Zodiak to host FAM Presidential Aspirants’ Debate

Advertisement
Walter Nyamilandu
Walter Nyamilandu
Nyamilandu: Faces opposition from Mijiga, and Phiri.

Zodiak Broadcasting Station (ZBS) will host a debate for Football Association of Malawi (FAM) presidential candidates.

According to a press release from ZBS that Malawi24 have seen, the show will be beamed ‘live’ on Zodiak television and will also be broadcast on Zodiak radio.

The debate has been scheduled to take place on Saturday, 5th December 2015 at Bingu International Conference Centre in Malawi’s capital, Lilongwe.

There are eleven days to go before FAM’s elections to take place in Mangochi on 12th December. Unlike in the two previous elections, this year there are three candidates who are competing for Chiwembe’s highest office.

Canada based Malawian, Willy Yabwanya Phiri, Wilkins Mijiga and incumbent Walter Nyamilandu are those that are eyeing the post.

Advertisement

69 Comments

  1. Kkkkkkkk koma anthu ena mukuona ngati walter amene angamugwese ndani? Musavutike ndipo pezani zina zochita, ndimafuna ndikuuzeniso kuti mukamati amatha mpila ndikumwela mukufuna kunena chani? Komaso musagawanise mitundu konse mukunenako mwagoonesa kuzikonda kwanu akulu, ukanakhala kuti uzapita nawo kokavotako mmmm iwe ndithu ukakavuta iwee, koma siyanisani ndale ndimpila. Mukazaamba kuzisata zamphila simuzasowa koma pano aaaaa ayi ndithu siilani ozisata.

  2. Zimafunika kusiilana izi. Ndikadakhala nyamilandu, ndikadatula pansi udindo poona mmene flames ikuchititsira manyazi chipani cha dpp komanso dziko la malawi

  3. Siindingaikire Comment coz Sindukavota nawo,kma #Nyamilandu Akangowinanso, Ndibwera ku #Malawi konko ndizapangitse ma By-Election coz Tatopa Naye,we need New Faces @ #FAM

  4. Football its not about how fast u run,bt its abt how wel u bounce.if someone wl say kwakuti kulibe mpira the world wl laugh @ him..no racism w r 1 in malawi.

  5. Ine Nyamilanduyu sindifuna ndikumuwona mmaso mwangamu,akagwele uko saliyekha mziko muno.FAM siyamunthu mmodzi akanapuma munthuyu abale chonde.

    1. Ine ndimadabwa kuti thawi zonse walter walter kodi alipo yekha?fifa chimodzimodzi mose mose muja ndina yamba kumva za blatter blatter palibe ena?ZACHINYENGO ZAZIPHUPHU SIZINGATHE kodi mukudziwa kuti ku FAM kuliso CASHGATE? afufuze

  6. Kudya msolo wa mphende nkhupitisilana ena alowemo and take flames into world cup tatopa ife ndikufera mu gear,Yes we can.

  7. Walter hs miserably failed in th administration of local futbal.luk @ th national team.where z th products of youth futbal?actualy wht r th platforms and sound structures of properly managing youth futbal so as 2 produce quality players and sustain their careers in th long run?wht hs changed in th standard of local futbal during th ‘century’ h hs bn at th helm?wy alwyz is h caught in th webs of corruption and office-abuse allegations?and wht bout th status of women’s footbal?isnt it surprzng tht Sulom hsnt imposed hm?thanx 4 th memories Nyamilandu bt its tym to leave.evrybody knws tht FAM and local futbal needs fixing bt w stopped bylvngtht u r th ryt guy to lead this task.imagin even sum sane wanderers fans r desperate 2 see u pack becauz ur misadministration shame them.make a wise decision nw othawyz if it wl happen tht u wl win again then it wl jst confirm th presence of weaknesses and unfairnes in th electoral system

  8. nyamirandu yemweyo amakhara nafe pamavuto ndi pa mtendere mwana okurira mumpira kokuno kumalawi akuziwa zomwe amalawi akuna.anawo fundo alimbe akungomuyoza nyamirandu mzawo olo tsiku limodzi sanawanyakhurepo amango nyakhura za mpira bisi kwaine onse voti mwana wanuwanu nyamilandu opanda ndeu ndi munthu zake ndi za mpira basi.omuyaza asiyeni aziyoza mulungu akuwaona cifukwa akuyoza mnthu opanda cifukwa.

    1. Kodi Water Nyamilandu Manda kwao ndikuti bwana. Pena pake sibwino kuika nkamwa chinthu choti sumeza, atumbuka ndi mpira zagwirizana patipo. God have mercy. Big shame on you.

  9. Thats a welcome development a zodiak,a malawi azimvere okha fundo za anthu amene akufuna kuzapikisana pa mpando wa malawi fa president.ena atha kukhala ndinzeru ndi upangiri amene ungathandize mpira wathu patsogolo,tinene zoona mpira m’malawi muno walowa pansi.flames pano ingotibulidwa ndi team ina iliyonse including tz.enawo nchito zamanja awo taziona.lets try something new.bye bye.

  10. It could have been better if the debates started b4 the nominations by the FAM affiliates. Otherwise we lost gud pple bcoz of the FAM affiliates!

  11. more fire Mijiga wawina kale iwee atumbuka alephera tiyendeseko ife akumwera sopano bcz zikuonesa kt palibe chigawo chotha mpira kuposa kumwera ndie apa tipase anthu akumwera enanu tiyeni ku simama ndi ku chipiku….ndat atumbukaso ayiiii ulendo uno zopusa…

Comments are closed.