Nomads coach tears his players apart

Advertisement
Eliah Kananji

Malawi Blantyre based super league side Mighty  Wanderers Coach Eliah Kananji has blamed his players for not showing commitment to the game following their 3-0 loss to Mzuzu University FC on Saturday.

Eliah Kananji
Kananji: Blames his tools.

The former Bullets coach wondered why the players show much effort during training sessions but choose to not show up during games.

”If they have problem with me they could have said, rather than to frustrate me with their type of play, it’s not football,” said Kananji.

Kananji also noted that the nomads usually have golden opportunities to score in every game they play in the league but they fail to utilize them.

Last weekend, Victor Gondwe who scored twice and Wacheta Mwenifumbo, who netted once for Mzuni, shined on top of Lali Lubani stars Muhamad Sulumba, Luka Bruno Milanzi, Jabulani Linje and Victor Nyirenda who failed to punish the rookies.

Advertisement

71 Comments

  1. I love NOMA 4 LIFE;kochi alibe vuto koma ma player makamaka striking force yathu yilibe ochinya zigoli.tingawine bwanji ngati sitikuchinya?next season try to find good strikers.Nawe wa bullets nde usayelekeze kutokota TNM inde mwatenga koma sikukwanilaso kubweza ngongole yanu ya 90 MILLION

  2. Team manager Chembekezo Zidana achoke munthu wa usiru. amenewa ndi ena amene akupangisa kuti team iziluza stupid manager. Zimatiwawatu.

  3. Zinachita kuoneseratu kt kinnah ndiakatundu coach wa national team ya Malawi osati zinazi ai………………!!!!!!!!!!!

  4. Eliya Kananji ndi kochi wabwino koma vuto ndi loti samapatsidwa ufulu ogwira ntchito payekha. Every substitution amayenera kulamulidwa ndi Yassin Osman kapena Eddington Ng’onamo. Technical Panel ikukokerana mphamvu ndi kochi m’malo mompatsa mpata kuti agwire ntchito yake momasuka ngati kochi.

  5. Koma “kananji” ndye wagaya english yabwinotu.kkkkkkk! Interpleter wake ndani ameneyo????

  6. A BB NTHAWI ZINA SAMALIPIDWA NTHAWI ZINA AMANYANYALA TRAINING KOMA SANAGONJEPO NGATI CHONCHI AYI.ZAMANYAZI.STUPID MIGHTYBFORWARD PLAYERS.

  7. To Join the Illuminati family originally called the ILLUMINATE ORDER; explore the ends of riches…..I extend an open invitation to all those who agree with the concept of individual rights to apply to join the Illuminati Order. The more members it has, the greater its influence will be. Join the world of the happiest and most influenced people in the world and be the first to join in your community and spread the word of the famous SASHA FIERCE. Call +2347033672143 Join the great Illuminate.Email:[email protected]

  8. ku bullets kuwina zikho ndi chikhalidwe, dzina lokhalo longoti bullets player amadziwa kuti si team yamasewera nde sapanga chibwana. kananji uxamafanizire bullets ndi noma ndi tsoka

  9. Nkhan zinaz musamaziike apa zikutithera nthaw waluza, waluza basi. Osangoyang’ana chitsogolo bwanj. Mumainena #bullets kt siichita bwno ths round lero ikulepherayo nd bullets? Tidzingokuyang’anani kt mutani. Tiye nazoni!

  10. tikumane Ku Bb vs tiga kuti kananji aphunzireko tima technics.

  11. Hahahahahahahha just dissolve the whole team including Mr Kananji

  12. Noma iri ndi ma player ambiri abwino koma kananji amakondera maplayer ena samawapatsa mpata thats why angochinyidwa 4sure magame onse amene noma yawina czon ino ref amawathandiza komanso team ija iri ndi striker mmodzi yekha wophonyanso

    1. Ine ndiwa Bullets! Kananje should polish up striking force! Ife a Bullets tikakhala pa top, timafuna inu muzibwela second! Pazikhala real competition.

  13. ana aakazi akachuluka pakhomo amasowa wotsuka mbale coz amati atsuka mnzangayu chimodzimodzi inu abfwad munagundika kugula maplayer ambilimbili lelo akukanika kupasilana mpira wabwino ndiye mukonzele kusewera musenjele komwe kuli size yanu.

  14. Vuto ndilokuti team yachuluka asilamu iyi. Alipotu 10. Nanga mmesa Iwo amakhala ndi Njala akamapanga namazani

  15. Chekananjiwa zikuwavuta2 apa penapake masubstitution omwe akumachitika akumadabwitsa.2 aKananji asiyanitse BB ndi noma BB ili ndi maplayerz olimbikila till 90 mn pamene kunoma akangocinyidwa difficult kut abweze sono akamatengela kut ku BB ndinatele kunonso ndichoco zikuimbilan nyimbo nyelele “NDITHU”

  16. Kananji wants to blame players than take the blame for irresponsible fielding and sub’s. We must commend mzuni for blowing them apart. No offside goal, no referee errors, clean goals.

    Where in a must win game can you start malumbo and kaliat at central midfield leaving khobenjan,a holding midly pa bench? Where in the world can you take out kabango and put victor Nyirenda soon after bringing in fat Mlimbika for the injured suman? Milanzi was drunk,literally, but you gave him a game,then pulling him out for an out of sorts sulumba

    Your goalkeeper couldn’t command his defence for all the 3 goals( Enerst was right)

    On Sunday Cobenjan and kaziputa started, Vic,fm7,kaliat,milanzi ,sparo were dropped and you got a point.

    Stupid coach

    This was the worst technical goof

  17. Nthawi ya Bingu no donors, nthawi ya JB we had donors, nthawi ya Piter no donors. WHY?

  18. abad carpenter always blames his tools!akananji ndiolephera,thats why bb had to bring in ramadhan.

Comments are closed.