Man arrested for stoning President Mutharika’s face on a billboard


Peter Mutharika
Peter Mutharika
Mutharika: Stoned

Chikondi Saidi aged 26 is in the hands of police after he was seen with a pile of stones at Lunzu, Blantyre stoning an image of Malawi President, Peter Mutharika, police say.

According to assistant Police publicist in the Southern region, Peter Mchiza, Saidi was netted after the law enforcers got tipped by some people in the area about the incident which took place close to Lunzu Primary School .

He was stoning Mutharika’s billboard which has messages about Decent and Affordable Housing Subsidy Programme which is being championed by the Democratic Progress Party (DPP) led government.

Police fear that the acts by Saidi who hails from Mazale village in Traditional Authority Kapeni in Blantyre culd have stirred violence.

1,317 thoughts on “Man arrested for stoning President Mutharika’s face on a billboard

  1. kkkkkkk koma Malawi zomangana wafika pena yaaa akayankha mlandu wotichani sono? haaa ine ndikapeza zima post zake ndimang’amba bullshit

  2. kkkkk mbuzi za anthu pali chifukwa chomumangira munthu pamenepo? Kodi mwatha mapulani chani? Mukuwona ngati nthawi yakamuzu ino? panotu tili mu fourth generation sizopusa mukupangazo.

  3. Kkkkkk apolice njala yomweyo mpaka misala. Ndayenda mayiko osiyana siyana ndikumawona zikwangwani za president zikung’ambidwa. What more peter, no,no,no iwe wapolisi wayamba misala. Talimbanani ndi awo akutibela ndalamawo. Apa wawonetsa moyo wawukapolo apa . Kapena anaba ndalama zija ndi abale ako? Bwanji osakamanga awo akugwira ntchito yowona za ndalama. M’masuleni munthuyo , pangani manyazi ndithu.

  4. aa wat z billbords? Z dis 1 maize? Or maybe z electricity? .aaa fokofu peter asandisokoneze mutu wanga owila karewu ndikukwera kwazi2 ngat mukumane naye wagendayo mumuuze kut adzatenge miyala ina kuno kut akammalizepo bwampiniyo. musayerekeze ku ndipeza ku inbox inu aphwawo a pitala ndikuswana ngat lambe ndi2

  5. aah guyz sanatumidwe ndi abigman kuti amumange muthuyo chinari chiganizo cha iye yekha maringa ndinjarayi ndikukhala kwantawuniko mwina angakwezeredwe maripiro zamanyi nkhosi ngati chiwara basi .,,,

  6. aah guyz sanatumidwe ndi abigman kuti amumange muthuyo chinari chiganizo cha iye yekha maringa ndinjarayi ndikukhala kwantawuniko mwina angakwezeredwe maripiro zamanyi nkhosi ngati chiwara basi .,,,

  7. Thats bullshit kodi apolice aku malawi bwanji kupusa? Nde akatsekula mulandu otichani? ok akakalowa mu khoti adzikalankhulana ndi billboard not wapolisi kapena wina aliyese chiboard cho chidzikayankha!! muthalikayo ndi mulungu?

Comments are closed.

Discover more from Malawi24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading