Unknown assailants shoot DPP Treasurer

Advertisement
Happy Kumwenda
Happy Kumwenda 2
SHOT: Kumwenda

Malawi ruling Democratic Progressive Party (DPP) treasurer for the Northern Region, Happy Kumwenda is admitted at St Johns Hospital in Mzuzu city after unknown men shot him with a gun Monday night , according to reports.

Malawi24 has been tipped that Kumwenda was shot on the back by three men who drove in a Saloon car shot him at his residence as he was talking to his guard at the gate.

“A saloon pulled up, there were three men in the car, one of them took a gun and shot me,” he said.

However, the DPP is yet to make a statement on the matter.

Happy Kumwenda
Deadly.

At the moment, Kumwenda reportedly says that he knows one of the people that shot him, something which police are not taking into account as of now and have reportedly instituted a probe into the matter.

 

WE WILL GIVE YOU UPDATES ON THIS MATTER.

Advertisement

139 Comments

  1. kuomberedwa kwamkuyu kuli ndizosatila zake amalawi takuziwani masiku ano mkafuna kuba mkulola kupha wachibare wanu kuti munamizire zoti ndiwachifwamba (kwa ine ndikuti bwezi akanafelathu madotolo msamupase mankhwala afe ameneyo kuba kwake kwamuyika mmavuto)

  2. wamwano ameneo ku bar kumeneko masiku achisangalalo ano taganizani mozama amalawi fut malo ameneo sangakhale ndimoyo ai akadafa ndithu koma amalimbilana azimai nanunso muzi mukamatumiza khani muziamba mwafufuza bwinobwino kenaka nkumapangano post khanio fut sichida chamasewela ai musatinamizepo apa cholinga akazi ake asakhumudwe, kuti amalimbilana mahule.

  3. What kind of pollitics are now you doing malawian! If you ahave aproblem with someone just approach to him/her and tolk ,if u see is big issue go to count ! Wy actualy u want to killing each other there in malawi there z no money .

  4. I disagree with you who are saying DPP is worst , you comparing with which party ? We never develop in northern region bcoz we r continue supporting JB but what development did we get from her when she was in power ? Jb is gud leader but not gud politician thus y everything was crazy when she was in power,if you can see Malawi politicians every time is for compain they don’t care about poor Malawians, can some1 tell us how much they getting now per month

  5. DPP kodi ndaleyanu ndiyophana or bwanja anthu akufa kamba ka chipani chanu ndinu masataniki kapena mukudziwa chani nanu one day mudzafa mulungu naye ndiogwiya nanu pa muchitidwe wanu.

  6. I wont judge him untill we here the monster side of the story. Zitha kutheka mwina a maniwa amanyengaso azikazi a anthu. We neva know! ! Its not always abt politics

  7. Eeee kumpoto ubwino wake oyimba anayimba kale kuti kukanakhala kadziko bwenzi dziko lake likanakhala DRC Mulungu akusamalireni m’bale.

  8. Is it a shootgate since it happened at the gate?kkkkkkkkkkkkkk……

  9. TIONE NGATI ANENE NGATI ZA NJAUJU KUTI THEY STILL INVESTIGATING A DPP KOMA ANTHU ALIBE MANYAZI KUOMBERA PA ZIFUKWA ZOFUNA KUBA NDALAMA ZA BOMA KIKI!

  10. bas ukali mesa DPP siyikuthandiza pankhan yakalamulidwe kadziko. ndendibwino kutha azitsongolelewo Malawi yanyanya et

  11. These could be the ones that killed Njauju. They are blood thirsty. Remember they have not yet been arrested. Now terrorising the northern state. Kuno ndiye tithana nawo.

  12. Politics is a dirty game, there is something behind remember Paul Mphwiyo’s story. anthu andale Zophana ndiye kudya kwao. akagwidwa anthuwa ziululikaso zambiri just wait see

  13. Aliyense adzafera ntchito yache..
    Yamikani Ambuye poti wakupulumutsani ku imfa ya dzidzizi.
    Muli ngati wina pompo nkungosiyiratu za ndale, nkukayamba kutumikira Mulungu.
    Mukuona bwaaaaa??????????

  14. Kwathira zipolopolo basi akupanga zopusa, ndikamabwera kumeneko anga ma piston awiri alipo kale opanga zachambayo kungondiuza ndizidzagwetsa m’modzimodzi bola sodayo osaumila!

  15. Osadanda a treasurer kungoti amangofuna kuyesera mfuti ngati ilibwino. Muafunse abro mphw….. zinali ngati momwemunso kenako nkumamva kuti dollar zasowa, watch out!!!!!!!

  16. Mfuti yakenso inali ya plastic.koma apa myenera kuti ndinu nokhanokha chifukwa maprophet analosera kale kuti m dpp mzakhala chipwilikiti

    1. Malawi is no longer fearing God nation bro, how can you say that yet satanic are ruling us?
      tell me how can we say that we fear God yet we accept homosexuality?

Comments are closed.