Man to serve 10 years in jail for violent crime

Advertisement
Arrested.

Arrested.A 29 year-old Malawian man in Ntchisi has been handed a 10-year jail term for stealing maize and stabbing the owner with a sharp knife.

Police in Ntchisi nabbed the man, Hejasi Tchale, after he was suspected of stealing maize belonging to Jonasi Sitola and stabbing him seven times on the arm.

According to police, the incident happened on the night of 17 November this year when the convict went to the house of Jonasi and stole a bag of maize. After hearing a strange sound, the owner started chasing after Tchale.

However, the convict stopped after running for a distance and the two started scrambling for the bag of maize. It was during the scramble that Tchale produced a knife and stabbed Jonasi seven times on the arm.

Tchale hails from Chipoka village in the area of Traditional Authority Kalumo in Ntchisi district.

Advertisement

44 Comments

  1. mwapanganji man muchingobwera kuno ku jons kuti mudzaone momwe anthu amasinthira moyo sudakadzabaso ee 10 years zizohezatu udzapeza ndiri ndi ana awiri ambwana

  2. Mwammangilanji munthuyu?? Mlekeni nayenso ali ndufulu wokuba monganso ufulu alinawo ma gau.Milandu ya anthu okuba ndi ena okupha sikumveka mpaka pano zaka zikutha milandu ikadaweruzidwabe pomwe osaukafe kupalamula lero sikulomwero nkhani yaweruzidwa + chigamulo mkupelekedwa.IMFA YA MATAFALE+CHASOWA kwa mangidwa anga????? #MULUNGU adzaweruza inu oweruza dziwani

  3. Zachepa zakazo….. Kuba + Kufuna kupha guys tawerengerani bho bho munakakha inu, muziganiza b4 kuyankhula.

  4. Anthu. Monga ma mp and president anthu amenewa amatiwotsa zinthu zoopla kwambiri akuziwa kuti Ku Malawi ntchito kulibe anthu ambiri adzikomo ndi osawuka akayitenga kuti k26000 ya fertilizer izi amatipanga chifukwa chokuti samatiwopa Koma I hop that people from Malawi will change our mind very soon tiyeni tikhale ngati anthu a ku south Africa ogwilitsana zochita boma likati no ife yes boma ikati yes ife no please guys

  5. who is a ntchisi magistrate guyz dis guy he doesn’t think whn he hand years to convicts why? koma asamayende kutali meneyu just send me his or her full name I will ssort this assholes for u pipo of ntchinsi infact of Malawi

  6. “this hapened on 17 november this year” hahahahahahahaha malawi24 imeneyooo

  7. zaka zachuluka mulandu wakuba chimanga chomwe ndichakudya boma lili masomphenya pa anthu pls njala ndikanyama kena

  8. Koma umphawi sikanthu inu kampeni kanuko 10yrs mukaseve anzanu amaombera mulandu wao umathera pa belo. Mmmm zakuvutani basi

  9. Mmmm sidzinachuruke coz munthu yu wapezeka olakwa pa
    milandu yiwiri; —
    –Kuba katundu…
    –Kuvulaza munthu ndi mpeni….

  10. Zakazo zachuluka zikadakhala zitatu bolani koma ten.majajinso mukuonjeza kwambiri mukuonangati zaka ten ndichibwana eti.

Comments are closed.