Police worried over acts of mob justice

Advertisement
Nicholas Gondwa

The country’s security body, Malawi Police Service (MPS) says it is worried over the increase in number of cases to do with mob justice.

This comes barely days after angry mobs in Blantyre, Phalombe, and Nsanje, last week set ablaze three suspected thieves.

In an interview, Malawi Police Service spokesperson, Nicholas Gondwa, said this is too bad in as far as the country’s security is concerned.

Nicholas Gondwa
Gondwa; We are worried.

He said this act is increasing now in the country though the country’s laws clearly state that everyone is innocent until proven guilty by the court.

“As the mother of security in the country, Malawi Police Service is worried with the increase of such acts. People have granted themselves powers to do whatever they want and we know that this is being done with the power of ignorance,” said Gondwa.

Meanwhile, Gondwa says MPS is mobilizing people on what to do with suspects.

He however, said people do this deliberately claiming they have been teaching them but they chose not to do be advised.

Advertisement

108 Comments

  1. Amazuzika ndi anthu amene amaba ali osauka kare pomwe amene akuba mabillion saganyongedwe chochi zimathera pansipansi ena akuba olemela kare kumalemelera lemelera ovutika kumangovutikirabe nanga amat apolice kumalimbana ndi anthu amene akupondereza amalawi

  2. Mawa ndinu popeza kwathu kuno tose mbava ngati sichoncho tawatchulani ndinu osabawo even our leaders pakufunika amalawi azanga tiziganiza akuphedwawo ndiwoba mkuku kma acash gate awalamula zaka zosapitirira 6 mukuona bwanji amalawi?;(

  3. So you wonder why? Lol you’re not serious. Bail is free the police say so but why do they in other stations demand for cash to effect bail in the cases that aren’t of that category?
    As I’m writing this comment a mob has burnt a house of a man who mystically killed a woman whom he suspected to have killed his three days old goat. The woman was first arrested by the police on this man’s demand then bail was granted when the relatives paid cash demanded by the police. When released the man is angry and he asks her, who released you? We shall see. In a short time the woman vomits blood and dies.
    On the other side our constitution is questionable here. The mob burnt his house and all his belongings that includes a sedan car.
    We’re not judges for judgement belongs to God.

  4. Mps has to discuss with the thieves not us, tell them to stop robberring our houses if u r falling to keep them in jail for life, if they think they can not stop,we can not stop too!! We r after them until we finish all thieves

  5. Mwaiwala zakuMzuzu munthu wina wafela ku Mzuzu central Hsptl lero atamenyedwa ndi anthu olusa…munthuyo anamenya hamala ya mutu mwamzache wina utsiku ndicholinga choti amudule kumalo obisika,….ndizomwe zinapangisa anthu olusa kumenya mkuluyo mpaka adakamugoneka ku Mzuzu central,, koma ndikunena pano chigawengacho chatisiya lero,, koma omenyedwa ndi Hamala akadali mu Chipatala

  6. Go deeper awotchedwe….ife tikuvutika kusaka makobiri maiko akutali ndiye wina azingobwera kuzatenga osagwesa thukuta? Stupid Mps for stopping us killing this thieves.

  7. akubawa akamabwera kuzaba amathanso kukupha kumene kapena kukusiyira chilema ndiye njira yake ndiyongowaveka mateyala. A police muziwe kuti ndichinthu chopweteka kukupatsa chilema komanso kukubela katundu wanyumbamo woti munthu watenga zaka 15 ukutolera chimunthu china ungobwera kamozi kuzatenga olo muli inuyo apolice mungamve bwanji?

  8. Wakubatu simunthu wa bwino… amakhawulitsa akakubera koma akagwidwa ndiye mkumavetsa chisoni….. ulendo uno tixichita kukagula ma teyala owotchera akuba…. #Mfiti xachabechabe

  9. Apolice ena ndiakuba ndipo ndi omwe akulimbikitsa umbava dziko. Amawapatsa mfuto kuti adzikabela, apolice ena ali ndi magulu aanthu akuba.

  10. And the weapons these thieves use are provided to them by the same police. Once these thugs are caught the police immediately grant bail to them.
    As is the fact people do apply mob justice because we had lost hope in policemen of Nyasaland.
    Malawi Police is too much corrupted by thugs.
    Tiziwaphadi akanyimbi omwe azigwidwa akupanga za umbanda.

  11. woyeee_e_e_e Blantyre, Nsanje & phalombe.Burn dem into ashes coz police now gets their salaries from stealing.

  12. Kubwezela ndi kulipsira zili mmanja mwa mulungu.Bible limati isakondwere pamene mdani wako wapeza mavuto.umenewo ndiye mzimu wa ambuye.There4 there z nothing 2 smile about.

