Four Councilors arrested for stealing public funds

Advertisement
Malawi24 Breaking News

Police in Mangochi have arrested four councilors for stealing money from the district’s council.

According to Mangochi police, they are yet to establish the amount of money the councilors swindled but they are investigating the issue. arrested

Police further said that they will hand over the case to Anti-Corruption Bureau (ACB) once they finish their investigations.

*This breaking news story is being updated, please visit this page again as more details will be published shortly.

If you want to receive all the breaking and latest Malawi news alerts via email, subscribe in the comment box below.

Advertisement

60 Comments

  1. Mbatata yikakula siyiwongoleka. Awa musawasiye akwizingeni, alowe khoti, liwaponye kundende. Awa ali pa school ya Ucashgate, mukawasiyilira mpaka kumaliza univesite yawoyo nde akayamba ntchito yokaba mabilioni ku Capital hill. Akufuna kuti aziti boma lilipoli lalephera kupanga zitukuko pamene iwo akuonongela dala ndalama za ife a Malawi. Uchindere pela. Ving’unu na ise yayiii!!!

  2. Yapa nde mwauyamba dala unyolo utangokhala pakhoma, akukwidzingeni basi, umbava opusa nawo umenewo. azimanga ogenda chikwangwani nde inu angakusieni?? Mukaisova konko pitani

  3. Ndibwino nangasi mmati ndi amayi ndi chipani chawo cha PP nanga akubawo ndi a PP? Mwawonatu baza zili m D pwi pwi mwaziona nanga muti chani pamenepo

  4. Amphatso ndiye mwafa makutu,kodi njala kapena. Nankha ati ku machinga tawelengani kachikena kape simumatha kusiyanisa machinga ndi mangochi eti?

  5. Yaaa ulamulilo ukamavuta ndichoncho iban bas asamatitenge ngati siyanthu tizasiya kuba zikazayamba kuyenda bwino tikhaulitsanapo pano

Comments are closed.