
With 2.8 million people in the country expected to face hunger this year, the Agricultural Development Corporation of Malawi (ADMARC) has assured Malawians that it has enough food to feed people in the country.
“We have 55 metric tonnes of maize of which 30 thousand tonnes was bought from Zambia whilst the other 25 thousand tonnes were accessed locally,” said spokesperson for ADMARC Agness Ndovi.
Ndovi added that the corporation has distributed maize to various depots throughout the country in order to maintain price.
“At the moment we are distributing maize in small market outlets of the country through our main markets,” she said.
Ndovi has since asked ADMARC staff to always alert the cooperation whenever maize is not available in their depots.
66 thoughts on “Malawians will not starve- ADMARC”
Comments are closed.

That’s nonsense bcoz people are already starving for Hunger
Amalawi ndalama zogulira chimanga azitenga kuti popeza bwana pita anasakazira ulendo waku usa? Ngati azigawa chaulere ndiyekuti sitivutika.
Are u serious? Dnt u know that pple are already starving?
Mmalo muti muzizazisa madepot akumizi mvula isanayambe mkukhalira kuzitama. Nde mvula ikayamba magalimoto yazapitisa chimanga kumadepot akumizi. Azikaunjikana mmadepot amtauni ngat kwawu kulibe Admarc. Zitsiru.
Chimodzimodzi mene amapangira feteleza wamacoupon. Pali ali phee koma akudziwa zoti mvula ikubwera. Nde azizanamizira mvula. Makhuluku amenewa. Zitsirunso
chimanga chombwera dzulo kuyamba kugulitsa lelo kutheratu ndiye. akumakhala ma tones angati?so should we trust u , kapena akumagula ndi ma vendor tifatu kuno!!!
Tumizani chimanga chambiri mmaADMARC kuti anthu asavutike osamangolengeza kuti tilinchimanga chochuluka pamene mukumabweretsa chochepa,revisit ur systems
Chilichonse ndale umbuli ndimatendadi
ngati chimanga pano chayamba kale kusowa mukugulitsa usiku kwa mavenda. mukakhuta osamalemba zopusa azanu tayamba kale kusowa kogula chimanga.
this is somehow insane,,,, muyende mmidzimu muone anthu mmene akuvutikila ndi njala
Ok
Horses starve while grass grows so too Malawians are starv’n while d silos ar full with d grain,ADMARC is 4 vendors not 4 poor village pple.U sayin Malawians will not starve while d ar already starv’n.
kodi kulikulo kuli mbuli zokhazokha eti?
Muzigawa?
Akagule. Kugawa chani
apa nde zanyanya,mpaka 20kg?zopuuusa! kukadakhala kut ma weapon fire ndiambwelekete tikadangoyambapo kuphulitsana bas.tiyenayon uko 20 kg yanuyo
Talking bullshit u guyz were iz the maize
How are you going to feed them? Are you going to go village to village and house to house to see if the people have food? You’ve got a humongous task on your hand if you don’t want the people of Malawi to starve.
They should find money and go buy.
no comment malawi is scrap country
Its not
what u mean is nt,luk at nw wats happening in our country every tym we face same problems.wn it gonna end up ?and our leaders thy doing nothng abt it
goverment doing nothng to our pple,we dt deserve free thngs from thm.bt atleast chakudya chisamasowe
Assurance as usual
Chimanga mwati chilipo chambili nanga bwanji anthu akugula malile 20kgs? Akulu anu amithatu tiyeni nazo
Taganizani. Malawi ili ndi anthu ambili. Ngati wina aliense atapite kumeneko kukagula ma 80 kg. Chitha mwansanga
Siife anaa oti kutinamiza