Girl commits suicide in Nkhotakota

Advertisement
Kasungu

A form four student at Lozi Secondary School in Nkhotakota, Cecelia Kazala, was found hanging in the early   hours of Wednesday morning after committing suicide, Malawi Police say. 

Death hangingAccording to her family members, the deceased, 21  cited no reason for the act but left a letter which strongly advised the members not to    accuse anyone for her death and asked the    father of her child to take responsibility for the   child she has left behind.

“Don’t accuse anyone on my demise. I have   decided to do this alone. The father of my daughter Chrissie should take responsibility.  I    wish you all the best,” reads the suicide note.

The 21 year-old woman went missing on Tuesday, only to be found dead a few metres from her house the next day.

According to postmortem results from   Nkhotakota district hospital, the deceased died due to strangulation.

Meanwhile, Nkhotakota Police have since ruled out foul play on the death of Kazala.

Advertisement

143 Comments

  1. Ya maganizo onse ndiomveka koma ndisusane ndiomwe akunena kuti ndisatana akugwira ntchito musanamizire satana bible linati izafika thawi even satan azakukanirani kuti indedi ndine wosokoneza koma na izi ayi mufuseni mwiniwake ngati ndine mwaona ndiye tisamare mukamamutamanda chonchi satan amakodwa osamamutchura azazorowera sharp wapita wapita lets luk onither isues dts all its time no wry

  2. Tiyeni Tipempherere Nkhotakota Chiwanda Chimenechi Chaonjeza Anthu Awiri Ozimangilira Week Imodzi.Kuti Tiwerengere Chaka Chonse Ndiambiri.Mzimu Wake Uuse Mumtendere.

  3. Chodandaulitsa ndichakuti wathawitsa dinkamu amuna asanaigwire ntchito mokwanira,komabe she has created space 4 others to live in replacement 4 her,RIP.

  4. MULTIPARTY NDI NKHONDO(H KAMUZU BANDA) INU ANA ASUKULU TISALOWELERE NDALE, NDALE NKANYAMA KOOPSA(JOSEPH NKASA) ~mau kwa amene akunena za CHASOWA.

  5. Ooooh mulungu wanga khululukileni munthu amenei, ife tilibe chiwelunzo. Inu ndiye mwini zonse, kwaife kupepha chikhululuko kwainu mwini zolengedwa zonse. Ameen

    1. wofa mu uchimo wakudzipha, wafa muuchimo bas, olo mutamulapira a million times Mulungu sangakhululuke chifukwa ndiye kut azitsutsa yekha pa mau ake omwe woti Kudzipha ndi Ntchimo. “Wafa wafa kulibe kulapirana (its a song)” Munthu wa nzeru amasalalitse chimaliziro chako Deuteronomy 32:28/Matthew 24:13

  6. A form four student? Why are we so stupid in this way Malawi’s? Read the Bible please so that we can get the ways to handle matters. It’s my plea to thee black stupid and foolish people who thinks that by killing our selves we’re solving problems.

    1. I think this is not a time to shouting to a suicide girl/everyone who committed suicide. We never know what makes a great matter like this.

      It could be better to pray for this problem than just to shout. I know for sure that demonic spirits is working hard. Is always there to force the people of God to do things which very contrary to our creator God almighty. Though it doesn’t mean that we be belongs to this spirits “no*

      . Devil is taking the chances after discovery that we mustn’t kill ourselve. Is sin. So is forcing pple to get a sin & away from God.
      We are still in God’s hand, & is the same God who will not let them (suicide pple) to go to hell.

  7. Komano mpaka kuzimangilila mavuto ake ndiochuluka motani zingavute zingawawe i can’t to died chifukwa chozimanga auze anthuena mavuto akokuti athandizepo mzimu wake uwuse mumtendele

  8. pepani akubanja limenelo poti mulungu anati muzafandithu koma chofera sanachitchure kaya ulinyumba ukungona ungowona yensu wafika

  9. That is a very bad. Lord have mercy on them because they do not known for what they are doing. Still almighty God have mercy on them coz is creation.

    1. Mwanena mawu abwino anthufe ndiwofunika kumaunikirana kuti tizidziwa vuto lililonse lilinditsiku lothela.kunali ayobu anakumana ndizokhoma kuma zinawathera.

  10. tikhoza kulankhula mmene tingathele koma chilungamo akuchuziwa ndi Mulungu, panopa ziko lafika poopsa kwambiri ngakhale kumbali imeneyi yopeza munthu atizimangililazi sionse amene akumazimangilila okha, zinachitikako kwina kwake anthu kuchokela limodzi pobwela kupezeka mmodzi wapezeka atizimangilila zosatila zake anthu paja ndemene anamupanga chipongwe nkumangilila pantengo, nde ineyo sindikulesa anthu kuti amazimangilila, koma ena amapangidwa chipongwe ndithu, koma zomvesa chisoni

  11. zosakhala bwino, amakhala satana akuwagwilitsa ntchito anthu ozimangilira. Sikumakhala kufuna kwawo koma devil ndi amene amawapangitsa.

  12. Sad. Life is so sweet. Always share the burdens of your mind with a trusted friend or relative. RIP Cecilia. May the Lord have mercy on you.

    1. mmmmmm their very few pple who cud understand u.others instead of listening they start judging u. I choose to keep silent but I tell u it hurts alot

    1. The reason we both can’t understand is that scientists have not been able to invert machines to measure mental pressure.

      1. Ambuye munampanga ndi manja anu ndipo ndi ntchito yamanja anu
        Tikukupemphani adayesetsa adakali moyo zamukanika kulimvesesa dziko lapansi ndipo wazikakamiza kuchosa moyo wache pazifukwa zoziwa iye ndi inu mulungu wozowa zobisika. Komabe musapepuse ntchito ya manja anu ambuye. Mulandireni ndi mtendere wosatha kuti waipayo achite manjanzi ndikiti azondikire kuti zonse ndizanu.

        Ause ndi mtendere wosatha Ambuye. Amen

    2. kuziphako,. thats being stupid,, c’mn joe u mean iwe mavuto ulibe? u do bt stil umapilira,,, nde uyu akuzpheranji? problems dnt last okay..! no need to feel sorry

Comments are closed.