Scare after woman kills her three kids in Mchinji

Advertisement
knife-blood

knife-bloodA few days after a Blantyre based man Charles Chipanda committed suicide after murdering his wife and step-son in Zingwangwa Township, a woman believed to be mentally ill in Mchinji has killed her three biological sons using a hoe handle.

The woman murdered the children in a garden where the family went to gather mangoes.

Police identified the woman as Violet Eliya, 38, of Manthalo village Traditional Authority (T/A) Mavwele in Mchinji district.

National police spokesperson Nicholas Gondwa said the three murdered children were aged eleven, nine, and five.

Police have since advised people in the country to take good care of people who are mentally challenged and make sure they are monitored in their movements.

Eliya is currently in police custody while police investigations on the matter are underway.

Advertisement

27 Comments

  1. Ndikabwera ndizawatsekulira milandu anthu awa Adokotala chifukwa chosabaya kulera wamisalayo 2 akubanja kwawo chifukwa chomusiyila wamisala ana ambirimbiri

  2. guys 2016 ma murder achuluka tipemphe chisomo cha mulungu

  3. Mungomumvesa mayiyu coz akuti anadwalapo misala ndye zikuoneka kt misalayo inagundkaso thats y wapha ana ake omwe azapanga regret kmaxo azalira zikazamukhuzumuka

  4. Dziwanda dzaswana dzili ndzidzukulu.Ambiri alandila kudzodza kwa dziwanda mphamvu yakumidima.#THOCCO vuto si anthuwa n tikhonza kupha anthu ambiri pa tsiku limodzi chifukwa sizinati mkuyamba chabe udziwe.Sizikufunika nkhondo ya kuthupi ya zida koma ya uzimu yopha dziwanda dzili mwa anthuwa pogwilitsa ntchito #PEMPHERO not only pemphero koma #LACHIKHULUPILIRO

  5. That’s the problem we have in Africa. We want to think kuti amisala amadziwa zomwe akuchita. Which is not the case n kuli misala yamitundumitundu. That woman was supposed to be ku chipatala n shud be admitted there now. So sad people had to wait for her to take three little ones

  6. Osangomupha bwanji? nanga akadzaphanso an2 ena? wamisala sangaphe an2 atatu nthawi imodz ndi mpini wakhasu unles t was knife. she was jst tired of feedn de kids

  7. Osangomupha bwanji? nanga akadzaphanso an2 ena? wamisala sangaphe an2 atatu nthawi imodz ndi mpini wakhasu unles t was knife. she was jst tired of feedn de kids

  8. Koma chakachi ndiye sitinachiyambe bwinotu. Tikhalira kuphana basi?

Comments are closed.