Police still investigating Machinjiri man’s gruesome murder

Advertisement
Machinjiri robbery

Malawi Police in Limbe, Blantyre City say they are still conducting investigations on the incident that occurred in Machinjiri Township where a man identified as Pirilani Wailesi was found dead with some body parts removed in a bush in the area.

Publicist for Limbe Police Pedzesai Zembeneko said the 25 year-old’s body was taken to Queen Elizabeth Central Hospital (QUECH) for a postmortem.

Machinjiri robbery
Pirilani Wailesi : Slain mercilessly.

Zembeneko said the police are also investigating to find the cause of the deceased’s death.

According to Zembeneko, for now they will not provide further information to the media on the incident.

Wailesi hailed from Mtema village in Chiradzulu district and was found in the bush with his teeth and private parts removed.

Advertisement

42 Comments

  1. Ngakhale yesu akukanpachika pantanda anthu okhulupilila pomunvela chisoni anali kulila kwaiye ambuye mukatikumbukile ife koma iye anayakha molimba ntima kuti ngati athuwa achitila izi ntengo wauwisi kulili owuma nde kumangokumbukila mulungu ndikumuyamika poti athu oipao nde ayamba kale kupha wathu nde kungokonzeka basi

  2. malawi,,, police,,,, sagwila akuba kapena zigawenga,, anthuwa ndi amozi,, zimayimbila ma fon,, kuti mukabe,, ku bangwe ife tikhala tikugwila anthu olezela kwa kachere,, ndiye police ingakuthandizeni chani,, mbuzi za apolice,,

  3. Ndili Ndi Mantha Kut Tizalankhulanji Pa Tsiku Lachiweruzo. Zonse Tikupeleka Kwa Mulungu Awone Nawo Chochita Onse Akupha Anzawo Iwo Nakhala Odyelera Sakuyang’anila Ayi Ali Tchelu Ndithu.Mukumbukire Anyamata Anaphana Okhaokha Aja Ku Blantyre Phunzitso Labwino Koma Mukukanikabe Kumva…………………

  4. Kafukufuku osa bala umboni!mwafufuza nkhani zingati?munabwela nkune kuti mwapezanji?poti ndife opanda mayina tuphedwa ngat nkhuku,akadzakhala wanu mwana kumchita zotele umboni ndiwochita adzapezeka
    #failluers.

  5. m fed up of hiyelin these fuckin issues. ur lucky if a had a sniper,a would hav made u return to de dust. bcoz u dont hav even a dot significances pon de world.fuck u de MURDER. !!!!!!!!!

  6. m fed up of hiyelin these fuckin issues. ur lucky if a had a sniper,a would hav made u return to de dust. bcoz u dont hav even a dot significances pon de world.fuck u de MURDER. !!!!!!!!!

  7. m fed up of hiyelin these fuckin issues. ur lucky if a had a sniper,a would hav made u return to de dust. bcoz u dont hav even a dot significances pon de world.fuck u de MURDER. !!!!!!!!!

  8. Kodi inu a Malawi 24 simunthu yemwe munkamunena kuti ndi mbava uja ameneyu? And amalawi onse akumalemba ma comment achisoniwa were in the forefront cursing the innocent man and celebrated the horrible death of the innocent victim. The first thing I expected you to do was to apologise to Malawians and the family of the victim for your misleading story. Muli ndi atolankhani otani?

    If you read my comment in your first miserable story on this guy, you will find that I denied vehemently that the guy is a thief bcoz evidence imachita kuonekeratu pa zithunzi zano kuti munthuyu waphedwa. I was only one of ten people out of more than 200 people who said the guy was a thief. And today I repeat what I said in my comment that ‘I don’t believe in your cheap thief theory’. I am a radical citizen who can’t be easily swayed by cheap propaganda than the other guys.

  9. kod misika yogulitsa ziwalo za Anthu ku Malawi pano likulu Lake lilikuti RIP innocent Man shame on killers and Woe to û

  10. Malawi police service osadandaula, ife a Mob justice service tikufufuza tikapeza anthu amenewa mumva..inu kafufuzan ogulitsa chamba, ogwilira ndi kuchotsa ana opepha miseu.

  11. Malawi government you have to increase number of police and police unite in the country, now in Malawi have more criminals than a number of police officers!

  12. Zifukwa zina zomwe zinthu zikutivuta mMalawi muno nzimenezi,Mmalo moika God patsogolo tili busy ndi kumphana enanso gay coz mvula Mulungunso wasunga shame on you stupid people

    1. ITx thanx but me I exclude coz I never taste man to man but man to girl so the stupid is a person who taste it ndaku3la u r number one I can’t include myself sorry

  13. Why guys? in hire SA people are killing each other whith a gan but this thing never so what are you doing whith human being skin? eish my malawi

Comments are closed.