Mwanza residents mercilessly kill suspected thief

Advertisement
Mwanza Thief

At a time when Malawi Police Service continues to warn people against mob justice, an irate mob in Mwanza district chose to ‘deal’ with a man they caught stealing their own way.

Mwanza Thief
Slain.

According to Police, the people  on 23rd December caught a man aged 47, whose names are yet to be given was caught breaking into a house together with his accomplice.

‘’They managed to break into two houses and when they were breaking into a third house, they were caught by the angry community members. The deceased friend managed to escape and the mob beat up the culprit severely to death.’’ Malawi Police Service posted on Facebook.

According to police, the slain thief died after he unceasingly bled internally.

‘’The Malawi Police Service is advising the general public however, to desist from taking the law into their own hands.’’, police have advised.

 

Advertisement

90 Comments

  1. Chimene chimawawa ndichakuti akubawa akatipanga chipongwe kaya kutikhapa kaya kugwiririla achibale anthu kaya kutipha kumene akathawa a Police sapanga kanthu koma mumadandaula bwanji tikapha wakubayo?Kodi bwanji a Police osamawauzanso akubawa kuti azingoba katundu koma asamaphe mwini nyumbayo?

  2. CHIMENE CHIKUNYASA MAU OKUTI AKUGANUZILIDWA KOMA ANTHUWO ACHITA KWAPEZA RED HANDED AKUCHITA ZONYANSA NDE NKUWONA ANTHU AKUNGOLANGA OKHA DEMOCRANCY IJA NDIMENEYI TIYENI NAYO OSADANDAULA

  3. it is a bad development that mob justice is growing throughout the country. i for one i dont support it coz there is no reason regardless of the offence that someone be killed by pipo just bcoz he or she was caught in an illegal act. despite the fact that malawi police is corrupted still there is a need to hand over suspected individuals to them.

  4. Ntchito ndi ina ili yonse yamanja mukagwila mbava kong’onthani

  5. Pano Malawi uphawi inamukwana ndie wina azigotenga zaulele a @ ngati mukufuna kuziwa zambili news zakunja masewelo ndizina pitan pa Facebook page yanu=#ziripati_cd_com

  6. Zinazi zikumaonjeza kwambiri, nanga munthu amugwira koyamba kuti amaba then kanthawi pang’ono umu ona watulukiranso ndi zimene anthu amakwiya nazo kwambiri ndi chifukwa chake anthu akumawatengera malamuro kumanja kwawo.

  7. Zoona tatopa nazo mbava izi wina atengerepo phunziro

  8. Ine sindikugwirizana nazo poti nokha mmati malawi is a God fearing country koma bola atagwira mbavayo akanangompasa chilango choti iye asazaiwale chimtengere iye kukulapa machimo ake. Ambuye atikhululukire tonsefe poti nafeso tingazaweruzidwe ndimweso omwe taweruza nawo mzathuyu

  9. …the police has urged the people not to take the law into their own hands… Which law, yoti usabe or usaphe? Yambani mwawaphunzitsa akubawo kuti asamabe, apo bii… atha onse!

  10. Killing mmaidziwa inu? as far as how de congestion is in our prisons,I think dis cud solve de problem of congestion in our prisons & pano ma magistrate alipo ochepa!hahahaha dis is jxt another penel code of easiest sentence! Mwanza….mwapulumutsa ndalama za boma

  11. please we should not be taking law into our own hands…let the law of the land play is role…What about the thieve politicians living in the glass house has any of you throw stone to the glass house

    1. adakakhala kuti adabwelapo pakhomo pako nkukubela mau wanenawa sudakasilira kudzawayankhulanso,akuba ndi anthu achabechabe osafunikilanso dziko

  12. Zinazi nzoziyamba dala,imfa ngati imeneyi oro Mulungu imamvetsa chison-kuphedwa kokuba,what a big shame!ma warning for those who think their so smart,don’t even think of doing it cos you’ll be nxt.anthu pano alusa .

    1. pamenepa ndiye kuti chiwelengero (headcount) cha mbava chachepa ndi imodzi. kkkkkk

  13. The first advice should go to those who have the desires of stealing that they should desist from stealing from the angry mob then to the public which has lost trust in the corruptive Malawi Police Services that they should desist from taking laws into their hands.

    Thieve now breath a sigh of relief as they hear of taking them to police. Alot of thieves are getting assisted by police officers and some thieves are police officers. Police desist from breaking complainants hearts by avoiding receiving bribes.

    Mob justice is evil. We shall realise the mement one of our relations gets killed innocent.

Comments are closed.