazi amatha kukhala ndi chisankho,wonse ali mu njila za kunja nga kumwa mowa.Kusuta fodya zoipa za mbiri anthu awa ali ngati makanda m’moyo wa uzimu khanda likalakwitsa pamakhala kumuongola chimodzimodzi anthu olowelera amafunika kuwaongola ndi mau auzimu,ndiye ngati kuchalich sakumapita,ku nzikiti sapezeka mukawaongolera kuti?Mesa pamene akunva nyimbo za uzimu ndipomwe angamalingalile kusendela ku chalichi?Musanapange chiganizo muziyamba mwakhala pansi kukambilana.Kuti nzabwino kapena ayi.

    1. ayi ndithu madam aysha,pali choona,choipa chimathawa pakanthu pakakhala mdima timafuna kuwala kuzepo tsono ku moyo ntheladi anthu ambili amakhala ali mundima cifukwa ndi zoipa zambili zimacitikako ndiye kumafunika kuti kuzisendela kuwala kuti anthu akazindikild kuti chomwe akupanga kumeneko nzolakwika,ndiye anthuwa angaunikiridwe bwanji ungamuuze dj kuti thimisa ndikufuna tikaswali tonse kuti timudziwe allah?Ndithudi anthu akucitako chipongwe chifukwa amakhala azazidwa ndi satana,koma pamene anvera gospel amatha kumapanga chisankho.Madam aysha mumadziwa kuti kudzela pa maliro,pa ukwati,pa mowa,pa mpingo anthu amatha kumudziwa Ambuye olo allah mpaka kukapulumuka?Ndiye mukufuna muyambe kukaniza chipulumutso?

    2. Ndiye munamva kuti chipembedzo cha chislima anthu akupelewela kuti mpaka mudzikana nyimbo za chi silam ku pub… Ngat a khristu samadandaula nyimboxao zikamaimbidwa ku bar ndiye kuti samaonapo Vuto… Koma nyimbo za chisilam siziyenera kuseweredwa penapaliponse kupatula pa zochitika za chisilamu ngati ma ukwati ndi zina zotero…ndiye ngati ndiwe mbuli pa chinthu china chake ndibwino kungokhala chete …..

  111. Keep it up asilamu akwa Chinsapo,ALLAH akulipileni malipiro ochuruka pantchito yomwe mwagwirayi.Anthu osakhulupilirawa kumawaonetsa choncho.Kuno kumangochi ndiye mumatidziwa,sitimafuna zachibwana ngati zimenezo zikumachitika remember issue ya nkhumba,Ng’ombe yofa yokha ija ndi zotijambula mu Mzikiti without informing the muslim umma ndi zina zotero.Mr Chafwifwa the owner of tha Pub,may Allah also make u among those who fears Allah like the way u’ve taken n for sure dont take Islam for granted

  112. By being a scam,Islam tarnishes its own image.
    Protecting a phoney god with threats really make Islam and the paedophile Allah look great.

Comments are closed.