
Chikondi Saidi aged 26 is in the hands of police after he was seen with a pile of stones at Lunzu, Blantyre stoning an image of Malawi President, Peter Mutharika, police say.
According to assistant Police publicist in the Southern region, Peter Mchiza, Saidi was netted after the law enforcers got tipped by some people in the area about the incident which took place close to Lunzu Primary School .
He was stoning Mutharika’s billboard which has messages about Decent and Affordable Housing Subsidy Programme which is being championed by the Democratic Progress Party (DPP) led government.
Police fear that the acts by Saidi who hails from Mazale village in Traditional Authority Kapeni in Blantyre culd have stirred violence.
1,317 thoughts on “Man arrested for stoning President Mutharika’s face on a billboard”
Comments are closed.

koma Malawi y?
Hope honourable amuna kasambala,u have to go for this case,we know u will help this man out
The street is fade up,such cases were only held during Kamuzuism era
kkkkkkk koma Malawi zomangana wafika pena yaaa akayankha mlandu wotichani sono? haaa ine ndikapeza zima post zake ndimang’amba bullshit
kkkkk mbuzi za anthu pali chifukwa chomumangira munthu pamenepo? Kodi mwatha mapulani chani? Mukuwona ngati nthawi yakamuzu ino? panotu tili mu fourth generation sizopusa mukupangazo.
Kkkkkk apolice njala yomweyo mpaka misala. Ndayenda mayiko osiyana siyana ndikumawona zikwangwani za president zikung’ambidwa. What more peter, no,no,no iwe wapolisi wayamba misala. Talimbanani ndi awo akutibela ndalamawo. Apa wawonetsa moyo wawukapolo apa . Kapena anaba ndalama zija ndi abale ako? Bwanji osakamanga awo akugwira ntchito yowona za ndalama. M’masuleni munthuyo , pangani manyazi ndithu.
He will be charged with an offence of malicious damage of posters
Akati democracy ndi imeyo maiko komwe ufulu wa democracy kulibe kumangana kamba ko genda chikwangwani, fusani America kapena RSA kulibe. Tasukusulani Amalawi
So bad
An image? What if it was at that Man? It would be more than a cashgate, STONEGATE
aa wat z billbords? Z dis 1 maize? Or maybe z electricity? .aaa fokofu peter asandisokoneze mutu wanga owila karewu ndikukwera kwazi2 ngat mukumane naye wagendayo mumuuze kut adzatenge miyala ina kuno kut akammalizepo bwampiniyo. musayerekeze ku ndipeza ku inbox inu aphwawo a pitala ndikuswana ngat lambe ndi2
Thus illiterate
aah guyz sanatumidwe ndi abigman kuti amumange muthuyo chinari chiganizo cha iye yekha maringa ndinjarayi ndikukhala kwantawuniko mwina angakwezeredwe maripiro zamanyi nkhosi ngati chiwara basi .,,,
aah guyz sanatumidwe ndi abigman kuti amumange muthuyo chinari chiganizo cha iye yekha maringa ndinjarayi ndikukhala kwantawuniko mwina angakwezeredwe maripiro zamanyi nkhosi ngati chiwara basi .,,,
Thats bullshit kodi apolice aku malawi bwanji kupusa? Nde akatsekula mulandu otichani? ok akakalowa mu khoti adzikalankhulana ndi billboard not wapolisi kapena wina aliyese chiboard cho chidzikayankha!! muthalikayo ndi mulungu?
Nkhope kuopya or Ine ndikhoza
achita bwino ku genda
What’s going peter ukufuna kulondola abrz ako?
Kkkkkk musiyeni ameneyo kagwile ama cashgate ndiye chaniso hahahaha
iz ndizoputsa tsopan mpaka pamenepo ndie anthu tidzikhala