Woman arrested for stealing village bank money

Advertisement
Money currency
Money
Money missing.

Malawi Police in Machinga district last week arrested a 23 year-old woman for stealing K751,425 belonging to Kanthumkhama village bank.

Machinga police confirmed the incident and identified the suspect as Elizabeth Mbewe who was until her arrest an executive committee member of Kanthunkhama village bank.

Machinga police spokesperson Davie Sulumba said some shortages were noticed in the group’s account and the members agreed to scrutinise their transactions.

“They found out that some transactions were not in line with the rules of running the affairs of the bank and other transactions were not endorsed in their register,” said Sulumba. The suspect will soon be brought to book to answer charges of theft which is contrary to section 271 of the penal code.

Mbewe hails from Naphuti village in the area of Traditional Authority Chinguza in Machinga district.

Advertisement

71 Comments

  1. mmm nanga madera enawa poti ena amafika pozipha chifukwa chosowa ndalama yobwenza izizi izi sizotjandiza nzongobweretsa mavuto kuti muone anthu avutikila kuti abwenze tindalama anakogolato mmmm chisoni wina nkungonyamula mmmm zingotha zatibweresera mavuto ambiri mmidzimu

    1. Women of malawi al these it’s coz of umphawi nothing else stop embaracing urself there’s lots of ways u can do to help u achieve in ur life not stealing someplps sweat

  2. Tikuti ndalama kulibe kubank pamene mukudzibela. Agalu inu this is not fear to the poor people. Oder this very unfear you must very stupt. I’m emmanuel from zanzibar, i’ll not back home (blantyre) like abeid kalume.

    1. Heeeeede Munthu Wakunja Kulemphera Kulemba Chizungu By The Way Who Was Ur English Teacher Go To Hell With Ur Poor Grammer If English Is Aproblem Why Cant U Write Chichewa Kufuna Kutchuka Basiiiiii

  3. Anthu akusonkha ndalama kupatsa ajakapu kuti eni, tatisungira. Ndiye wochangamuka pa tawuni akumazitenga kukapikula ufa ndi simenti ku Tete, Chipata, Petauke kapena Dar es saalam. Kuthamanga, ikaduka ndiye akuthawa usintha ma contacts. Ndiye opusa aja akumapita kunyumba ukatola zotsala monga mabedi, mbale, mitsuko, mphasa kuti agulitse apeze zawo. Pitlizani ndi bank mkhonde yanuyo. Ena azingobwera kutenga zose kulowa nazo pa Mozambique. Malawi ino? Kadziko kochepa koma anthu akumangoganiza how to rob someone or group. Anthu mantha adatha. Atapusa kwambiri nthawi ya Ngwazi. Tisiye ukhulupilira munthu or gulu la anthu.

  4. Kkkkkkkkkkk koma ma thokozani!! Zot kuli miracle money simukuzwa hhhhhh mpaka kuba za vg bank hmmmmm zochtitsa manyaz ma thoko!!!

Comments are closed.