Full time: Malawi 3-0 Djibouti

Advertisement
Malawi Flames
Flames.
Flames.;Record second win.

A spirited performance earned Malawi national football team a second win in the Cecafa after they beat Djibouti 3-0 at the tourney underway in Ethiopia.

First half goals from Gerlad Phiri Jnr and John Banda placed the Flames up before recess.

In the second half after a 15 minutes of play, Chiukepo Msowoya sealed the winner in a match Schumacher Kuwali was shown matching orders after what is deemed to be foul language on the ref.

Malawi beat Sudan 2-1 on Monday and now await to play South Sudan on Friday.

Full match report to follow.

Advertisement

427 Comments

  1. Angopezerera yofaifa ti ma team topanda mayina nde mpaka tibooke m’mimba? Ife tkudikira Malawi ikazatibula achina Kenya ndazizawo osat matakatakawa asaa

  2. As for me this is not worth celebrating when u are not performing well in big showpieces … Qualify for Afcon, then it’ll be worth chanting. Otherwise, where on FIFA ranking do these victimised teams stand…??

  3. Am happy for Malawi to start good in tournament.Anthu amanyoza kwambiri flames ikaluza koma pano asiya kuinyoza koma kumanena za maclub ngat anthuo sakumalawi.aņthu osasiyanitsa dziko ndi club. be asportman please fans. let’s put our BB.NOMA or Wat aside and support our nation team together. as one

  4. congrants my team Djibout 3-0 kwaife ndikachiyani last time malawi inati chinyapo 8-0 pano tilibwino ndithu next time izatha draw

  5. Guys l don’t understand ,try to explain what is a different between flames & BB .what l know is flames is national team not that BB club wamva amene walemba apa za BB kkkkkk flames moto lawi lawi

  6. Tonse ndi amalawi amwene national team si bullets kapana wanders,mafko, ayi musatelo mukulakwitsa mukasankha amwesa zigolio anlimo okha mmmmn kaduka. Congratulations frame

  7. congratulations flames.you are doing a nice job down there,keep it up.together we are one as a team no matter what team i belong.keep it up guys.thnks to our new coach

  8. Football in africa is greatly improving… If we won wth more gaols yrs back dont expect the same today… Work up guyz and selebrate for the win! We r living living in a world of evolution reformation!

    1. awa a malawi24 ndi aulesi eti kuchoka mpira uli pa 77 minutes ati kukhala ndi chikhulupiriro mwa chiukepo kuti amachinya chotsiriza, zoti adani anabweza iwo sakudziwa

  9. aaaaaaaaaaassssaaaaaaaaaaaaaah. tean ija yalongosokadi eti??? ya ya ya ya ya ya ya ya apa ndiye timati malawi awone kusintha amene amaikonda flames just coment on me kuti viva pure green!!!!!!!! and viva flames!!!!!!!

  10. Kuteroko en sakusangalala kuti Flames yawina. Ikamaludza kumtima mbeee! Cholinga adzipedza choyankhula. Conglatulations ma Flames.

  11. I Think There Is Something Wrong With The New Coaching Panel. How Can They Manage To Make The Team Win When They Are Used To Losing? This Is Like Escom’s Fault Of Giving Electricity Non Stp For Two Days Running Without A Black Out…Kkkkkkk That’s My Team!!! Congrats N Keep It Up Lads!!!

  12. Kumangodziwa kusapotera ma team akunja osakonda dziko lanu?anthu amene mumangodziwa kunyoza ngati mungakoche malawi ndikuwina mukagwele..congrats flames

  13. malawi now yuor coming up as worm heart of malawi indeed the warm heart if flames of fire,,,,proud of guyz

  14. Wow,we r proud of u guyz.continue working very hard.you are giving us interest of following you now.

  15. Flames ndiye team yanga imado dhadada.

  16. Big Up Boys, We can bring a Cup…. Go Boys Go Flames. This Panel is better than panel we had in Cosafa. Flames now in quarter finals.

  17. Bro that’s the likes of Djibouti. An easy beaten, and 3-0 to them it’s an improvement to Malawi it’s underperformance

  18. i like this team’s spirit…it doesnt give up..no matter how bad the results they get..DJIBOUTI… !!!!hope one day they will be one of hard teams to face…!!!anywez big up flames..

  19. flames ikuziwa kani ikulimbikila chocho koma akangoluza eish!!! nde wakumunda basi nde tikungowafunila zabwino kuti mwina amalawi nafeso tingapangeko bili

    1. #robert,is there anythng about bb here?that’s the problem wth bb supporters.u thnk bb alone cud hv done that.lol it was becoz of team spirit not individual spirit as bb supporters might think.

  20. Ngati musanatenge “juju” (mankhwala)Ambuye alemekezeke koma ngati mwatenga mankhwala akulangeni

  21. In the battle for victory only the strong and the hardworker surpasses everyone. Continue beating them, flames players we are with you

    1. ndi mpira uwu achimwene.timu yomweyi tinaichinya 8-1.game yotsatira tinaichinya 3-0.sono izi sizachilendo.more fire the flames!!!

  22. واووو حصلة على 5000 طلب صداقة و 500 لايك لصورت حسابي من خلال هذا الموقع بالمجان: www*ste*pw غير النجمة بالنقطة وادخل واستفد أنت أيضا

  23. ace watha kale ao anaona dzao dzaku galaxy fm konko kkkkkk koma nkhani ndiyakuti mpira watha malawi leading by 3 : 0 full tym. scorls by junio , j banda and chiukepo

  24. Search FAM page game started 1300hr and its 3-0 Malawi leading with goals from chiukepo Gerad phiri and John Banda not in order

  25. Kkkkkkkkkkk djibuti sanawinepo pa malawi ayi ndiye sikuti muwone ngati zidabwisa ayi mulungu analemba basi kuti izingoluza ikakumana ndi flmes monga anthu osauka okhaokha kupindilana ndevu nkamwa kkkkkkkkkk

  26. Paja timu imeneyi ndi ija imene timaikwapula kwambiri ija, ndipo ikangomva kuti asewera ndi Malawi, amangodziwiratu kuti zigoli zizidza dengu, ndiye tiye nawoni basi, akanene chilungamo!

  27. Pa galaxy fm sports amati game iyamba 3 koloko nthawi yakuno kumudzi pano 3 kolokoyo sinakwane malawi 24 mukuti malawi ikutsogola 3-0, ndiye pamenepa tikhulupilire ndani?

    1. Kkkkkkkkkkk! Za Galakisenso iiiiiiiih amzanu augogodi ozisata achita nazo kale! Pano mpira watha inu mukudikilira 3koloko kaya zanu izo ndi a galakise anuwo

Comments are closed.