Primary school teacher arrested for raping a pupil

Advertisement
Arrested

ArrestedPolice in Malawi’s capital city,Lilongwe have nabbed Sofiano Samiton, an ODL teacher at Mchoka Primary School, for allegedly raping a standard 6 pupil.

National Police Publicist, Rhoda Manjolo, confirmed the development saying that Samiton allegedly raped the pupil in July this year in Kabudula village.

“The suspect who was an ODL teacher dragged the victim to a bush and forced himself into her and later the suspect told the victim that he will assist her during final examinations,” said Manjolo.

Police are urging the general public not to take advantage of vulnerable people especially younger girls or people with mental problems.

Rape cases have been on the rise in the country, but the Police and judiciary are trying their level best in dealing with perpetrators of rape.

Advertisement

87 Comments

  1. Mkulu Ameneyu Kpanda Mantha Kwake Inu, Kuchta Zmenezo Pafp Nd Capital Hill. Kkkk! Anafunika Kumudz Kmwe Amaona Ngt M’phunzts Amachokera Kumwamba. Kk

  2. ODL ikuyenera kuthesedwa chifukwa ambiriwa alibe tarrent for teaching student koma zigololo ndi ana ophunzira

  3. ana aakazi afikapo masiku ano en ndukhulupilira kuti anagwilizana amenewo

  4. This is not a case of rape but defilement. Please our good jornalists!

  5. Apolice nditi kapena ojambulayi mchitsiru bwanji Mphunzitsi wake alikuti.Kungowona mikono yonjata munthu wake palibepo ndiye kuyilephera ntchito kumeneko.Anzanu kuno ku S Africa akamati wagwira munthu wogwoiririra amamujambula zimenezo mulekeretu tikufuna nkhani yowona yokha yokha boza basi

  6. Mwamuna ndi mamuna amagona ndi nkazi aliyese amene wavomeleza kuti eee,,ngakhaleso mulongo wako utha kugona naye? inde ngati wavomereza kutelo. tsono ngati mwana wa xulyo adavomeleza kutelo nde mukuwona ngati mwalimuyo akadatani?

  7. Yalakwa yalakwa, sir wo akadatani poti anatani kale, basi popanda nseu pakhale nsewu,popanda njira pakhale njira, mwina pamwanayo pamafunika njira sir aisekula

  8. Kodi kape ameney ngat alibe mkazi osangopta ku Bar akatnge hule bwaj kuti azngokwatilana….? chocho azikanamizila satana

  9. _na ena amaonjeza mwana wang’onong’ono thako kulifwamphula ngati mkulu zimiyendo pamtunda choncho teacher asalakwe?. komanso ODL mungoolela osayeza enawa ndiamisala inu mungoola ndi nyasisi zomwe yabooka kkkk

  10. I remember those days when a teacher used to be a role model.The recruitment of these young guys from secondary school into education system contribute alot to the downfall of its standards.These young single
    teachers tend to test their weapons on innocent girls.Its high time we regulate age and marital status in recruitment of teachers.

  11. Ntchito za katundu wake zikumuchitira umboni

  12. Wasankha Kukalandira Chakudya Chaboma Osat Ndalama Zaboma. Chisankho Nd Chake Kma Wazunztsa Ma Dependant Ake. Nzomvetsa Chisoni Coz Mmidzmu Muli Mbeta Zambiri Hevy. Angosungitsa Malo Antchto Akabwera Adzaptrize.

Comments are closed.