Crooked Police officers helping thieves in Mangochi

Advertisement
Malawi

policeMalawi Police officers in the southern district of Mangochi are reported to have been sending thugs to steal from people at night in the district.

According to reports, the officers have been giving thugs a list of people believed to have property worth millions of Kwacha in the district so that the thugs should steal from the residents. The cops assure the thugs that they will have a police bail once they are arrested.

After a spate of robberies in the district, residents embarked on a sweeping exercise that led to the arrest of two suspects who mentioned some police officers as their crime bosses.

Mangochi Police spokesperson Rodric Mayida confirmed the development but refused to mention the names of the officers involved.

Meanwhile, residents of Mangochi have threatened to take laws into their hands if the officers are not arrested and dragged to court.

Advertisement

96 Comments

  1. Wapolice woteloyo azivala kabudula wa kakhi ndi ka skiper ka black, kuti aziwonekera patali anthu azingoti uyo!!!!! galu wapolice wakuba.

  2. Fuck dem up!!! Apolisi a pa mangochi ndi mbavadi even a pa roadblock pa m’baluku nawonso amatibera tikamadusa ndi katundu wa Joni….

  3. Zikapanda kuyenda bwino za mlandu uwu okha, ife nde tagwilizana kti tiyendera payere payere mopanda kuopa ngakhaleso kuwelengera udindo wa munthu. Zatikwana tizichita kuynda ngati tili dziko la eni. Maka maka uyu wapolisi yemwe akumutcha kti #KACHIPANDE aziona ndipo tibweza pachilichose chomwe akhala akuchita.

  4. Zikapanda kuyenda bwino za mlandu uwu okha, ife nde tagwilizana kti tiyendera payere payere mopanda kuopa ngakhaleso kuwelengera udindo wa munthu. Zatikwana tizichita kuynda ngati tili dziko la eni. Maka maka uyu wapolisi yemwe akumutcha kti #KACHIPANDE aziona ndipo tibweza pachilichose chomwe akhala akuchita.

  5. chifukwa chani mukubisa maina a police? koma chilungamo chioneka pankhani imeneyi? Tikudikila ndi chidwi tione mene zithele!

  6. Inu amenewo? Simangochi yokhayotu paliponse apolisi akuchita izi. Kuyambira lero wa polisi aliyense mfuti azisiya ku office.

  7. Mungowasamutsako KuMangochiko Azolowela mukawawasiye kopanda magetsi kopanda misewo yabwino

  8. Akulu anat mbuzi imadyapamene yamangililidwa apa mbuziyi ndiye sinadye bwino iyenela kuphedwa chifukwa tikayisiya ititukwanitsa zachisoni wapolice kkkkkkkkkk

  9. Akulu anat mbuzi imadyapamene yamangililidwa apa mbuziyi ndiye sinadye bwino iyenela kuphedwa chifukwa tikayisiya ititukwanitsa zachisoni wapolice kkkkkkkkkk

  10. If this is true then malawi police services should stop it fanctions here in malawi and legalise mob justice, I think this will be better than these wolves in a sheep skin.

  11. Mmmmmm a police ndi mbava, wina anali pa chimwala amaphunzitsa anthu kuba kwa mwatakata deal itafoila anamutumiza pa boma. Alipo ambiri & Bola kumangowaotcha.

  12. Police yapano ukulepha ntchito achinyamata asanafufuze kuti khalidwe lowo komwe amakhala ndiwotani? Mavuto amenewa akuluka, tisanamizile kuti akulandila ndalama zochepa ayi mene akayamba ntchito salary amaziwa kale kuti ndi 52pin bwanji samakana ntchitoyo

    1. Its 2ru..kachpanded anali muth wausilu,even ineyoso anandwonesapo mbonaona..bt ppo shud also b listng de names of others

  13. Ndikudziwa kuti wapolice wina akuwelenga macomments wa yangai uwelengeso galu wolandira zonyenyeka iwe,,ngati umapanga nawo nkhalidwe umenewu udzawona zoophya kuno nzako wina anadulidwa manja nkhani zake zomwezi,,shut up!

    1. Kungomugwila… dulilanitu mikono yake yonse mukapanda kumutero ndikumupititsa chabe kuchitolokosi/kundende sakakhalako koma mulangilethu anthu amchitidwe oyipa iya!

  14. Ndye MMalaw ameneyo alwz need money without consder any consquences that wl come through those shupiti waz,akumawalembanso ntchto ngat ku G4s

  15. What a hypocrite !! pretending to help but on the ground engaging in malpractices which always leads to catastrophic outcomes , THAT’S ABSURD !!

  16. That’s it! And it is not only Mangochi but across the country. Keep reporting Malawi24. We rely on you. This is role of media. Investigate and report for public to know.

  17. Why is he refusing to name the officers? Ndiye kuti iye (Maida’yo) alinawo m’gululo. Koma ngati akutero I just beg the pipo should take the law into their hands.
    Police inali kale!!!! Nowadays aaaaa!!!!!!

  18. tandipatsen phone number ya mabwana akupolisi ya ku mangochi ko mwina nafe angatipatse deal si bail akumapeleka ulere

Comments are closed.