
Daring thugs on Monday stole a gun from a police officer as she was guarding World Vision International office premises in Thyolo district, Malawi police officials say.
The thugs injured the officer during the robbery and she is receiving treatment at the district’s hospital.
Police identified the officer as Elida Kusakala who was guarding World Vision International offices in the district.
Reports show that the thugs attacked the police officer as she was doing rounds in front of the building with two other officers.
It is said that these criminals tied up the guard who was watching over the premises but it is not known whether the thugs had planned to steal at the institution.
Kadadzera said that it has also been established that the thugs went away with the officer’s gun. He said they had not yet arrested anyone on the matter saying investigations are still underway.
125 thoughts on “Thugs steal a gun from a police officer”
Comments are closed.

Ntchito za ana amunna ndi amuna basi zimawonekelatu nthawi yowumba madongo mkazi samaumbapo mfuti koma wa muna
Komabe nzoona zenizeni zomwe ukunenazo.ntundu wakuba ndi wakuba ndithu.
Hahahahaha malawi yanga
Inu a #Malawi24 u re coming pano while this happened 4days ago,it was the same day u posted this is when then #Gun was found in a tea estate ku Thyolo komweko,pliz try 2break the News as soon as it happens,
arrest all her boy freands mfuti imeneyo ipezeka basi otherwise it’s zero pa ten
Ine kumvera mkasa song ANALIRA on repeat, mkango kulandidwa nyama mu territory chimodzimozi wakuba walanda mfuti wapolice kkkkkkkkkkk shame
Moyo sagula Sister, Wachita bwino kumusila mfutiyo wakumbayo, bwenzi atakupweteka ulele, kunja kwavuta uku . Usafele ntchito .
Anthu aku thyolo ndi mbavadi ,ndaonera olamulira ochokera kwa che Moto (Ndata)
Ndipang’ono pamenepo aunt tiyamba kukugwilira kenako ndikukulanda mwado ndi mfutiyo wanvaaaaaa
Iye amalondela ndimfuti ife tatenga tipangile chuma asa abwereso wina tizatenganso gulu lathu equip ikusowa
Wapolice pamene wakhala nfuti imakhalapomwepo,pepani, munthu sungayiwalile mwendo wako poyenda,
Wapolice pamene wakhala nfuti imakhalapomwepo,pepani, munthu sungayiwalile mwendo wako poyenda,
tha’ts a problem of not well trained ,am always left after interviews 4 having a triangular shaped head
tha’ts a problem of not well trained ,am always left after interviews 4 having a triangular shaped head
Its her boyfriend that stole the gun because real thugs would stole the gun and kill her
Its fine as long as she is alive.
Pamakamulo a asilikali akunena kuti asilikali azikhala awiri kapena kuposela apa. Here u talk of only a woman police, was she alone?? If others were there what did they do in order to overcome robbers?? Apolisi timadalira inutu ndie msazionese ngati ngati ndinu ofooka. Mayi osakhumudwa, zimachitika pa moyo wa munthu. Limbikilani ntchito. Mukazagwira wakuba aliyense bwezerani chiwembucho. Koma osapha. TAPULIKANA??? Tilichete pa RUMPHI. MONILE MOSE.
Kkkkkkkkkk koma ndi wa police amene? Awachita bwino adzichenjera.
Kkk this is my riffle,it is my best friend,without my riffle i am useless kkk.
kkkkkkkkkkkkk.bullshit