Chiukepo, Bokosi share top scorers award

Advertisement
Innocent Bokosi

The battle for the golden boot award in the 2015 Malawi Super League season is over as it has produced joint top goal scorers namely Innocent Bokosi of Red Lions and Chiukepo Msowoya of Big Bullets.

Both Msowoya and Bokosi bagged 14 goals.

Innocent Bokosi
Bokosi (in red) tied with Chiukepo on 14 goals.

Msowoya had 13 goals before netting one goal in Sunday’s match against Civo United at Civo Stadium in Lilongwe.

The Big Bullets forward was required to score more than a goal against the 2015 Standard Bank Cup champions to overtake Bokosi.

The strikers will now share the Mk100,000 that was put aside for the golden boot award winner.

However, Msowoya and Bokosi failed to match the record set by Moyale Barrack’s Gastin Simkonda who netted 17 goals last season.

Advertisement

66 Comments

  1. Koma a noma mukumva bwanji kumayamikila ma player ama team ena inu mulibe ma player? Nanga anuwo amamenya league iti? Zigoli zawo ndi zingati? Kkkkkkkkkkk

  2. # memory ndi anoma anzako yakula ndinsanje m’malo moti muzikamba za Sulumba 5 goals 28 games mukulimbikira Geneza ngati ndiwa noma akugawirani ndalamazo, mufa ndi nsanje anzanu chikho ndiye tatenga mk15m pompo kuti dii

  3. Kkkkk walandila ndrama zingat??150, 000 neba ndye ukuona ngat amupasa ndrama zambiri eti nanga kuja adakatenga chithumwa kuja akapeleka chiyani ndramayo yachepa potengela ndithawi yomwe imatalikilla ka

  4. Chiukepo zamanyazi zuro kuthamangirj kwa ref kuti amulembe kuti wachinya chigoli kkkk ref ati wopanda mzeru iwe et?ukuwona ngati ndasizina?civo yazibaya yokha iyi hahahaha!chiukepo,fisher akapume akalamba awa azafera graund.

    1. Kkkkkk wagwanayobe khalamba wanuyo R150 000 ingamupindulile chiyani nanga mwana adamukhwimila uja kwamakolo ake akapeleka chiyani sikhani zotukwana apa ai player yemwe amandisangalasa ndiuja munamupanga sadaka uja #Daga eish RIP INE NOMA 4LIFE BYEEEE

    2. Koma anamveysa chisoni munthu kulilira chigoli…..Chimdala chanuchi ife sichimatiwaza ndiponso amanveka ndimbiri zoipa heavyyy

  5. kkkk ndie kuti amafuna kuba cha no. 15 chija madalawa ? Bokosi he is a gud striker awa zachulukitsa ndi zamapenote kip it up bokosi

    1. Ndye ukut striker ameneyo hahaha dolo ndinzakeyo bas muone eye amupasa 100,000 ingamuthandize chiyani ndye mufuse bokosi kut walandila ndrama ndichani kkkkk muzizisata osamangodya mango ai ok

  6. Ma game onse omenyedwa top goal scorer kumakhara ndi 14goals basi kkkkk koma chonchi mkumati frames ingafike pati mastriker ake bwembayu

    1. Iwe ukufuna unene kuti chani ndikunena zama top goal scorer not kuti zigoli zikuchepa kuti akwanise kuteteza frames ndiye ngati iweyo ukuziwa zampira ukhare ndikuIndikira usanapange respond uzimva chomwe munthu wanena sindinanyoze prayer wa club kharani maso man

    2. Iweso sunamve chomwe muthuyo wayakhula ka vomelezani kumalawi kulibe mastriker sindikutengela term yomwe ndimakwela ai komaso sindigwela term yamakepe ndatchula muthu apa ndye kape wina atukwane tilandana account uwonatso

    3. Honestly ma striker ochinya akuvuta and its a world crisis mateam ngati Chelsea,madrid,liverppol Ac milan akufuna ma striker komano pamsika palibe

    1. ukafuse tshabalala zomwe adaona ndi khune wa sundowns pa ma fina
      ls a Telkom knockout. ngati zigori za ma penalty samawerengera wav

Comments are closed.