  13. Mob justice iz one major practice that can help to curb such impudents az we all knw security is compromised in our country

  14. With the current situatin in crimes here in Malawi i think mob justice is viable. The society is at siege with these thieves. We can not condon this. We have to eleminate them in our society for they are a setback to development. If police is ready to eliminate them in the society they have to come open and act. We hear they are part of this malpractice. We will burn them to ashes once caught.

  15. Mob-justice is the best deal to endup such conduct.for so long,we have been looking for ways on how to terminate such apalling behaviour,my appeal to all security holders,is that let this system of mob-justice be legarised.

  16. Of course,it’s the duty of the MPS to maintain peace,law & order therefore likely to bring this public notice BUT mbavazi zikuyenjeza…ndiyenso zimakhala zavala mikuzi ngakhale kuzibweretsa ku police station m’mawa ziri pa street chimodzimodzi kunjonja!

  17. Tikakuimbilani fon mumabwera after an hr or 2. Komanso simukusamala ma Land Cruiser! Plse increase yo speed othewise more fire Mob Justice

  18. mukukanika kulanga mbava A malawi police,,,,,and mob justice is the Best altenative,,,,,,kut muonetsetse amene zikumawagwerawa sikut limakhala tsoka ayi amakhala agwidwa in that act,,,,,koma akatengedwa ndi police zimapezeka kut mawalake akutibelanso anthu ake omwewo omwewoo

  19. Akuba akubwerekedwa mfuti ndi apolice,ndizosadabwitsa mbava kupita nayo kupolic uva 2dez yatuluka. Anthuwa ndi amodzi. Mukagwira kawalala avekedwe teyala nthawi yabwino basi. Aphulitsidwe maso komaso manja adulidwe ndi miyendo ngat akufuna akhale ndi moyo kut asadzabeso apo biiiii kong’onthani oyimba anaimba kale za mbava

  20. Yes, this will continue. And it must continue. We have the police, but crime rate is still high. Wat else are we going to do? Burn them to death! And i hail it as an important milestone towards achieving the fight against crime in Malawi.

  21. Malawi police 2 much bribe we catch a thief and took hm to police station after 2 days he will be released on fake bail the same day will hear that same person was stealing somewhere ife monga amalawi tigwilane manja pothetsa umbava tikagwila mbala ikuba tilange ndithu kaya kupha kumene anthu akuba alibe ntchito ndianthu obwezeletsa amzawo pambuyo

    1. Kupheratu!! Ine Anandiberapo Kungondisiira Zovala Zomwe Ndinavala, Ndiye Sindingamvere Chisoni Wakuba, Bwanji Asanandimvere Ineyo Pondibera?

  22. So if mob justice is best answer to deal with a thief why do you run away when u realise that u hv killed someone when cops are coming? Pls lets not take matters in our own hands, am not sure police can release someone if he found guilty nooo

    1. Kod iwe waganiza bwanji kubakira zigawenga ngat zimenezi? Vuto sunabeledwe kapena kuona munthu atabeledwa, sibwezi utayasamula choncho. Akuba ndi akupha choncho akuyenela kuphedwa.

    2. ine akuba anandiendetsa ndipanti ekha anandila msapato trouser malaya ndikundilanda salary yonse chaka cha 2005 mwezi wa august sindimaiwala kuyambira pompo anthu akangogwira wakuba ine ndimalanga nao kaya atakhala kuti wakubayo akuphedwa ndidzapha nao ndithu

    3. I didnt insult anyone of u and i cant, so if u think u are clever enough to come up with your insult u betta shut ur mouth What can u do if a thief is ur brother and people are stoning him to death or burn him? Can u go join them and kill ur brother? This manner always done by people who hv no spritual hearts, but Bible always tells us that “we all sinned and became dwindling in his kingdom” where do we take powers to judge others for their wrong doing? May God forgive and free the demon out of all of u who opose these words and insult, I may not blame u guys especially that one who produce stong words, but am highly blame evil inside you Amen

    4. You Must be crazy man,i think sunabeledwepo,dikila amati ukanama sikuchedwa kucha adzakubela nde udzawapitise kupolice wamva!

    5. Brothers do u know what? Devil is tricking nowadays, punishing someone for what he has done makes u to be inhuman, That is why God gave us people who deal with these people so if police corupt thats for the almighty to jugde, but for all of us mob justice is fruit of devil, even me i hv been robbed for several times but i hv never take my hand against the robber because God has never give me a power to deal with this kind of people, some of u u go to church and u even know what Jesus did when people catches a woman who commited a sin and atempt to stone her to death do u remember what Jesus told them?? “if any of you has never sinned must start stone this woman” was there anyone who went on with this?? Why?? Dont let devil to manipulate u for his own goodness against God

    6. indiana umakhala kuti kodi? unayamba waberedwapo kapena bale wako? unakumanapo ndi mbava face-face? unakadansaulapo ku police ulibe ndalama or bale woziwika? Apolice akumalawi ali ndi vuto too much corruption. their are not passionate with there work

