Just in: Moses Kunkuyu dumps Peoples Party

Advertisement
Moses Kunkuyu
Moses Kunkuyu
Kunkuyu: Out of PP.

Malawi’s ex ruling Peoples Party (PP) deputy publicist Moses Kunkuyu has resigned from the party, Malawi24 can confirm.

Kunkuyu, former Blantyre City South Member of Parliament, made the revelations a few minutes ago at a presser currently underway at Mount Soche Hotel in Blantyre

Kunkuyu, hit headlines as one of the youthful law makers in the August House during the Bingu wa Mutharika era before Mutharika died and Joyce Banda picked him as Minister of Information under.

He has since not cited reasons for his leaving PP.

Advertisement

93 Comments

  1. Ndale zomayamba chifukwa cha umphawizitu zimatero…..chonchi mukuononga mbiri ya achinyamata kuti achinyamata ake akumalowa ndale atalema ndi umphawi nde nzeru zikumathawa akaona ndalama……..khalani pansi basi musakasokonezenso kwina.

  2. Konkuyu,umalimbana Ndi Pp Themu mwana wa jzu wachepa kapepese kwa jzu ndi pp Themu mcp ikuganizira,chita ngat sausage gwengwe uyambe campeini mcp 2019 idzakuganizira

  3. Rubbish,stupid,So what ? myopic ,greedy ,liars,thieves,malawi politicins.Why dont you talk abt developing malawi ? We r tired of hearing of politicians changing parties,following where GVT pulse is, stupid.We want politicians who cn bring developments.

  4. That is frastration. He Thought He would be the one to be the acting president.His dreams haven’t come true.

  5. Sangawine kwathu ku Dedza south MCP idamanga nthenje ife pambuyo pa Chakwera #2019 government in waiting

  6. thus y I hate politics serious. wts all dis bullshit? I dnt blv in politics. akatero akaloweso DPP azikanena zabwino zabwino zokha zokha. ikadzaluzaso adzatuluka kukalowaso cholamula. pachiphwisi panu andale nonse!

  7. Kkkk mr kumkuyu…what ajourney so which way? where to.Mwamudyeradyera JB mukumuthawa…Free advise, make adecision that will never let u down..Politics in malawi has destined aclimax of regionalisn and tribalism.The time u were in blantyre u could maintain ur seat if u were focusing onthe welfare of the pple and not wasting ur energy with political prostitution..Ofcourse you went to Dedza after u sensed danger of stiff competition.Now u made amistake to stand on a pp ticket in aconstituency where MCP is their culture..It could be better if u had decided to even stand as an independent…It is my hope that ku PP mwatengako zokwanira kuti muchite survive….leave politicts to politicians……..

  8. nngti kuli mnthu wandyera munthu wake ndiyemweyu munthu siwandale amakofuna popezera ndalama basi osati pautsogoler palimbe munthu utsogoleri mulimbe.tikumuziwa nzeru zake sitsimtsogoleri.

  9. Relo malawi ndi malawi yamoto
    tiyen tizingo kwatiwan amuna okhaokha bas akaziso chimodzimodzi osalimbanaso ndi ndary

  10. Inu andale ndi athu adyera awa ndiye ife musatiuze kti breaking news timvaso kti ampatsa udindo ku dpp mxie cashgate country in the word

  11. Hahaha zake izo ine ndili nchipani changa msogoleri ndine vice mkazi wanga ku youth wing kuli mwana and none of us can resign our party coz we are united ndipo palibe analowa nchipani chathu ncholinga chozadyera nzake.

  12. Ambiritu mtizipanimu ndi aganyu basi. tindalama ta cashgate akamanana muwaona akutuluka. Even osokosa pa fb ambiriwa ndi ulovatu basi. Akawalipirira rent ndiye iiii kutukwana anzaofe kwabasi. Mutipeze ku kongeresi kuno.

Comments are closed.