MCP members exchange blows

Advertisement
Samuel Kaphuka
Samuel Kaphuka
Kaphuka: Confirmed of the fracas.

Opposition Malawi Congress Party (MCP) members invaded the party’s headquarters in Blantyre where they exchanged blows with top officials, Malawi24 has learnt.

MCP executive committee member for the Southern region, Samuel Kaphuka, confirmed the development adding that some members have been injured in the process.

“I was there, people came and invaded our office, and everyone was running away for his or her life. But for the meantime allow me not to say much as we are yet to investigate on the matter,” said Kaphuka.

Meanwhile the number of officials believed to have been injured is not yet known.

 

Advertisement

127 Comments

  1. Chakwela pa nyaaa pako
    Pa mtumbo pako
    Mbuzi ya muthu
    Zomwe umamenyesela mtundu wanga ndi chain
    Mutu kukula ngati basi
    Ma suit ngati anapachika pa mtengo
    Wanva kape iwe
    Nde wins ati nyo nyo pano

  2. Kodi inu MAKADET a DPP, anyamata azikwanje mwasowa chochita eti? Nchifukwa chake mukukanika kulamulira dzikoli; kukacha chaphindu chomwe mukudziwa nditukwana MCP basi. MCP ndi dilu!! 2019 boma!!!!

  3. das being naive as leaders of da oplosiition, in any way if dea is a concern dey suld hav tabled it to da concerned authority. Africans let stop bing ebackword otherwse we sal continiously be underminded by great ctries, we betta unite for prosperity and dev for da next generation tu come thanx.

  4. Mwati ayuth amakumbukila chikale, koma alipo anamumanga nyakula? Kkkkk midala asiyileni achinyamata ayendetse chipani cha MCP, kunali thawisa wako angakutsomphole

  5. Hahaha mwapanga evolve from MCP to FCP, haaa #fighting #congres #party phanani tichepetse population..ndipo enanu mukuzitcha a MCP ndinu amalawi koma? Kapen makolo anu sanakuuzeni history? Mulekeretu zimenezo.

  6. Kikikikiki.. Why gentlemen? Where is contact and dialogue? Where are the four cornerstones? So mother party might not have changed iron stick treatment of anthu owukila? Kikikikikikiki

  7. nkhaniyo nde wailemba zako za tobacco koma bola aphwasulana basi anazolowera kumenya anthu pa misonkhano kupha achina sangala, matenje, chiwanga, a gadama ndi ena nde piano akudabwa zomwe akuchita anzawo ALI aaaaaaaaa tizingomenyana tokhatokha Master Chakwera ALI ku parliament kusokonezako naenso kukamba zopanda nzeru kuti sha chipani cha magazi Mulungu amachifulatiradi eti, komaso yese osasusana ndi MCP wapha nawo a chiwanga sangala matenje ndi gadama just to mention but afew monga baibulo linena kuti wosasusana nafe ngwogwirizana nafe.

  8. Ma guys a MCP akupulana ku BT,mfazi mukulesanu kaya ife taona akuthyapana

  9. Munaonelapo film ya ROBOT ya chichewa?kodi CHIPI amafana ndi president wa chipani chiti?

  10. Zabodza zmenezo, amamenyana ma member a MCP Kapena anthu amene anakhala pa office ya MCP?

  11. Zabodza sizisowa! Mutu wankhani ndi nkhani zikusiyana bwanji? Malo amene ukunenawo pamakhala onenelela mabasi obwera ku lilongwe komaso pali mashop,kodi pamene pali office aliyense okhalapo amagwira ntchito mu office? Komaso nkhaniyi mmalema ngati wina amakuthamangitsani ndinudi atola nkhani enieni kapena mudatulukila pawindo bwanji. Shame on you!!!!

    1. Vuto siolemba koma iweyo. Suziwa kuti malo onseaja ndi a MCP ndipo enao amangopanga rent? Upite ukaonesese bwinolomwe analemba kuti MCP headquarters

  12. Ndale zapa Malawi,nokhanokho mumenyelananji?tiyeni mugwilane manja. MCP ndipani chachikulu .zikapitilila chomchi,aaa kaya.

  13. Koma chipani ichi chili ndi magazi m’manjadi eti? mpaka kusinthana zibonyongo nokhanokha! Nanga kuti muzalamulire nde kuti muzatha mtundu wonse wa a Malawitu!…mapazi anu anyani a MCP!

  14. WWE at MCP headquarter in BT Chakwela join Authality and muthalika thnks if it is gud to join authority. Monday raw night is DDP tag team agains Man of god + man of politics #chakwela and referee Atupele mwana wa Muluzi

  15. Anthu azimenyana mu banja ndiye mukanene mundale.. Amene anayambitsa ndi Alomwe amene ali mu MCP. Alomwe sianthu anzeru ndaonela Ibu.

    1. kumangot mchewa kutichani stupit…alomwe takuziwani kamba ka Bingu..ma hule ambiri ndi alomwe,opemphapempha alomwe,,mbava alomwe zopusa basi,,akamat malaw ndiosauka ife timangot alomwe zitsiru koposa ndi bwampini….

    1. Mizimu Yalusa Kuli Chilala Cha Magazi.Mwazi Oti Apelekere Nsembe Ngati Wa A China Solobala Sakuupeza.You Can Even Look At Their Leader He Is Spiritualy Affected Lol!

  16. Akulu-akulu ndeu ndaona ine dzulo ku office ya mcp ku bt, siyachibwana. Mpaka pano sindikubvetsa, anthu amamenyana ndi dzipika komaso kugendana ndi maduka a jerwa

    1. Sibodzayi its true coz I was there mmene amabanduranamo. Vuto atola nkhani penapake sakumadziwa chomwe akulemba. Zin2 zi zachitikira mu Blantyre momuno.

  17. Inconsistencies in the news make me to doubt its validity. the heading reads: MCP members fight in Blantyre, and the story says: Opposition Malawi Congress Party (MCP) members invaded the party’s headquarters in Lilongwe where they exchanged blows with top officials. Which is which Blantyre of Lilongwe?

    1. Flames ayikanila kumenya Cecafa. Few dys later, flame imenya ndi Sudan mu game yoyamba ya Cecafa. Ungodziwilatu kuti sakudziwa kuti zinthu zikuyenda bwanji. They just write hearsays!

  18. Heheheee! Koma kumeneko,,,,,u r failing to run ur own party how will u b able to run a big country like mw,,,aishoshe aione!kkk

Comments are closed.