Step father nabbed for murdering daughter

Advertisement
Arrested

ArrestedMalawi Police in Chiradzuru district are keeping in custody a 42 year-old man for killing his stepdaughter who had eaten his sugarcane without permission.

Chiradzuru police publicist Victoria Chirwa identified the suspect as Mackson Makoka and the deceased as Chimwemwe Ndawala.

]The publicist said on this day, the deceased took her friends to his father’s garden where they started eating sugarcane.

Makoka found the girls eating the sugarcane and he furiously started hitting his daughter with a stick for leading.

The girls suffered some injuries and she was taken to a nearby hospital on the same day where she was treated as an outpatient but the pains continued.

She went to the hospital again on the next day and she died while receiving treatment.

Makoka hails from Maulana village in the area of Traditional Authority Mpama in the district and is expected to appear before court soon to answer murder charges.

Advertisement

157 Comments

  1. Izi zoopsa kwambiri amalawi anzanga nkhanza zamtunduu sibwino zizichitika mdiko lamalawi ayi nkuluo akapasidwe chilango chokwima potengera ena mwa anthu ngati awa asazachitenso {violence} yakhumudwisa amalawi

  2. Izi zoopsa kwambiri amalawi anzanga nkhanza zamtunduu sibwino zizichitika mdiko lamalawi ayi nkuluo akapasidwe chilango chokwima potengera ena mwa anthu ngati awa asazachitenso {violence} yakhumudwisa amalawi

  3. Izi zoopsa kwambiri amalawi anzanga nkhanza zamtunduu sibwino zizichitika mdiko lamalawi ayi nkuluo akapasidwe chilango chokwima potengera ena mwa anthu ngati awa asazachitenso {violence} yakhumudwisa amalawi

  4. Izi zoopsa kwambiri amalawi anzanga nkhanza zamtunduu sibwino zizichitika mdiko lamalawi ayi nkuluo akapasidwe chilango chokwima potengera ena mwa anthu ngati awa asazachitenso {violence} yakhumudwisa amalawi

  5. Amati akaphika nkhuku pakhomo pake,ziwalo zomwe amadya mkuluyu amamanga ndi linya coz its nothin’ else apart frm umbombo.Let him rote in prison cells wth his evil mind.Kulakwa kwambiri and am sure sanabvale pant on tht dy.A BUSTARD!!!!

  6. Mmmm kma nkulakwa kma nde njala yashupa mwatani kd achewanu bwelani kunu kumpoto chimanga chiliko kuno osapayana mwamvela munavotela chipuwa nichamene chilengesa

  7. U need to find cause of death after reading the death report. Dont jump into conclusion plz.

  8. Iiiiii abale mzimbe weni weniu mpaka munthu kuphedwa ngati amaba? Kodi akulu samati mwana wamzako ndiwako yemwe,uyu akaseve basi ana okupeza adzichita kuopa chakudya chifukwa chakuti sanandiloleze zandipatsa mantha.

  9. Iiiiii abale mzimbe weni weniu mpaka munthu kuphedwa ngati amaba? Kodi akulu samati mwana wamzako ndiwako yemwe,uyu akaseve basi ana okupeza adzichita kuopa chakudya chifukwa chakuti sanandiloleze zandipatsa mantha.

  10. Eish koma mai okupeza ,bambo okupeza ayindithu siabwino ine umboni ndilinawo anthuwa amakhala ankhaza nanga Sugarcane kapena kuti mzimbe ikhale yophera munthu mmm

  11. Eish koma mai okupeza ,bambo okupeza ayindithu siabwino ine umboni ndilinawo anthuwa amakhala ankhaza nanga Sugarcane kapena kuti mzimbe ikhale yophera munthu mmm

  12. Ichi nchirombo ichi, chikufunika chikaone makako basi. Eish s/cane????? Palibeno zomachedwa nkumufunsa mafunso apa, wautali akadindidwe basi

  13. Ichi nchirombo ichi, chikufunika chikaone makako basi. Eish s/cane????? Palibeno zomachedwa nkumufunsa mafunso apa, wautali akadindidwe basi

  14. mwana samamufuna ndikale chifukwa siwawo amangofunapo bumbu la mayi wakewo basi chitsilu chamunthu chikafele kundende basi.

  15. mwana samamufuna ndikale chifukwa siwawo amangofunapo bumbu la mayi wakewo basi chitsilu chamunthu chikafele kundende basi.

  16. I don’t want to seem like a villian,.but of ALL reasons one would find to murder someone, why sugarcane??? .. You’ve ended sumbodys life just like “that” for nothing. #Shupiti. Why Malawi??

  17. I don’t want to seem like a villian,.but of ALL reasons one would find to murder someone, why sugarcane??? .. You’ve ended sumbodys life just like “that” for nothing. #Shupiti. Why Malawi??

  18. He did that bicoz of anger and I think ndimayankhidwe amwanayu kuti madarao afike pomumenya ,I hope kunali kukwapura chabe like momwe makoro amapangira sometimes,,its not about nzimbe koma mayankhidwe and inkwiyo contributed to sad death of young human being,, so sad,,,

  19. He did that bicoz of anger and I think ndimayankhidwe amwanayu kuti madarao afike pomumenya ,I hope kunali kukwapura chabe like momwe makoro amapangira sometimes,,its not about nzimbe koma mayankhidwe and inkwiyo contributed to sad death of young human being,, so sad,,,

    1. Sizimandisangalatsa kukangotuluka nkhani ina yochokera ku mpoto anthu kumakhala kunyoza Atumbuka amaiwala kuti ku Mpotoko kuliso mitundu ya anthu osiyanasiyana.

    1. Sizimandisangalatsa kukangotuluka nkhani ina yochokera ku mpoto anthu kumakhala kunyoza Atumbuka amaiwala kuti ku Mpotoko kuliso mitundu ya anthu osiyanasiyana.

  20. Kma mmakomomu mwavuta zoona bambo wamkulukulu kukamupha mwana nkhani yamzimbe nkhaza zotan zimenezi amalawi hhhh may her soul RIP

  21. Kma mmakomomu mwavuta zoona bambo wamkulukulu kukamupha mwana nkhani yamzimbe nkhaza zotan zimenezi amalawi hhhh may her soul RIP

  22. my mother country zamanyazi nzimbe paka kumuchosela munthu moyoiiiiiiiii! Boma lo tembereredwa kusonyeza kuti ndizitchitozawo

  23. my mother country zamanyazi nzimbe paka kumuchosela munthu moyoiiiiiiiii! Boma lo tembereredwa kusonyeza kuti ndizitchitozawo

  24. Umbuli tmati umbulio zowona munthu wanzelu zake angapange zimenezi? Aaaaaa akuchita kuwoneratu kt njala yavuta bas kumenya mwana life in prison uyo or else anyongedwe bas

  25. Umbuli tmati umbulio zowona munthu wanzelu zake angapange zimenezi? Aaaaaa akuchita kuwoneratu kt njala yavuta bas kumenya mwana life in prison uyo or else anyongedwe bas

Comments are closed.