Ex Flames goalkeeper Trust Lunda critically ill

Advertisement
KCH
KCH
Lunda remains at KCH.

Former Malawi national team and Big Bullets goalkeeper  Trust Lunda is in hospital critically down with cancer and is currently receiving medication at Kamuzu central hospital in Lilongwe, Malawi24 can report.

The team’s vice general secretary Kelvin Moyo confirmed this to Malawi24 on Sunday afternoon.

Moyo said Lunda has been suffering from the cancer for sometime now and Bullets management is taking care of anything required for his treatment.

Currently he is under the watch of Bullets officials in the capital.

Lunda served Bullets and the national team until he was off the pitch five years ago.

MORE TO FOLLWO

Advertisement

87 Comments

  1. i go thru some of your coment amalawi,ena kuyakhula ngat munalegedwa ndi satana ena zamzeru koma choti muziwe God z wotching, trust yes anali wathu end takhala naye especially muthawi yowawawisa now he z back from south africa wea he went, wabwela akudwala instead of kuti timuyikise m’mapephelo tikuyakhula zopusa

  2. Kolani ikutiuza kuti kwaiwe onyoza utenda wazako ziwa kuti mulungu alipafupi nawe@kwaine ndingoti mulungu mwini chison mwini chifundo chambili amuchilise nyamatayu

  3. Guys before u throw in ur comment think twice coz Moto umapita kumene kwatsala tchire Tommorrow its U,Mw24 Can u pliz shade more light on the topic Nice time!!!!

  4. Guys sikulozedwa uku km vuto ndilokuti kuntchuka mumachi manyazi ndi matenda mmalo moto mukamva kuwawa muzithamangira kuchipatala mumachita manyazi mapeto ake kumapita kuchipatala zitavuta kale cancer anthu akuchila ikaziwika nsanga ine umboni ndilinawo athu akuchila koma mavuto ndi manyazi

    1. Mwayambapotu Bullets Kuiona Kuloza Kwabas Ameneyi Anachoka Kalekale Ku BB Cghmene Chkfnka Nd Thandzo Bas Kt Iye Apabwno Osa Zmene Ukunenazo Ndyekt Atsu Uja Noma Inalozaso Munthu Opanda Mwambo Iwe Ndpo Nzeru Ulibeso Ukamafna Kunena Uzyamba Waganzakaye Greatford Masa Henry G Nkhoma Desire Wa Hastings Mpaso Millie Merrick Kumvana Charlyn Lyton Yohane Ve Gabadin Nanthala Victoria Wa Kennedy Runnel Jonas

  5. Munthu kuponya mpira mpaka national team nkumavutika?Koma luso la mpira silipasidwa ulemu chifukwa chani?koma player akamwakira ndie zokamba mbweee.

  6. Dnt say abullets help aliyense akhoza kuthandiza.we r talking of trust’s lyf here!!come on guys on the other hand here FAM has no choice we want their hand the man is unconscience …players are suffering thy r not payed well …provide some money guys send him out side the country…save trust..save trusty

  7. Eish…what is happening to our legends? Wishing u a quick recovery legend!!

  8. It’s good to be serious sometime Trust never saved only Bullets,let’s join hands & save life here rather than pointing out who is responsible even FAM must do something…may the healing hand of our Lord touch him

  9. Wishing Trust Lunda God’s healing. Sad that some people may have stolen money at the gates when Trust was manning the goal posts for a full house at the stadiums but are nowhere to come to assist trust at this time of great need. God will punish them.

  10. kodi inu a malawi 24, mukudziwa kuti ndi mlamdu kunka nafalisa matenda a munthu ngati mwini wake sanapereke consent? r u tellin mi kuti mwanva kuchoka pakamwa pake or else mukungomva mwa anthu? amasumilidwatu anthu

  11. Mmm guys osanyoza ku Central kuli chithandizo cha cancer chabwino than zipatala zina zimene mumaziganizira inuzo. Wina anapalitsa bala la khansa Dr ataona ngati ndi chotupa chabe ndipo zotsatira zake anamwalira.

  12. Don’t be deceived, no hospital can heal cancer. Call on 0888522571 for true healing from the lord. Speak to Heston Munthali for a testimony. God bless you

Comments are closed.