
With 2.8 million people in the country expected to face hunger this year, the Agricultural Development Corporation of Malawi (ADMARC) has assured Malawians that it has enough food to feed people in the country.
“We have 55 metric tonnes of maize of which 30 thousand tonnes was bought from Zambia whilst the other 25 thousand tonnes were accessed locally,” said spokesperson for ADMARC Agness Ndovi.
Ndovi added that the corporation has distributed maize to various depots throughout the country in order to maintain price.
“At the moment we are distributing maize in small market outlets of the country through our main markets,” she said.
Ndovi has since asked ADMARC staff to always alert the cooperation whenever maize is not available in their depots.
66 thoughts on “Malawians will not starve- ADMARC”
Comments are closed.

Fans imavutika kushopa chimanga!mavenda boomer amapeza metre,zauchikape!!
Ku Malawi mkwausilu…chimanga chilipocho mukangogulitsa kuchibuku…Timwe bota bax…Ndalama zake mudye inuyo…ZAUSILU.!!
Ngati Kuli 2.8 milion tones, bwanji ku Gawanani admark ku machinga anabweletsa 90 bags yokha? ndikutha isanakwane 10 koloko? mukunamiza ndani?
Koma onsewa anagula mmera wo?
We are already starving no maize @ nearest market here Kasungu
That’s our habit. That’s our yearly living. No strange on that.
Ndili ndichisoni pomva izi chifukwa ku admarc chikabwera chimanga akugura ndima venda ndpo truck yomwe yanyamura chimangacho sifika komwe amakachisitsa kwina ndpo ineyo maumboni alipo maka kumachinga nde zanyanya
Tamanenani zoona chimanga chake chili kuti? anthu akuvutika ndi njala pano.
that’s nice. koma mumuwuzenso Vendor akhale ndi mkhalidwe chonde asayandikile ku ADMARC.
why long ques
Mw ali pamoto wa lawilawi koma wothesa zosezi ndiye namalenga
When r u going 2 start ? Komanso chimanga zogulisa usiku zitheletu anthu apanda chisoni inu
Ngat mwadya maban,mukanamize abale anu.pano anthu ayamba kale kugona nd njala ndye inu muzthoka zachamba
kodi kumalawi kuno kuli anthu 2.8 million y cant u keep maize 4 atleast half of the population
kuno kwathiu chilichonse ndi pa mzere chifukwa ca uphawi.
I would rather they starve a bit. They should know that stealing, corruption, overfishing, overpopulation, and all the other things malawians do have consicueses . Aziwe kuti mukaba ndalama, mukasiya sukulu muzavutika. Palibe atagawe chimanga. No country does that. Amalawi aphunzire kuganizila za kutsogolo, and know the consicueses of what they are doing on the present day.
bwanji mpaka pano ma ADMARC simunatsegulebe
bwanji mpaka pano ma ADMARC simunatsegulebe