    7. #Indiana #Sam #Maosa #Phiri in our family we dont have thieves and am only son in our family lest r women and if i can found one of our relatives people r busy stoning hm bcz he was stealing and there is aproof i can join them killing hm so that others may take a lesson

    8. #Jericho ukanena zoberedwazo ndiye ndaberedwapo nyumba yanga yathyoledwapo sipamadusa miyezi itatu osaberedwa zomenya anthu akabazi kunali kwathu koma linali tsiku limodzi limene akuba anathyola nyumba ya aneba mwasoka anathawa nkugwidwa mmodzi ine ndiamene ndinayambisa kupha kumenya wakuba usiku waku limenero, moti mmene ndimapita kukagona ndinasiya munthu uja ali wefuwefu Apolice anamtenga usiku omwewo, nditagona ndinayamba kulota mwana wamkazi ali ndi mabala thupi lonse atavala zoyera amandifunsa kodi ndi phindu lanji lomwe wapeza utamenya muthu uja? Ndinati palibe Mulungu wakwiya nawe taona tsoka lizingokusata munthu mwammenya uja likamafika mmawa chamma 10am akutengedwa ndi angelo iwe uzuznzika mpaka utalapa ndikhala munthu modzi amene uzasuse khalidwe umenewu, mmawa lake cha mma 10 ndinamva zoti wakuba uja wamwalira koma ndinasowadi mtendere ngati kuti ndapha ndine, nyengo zanga zinasokonela biznez yanga inatheratu pa mwezi umodzi, patatha miyezi 4 nkulu wanga anaphedwa ku S.A atampeza ataba za Nigeria wina kumeneko, ndipamene ndinazindikila Mulungu amafuna kundiphunzitsa china chake mpaka ndinazipereka kwa Mulungu ndiku lapa moti ndinanenesa ndizatsutsa nkhalidwe otelewu pamene ndamva kapena kuona anthu akupanga zotelezi, ndi zintchito za Satana zimenezi osamenya kapena kupha munthu akakubelani Mulungu naye azakupangila chifundo, zimene wakuberazo Mulungu amabweza x2

    9. #Chris nkhani ndiyakuti usamuweluze nzako pachimene wapanga or wakupangila Mulungu ndiamene amaweluza, pa zonse Chikondi ndicho chikuvuta, tonse ndife olengedwa ake Mulungu sanasiye lupanga mdzanja la wina aliyense guys musakhale ngati simupemphera ndizowawa ofcoz kuberedwa, koma tizipempha moyo wauzimu kwa Mulungu muzandikhulupilira

    10. Chris Mulungu sasangalara kumene ndi mchitidwe wakubawo moti pali chilango chimene chimasatilapo ukaba, koma Mulungu sakutipasa mphamvu yomulanga watibeyo, koma tipite naye kwa adindo amene Mulungu awaika, sizovuta kusatila njila yake

    11. Iwe ukudziona olungamawe chiyese tsoka chifukwa we all sinned and fall short b4 the glory of God.Enanuso apa ndinu akuba kungoti mumaba mwa masamu simumayenda usiku.What u ought 2 kno z that ahead of us there z a great day.Tsiku la chiweluzo.Ngakhale mutatchuka ndi kupha anthu akuba mmatambalawa simuzalandila kanthu kwa mulungu kma muzayankha mulandu.Akuba oziwika bwino mumawadziwa mma areas anuwo koma u stay quite cz they hv money en security. Watch out. Palibe osalakwa…palibe wamuyaya.

    12. Indiana Sam Maosa Phiri thank you for this comment. Made me see that some of my fellow Malawians are no better than Isis and . But you are saying the truth

    13. @indiana God bless u bro…tose titasata zimenezo thngz wil b gud…pipo dnt no kt tchimo mukapusa limapanga tchimo…bible imalesa kupha ife tikupha yyyy??? Tiyen tizipepherera dziko lathu kut atha asithike guys….and mulungu acita kathu…

  23. u knw what,inuyo apolice ndi amene mumayambisa cz munthu tikamubwelesa ku police ataba zithu(ndipo timakhala ndi evedence)pokutha masiku awiri or atatu amapezeka mwamutulusa,that is why ntchito tizigwila tokha,mob justice must rise,apolice mwatilaka inu

  24. Wen ur failing to do ur job,dis is de result,and yes these ppl their doing gud job cuz they,re sick with these thugs and thy find abeter way to deal with lazy ppl who want to get things for free.

  25. mob justice is the only good solution ,mbava zatikwana m’madela mwathumu a police sakuthandiza ,instead of keeping them behind bars they are releasing them to keep terrorising our communities, mbava zilibe chisoni ,us as a community we will not spare or hand over them to our crooked police , burn burn burn

Comments are closed.