Young boy in Bangwe drowns

Advertisement
Drowning

DrowningA 11 year-old boy from Bangwe Township in Malawi’s commercial Blantyre city died on Sunday after drowning in Mwipase stream where he went to swim with friends.

Limbe Police Station Public Relations Officer Widson Nhlane confirmed the incident and identified the boy as Frank Charles.

“The dead body has been taken to Queen Elizabeth Central Hospital (QECH) in Blantyre for postmoterm,” Nhlane said.

Charles hails from the area of Traditonal Authority Mabuka in Mulanje District.

Police have since advised parents to monitor their children so that they do not go to the river when they are not in the company of adults.

 

Advertisement

35 Comments

  1. Abale ndithandizeni mwina sindikumvetsetsa! Akamati makolo asamalore ana awo kupita okha ku mtsinje without munthu wamkulu akutanthauzanji? Ndanena izi pazifukwa izi:-

    1. Ngati mwanayo ali wosamva makolo angapange bwanji?

    2. Munthu wamkulu wake uti amene angalore kusiya ntchito zake nkumawatsatira ana ku mtsinje?

    3. Ngati makolowo ali a pantchito kapena business asiye aziwalondera anawo?
    Chonde ndiyankhenkoni kuti umbuli undichokere!!!

  2. Mukuti makolo azizonda ana awo ngati onse amagwira ntchito nde akanapange bwanji kumaganiza nthawi zina

  3. sometimes ngozi zinazi tikhoza kuzipewa kwa ife makolo, ana athuwa tisamawalore kupita kosambira opanda munthu owayanganira. may the soul of the boy rest in peace.

  4. What shameful journalists we have in Malawi! How can u write, “a 11!” Which xul of articles did u go? Next time try to write, “an 11”

    1. sometimes imakhala writing error. it may happen kuti mwinakeyo amafuna atalemba an but unfortunately analemba a. i hope u understand. every one makes this mistake when writing.

    2. Komanso kulemba uku ( Sad News: Young boy in Bangwe drowns A 11 year-old boy from Bangwe Township ) akukhala ngati wina wake nde wamumilitsa mwanayo, asanatumize aziiona kaye ma spelings, cormers, panctuation marks and the like, otherwise sizimakhala bwino kupupuluma kutulutsa ya ma mistake ambili, they give out their news to all people not just us malawians

Comments are closed.